< Masalimo 113 >

1 Tamandani Yehova. Mutamandeni, inu atumiki a Yehova, tamandani dzina la Yehova.
Pujilah TUHAN! Hai hamba-hamba TUHAN, pujilah nama TUHAN!
2 Yehova atamandidwe, kuyambira tsopano mpaka muyaya.
Nama-Nya akan dimasyhurkan, sekarang dan sepanjang masa.
3 Kuyambira ku matulukiro a dzuwa mpaka ku malowero ake, dzina la Yehova liyenera kutamandidwa.
Dari timur sampai ke barat nama TUHAN harus dipuji.
4 Yehova wakwezeka pa anthu a mitundu yonse, ulemerero wake ndi woposa mayiko akumwamba.
TUHAN berkuasa atas segala bangsa, keagungan-Nya mengatasi langit.
5 Ndani wofanana ndi Yehova Mulungu wathu, Iye amene amakhala mwaufumu mmwamba?
Siapa seperti TUHAN Allah kita? Ia bertakhta di tempat yang tinggi.
6 amene amawerama pansi kuyangʼana miyamba ndi dziko lapansi?
Tetapi Ia membungkukkan diri untuk memandang langit dan bumi.
7 Iye amakweza munthu wosauka kuchoka pa fumbi ndi kutukula munthu wosowa kuchoka pa dzala;
Orang miskin diangkat-Nya dari debu, dan orang melarat dari abu.
8 amawakhazika pamodzi ndi mafumu, pamodzi ndi mafumu a anthu ake.
Mereka didudukkan-Nya bersama para penguasa, bersama para bangsawan dari umat-Nya.
9 Amakhazikitsa mayi wosabereka mʼnyumba yake monga mayi wa ana wosangalala. Tamandani Yehova.
Ia menganugerahkan anak-anak kepada istri yang mandul, menjadikan dia ibu yang berbahagia dan terhormat di rumahnya. Pujilah TUHAN!

< Masalimo 113 >