< Masalimo 114 >

1 Pamene Israeli anatuluka mu Igupto, nyumba ya Yakobo kuchoka ku mtundu wa anthu a chiyankhulo chachilendo,
Quand Israël est sorti d'Égypte, la maison de Jacob d'un peuple de langue étrangère,
2 Yuda anasanduka malo opatulika a Mulungu, Israeli anasanduka ufumu wake.
Juda est devenu son sanctuaire, Israël sa domination.
3 Nyanja inaona ndi kuthawa, mtsinje wa Yorodani unabwerera mʼmbuyo;
La mer le vit et s'enfuit. Le Jourdain a été repoussé.
4 mapiri analumphalumpha ngati nkhosa zazimuna, timapiri ngati ana ankhosa.
Les montagnes ont sauté comme des béliers, les petites collines comme des agneaux.
5 Nʼchifukwa chiyani iwe unathawa? iwe mtsinje wa Yorodani unabwereranji mʼmbuyo?
Qu'est-ce qui t'a fait fuir, toi la mer? Vous, Jordan, vous avez fait demi-tour?
6 inu mapiri, munalumphalumphiranji ngati nkhosa zazimuna, inu timapiri, ngati ana ankhosa?
Vous, montagnes, que vous avez fait sauter comme des béliers? Vous êtes des petites collines, comme des agneaux?
7 Njenjemera pamaso pa Ambuye iwe dziko lapansi, pamaso pa Mulungu wa Yakobo,
Tremblez, terre, devant la présence du Seigneur, en présence du Dieu de Jacob,
8 amene anasandutsa thanthwe kukhala chitsime, thanthwe lolimba kukhala akasupe a madzi.
qui a transformé le rocher en une mare d'eau, le silex en une source d'eau.

< Masalimo 114 >