< Miyambo 7 >
1 Mwana wanga, mvera mawu anga; usunge bwino malamulo angawa.
Ka capa, kak awi kqawn ve ngai nawh, kak awipek khqi boeih ve kym lah.
2 Utsate malamulo anga ndipo udzakhala ndi moyo; samala malangizo angawa monga uchitira ndi maso ako.
Kak awipek khqi ce haana nawh hqing pyi; kak awipek boeih ve mik amyihna qeetna.
3 Uchite ngati wawamangirira pa zala zako, ndiponso ngati kuti wawalemba pa mtima pako.
Na kutawh byn nawh nak lingbyi catlap awh qee.
4 Nzeru uyiwuze kuti, “Iwe ndiwe mlongo wanga,” ndipo khalidwe lomvetsa bwino zinthu ulitchule kuti, “Bwenzi langa lapamtima.”
Cyihnaak venawh, “Ka nanu nang ni,” ti nawh, zaaksimnaak ce nam cawtnu na khy.
5 Zidzakuteteza kwa mkazi wachigololo ndiponso zidzakuthandiza kusamvera mawu oshashalika a mkazi wachilendo.
Nuk chee lakawh ni doen nawh khawsak amak leek nu a sykzoeknaak awhkawng a ni doen naak ham.
6 Tsiku lina pa zenera la nyumba yanga ndinasuzumira pa zenera.
Ka im chawhhlep ak poek awhkawng qyym nyng,
7 Ndinaona pakati pa anthu opusa, pakati pa anyamata, mnyamata wina wopanda nzeru.
Kawlung amak soep cadawng khqi ang lak awh cadawng poekthainaak amak ta ce hu nyng saw,
8 Iye ankayenda njira yodutsa pafupi ndi nyumba ya mkaziyo, kuyenda molunjika nyumba ya mkaziyo.
Nula a awmnaak lamkil benna ce cet nawh a im lam ce pan hy.
9 Inali nthawi yachisisira madzulo, nthawi ya usiku, kuli mdima.
Khawmy nawh khawmthan, thanlung khuiawh ce nula im lam ce pan hy.
10 Ndipo mkaziyo anadzakumana naye, atavala ngati munthu wachiwerewere wa mtima wonyenga.
Ce nula taw pum ak zawi suihsak ing hlawihhlan qu nawh thailatnaak ing ak khawsa ni.
11 (Mkaziyo ndi wolongolola ndiponso nkhutukumve, iye ndi wosakhazikika pa khomo.
A hyy tho nawh imawh awm poekpoek ham am ngaih nawh a khawphaa ing dym am ngaih hy.
12 Mwina umupeza pa msewu, mwina umupeza pa msika, ndipo amadikirira munthu pa mphambano iliyonse).
Tuhqoe awm imkawt awh, imkil awh, lamkil a hoeiawh van nawh sui hy.
13 Tsono amagwira mnyamatayo ndi kupsompsona ndi nkhope yake yopanda manyazi amamuwuza kuti,
A huh cadawng ce tunawh mawk hy, a hat thlang amyihna a venawh,
14 “Ndinayenera kupereka nsembe zachiyanjano. Lero ndakwaniritsa malumbiro anga.
“Kaiawh qoepnaak hyih phum ham ka taak ce, tuhngawi kak awikam amyihna pha hawh hy.
15 Choncho ndinabwera kudzakumana nawe; ndinkakufunafuna ndipo ndakupeza!
Ceamyihna awm saw nang ak do ham ingkaw ak sui hamna law nyng, nang nihuk khoem nyng.
16 Pa bedi panga ndayalapo nsalu zosalala zokongola zochokera ku Igupto.
Ka ihkhunawh hiphaih ak leek soeih, Egypt hiphaih ce phaih nyng.
17 Pa bedi panga ndawazapo zonunkhira za mure, mafuta onunkhira a aloe ndi sinamoni.
Ka ihkhun ce myrrah, aloe ingkaw thikuii ing hloen boeih hawh nyng.
18 Bwera, tiye tikhale malo amodzi kukondwerera chikondi mpaka mmawa; tiye tisangalatsane mwachikondi!
Law lah, mymcang khaw a thaih hlan dy lungnaak ing nawm haih lah sih, lungnak ingawh ngaihsoep sak lah sih nyng.
19 Mwamuna wanga kulibe ku nyumbako; wapita ulendo wautali:
Imawh ka vaa am awm hy, khawlawnk hla na khinna dii hy.
20 Anatenga thumba la ndalama ndipo adzabwera ku nyumba mwezi ukakhwima.”
Tangka bawm khyn nawh, pihla a lum hlan dy am voei law hly hy,” ti na hy.
21 Ndi mawu ake onyengerera amamukakamiza mnyamatayo; amukopa ndi mawu ake oshashalika.
Ak awitui ing sykzoek nawh, am kyihcah qunaak ing lam hang pyi hy.
22 Nthawi yomweyo chitsiru chimamutsatira mkaziyo ngati ngʼombe yopita kukaphedwa, monga momwe mbawala ikodwera mu msampha,
Cedawngawh him hamna a mi sawi vaitaw, ak qaw ami phepnaak qui aawi hamna ak cet,
23 mpaka muvi utalasa chiwindi chake, chimakhala ngati mbalame yothamangira mʼkhwekhwe, osadziwa kuti moyo wake uwonongeka.
Pha ing a thih hly a siim kaana ang hlaa ing ding nawh dawng lam a pan amyihna nula hu nace baang pahoei hy.
24 Tsono ana inu, ndimvereni; mvetsetsani zimene ndikunena.
Cedawngawh ka capa khqi aw, kak awi ve ngai unawh, kam khaa awhkaw awi ak cawn law ve haana lah uh.
25 Musatengeke mtima ndi njira za mkazi ameneyu; musasochere potsata njira zake.
Nak kawlung ing a lamawh koeh hquut sei taw, a lampyi awhkawng ce pleeng seh nyng.
26 Paja iye anagwetsa anthu ambiri; wapha gulu lalikulu la anthu.
Anih ing thlang khawzah leembai sak nawh, a him khqi awm thlang khawzah ni.
27 Nyumba yake ndi njira yopita ku manda, yotsikira ku malo a anthu akufa. (Sheol )
A im taw Ceeikhui cehnaak lamna awm nawh, thihnaak imkhui na ak sawikung ni. (Sheol )