< Masalimo 114 >

1 Pamene Israeli anatuluka mu Igupto, nyumba ya Yakobo kuchoka ku mtundu wa anthu a chiyankhulo chachilendo,
Der Israel drog ud af Ægypten, Jakobs Hus fra et Folk, som havde et fremmed Maal,
2 Yuda anasanduka malo opatulika a Mulungu, Israeli anasanduka ufumu wake.
da blev Juda til hans Helligdom, Israel til hans Herredømme.
3 Nyanja inaona ndi kuthawa, mtsinje wa Yorodani unabwerera mʼmbuyo;
Havet saa det og flyede; Jordanen vendte om og løb tilbage.
4 mapiri analumphalumpha ngati nkhosa zazimuna, timapiri ngati ana ankhosa.
Bjergene sprang som Vædre, Højene som unge Lam.
5 Nʼchifukwa chiyani iwe unathawa? iwe mtsinje wa Yorodani unabwereranji mʼmbuyo?
Hvad skete dig, du Hav! at du flyede? du Jordan! at du vendte om og løb tilbage?
6 inu mapiri, munalumphalumphiranji ngati nkhosa zazimuna, inu timapiri, ngati ana ankhosa?
I Bjerge! at I sprang som Vædre? I Høje! som unge Lam?
7 Njenjemera pamaso pa Ambuye iwe dziko lapansi, pamaso pa Mulungu wa Yakobo,
Bæv, o Jord! for Herrens Ansigt, for Jakobs Guds Ansigt;
8 amene anasandutsa thanthwe kukhala chitsime, thanthwe lolimba kukhala akasupe a madzi.
han, som forvandler Klippen til en vandrig Sø, Flint til et Kildevæld!

< Masalimo 114 >