< Masalimo 10 >
1 Nʼchifukwa chiyani Yehova mwayima patali? Chifukwa chiyani mukudzibisa nokha pa nthawi ya mavuto?
Kathutkung: Panuekhoeh Oe BAWIPA, bangkongmaw ahlanae koe na kangdue. Bangkongmaw runae tueng nah na kâhro.
2 Mwa kunyada kwake munthu woyipa asaka wofowoka, amene akodwa mʼnjira zimene iye wakonza.
Tamikathoutnaw ni kâoupnae lahoi tami karoedengnaw hah a rektap awh. A sak awh e ni amamouh letlang man naseh.
3 Iye amatamandira zokhumba za mu mtima wake; amadalitsa aumbombo ndi kuchitira chipongwe Yehova.
Tamikathoutnaw teh amamae lungngainae dawk ouk a kâoup awh. Kahounlounnaw ni BAWIPA a hnoun awh teh, a dudam awh.
4 Mwa kunyada kwake woyipa safunafuna Mulungu; mʼmaganizo ake wonse mulibe malo a Mulungu.
Tamikathoutnaw ni kâoupnae lahoi Cathut tawng ngai awh hoeh. A pouknae dawkvah, Cathut awm hoeh ati awh.
5 Zinthu zake zimamuyendera bwino; iye ndi wamwano ndipo malamulo anu ali nawo kutali; amanyogodola adani ake onse.
Lawkcengnae teh ahni hoi ahla arasang dawkvah, a tarannaw pueng hah a dudam.
6 Iye amadziyankhulira kuti, “Palibe chimene chidzandigwedeze. Ndidzakhala wokondwa nthawi zonse ndipo sindidzakhala pa mavuto.”
A lungthung hoi, kâhuen mahoeh, nâtuek hai runae kâhmo mahoeh telah a pouk.
7 Mʼkamwa mwake mwadzaza matemberero, mabodza ndi zoopseza; zovutitsa ndi zoyipa zili pansi pa lilime lake.
A pahni teh thoebonae, dumnae hoi repcoungroenae lawk hoi akawi. A lai rahim vah runae hoi payonnae teh ao.
8 Iye amabisalira anthu pafupi ndi midzi, kuchokera pobisalapo amapha anthu osalakwa, amayangʼanayangʼana mwachinsinsi anthu oti awawononge.
Kho tangkuem lampawp koe a tahung teh, tami ni hmuhoehnae koe yonnae ka tawn hoeh e naw hah a thei awh. Tami ka roedeng e hah arulahoi a pawp awh.
9 Amabisalira anthu ngati mkango pa zitsamba. Amabisalira kuti agwire anthu opanda mphamvu; amagwira anthu opanda mphamvu ndi kuwakokera mu ukonde wake.
Sendek ni a kâkhu dawk hoi a pawp e patetlah arulahoi tami ouk a pawp. Tami ka roedeng hah man hanlah a pawp. A tamlawk hoi a sawn toteh tami ka roedeng a kâman.
10 Anthuwo amawapondaponda ndipo amakomoka; amakhala pansi pa mphamvu zake.
Hottelah, karoedengnaw hah a thaonae lahoi rawp sak nahanlah, ka rahnoumca lah a tabo awh.
11 Iye amati mu mtima mwake, “Mulungu wayiwala, wabisa nkhope yake ndipo sakuonanso.”
A lungthung hoi, Cathut ni a pahnim toe. A minhmai hai a hro toe. Nâtuek hai hmawt mahoeh toe telah a pouk.
12 Dzukani Yehova! Onetsani dzanja lanu Inu Mulungu. Musayiwale anthu opanda mphamvu.
Oe BAWIPA, thaw haw. Oe Cathut, na kut dâw haw. Kârahnoumnaw hah pahnim hanh.
13 Nʼchifukwa chiyani munthu woyipa amachitira chipongwe Mulungu? Chifukwa chiyani amati mu mtima mwake, “Iye sandiyimba mlandu?”
Bangkongmaw tamikathoutnaw ni Cathut banglahai a noutna awh hoeh. A lungthung hoi, banglah pouk mahoeh ouk ati awh.
14 Komatu Inu Mulungu, mumazindikira mavuto ndi zosautsa, mumaganizira zochitapo kanthu. Wovutikayo amadzipereka yekha kwa Inu pakuti Inu ndi mthandizi wa ana amasiye.
Hateiteh, lungreithai hoi runae teh na pakhingpalang teh, na kut hoi moipathung hanlah na hmu toe. Karoedengnaw, teh nang koe a kâhnawng awh teh, nang teh, na pa ka tawn hoeh naw kabawmkung lah na o.
15 Thyolani dzanja la woyipitsitsa ndi la munthu woyipa; muzengeni mlandu chifukwa cha zoyipa zake zimene sizikanadziwika.
Tamikathoutnaw hoi tamikayonnaw e kut hah khoe pouh nateh, ceitakhai e awm laipalah, hawihoehnae pueng koung pâphue pouh haw.
16 Yehova ndi Mfumu kwamuyaya; mitundu ya anthu idzawonongeka kuchoka mʼdziko lake.
BAWIPA teh a yungyoe hoi a yungyoe totouh siangpahrang doeh. A ram thung hoi miphunnaw koung a kahma awh.
17 Mumamva Inu Yehova, zokhumba za osautsidwa; mumawalimbikitsa ndipo mumamva kulira kwawo.
Repcoungroe e hoi na pa ka tawn hoeh naw koevah, kângingnae sak hanelah, talai taminaw ni repcoungroe hoeh nahanelah,
18 Kuteteza ana amasiye ndi oponderezedwa, ndi cholinga chakuti munthu amene ali wa dziko lapansi asaopsenso.
BAWIPA, kârahnoumnaw e ngainae teh na panue teh, ahnimouh lawkceng hanelah na hnâ teh na pakeng pouh.