< Miyambo 31 >
1 Nawa mawu a mfumu Lemueli wa ku Massa amene anamuphunzitsa amayi ake:
Goe da gogolosu sia: amo hina bagade Lemiuele ea: me da ema sia: i,
2 Nʼchiyani mwana wanga? Nʼchiyani mwana wa mʼmimba mwanga? Nʼchiyani iwe mwana wanga amene ndinachita kupempha ndi malumbiro?
“Di da na dogolegei manodafa. Na da Godema sia: ne gadoiba: le, E da di nama i. Na da dima adi adoma: bela: ?
3 Usapereke mphamvu yako kwa akazi. Usamayenda nawo amenewa popeza amawononga ngakhale mafumu.
Dia gasa huluane dagosa: besa: le, wadela: i uda adole lasu hou maedafa hamoma. Dia muni amoga mae galagama, wadela: i uda adole lasu amoga. Amo wadela: i uda da hina bagade dunu wadela: lesimusa: dawa:
4 Iwe Lemueli si choyenera kwa mafumu, mafumu sayenera kumwa vinyo. Olamulira asamalakalake chakumwa choledzeretsa
Lemiuele! Nabima! Hina bagade dunu da waini (adini) hame manu da defea. Amola ilia waini hame hanamu da defea.
5 kuopa kuti akamwa adzayiwala malamulo a dziko, nayamba kukhotetsa zinthu zoyenera anthu osauka.
Be ilia da adini nasea ilia da sema gogolesa amola ilia da hame gagui dunu ilia moloiwane fofada: su hame dawa: sa.
6 Perekani chakumwa choledzeretsa kwa amene ali pafupi kufa, vinyo kwa amene ali pa mavuto woopsa;
Adini da amo dunu bogolalebe ilia liligi, amola nowa dunu da da: i dioi bagade galea amo ilia liligi.
7 amwe kuti ayiwale umphawi wawo asakumbukirenso kuvutika kwawo.
Amaiba: le, ilia nawene, hame gagui hou amola da: i dioi hou gogolema: ne manu da defea.
8 Yankhula mʼmalo mwa amene sangathe kudziyankhulira okha. Uwayankhulire anthu onse osiyidwa pa zonse zowayenera.
Nowa dunu da ha: gi sia: mu gogolei galea, amo fidima: ne ha: gi sia: ma. Gasa hame dunu fidima: ne ouligima!
9 Yankhula ndi kuweruza mwachilungamo. Uwateteze amphawi ndi osauka.
Ili fidili, molole sia: ne fofada: ma. Moloiwane hame gagui amo gaga: ma amola fidima: ne fofada: ma!”
10 Kodi mkazi wangwiro angathe kumupeza ndani? Ndi wokwera mtengo kuposa miyala yamtengowapatali.
Moloidafa uda lamu da hogoi helele gasa bagade ba: sa. Moloidafa uda ea lasu da igi noga: i muni bagadega lasu amo bagadewane baligisa.
11 Mtima wa mwamuna wake umamukhulupirira ndipo mwamunayo sasowa phindu.
Amo uda ea egoa da idua ea hou da moloidafa dafawaneyale dawa: sa. Amola egoa da eso huluane liligi defele gagui dialumu.
12 Masiku onse a moyo wake mkaziyo amachitira mwamuna wake zabwino zokhazokha osati zoyipa.
Amaiwane uda esalea, egoa noga: le fidisa amola egoama da: i diosu hame iaha.
13 Iye amafunafuna ubweya ndi thonje; amagwira ntchito ndi manja ake mwaufulu.
E da eso huluane hawa: hamosa esala. E da wulo gobea ha: sa amola abula amuna esala.
14 Iye ali ngati sitima zapamadzi za anthu amalonda, amakatenga chakudya chake kutali.
E da dusagai bagade defele, ha: i manu amo soge sedadega gaguli maha.
15 Iye amadzuka kusanache kwenikweni; ndi kuyamba kukonzera a pa banja pake chakudya ndi kuwagawira ntchito atsikana ake antchito.
Agoaiwane uda e da hame hadigia, wa: legadole, ea sosogo fi amogili ha: i manu gobesa, amola ea fidisu a: fini ilima hawa: hamosu hamoma: ne olelesa.
16 Iye amalingalira za munda ndi kuwugula; ndi ndalama zimene wazipeza amalima munda wamphesa.
Amaiwane uda e da soge ba: lalu bu amo soge bidilasa. Amola muni ea lai amoga e da amo soge ganodini waini hawa: bugisa.
17 Iye amavala zilimbe nagwira ntchito mwamphamvu ndi manja ake.
Agoaiwane uda e da gasa bagade gala. Amola e da hawa: obenane gasa bagade hamosa.
18 Iye amaona kuti malonda ake ndi aphindu, choncho nyale yake sizima usiku wonse.
E da ea hamobe huluane ea lamu defei amo dawa: Amola e da gasibi galu mae helefili, hawa: hamonana.
19 Iye amadzilukira thonje ndipo yekha amagwira chowombera nsalu.
Amaiwane uda da hifawane gobea ha: le, amola ea abula hi fawane amuna.
20 Iye amachitira chifundo anthu osauka ndipo amapereka chithandizo kwa anthu osowa.
E da hame gagui dunu ilima asigiba: le, liligi iaha.
21 Iye saopa kuti banja lake lifa ndi kuzizira pa nyengo yachisanu; pakuti onse amakhala atavala zovala zofunda.
Anegagi eso doaga: sea e da hame da: i diosa. Bai e da ea sosogo fi ilia anegagi abula hahamoi dagoiba: le.
22 Iye amadzipangira yekha zoyala pa bedi pake; amavala zovala zabafuta ndi zapepo.
E da ea sosogo fi ilia golamusa: fafai amo da: iya abula ida: iwane fa: sisa. Amola e da oga: yei abula amo sala.
23 Mwamuna wake ndi wodziwika pa chipata cha mzinda, ndipo amakhala pakati pa akuluakulu a mʼdzikomo.
Egoa da dunu huluane ilia e dawa: Amola e da ea fi ganodini bisilua esala.
24 Iye amasoka nsalu zabafuta nazigulitsa; amaperekanso mipango kwa anthu amalonda.
Amaiwane uda da abula amola idinigisu bulu hahamosa. Amalalu, e da bidi lasu dunu ilima amo liligi bidi lasa.
25 Mphamvu ndi ulemu zimakhala ngati chovala chake; ndipo amaseka osaopa zamʼtsogolo.
Amola amo uda e da gasa bagade amola eno dunu da ema nodosa. Amola e da fa: no misunu hou amoga hame beda: sa.
26 Iye amayankhula mwanzeru, amaphunzitsa anthu mwachikondi.
Amola e da asabole, dawa: le sia: sa.
27 Iye amayangʼanira makhalidwe a anthu a pa banja lake ndipo sachita ulesi ndi pangʼono pomwe.
Amola amo uda da mae hihini amola hame helefisa. E da ea sosogo fi ilia hanai liligi huluane defele hamosa.
28 Ana ake amamunyadira ndipo amamutcha kuti wodala; ndipo mwamuna wake, amamuyamikira nʼkumati,
Ea mano amola egoa da ema hahawane nodosa.
29 “Pali akazi ambiri amene achita zinthu zopambana koma iwe umawaposa onsewa.”
Egoa da ema amane sia: sa, “Uda oda da noga: i, be dia hou da uda huluane ilia hou baligidafa.”
30 Nkhope yachikoka ndi yonyenga, ndipo kukongola nʼkosakhalitsa; koma mkazi amene amaopa Yehova ayenera kutamandidwa.
Uda mogili da ogogole obebenale hamosa. Amola noga: iwane ba: su hou da fisi dagoi ba: mu. Be nowa uda da Hina Gode Ea hou ida: iwane dafawaneyale dawa: sea, amo udama nodomu da defea.
31 Mupatseni mphotho chifukwa cha zimene iye wachita ndipo ntchito zake zimutamande ku mabwalo.
Amaiwane uda da noga: le hamoiba: le, e da dabe ea hamoi defele lamu da defea. Amola dunu huluane ema nodomu da defea. Sia: Ama Dagoi