< Miyambo 9 >

1 Nzeru inamanga nyumba yake; inayimika nsanamira zake zisanu ndi ziwiri.
Bwanya atongi ndako na ye, atelemisi yango na makonzi sambo;
2 Inapha ziweto zake ndipo yasakaniza vinyo wake; inasakaniza vinyo wake ndi kuyala tebulo lake.
abomi banyama na ye, akamoli masanga na ye ya vino mpe, na sima, atandi mesa.
3 Nzeruyo inatuma adzakazi ake, kuti akakhale pamwamba penipeni pa mzinda ndi kukalengeza kuti,
Atindi basali na ye ya basi mpo ete babelela wuta na basonge ya bangomba ya engumba:
4 “Aliyense amene ali munthu wamba, abwere kuno!” Kwa onse opanda nzeru inkanena kuti,
« Tika ete moto nyonso oyo azangi mayele aya awa! » Atindi maloba epai ya bato oyo bazangi bososoli:
5 “Bwerani, dzadyeni chakudya changa ndipo dzamweni vinyo amene ndakonza.
« Boya kolia bilei na ngai mpe komela vino oyo nakamoli,
6 Lekani zopusa zanu kuti mukhale ndi moyo; yendani njira ya nzeru yomvetsa zinthu.”
botika nzela na bino ya bozoba mpe bokozala na bomoi, botambola na nzela ya mayele. »
7 Aliyense amene amayesa kukonza munthu wonyoza amadziputira minyozo; aliyense amene amadzudzula munthu woyipa amadetsa mbiri yake.
Moto nyonso oyo apamelaka motioli amilukelaka kosambwa, moto nyonso oyo apamelaka moto mabe amilukelaka ngambo.
8 Usadzudzule munthu wonyoza kuti angadzadane nawe; dzudzula munthu wanzeru ndipo adzakukonda.
Kopamela motioli te, noki te akoyina yo; kasi pamela moto ya bwanya, mpe akolinga yo.
9 Ukalangiza munthu wanzeru ndiye adzapitirira kukhala wanzeru; ukaphunzitsa munthu wolungama ndiye adzawonjezera kuphunzira kwake.
Teya moto ya bwanya, mpe akokoma lisusu na bwanya koleka; teya moto ya sembo, mpe akobakisa lisusu boyebi na ye.
10 Kuopa Yehova ndiye chiyambi cha nzeru; kudziwa Woyerayo ndiko kukhala womvetsa bwino zinthu.
Kotosa Yawe ezali mosisa ya bwanya; koyeba Mosantu, yango nde kozala mayele.
11 Chifukwa cha ine nzeru, masiku ako adzachuluka, ndipo zaka za moyo wako zidzawonjezeredwa.
Pamba te, na nzela na ngai, mikolo ya bomoi na yo ekokoma ebele, mpe mibu ya bomoi na yo ekobakisama.
12 Ngati ndiwe wanzeru, nzeru yakoyo idzakupindulitsa; ngati ndiwe wonyoza ena, udzavutika wekha.
Soki ozali moto ya bwanya, bwanya na yo ezali mpo na litomba na yo moko; kasi soki ozali motioli, yo moko kaka nde okomona pasi.
13 Uchitsiru ndi mkazi waphokoso, wopulikira ndiponso wosadziwa zinthu.
Mwasi ya zoba azali mwasi ya makelele, ayokaka te mpe azanga mayele,
14 Iye amakhala pa mpando, pa khomo la nyumba yake, pamalo aatali a mu mzinda,
avandaka na ekuke ya ndako na ye, atiaka kiti na ye na bisika ya likolo ya engumba,
15 kuti aziyitana anthu ongodutsa, amene akunka nayenda njira zawo.
mpo na kobenga baleki nzela, bato oyo bazali kokende na nzela na bango.
16 Amati, “Onse amene ndi anthu wamba abwere kuno,” ndipo kwa wopanda nzeru amati,
Tika ete moto oyo azangi mayele aya awa! Atindi maloba epai ya bato oyo bazanga bososoli:
17 “Madzi akuba ndiye amatsekemera; chakudya chodya mobisa ndi chokoma!”
« Mayi oyo bayibi ezalaka elengi, mpe lipa oyo baliaka na kobombama ezalaka kitoko. »
18 Koma amunawo sadziwa kuti akufa ali kale komweko, ndi kuti alendo ake alowa kale mʼmanda akuya. (Sheol h7585)
Kasi bayebi te ete epai na ye nde bakufi basanganaka, mpe ete babengami na ye bazali kati na mokili ya bakufi. (Sheol h7585)

< Miyambo 9 >