< Masalimo 113 >

1 Tamandani Yehova. Mutamandeni, inu atumiki a Yehova, tamandani dzina la Yehova.
Halleluja! Kiittäkäät te, Herran palveliat, kiittäkäät Herran nimeä!
2 Yehova atamandidwe, kuyambira tsopano mpaka muyaya.
Kiitetty olkoon Herran nimi, nyt ja ijankaikkisesti!
3 Kuyambira ku matulukiro a dzuwa mpaka ku malowero ake, dzina la Yehova liyenera kutamandidwa.
Auringon koitosta hänen laskemiseensa asti olkoon Herran nimi kiitetty!
4 Yehova wakwezeka pa anthu a mitundu yonse, ulemerero wake ndi woposa mayiko akumwamba.
Herra on korkia ylitse kaikkein pakanain, ja hänen kunniansa ylitse taivasten.
5 Ndani wofanana ndi Yehova Mulungu wathu, Iye amene amakhala mwaufumu mmwamba?
Kuka on niinkuin Herra meidän Jumalamme, joka niin korkialla asuu?
6 amene amawerama pansi kuyangʼana miyamba ndi dziko lapansi?
Ja kuitenkin katsoo alimmaisia taivaassa ja maassa;
7 Iye amakweza munthu wosauka kuchoka pa fumbi ndi kutukula munthu wosowa kuchoka pa dzala;
Joka köyhän tomusta ylentää, ja vaivaisen loasta korottaa,
8 amawakhazika pamodzi ndi mafumu, pamodzi ndi mafumu a anthu ake.
Istuttaaksensa häntä päämiesten sivuun, kansansa päämiesten sivuun;
9 Amakhazikitsa mayi wosabereka mʼnyumba yake monga mayi wa ana wosangalala. Tamandani Yehova.
Joka hedelmättömät saattaa huoneesen asumaan, että hän riemuiseksi lasten äidiksi tulee. Halleluja!

< Masalimo 113 >