< Masalimo 111 >

1 Tamandani Yehova. Ndidzathokoza Yehova ndi mtima wanga wonse mʼbwalo la anthu olungama mtima ndi pa msonkhano.
Хвалим Те, Господе, од свега срца на већу праведничком и на сабору.
2 Ntchito za Yehova nʼzazikulu; onse amene amakondwera nazo amazilingalira.
Велика су дела Господња, драга свима који их љубе.
3 Zochita zake ndi za ulemerero ndi zaufumu, ndipo chilungamo chake ndi chosatha.
Дело је Његово слава и красота, и правда Његова траје довека.
4 Iye wachititsa kuti zodabwitsa zake zikumbukirike; Yehova ndi wokoma mtima ndi wachifundo.
Чудеса је своја учинио да се не забораве; добар је и милостив Господ.
5 Amapereka chakudya kwa amene amamuopa Iye; amakumbukira pangano lake kwamuyaya.
Храну даје онима који Га се боје, памти увек завет свој.
6 Waonetsa anthu ake mphamvu ya ntchito zake, kuwapatsa mayiko a anthu a mitundu ina.
Силу дела својих јавио је народу свом давши им наследство народа.
7 Ntchito za manja ake ndi zokhulupirika ndi zolungama; malangizo ake onse ndi odalirika.
Дела су руку Његових истина и правда; верне су све заповести Његове;
8 Malamulo ndi okhazikika ku nthawi za nthawi, ochitidwa mokhulupirika ndi molungama.
Тврде су за ва век века, основане на истини и правди.
9 Iyeyo amawombola anthu ake; anakhazikitsa pangano lake kwamuyaya dzina lake ndi loyera ndi loopsa.
Избављење посла народу свом; постави зававек завет свој. Име је Његово свето, и ваља Му се клањати.
10 Kuopa Yehova ndicho chiyambi cha nzeru; onse amene amatsatira malangizo ake amamvetsa bwino zinthu. Iye ndi wotamandika mpaka muyaya.
Почетак је мудрости страх Господњи; добра су разума сви који их творе. Хвала Његова траје довека.

< Masalimo 111 >