< Miyambo 6 >

1 Mwana wanga, ngati wamuperekera mnansi wako chikole, ngati walonjeza kumulipirira mlendo,
Ka ca, na hui ham rhi na khang tih kholong ham na kut na tum atah,
2 ngati wagwidwa ndi zimene iwe unanena, wakodwa ndi mawu a mʼkamwa mwako.
Na ka dongkah olthui loh n'hlaeh coeng tih na ka dongkah olthui loh n'khaih.
3 Tsono popeza iwe mwana wanga wadziponya mʼmanja mwa mnansi wako, chita izi kuti udzipulumutse: pita msanga ukamupemphe mnansi wako; kuti akumasule!
Te te na saii dongah ka ca aw, na huul uh cakhaw na hui kah kut ah ni na pha hae. Te dongah cet, mawn lamtah na hui hloep laeh.
4 Usagone tulo, usawodzere.
Na mik te ih sak boeh, na mikkhu te ngam boeh.
5 Dzipulumutse monga imachitira mphoyo mʼdzanja la mlenje, ndi monga imachitira mbalame mu msampha wa munthu wosaka.
Kut dongkah kirhang bangla sayuep kut dongkah vaa bangla namah huul uh laeh.
6 Pita kwa nyerere, mlesi iwe; kaonetsetse njira zake kuti uphunzirepo kanthu!
Kolhnaw aw lunghi taengla cet lah, anih kah khosing ke hmu lamtah cueih van lah.
7 Zilibe mfumu, zilibe woyangʼanira kapena wolamulira,
A taengah rhalboei khaw, rhoiboei khaw, aka taemrhai ham khaw om mai pawh.
8 komabe zimasungiratu chakudya chake nthawi ya chilimwe ndipo zimatuta chakudyacho nthawi yokolola.
Khohal ah a buh te a soepsoei tih cangah ah a caak te a yoep.
9 Kodi uzingogonabe pamenepo mpaka liti mlesi iwe? Kodi tulo tako tidzatha liti?
Kolhnaw aw me hil nim na yalh vetih na ih lamloh me vaengah nim na thoh ve?
10 Ukati ndingogona pangʼono, ndingowodzera pangʼono ndingopinda manjawa pangʼono kuti ndipumule,
Bet ih, bet ngam, kut poem bet neh na yalh.
11 umphawi udzakugwira ngati mbala ndipo usiwa udzafika ngati munthu wachifwamba.
Te vaengah na khodaeng te aka cet paitai bangla, na tloelnah loh photling aka bai hlang bangla ha pawk ni.
12 Munthu wachabechabe, munthu woyipa, amangoyendayenda ndi kumayankhula zoyipa,
Aka muen hlang neh boethae hlang tah a ka dongkah olhmaang nen ni a pongpa.
13 amatsinzinira maso ake, namakwakwaza mapazi ake ndi kulozaloza ndi zala zake,
A mik neh a mikhip, a kho neh a thui, a kutdawn neh a thuinuet.
14 amalingalira zoyipa ndi mtima wake wachinyengo ndipo nthawi zonse amangokhalira kuyambitsa mikangano pakati pa anthu.
A lungbuei kah a calaak neh a tuetang takuem ah boethae bueng a paem tih, tingtoehnah neh hohmuhnah a khuen.
15 Nʼchifukwa chake tsoka lidzamugwera modzidzimutsa; adzawonongeka msangamsanga popanda chomupulumutsa.
Te dongah amah kah rhainah loh buengrhuet a thoeng thil vetih hoeihnah om kolla khaem pahoi ni.
16 Pali zinthu zisanu ndi chimodzi zimene Yehova amadana nazo, zinthu zisanu ndi ziwiri zimene zimamunyansa:
He parhuk he BOEIPA loh a thinah tih a hinglu dongah tueilaehkoi khuikah tueilaehkoi parhih tah.
17 maso onyada, pakamwa pabodza, manja akupha munthu wosalakwa,
A honghi lai aka ludoeng kah a mik, ommongsitoe kah thii aka long sak kah a kut,
18 mtima wokonzekera kuchita zoyipa, mapazi othamangira msanga ku zoyipa,
Boethae kopoek aka paem lungbuei, boethae dongla aka yong paitok kho,
19 mboni yonama yoyankhula mabodza komanso munthu amene amayambitsa mikangano pakati pa abale.
A hong kah laipai loh laithae ol a sat tih pacaboeina lakli ah tingtoehnah la a khuen.
20 Mwana wanga, usunge malamulo a abambo ako; ndipo usataye zimene anakuphunzitsa amayi ako.
Ka ca, na pa kah olpaek te kueinah lamtah na nu kah olkhueng phap sut boeh.
21 Zimenezi uzimatirire pa mtima pako masiku onse, uzimangirire mʼkhosi mwako.
Na lungbuei ah rhawp hlaengtang lamtah na rhawn ah rhawp laikoeinah lah.
22 Ukamayenda, zidzakulozera njira; ukugona, zidzakulondera; ukudzuka, zidzakuyankhula.
Na caeh vaengah nang m'mawt vetih na yalh vaengah nang te n'tawt ni, na haenghang vaengah nang n'lolmang puei ni.
23 Paja malamulo awa ali ngati nyale, malangizowa ali ngati kuwunika, ndipo chidzudzulo cha mwambo ndiwo moyo weniweni,
Olpaek tah hmaithoi ni, olkhueng khaw vangnah ni, thuituennah dongkah toelthamnah khaw hingnah longpuei ni.
24 kukupulumutsa kwa mkazi wadama, zimenezi zidzakutchinjiriza kwa mkazi wadama, ndi kukuthandiza kuti usamvere mawu oshashalika a mkazi wachiwerewere.
Huta thae taeng lamkah neh kholong nu ol hnal lamloh nang aka ngaithuen ham ni.
25 Mu mtima wako usakhumbire kukongola kwake, asakukope ndi zikope zake,
A sakthen te na thinko nen khaw nai boeh, a mikkhu neh nang te n'hloih boel saeh.
26 paja mkazi wadama amakusandutsa kukhala ngati nyenyeswa za buledi ndipo mkazi wa mwini wake amasokonezeratu moyo wako wonse.
Pumyoi nu tah buh hluem ham ni, tedae hlang yuu loh hinglu phutlo khaw a hoem.
27 Kodi munthu angathe kutenga moto zovala zake osapsa?
Hlang kah a rhang dongah hmai a poep lalah a himbai te hoeh mahpawt a?
28 Kodi munthu angathe kuyenda pa makala amoto mapazi ake osapserera?
Hlang pakhat te hmai-alh dongah a caeh lalah a kho te duih mahpawt a?
29 Ndizo zimachitikira munthu amene amagonana ndi mkazi wa munthu wina. Aliyense wokhudza mkazi wotere adzalangidwa.
A hui kah yuu te aka kun thil tih aka ben tah pakhat khaw hmil tangloeng mahpawh.
30 Paja anthu sayinyoza mbala ikaba chifukwa chakuti ili ndi njala.
A hinglu kah a lamlum dip sak hamla a huen atah hlanghuen te hlang loh hnoelrhoeng mahpawt a?
31 Komabe ngati mbalayo igwidwa iyenera kulipira kasanu nʼkawiri, ngakhale kulandidwa katundu wa mʼnyumba mwake.
A hmuh uh atah a pueh parhih la a sah saeh lamtah a im kah a boei a rhaeng te boeih a phai saeh.
32 Munthu wochita chigololo ndi wopanda nzeru. Wochita zimenezi amangodziwononga yekha.
Lungbuei aka talh huta tah samphaih, a hinglu aka phae long ni te te a saii.
33 Adzalandira mabala ndi mʼnyozo, ndipo manyazi ake sadzamuchokera.
Tlohtat neh yah a dong vetih anih kokhahnah te hmata mahpawh.
34 Paja nsanje imachititsa mwini mkaziyo kukalipa, ndipo sadzachita chifundo pobwezera.
Phulohnah khohnin ah a va kah kosi neh thatlainah dongah lungma ti mahpawh.
35 Iye savomera dipo lililonse; sangapepeseke ngakhale umupatse mphatso zochuluka motani.
A mikhmuh kah tlansum pakhat khaw khuen pah pawt vetih kapbaih yet cakhaw huem pah mahpawh.

< Miyambo 6 >