< Miyambo 9 >

1 Nzeru inamanga nyumba yake; inayimika nsanamira zake zisanu ndi ziwiri.
Nyansa asi ne fie; watwa nʼafadum nson ho.
2 Inapha ziweto zake ndipo yasakaniza vinyo wake; inasakaniza vinyo wake ndi kuyala tebulo lake.
Wasiesie nʼaduane afra ne nsã wato ne ɛpono.
3 Nzeruyo inatuma adzakazi ake, kuti akakhale pamwamba penipeni pa mzinda ndi kukalengeza kuti,
Wasoma ne mmaawa, na ɔfrɛ firi kuropɔn no sorɔnsorɔmmea hɔ sɛ,
4 “Aliyense amene ali munthu wamba, abwere kuno!” Kwa onse opanda nzeru inkanena kuti,
“Momma ntetekwaafoɔ nyinaa mmra ha!” Ɔka kyerɛ wɔn a wɔnni atemmuo sɛ,
5 “Bwerani, dzadyeni chakudya changa ndipo dzamweni vinyo amene ndakonza.
“Mommra mmɛdi mʼaduane na monnom nsã a mafra no.
6 Lekani zopusa zanu kuti mukhale ndi moyo; yendani njira ya nzeru yomvetsa zinthu.”
Monnya mo ntetekwaasɛm no na mobɛnya nkwa; monnante nteaseɛ akwan so.”
7 Aliyense amene amayesa kukonza munthu wonyoza amadziputira minyozo; aliyense amene amadzudzula munthu woyipa amadetsa mbiri yake.
Deɛ ɔtenetene ɔfɛdifoɔ no frɛ ahohorabɔ; na deɛ ɔka amumuyɛfoɔ anim no nya ɔyea.
8 Usadzudzule munthu wonyoza kuti angadzadane nawe; dzudzula munthu wanzeru ndipo adzakukonda.
Ɛno enti, nnka ɔfɛdifoɔ anim na ɔmmɛtane wo; ka onyansafoɔ anim na ɔbɛdɔ wo.
9 Ukalangiza munthu wanzeru ndiye adzapitirira kukhala wanzeru; ukaphunzitsa munthu wolungama ndiye adzawonjezera kuphunzira kwake.
Ma onyansafoɔ akwankyerɛ na ɔbɛkɔ so ahunu nyansa; kyerɛkyerɛ ɔteneneeni na ɔde bɛka nʼadesua ho.
10 Kuopa Yehova ndiye chiyambi cha nzeru; kudziwa Woyerayo ndiko kukhala womvetsa bwino zinthu.
Awurade suro yɛ nyansa ahyɛaseɛ Ɔkronkronni no ho nimdeɛ yɛ nteaseɛ.
11 Chifukwa cha ine nzeru, masiku ako adzachuluka, ndipo zaka za moyo wako zidzawonjezeredwa.
Me mu na wo nna bɛdɔɔso, na wɔde mfeɛ bɛka wo nkwa ho.
12 Ngati ndiwe wanzeru, nzeru yakoyo idzakupindulitsa; ngati ndiwe wonyoza ena, udzavutika wekha.
Sɛ woyɛ onyansafoɔ a, wobɛnya wo nyansa ho mfasoɔ; sɛ woyɛ ɔfɛdifoɔ a, wo nko ara na ɛbɛhunu amane.
13 Uchitsiru ndi mkazi waphokoso, wopulikira ndiponso wosadziwa zinthu.
Ɔbaa ɔkwasea yɛ ɔkasafoɔ; ɔnni ahohyɛsoɔ na ɔnni nimdeɛ.
14 Iye amakhala pa mpando, pa khomo la nyumba yake, pamalo aatali a mu mzinda,
Ɔte ne fie ɛpono ano, na ɔte akonnwa a ɛsi kuropɔn no sorɔnsorɔmmea,
15 kuti aziyitana anthu ongodutsa, amene akunka nayenda njira zawo.
na ɔfrɛfrɛ wɔn a wɔtwam hɔ, wɔn a wɔnam wɔn kwan so tee sɛ,
16 Amati, “Onse amene ndi anthu wamba abwere kuno,” ndipo kwa wopanda nzeru amati,
“Momma ntetekwaafoɔ nyinaa mmra ha” ɔka kyerɛ wɔn a wɔnni atemmuo sɛ,
17 “Madzi akuba ndiye amatsekemera; chakudya chodya mobisa ndi chokoma!”
“Nsuo a wɔwia no yɛ fremfrem na aduane a wɔdi no ahintaeɛ no yɛ dɛ!”
18 Koma amunawo sadziwa kuti akufa ali kale komweko, ndi kuti alendo ake alowa kale mʼmanda akuya. (Sheol h7585)
Nanso wɔnnim koraa sɛ awufoɔ wɔ hɔ sɛ nʼahɔhoɔ wɔ ɛda no ase tɔnn. (Sheol h7585)

< Miyambo 9 >