< Masalimo 114 >

1 Pamene Israeli anatuluka mu Igupto, nyumba ya Yakobo kuchoka ku mtundu wa anthu a chiyankhulo chachilendo,
Kad Israēls izgāja no Ēģiptes, Jēkaba nams no svešas valodas ļaudīm,
2 Yuda anasanduka malo opatulika a Mulungu, Israeli anasanduka ufumu wake.
Tad Jūda Viņam tapa par svētu daļu, un Israēls par Viņa valstību.
3 Nyanja inaona ndi kuthawa, mtsinje wa Yorodani unabwerera mʼmbuyo;
Jūra redzēja un bēga, Jardāne griezās atpakaļ;
4 mapiri analumphalumpha ngati nkhosa zazimuna, timapiri ngati ana ankhosa.
Kalni lēkāja kā auni, pakalni kā jēri.
5 Nʼchifukwa chiyani iwe unathawa? iwe mtsinje wa Yorodani unabwereranji mʼmbuyo?
Kas tev bija, jūra, ka tu bēdz, un tev, Jardāne, ka tu atpakaļ griezies?
6 inu mapiri, munalumphalumphiranji ngati nkhosa zazimuna, inu timapiri, ngati ana ankhosa?
Jums, kalni, ka jūs lēkājāt kā auni, pakalni, kā jēri?
7 Njenjemera pamaso pa Ambuye iwe dziko lapansi, pamaso pa Mulungu wa Yakobo,
Priekš Tā Kunga drebi, zeme, Jēkaba Dieva priekšā,
8 amene anasandutsa thanthwe kukhala chitsime, thanthwe lolimba kukhala akasupe a madzi.
Kas klinti pārvērsa par ezeru un akmeņus par ūdens avotiem.

< Masalimo 114 >