< Masalimo 108 >
1 Nyimbo. Salimo la Davide. Mtima wanga ndi wokhazikika, Inu Mulungu; ndidzayimba nyimbo, inde ndidzayimba nyimbo zotamanda ndi moyo wanga wonse.
Oluyimba. Zabbuli ya Dawudi. Omutima gwange munywevu, Ayi Katonda; nnaayimbanga ne nkutendereza n’omwoyo gwange gwonna.
2 Dzukani, zeze ndi pangwe! Ine ndidzadzutsa mʼbandakucha.
Muzuukuke, mmwe entongooli n’ennanga ey’enkoba, nzija kuyimba okukeesa obudde.
3 Ndidzakutamandani Yehova, pakati pa anthu a mitundu ina; ndidzayimba za Inu pakati pa anthu a mitundu ina.
Nnaakutenderezanga, Ayi Mukama, mu bantu bonna, nnaakuyimbiranga mu mawanga gonna.
4 Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu, kutalika kwake kuposa kumwamba; kukhulupirika kwanu kumafika mlengalenga.
Okwagala kwo kunene, kutumbiira okutuuka ku ggulu; n’obwesigwa bwo butuuka ku bire.
5 Kwezekani Inu Mulungu, kuposa mayiko akumwamba, ndipo ulemerero wanu uphimbe dziko lonse lapansi.
Ogulumizibwenga, Ayi Katonda, okuyisa eggulu; n’ekitiibwa kyo kibune ensi yonna.
6 Tipulumutseni ndi kutithandiza ndi dzanja lanu lamanja kuti iwo amene mumawakonda apulumutsidwe.
Tulokole otuyambe n’omukono gwo ogwa ddyo, abo booyagala banunulibwe.
7 Mulungu wayankhula kuchokera ku malo ake opatulika: “Mwachipambano Ine ndidzagawa Sekemu ndipo ndidzayesa chigwa cha Sukoti.
Katonda ayogedde ng’asinziira mu kifo kye ekitukuvu n’agamba nti, “Nga nzijudde essanyu, ndisala mu Sekemu, era n’Ekiwonvu kya Sukkosi ndikigabanyagabanyaamu.
8 Giliyadi ndi wanga, Manase ndi wanganso; Efereimu ndi chipewa changa chodzitetezera, Yuda ndi ndodo yanga yaufumu.
Ensi ya Gireyaadi yange, n’eya Manase nayo yange. Efulayimu mwe muli abalwanyi bange abazira; ate mu Yuda mwe munaavanga bakabaka.
9 Mowabu ndi mbale yanga yosambiramo ndidzaponya nsapato zanga pa Edomu; ndidzafuwula mopambana pa Filisitiya.”
Mowaabu be baweereza bange abawulize; ate Edomu be baddu bange; Abafirisuuti ndibaleekaanira mu ddoboozi ery’omwanguka ery’obuwanguzi.”
10 Ndani adzandifikitsa ku mzinda wotetezedwa? Ndani adzanditsogolera ku Edomu?
Ani anantuusa ku kibuga ekigumu ekinywevu? Ani anankulembera okunnyingiza mu Edomu?
11 Kodi sindinu Mulungu, Inu amene mwatikana ndipo simuperekezanso magulu athu ankhondo?
Si ggwe, ayi Katonda, atusudde, atakyatabaala n’amaggye gaffe?
12 Tithandizeni ife kulimbana ndi mdani, pakuti thandizo la munthu ndi lopanda pake.
Tudduukirire nga tulwanyisa abalabe baffe, kubanga obuyambi bw’abantu temuli nsa.
13 Chifukwa cha Mulungu wathu, ife tidzapeza chipambano, ndipo adzapondereza pansi adani athu.
Bwe tunaabeeranga ne Katonda tunaabanga bawanguzi; kubanga y’anaalinnyiriranga abalabe baffe wansi w’ebigere bye.