< Masalimo 112 >

1 Tamandani Yehova. Wodala munthu amene amaopa Yehova, amene amakondwera kwambiri ndi malamulo ake.
Kaksakin LEUM GOD! Insewowo el su sunakin LEUM GOD, Su arulana engan in akos ma sap lal.
2 Ana ake adzakhala amphamvu mʼdziko; mʼbado wa olungama mtima udzadalitsidwa.
Tulik nutin sie mwet wo fah ku in facl Israel; Fwil natul fah akinsewowoyeyuk.
3 Kulemera ndi chuma zili mʼnyumba yake, ndipo chilungamo chake ndi chosatha.
Sou lal ac fah arulana kasrup, Mwe insewowo lal ac fah yokyokelik nwe tok.
4 Ngakhale mu mdima kuwala kumatulukira olungama mtima; wokoma mtima, wachifundo ndi wowongoka mtima.
Kalem tolak in lohsr uh nu sin mwet wo, Aok, yorolos su kulang, pakoten, ac suwoswos.
5 Zinthu zabwino zidzabwera kwa iye amene amapereka mowolowamanja ndi wokongoletsa mwaufulu, amene amachita ntchito yake mwachilungamo.
Insewowo mwet se su engan in sangwin mwe kasru nu sin mwet, Ac su oru orekma lal ke pwaye ac suwohs.
6 Ndithu sadzagwedezeka; munthu wolungama sadzayiwalika mpaka muyaya.
Sie mwet suwoswos el fah tu na ku. El ac fah esamyuk in pacl nukewa.
7 Saopa akamva zoyipa zimene zachitika; mtima wake ndi wokhazikika ndipo amadalira Yehova.
El tia motok in lohng pweng koluk; Lulalfongi lal oakiyuki ku in LEUM GOD.
8 Mtima wake ndi wotetezedwa, sadzakhala ndi mantha; potsiriza pake adzayangʼana adani ake mwachipambano.
El tia fosrnga ku sangeng; El etu na lah el ac liye ke mwet lokoalok lal ah kutangyukla.
9 Wopereka mphatso zake mowolowamanja kwa osauka, chilungamo chake chimanka mpaka muyaya; nyanga yake idzakwezedwa mwaulemu.
El sang yohk nu sin mwet enenu, Ac kulang lal tiana srikeni; El ac fah ku, ac ac fah akfulatyeyuk el.
10 Munthu woyipa adzaona zimenezi ndipo adzapsa mtima; adzakukuta mano ake ndipo adzasungunuka. Zolakalaka za anthu oyipa sizidzachitika konse.
Mwet koluk elos liye ma inge ac kasrkusrak; Elos suilya in srunga lalos, ac tilelik; Finsrak lalos nukewa wanginla pac.

< Masalimo 112 >