< Masalimo 114 >
1 Pamene Israeli anatuluka mu Igupto, nyumba ya Yakobo kuchoka ku mtundu wa anthu a chiyankhulo chachilendo,
Idi pimmanaw ti Israel idiay Egipto, ti sangkabalayan ni Jacob manipud kadagita a gangannaet a tattao,
2 Yuda anasanduka malo opatulika a Mulungu, Israeli anasanduka ufumu wake.
nagbalin ti Juda a nasantoan a lugarna, ti Israel a pagarianna.
3 Nyanja inaona ndi kuthawa, mtsinje wa Yorodani unabwerera mʼmbuyo;
Kimmita ti baybay ket nagtaray; nagsubli ti Jordan.
4 mapiri analumphalumpha ngati nkhosa zazimuna, timapiri ngati ana ankhosa.
Limmagto a kasla kalakian a kalding dagiti bantay, limmagto a kasla karnero dagiti turturod.
5 Nʼchifukwa chiyani iwe unathawa? iwe mtsinje wa Yorodani unabwereranji mʼmbuyo?
Baybay, apay a timmarayka? Jordan, apay a nagsublika?
6 inu mapiri, munalumphalumphiranji ngati nkhosa zazimuna, inu timapiri, ngati ana ankhosa?
Dakayo a banbantay, apay a limmagtokayo a kasla kadagiti kalakian a kalding? Dakayo a babassit a turturod, apay a limmagtokayo a kasla kadagiti karnero?
7 Njenjemera pamaso pa Ambuye iwe dziko lapansi, pamaso pa Mulungu wa Yakobo,
Agpigergerka lubong, iti sangaonan ti Apo, iti imatang ti Dios ni Jacob.
8 amene anasandutsa thanthwe kukhala chitsime, thanthwe lolimba kukhala akasupe a madzi.
Pinagbalinna ti bato a dan-aw ti danum ken ti natangken a bato nga ubbog ti danum.