< Masalimo 101 >

1 Salimo la Davide. Ndidzayimba za chikondi ndi chiweruzo chanu cholungama; kwa Inu Yehova ndidzayimba matamando.
Ngizahlabela ngomusa lesahlulelo; ngizahlabela kuwe, Nkosi.
2 Ndidzatsata njira yolungama; nanga mudzabwera liti kwa ine? Ndidzayenda mʼnyumba mwanga ndi mtima wosalakwa.
Ngizaziphatha ngenhlakanipho ngendlela eqotho. Uzakuza nini kimi? Ngizahamba ngobuqotho benhliziyo yami phakathi kwendlu yami.
3 Sindidzayika chinthu chilichonse choyipa pamaso panga. Ine ndimadana ndi zochita za anthu opanda chikhulupiriro; iwo sadzadziphatika kwa ine.
Kangiyikubeka phambi kwamehlo ami into embi. Ngiyakuzonda ukwenza kwabaphambukayo; kakuyikunamathela kimi.
4 Anthu a mtima wokhota adzakhala kutali ndi ine; ine sindidzalola choyipa chilichonse kulowa mwa ine.
Inhliziyo ephambeneyo izasuka kimi; kangiyikumazi omubi.
5 Aliyense wosinjirira mnansi wake mseri ameneyo ndidzamuletsa; aliyense amene ali ndi maso amwano ndi mtima wodzikuza, ameneyo sindidzamulekerera.
Ohleba umakhelwane wakhe ensitha, yena ngizamquma. Ophakeme ngamehlo, lolenhliziyo ezikhukhumezayo, yena kangiyikumvumela.
6 Maso anga adzakhala pa okhulupirika mʼdziko, kuti akhale pamodzi ndi ine; iye amene mayendedwe ake ndi wosalakwa adzanditumikira.
Amehlo ami azakuba kwabathembekileyo belizwe, ukuze bahlale lami. Ohamba endleleni eqotho, yena uzangikhonza.
7 Aliyense wochita chinyengo sadzakhala mʼnyumba mwanga. Aliyense woyankhula mwachinyengo sadzayima pamaso panga.
Owenza inkohliso kayikuhlala phakathi kwendlu yami; okhuluma amanga kayikuma phambi kwamehlo ami.
8 Mmawa uliwonse ndidzatontholetsa anthu onse oyipa mʼdziko; ndidzachotsa aliyense wochita zoyipa mu mzinda wa Yehova.
Insuku zonke ekuseni ngizabaquma bonke ababi belizwe, ukuze ngibaqume basuke emzini weNkosi bonke abenzi bobubi.

< Masalimo 101 >