< Masalimo 111 >

1 Tamandani Yehova. Ndidzathokoza Yehova ndi mtima wanga wonse mʼbwalo la anthu olungama mtima ndi pa msonkhano.
Treño t’Ià! andriañeko t’Iehovà an-kaliforan-troke añivo’ ty fivori’ o vañoñeo, naho amy valobohòkey.
2 Ntchito za Yehova nʼzazikulu; onse amene amakondwera nazo amazilingalira.
Jabahinake o tolon-draha’ Iehovào; hene biribirie’ o mifale ama’eo.
3 Zochita zake ndi za ulemerero ndi zaufumu, ndipo chilungamo chake ndi chosatha.
Lifots’ engeñe naho volonahetse o sata’eo, nainai’e ty havantaña’e.
4 Iye wachititsa kuti zodabwitsa zake zikumbukirike; Yehova ndi wokoma mtima ndi wachifundo.
Nanoe’e ho tiahy o fitoloña’e tsitantaneo; matarike naho mpanolots’arofo t’Iehovà.
5 Amapereka chakudya kwa amene amamuopa Iye; amakumbukira pangano lake kwamuyaya.
Anjotsoa’e mahakama o mañeveñe ama’eo; ho tiahi’e nainai’e i fañina’ey,
6 Waonetsa anthu ake mphamvu ya ntchito zake, kuwapatsa mayiko a anthu a mitundu ina.
Fa naboa’e am’ ondati’eo ty haozara’ o fitoloña’eo, amy nanolora’e iareo ty lova’ o kilakila ‘ndatioy.
7 Ntchito za manja ake ndi zokhulupirika ndi zolungama; malangizo ake onse ndi odalirika.
To naho mahity o satam-pità’eo; vantañe iaby o fandilia’eo.
8 Malamulo ndi okhazikika ku nthawi za nthawi, ochitidwa mokhulupirika ndi molungama.
Ie noriza’e tsy ho modo nainai’e donia, fa nanoeñe am-pigahiñañe naho an-kavañonañe.
9 Iyeyo amawombola anthu ake; anakhazikitsa pangano lake kwamuyaya dzina lake ndi loyera ndi loopsa.
Nihitrife’e fijebañañe ondati’eo linili’e ho nainai’e i fañina’ey masiñe naho mampañeveñe ty tahina’e.
10 Kuopa Yehova ndicho chiyambi cha nzeru; onse amene amatsatira malangizo ake amamvetsa bwino zinthu. Iye ndi wotamandika mpaka muyaya.
Fifotoran-kihitse ty fañeveñañe am’ Iehovà; hene mahilala ze mañorike aze. mizoañe nainai’e ty fandrengeañe aze.

< Masalimo 111 >