< Masalimo 100 >

1 Salimo. Nyimbo yothokoza. Fuwulani kwa Yehova mwachimwemwe, inu dziko lonse lapansi.
Zaburi mar goyo erokamano. Gouru koko gi mor ne Jehova Nyasaye, un piny duto.
2 Mulambireni Yehova mosangalala; bwerani pamaso pake ndi nyimbo zachikondwerero.
Lamuru Jehova Nyasaye ka umor; biuru e nyime kuwero wende mamor.
3 Dziwani kuti Yehova ndi Mulungu. Iye ndiye amene anatipanga ndipo ife ndife ake; ndife anthu ake, nkhosa za pabusa pake.
Ngʼeuru ni Jehova Nyasaye en Nyasaye. En ema nochweyowa, kendo wan mage; wan joge, kendo wan rombene mokwayo.
4 Lowani ku zipata zake ndi chiyamiko ndi ku mabwalo ake ndi matamando; muyamikeni ndi kutamanda dzina lake.
Donjuru e rangeyene kugoyo erokamano bende biuru e laru mare kupake. Goneuru erokamano kendo pakuru nyinge.
5 Pakuti Yehova ndi wabwino ndipo chikondi chake ndi chamuyaya; kukhulupirika kwake nʼkokhazikika pa mibado ndi mibado.
Nimar Jehova Nyasaye ber kendo herane osiko nyaka chiengʼ; adierane ochwere e tienge duto.

< Masalimo 100 >