< Masalimo 113 >

1 Tamandani Yehova. Mutamandeni, inu atumiki a Yehova, tamandani dzina la Yehova.
Treño t’Ià. mandrengea, ry mpitoro’ Iehovà, bangò ty tahina’ Iehovà.
2 Yehova atamandidwe, kuyambira tsopano mpaka muyaya.
onjoneñe ty tahina’ Iehovà, henane zao naho nainai’e donia.
3 Kuyambira ku matulukiro a dzuwa mpaka ku malowero ake, dzina la Yehova liyenera kutamandidwa.
Boak’ ami’ty fanjiriha’ i àndroy pak’ami’ty fitsofora’e, le bangoañe ty tahina’ Iehovà.
4 Yehova wakwezeka pa anthu a mitundu yonse, ulemerero wake ndi woposa mayiko akumwamba.
Andigiligi’ ze hene fifeheañe t’Iehovà, andindi’ o likerañeo ty enge’e.
5 Ndani wofanana ndi Yehova Mulungu wathu, Iye amene amakhala mwaufumu mmwamba?
Ia ty mañirinkiriñe Iehovà Andrianañaharentika, Mpiambesatse an-dindìñe añe,
6 amene amawerama pansi kuyangʼana miyamba ndi dziko lapansi?
Mibotreke re hivazohoa’e o likerañeo naho ty tane toy.
7 Iye amakweza munthu wosauka kuchoka pa fumbi ndi kutukula munthu wosowa kuchoka pa dzala;
Ampitroare’e boak’ an-debok’ ao o rarakeo vaho ongaha’e am-botren-ditsak’ ao ty mpisotry,
8 amawakhazika pamodzi ndi mafumu, pamodzi ndi mafumu a anthu ake.
hampindreza’e fiambesatse amo roandriañeo, amo ana-dona’ ondati’eo
9 Amakhazikitsa mayi wosabereka mʼnyumba yake monga mayi wa ana wosangalala. Tamandani Yehova.
Ampitaiae’e añ’anjomba’e ao ty betsiterake, hifalea’e te renen’ anake. Treño t’Ià!

< Masalimo 113 >