< Masalimo 100 >
1 Salimo. Nyimbo yothokoza. Fuwulani kwa Yehova mwachimwemwe, inu dziko lonse lapansi.
Kasakkung: panuekhoeh Talai taminaw pueng BAWIPA teh pholen awh.
2 Mulambireni Yehova mosangalala; bwerani pamaso pake ndi nyimbo zachikondwerero.
BAWIPA thaw hah lunghawi laihoi tawk awh. A hmalah la sak laihoi tho awh.
3 Dziwani kuti Yehova ndi Mulungu. Iye ndiye amene anatipanga ndipo ife ndife ake; ndife anthu ake, nkhosa za pabusa pake.
BAWIPA teh Cathut doeh tie hah panuek awh. Ahni ni maimouh na sak toe. Maimouh teh amae lah o awh. Maimouh teh amae tami lah o awh, ama koe ka pâ e tuhu lah o awh.
4 Lowani ku zipata zake ndi chiyamiko ndi ku mabwalo ake ndi matamando; muyamikeni ndi kutamanda dzina lake.
Lunghawilawkdeinae lahoi longkha dawk kâen awh, pholen laihoi a takhang dawk kâen awh. Ama koe lunghawi awh nateh, a min hah yawhawi poe awh.
5 Pakuti Yehova ndi wabwino ndipo chikondi chake ndi chamuyaya; kukhulupirika kwake nʼkokhazikika pa mibado ndi mibado.
Bangkongtetpawiteh, BAWIPA teh ahawi, a pahrenlungmanae teh a yungyoe a kangning, yuemkamcunae teh a yungyoe a cak.