< Masalimo 114 >
1 Pamene Israeli anatuluka mu Igupto, nyumba ya Yakobo kuchoka ku mtundu wa anthu a chiyankhulo chachilendo,
Když vycházel Izrael z Egypta, a rodina Jákobova z národu jazyka cizího,
2 Yuda anasanduka malo opatulika a Mulungu, Israeli anasanduka ufumu wake.
Byl Juda posvěcením jeho, Izrael panováním jeho.
3 Nyanja inaona ndi kuthawa, mtsinje wa Yorodani unabwerera mʼmbuyo;
To když vidělo moře, uteklo, Jordán nazpět se obrátil.
4 mapiri analumphalumpha ngati nkhosa zazimuna, timapiri ngati ana ankhosa.
Hory poskakovaly jako skopci, pahrbkové jako jehňata.
5 Nʼchifukwa chiyani iwe unathawa? iwe mtsinje wa Yorodani unabwereranji mʼmbuyo?
Coť bylo, ó moře, že jsi utíkalo? Jordáne, že jsi nazpět se obrátil?
6 inu mapiri, munalumphalumphiranji ngati nkhosa zazimuna, inu timapiri, ngati ana ankhosa?
Ó hory, že jste poskakovaly jako skopci, pahrbkové jako jehňata?
7 Njenjemera pamaso pa Ambuye iwe dziko lapansi, pamaso pa Mulungu wa Yakobo,
Pro přítomnost Panovníka třásla jsem se já země, pro přítomnost Boha Jákobova,
8 amene anasandutsa thanthwe kukhala chitsime, thanthwe lolimba kukhala akasupe a madzi.
Kterýž obrací i tu skálu v jezero vod, a škřemen v studnici vod.