< Masalimo 100 >

1 Salimo. Nyimbo yothokoza. Fuwulani kwa Yehova mwachimwemwe, inu dziko lonse lapansi.
Leiset pumpin Pakai a kipana samphong’un,
2 Mulambireni Yehova mosangalala; bwerani pamaso pake ndi nyimbo zachikondwerero.
kipah tah’in Pakai chu chibai boh’un vahchoila sapum pumina-angah hungun
3 Dziwani kuti Yehova ndi Mulungu. Iye ndiye amene anatipanga ndipo ife ndife ake; ndife anthu ake, nkhosa za pabusa pake.
Pakai Pathen ahi tin hettohna phongdoh un, Aman eisem uva eiho ama a ihiu ahi. Eiho ama mite ihiuvin a-an a kivah akelngoite ihiuve.
4 Lowani ku zipata zake ndi chiyamiko ndi ku mabwalo ake ndi matamando; muyamikeni ndi kutamanda dzina lake.
Thangvah pum in akulpi sungah lut un, vahchoi pum in ainsungah lut in, Akom a kipa thu sei un, amin thangvah’un.
5 Pakuti Yehova ndi wabwino ndipo chikondi chake ndi chamuyaya; kukhulupirika kwake nʼkokhazikika pa mibado ndi mibado.
Pakai phatna jehchun, ami ngailutna longlou hi tonsot'in aumjinge, chuleh akitah nahi akhang khangin aumjinge

< Masalimo 100 >