< Masalimo 101 >

1 Salimo la Davide. Ndidzayimba za chikondi ndi chiweruzo chanu cholungama; kwa Inu Yehova ndidzayimba matamando.
Davidin Psalmi. Minä veisaan armosta ja oikeudesta: sinulle, Herra, minä veisaan.
2 Ndidzatsata njira yolungama; nanga mudzabwera liti kwa ine? Ndidzayenda mʼnyumba mwanga ndi mtima wosalakwa.
Minä tahdon vaarin ottaa oikiasta tiestä, koskas minun tyköni tulet: minä tahdon vaeltaa sydämeni vakuudessa minun huoneessani.
3 Sindidzayika chinthu chilichonse choyipa pamaso panga. Ine ndimadana ndi zochita za anthu opanda chikhulupiriro; iwo sadzadziphatika kwa ine.
En minä ota pahaa asiaa eteeni: minä vihaan väärintekiöitä, ja en salli heitä olla tykönäni.
4 Anthu a mtima wokhota adzakhala kutali ndi ine; ine sindidzalola choyipa chilichonse kulowa mwa ine.
Nurja sydän olkoon minusta pois: en minä kärsi pahaa.
5 Aliyense wosinjirira mnansi wake mseri ameneyo ndidzamuletsa; aliyense amene ali ndi maso amwano ndi mtima wodzikuza, ameneyo sindidzamulekerera.
Joka lähimmäistänsä salaa panettelee, sen minä hukutan: en minä kärsi ylpeitä ja röyhkeitä.
6 Maso anga adzakhala pa okhulupirika mʼdziko, kuti akhale pamodzi ndi ine; iye amene mayendedwe ake ndi wosalakwa adzanditumikira.
Minun silmäni katsovat uskollisia maan päällä, että he asuisivat minun tykönäni: joka vaeltaa oikialla tiellä, se pitää oleman minun palveliani.
7 Aliyense wochita chinyengo sadzakhala mʼnyumba mwanga. Aliyense woyankhula mwachinyengo sadzayima pamaso panga.
Petollisia ihmisiä en minä pidä huoneessani: ei valehteliat menesty minun tykönäni.
8 Mmawa uliwonse ndidzatontholetsa anthu onse oyipa mʼdziko; ndidzachotsa aliyense wochita zoyipa mu mzinda wa Yehova.
Varhain minä hukutan kaikki jumalattomat maasta, hävittääkseni kaikkia pahantekiöitä Herran kaupungista.

< Masalimo 101 >