< Masalimo 10 >
1 Nʼchifukwa chiyani Yehova mwayima patali? Chifukwa chiyani mukudzibisa nokha pa nthawi ya mavuto?
Akore te Ihe mijohañe añe, ry Iehovà? Ino ty ietaha’o an-tsan-kasotriañe?
2 Mwa kunyada kwake munthu woyipa asaka wofowoka, amene akodwa mʼnjira zimene iye wakonza.
Am-pirengevohañe ty añoridaña’ o raty tserekeo o rarakeo; f’ie tsepahe’ o fikitroha’eo avao.
3 Iye amatamandira zokhumba za mu mtima wake; amadalitsa aumbombo ndi kuchitira chipongwe Yehova.
Sengè’ i tsivokatsey o fañirian-tro’eo, tata’e ty fatitiañe, naho inje’e t’Iehovà.
4 Mwa kunyada kwake woyipa safunafuna Mulungu; mʼmaganizo ake wonse mulibe malo a Mulungu.
Ty tsivokatse amy fitoeboran-tarehe’ey, tsy mitsoek’ aze; ty hoe avao ro fitsakorea’e: Tsy eo ze o Andrianañahare zao.
5 Zinthu zake zimamuyendera bwino; iye ndi wamwano ndipo malamulo anu ali nawo kutali; amanyogodola adani ake onse.
Miraorao nainai’e o sata’eo; kanao mitiotiotse ambone, tsy am-pahaisaha’e eo o fizakà’oo, le fonga ibohaboha’e o malaiñ’ azeo.
6 Iye amadziyankhulira kuti, “Palibe chimene chidzandigwedeze. Ndidzakhala wokondwa nthawi zonse ndipo sindidzakhala pa mavuto.”
Hoe ty aereñeren-tro’e: Tsy hasiotse iraho, ndra an-tsa an-tsa tsy ho ampoheke ka.
7 Mʼkamwa mwake mwadzaza matemberero, mabodza ndi zoopseza; zovutitsa ndi zoyipa zili pansi pa lilime lake.
Pea hateràñe naho katramo naho fisenge-hery i falie’ey; kilily naho haloloañe ty ambane’ i famele’ey.
8 Iye amabisalira anthu pafupi ndi midzi, kuchokera pobisalapo amapha anthu osalakwa, amayangʼanayangʼana mwachinsinsi anthu oti awawononge.
Itoboha’e o fivoñonañe an-drovao amo fietahañeo hamonoa’e ty vantañe; jilojilovem-pihaino’e ty tsy amam-pañimba.
9 Amabisalira anthu ngati mkango pa zitsamba. Amabisalira kuti agwire anthu opanda mphamvu; amagwira anthu opanda mphamvu ndi kuwakokera mu ukonde wake.
Ie mitingañe añetak’ ao hoe liona ami’ty fitsifira’e; mitampoñe hitsepake ty rarake, hiambotrak’ ami’ty mpisotry, hikozozota’e amy harato’ey.
10 Anthuwo amawapondaponda ndipo amakomoka; amakhala pansi pa mphamvu zake.
Mibotreke re, mifinake; vaho mikorovok’ amy figorea’ey i pìtso-pañolotsey.
11 Iye amati mu mtima mwake, “Mulungu wayiwala, wabisa nkhope yake ndipo sakuonanso.”
Hoe re an-troke ao: Fa nandikofan’ Añahare, fa naeta’e ty lahara’e; tsy ho vazoho’e ka.
12 Dzukani Yehova! Onetsani dzanja lanu Inu Mulungu. Musayiwale anthu opanda mphamvu.
Miongaha ry Iehovà; ry Andrianañahare, zonjò ty Fità’o; ko amoea’o o mpirekeo.
13 Nʼchifukwa chiyani munthu woyipa amachitira chipongwe Mulungu? Chifukwa chiyani amati mu mtima mwake, “Iye sandiyimba mlandu?”
Akore te ati’ o tsivokatseo t’i Andrianañahare, ie manao an-tro’e ao ty hoe: Tsy ipaia’e?
14 Komatu Inu Mulungu, mumazindikira mavuto ndi zosautsa, mumaganizira zochitapo kanthu. Wovutikayo amadzipereka yekha kwa Inu pakuti Inu ndi mthandizi wa ana amasiye.
Toe vazoho’o; eka fa oni’o ty ampoheke naho ty embetse le ho valeam-pità’o, ihe ro iatoa’ ty tsy aman’imba; vaho mpañimba ty bode-rae.
15 Thyolani dzanja la woyipitsitsa ndi la munthu woyipa; muzengeni mlandu chifukwa cha zoyipa zake zimene sizikanadziwika.
Pozaho ty sira’ o tsivokatseo naho i piaroteñey, karaofo ty haratia’e ie tsy nilefe tsikaraheñe.
16 Yehova ndi Mfumu kwamuyaya; mitundu ya anthu idzawonongeka kuchoka mʼdziko lake.
Mpanjaka nainai’e t’Iehovà; fa mongotse an-tane’e eo o fifeheañeo.
17 Mumamva Inu Yehova, zokhumba za osautsidwa; mumawalimbikitsa ndipo mumamva kulira kwawo.
Ry Iehovà, fa jinanji’o ty halali’ o tretram-poo; hafatraro ty arofo’ iareo atokilaño o ravembia’oo;
18 Kuteteza ana amasiye ndi oponderezedwa, ndi cholinga chakuti munthu amene ali wa dziko lapansi asaopsenso.
Hañomea’o to o bode-raeo naho o forekekeñeo, tsy hampinevenevera’ ondaty an-tane atoio ka.