< Masalimo 113 >

1 Tamandani Yehova. Mutamandeni, inu atumiki a Yehova, tamandani dzina la Yehova.
Louvado seja Yah! Louvado sejam os servos de Iavé, Louvado seja o nome de Yahweh.
2 Yehova atamandidwe, kuyambira tsopano mpaka muyaya.
Bendito seja o nome de Yahweh, a partir deste momento e para sempre mais.
3 Kuyambira ku matulukiro a dzuwa mpaka ku malowero ake, dzina la Yehova liyenera kutamandidwa.
Desde o nascer do sol até o seu pôr-do-sol, O nome de Yahweh é para ser elogiado.
4 Yehova wakwezeka pa anthu a mitundu yonse, ulemerero wake ndi woposa mayiko akumwamba.
Yahweh é alto acima de todas as nações, sua glória acima dos céus.
5 Ndani wofanana ndi Yehova Mulungu wathu, Iye amene amakhala mwaufumu mmwamba?
Que é como Yahweh, nosso Deus, que tem seu assento no alto,
6 amene amawerama pansi kuyangʼana miyamba ndi dziko lapansi?
quem desce para ver no céu e na terra?
7 Iye amakweza munthu wosauka kuchoka pa fumbi ndi kutukula munthu wosowa kuchoka pa dzala;
He levanta os pobres da poeira, e levanta os necessitados do amontoado de cinzas,
8 amawakhazika pamodzi ndi mafumu, pamodzi ndi mafumu a anthu ake.
that ele pode colocá-lo com príncipes, mesmo com os príncipes de seu povo.
9 Amakhazikitsa mayi wosabereka mʼnyumba yake monga mayi wa ana wosangalala. Tamandani Yehova.
Ele instala a mulher estéril em sua casa como uma alegre mãe de filhos. Louvado seja Yah!

< Masalimo 113 >