< Masalimo 110 >

1 Salimo la Davide. Yehova akuwuza Mbuye wanga kuti, “Khala ku dzanja langa lamanja mpaka nditasandutsa adani ako kukhala chopondapo mapazi ako.”
Dāvida dziesma. Tas Kungs sacījis uz manu Kungu: “Sēdies pa Manu labo roku, tiekams Es Tavus ienaidniekus lieku par pameslu Tavām kājām.”
2 Yehova adzakuza ndodo yamphamvu ya ufumu wako kuchokera mʼZiyoni; udzalamulira pakati pa adani ako.
Tas Kungs sūtīs Tava stipruma scepteri no Ciānas; valdi Savu ienaidnieku vidū.
3 Ankhondo ako adzakhala odzipereka pa tsiku lako la nkhondo. Atavala chiyero chaulemerero, kuchokera mʼmimba ya mʼbandakucha, udzalandira mame a unyamata wako.
Tavā kara dienā Tavi ļaudis labprātīgi parādās svētā glītumā; Tavi jaunekļi Tev nāk kā rasa no ausekļa.
4 Yehova walumbira ndipo sadzasintha maganizo ake: “Ndiwe wansembe mpaka muyaya monga mwa unsembe wa Melikizedeki.”
Tas Kungs ir zvērējis un Tam nebūs žēl: “Tu esi priesteris mūžīgi pēc Melhizedeka kārtas.”
5 Ambuye ali kudzanja lako lamanja; Iye adzaponda mafumu pa tsiku la ukali wake.
Tas Kungs pie Tavas labās rokas satrieks ķēniņus Savas dusmības dienā.
6 Adzaweruza anthu a mitundu ina, adzadzaza dziko lapansi ndi mitembo ndipo adzaphwanya olamulira a pa dziko lonse lapansi.
Viņš turēs tiesu pagānu starpā; Viņš piepildīs zemi ar miroņiem. Viņš satrieks to, kas ir galva pār lielu zemi.
7 Iye adzamwa mu mtsinje wa mʼmbali mwa njira; choncho adzaweramutsa mutu wake.
Viņš dzers no upes uz ceļa, tādēļ Viņš pacels galvu.

< Masalimo 110 >