< Miyambo 30 >
1 Nawa mawu a Aguri mwana wa Yake wa ku Masa: Munthuyo anati kwa Itieli, “Inu Mulungu, ine ndatopa. Inu Mulungu, ine ndatopa. Ndalefukiratu.
Goe da gogolole sia: su A: ige (Ya: ige egefe) da amane sia: i, “Gode da namagai hame! Gode da namagai hame! Na da gasa hame hahani galebe.
2 “Ine ndine munthu wopusa kuposa anthu onse; ndilibe nzeru zomvetsa zinthu zonga za munthu.
Na da dunu agoai hame. Na da ohe agoai esala. Dunu da dawa: su noga: iwane dialumu da defea. Be na da agoaiwane dawa: su da hame galebe.
3 Sindinaphunzire nzeru, ndipo Woyerayo sindimudziwa.
Na da bagade dawa: su hamedafa lai amola na da Gode ea hou hamedafa dawa:
4 Kodi ndani anakwera kumwamba ndi kutsikako? Ndani anafumbatapo mphepo mʼmanja mwake? Ndani anamanga madzi mʼchovala chake? Ndani anakhazikitsa mathero onse a dziko lapansi? Dzina lake ndani? Ndiwuze ngati ukudziwa! Ndipo mwana wake dzina lake ndani?
Nowa da Hebene hou huluane dawa: bela: ? Nowa da fo ea loboga gagubala: ? Amola nowa da abula gadelaiga hano gadoba: bela: ? Amola osobo bagade ea bega: huluane da nowa ea alalo ilegebela: ? Amola dia dawa: loba, e da nowala: ? Amola e da nowa ea manola: ?
5 “Mawu ali wonse a Mulungu ndi opanda cholakwika; Iye ndi chishango kwa amene amathawira kwa Iye.
Gode E da Ea moloidafa hou hamomu ilegele sia: i, E da dafawane hamomu. Amola, E da Gaga: sudafa, amola nowa dunu da E hogoi helesea, amo dunu da gaga: su ba: mu.
6 Usawonjezepo kanthu pa mawu ake, kuopa kuti Iye angadzakudzudzule ndi kukupeza kuti ndiwe wabodza.”
Gode Ea sia: dafa amoga dia hanai sia: mae gilisima. Di da amane hamosea, E da dima gagabomu, amola eno dunu dawa: ma: ne Gode da di da ogogole olelesu dunu olelemu.”
7 “Inu Yehova, ndikukupemphani zinthu ziwiri musandimane zimenezo ndisanafe:
Na da Dima adole ba: sa, “Gode! Na da liligi aduna Dima lalalu bogomu da defea.
8 Choyamba, mundichotsere kutali nane mabodza ndi chinyengo. Chachiwiri, ndisakhale mʼmphawi kapena munthu wachuma. Koma muzindidyetsa chakudya chondikwanira tsiku ndi tsiku
Na ogogolalosa: besa: le, na Dia fidima. Na bagade gagui agoai esalosa: besa: le o hamedafa gagui agoai esalosa: besa: le, Dia na fidima. Amaiba: le, ha: i manu na dafawane esaloma: ne lamu liligi defele nama ima.
9 kuopa kuti ndikakhuta kwambiri ndingayambe kukukanani, nʼkumanena kuti, ‘Yehova ndiye yaninso?’ Kuopanso kuti ndikakhala wosauka ndingayambe kuba, potero nʼkuyipitsa dzina la Mulungu wanga.”
Na da Di gogolesa: besa: le, liligi bagadedafa nama mae ima. Amola na da liligi hamedafa gaguiba: le, wamolasa: besa: le amola Dia Dio wadela: sa: besa: le, liligi fonobahadi nama ima.
10 “Usamusinjirire wantchito kwa mbuye wake kuopa kuti angakutemberere ndipo iweyo nʼkupezeka wolakwa.”
Di da hawa: hamosu dunu amo ea hou ea hina dunuma baligidu sia: mae sia: ma. Amane hamosea, hawa: hamosu dunu da dima gagabumu, amola dia hamoi defele, di da se nabimu.
11 “Alipo ena amene amatemberera abambo awo, ndipo sadalitsa amayi awo.
Dunu oda ilia da eda se nabima: ne, gagabusa. Amola eme amoma nodone hame asigisa.
12 Pali ena amene amadziyesa okha oyera mtima komatu sanachotse zoyipa zawo.
Dunu oda ilia da amane dawa: sa, ilisu ilia da moloiwaneyale dawa: sa. Be ilia da ledodafa gala.
13 Pali ena ndi odzitukumula kwambiri, amene amakweza zikope modzitukumula.
Goe da dunu eno ilia da amane dawa: su, ilia da ili da moloiwaneyale dawa: su. Dafawane! Ilia da ilisu noga: iwaneyale dawa: sa.
14 Pali ena amene mano awo ali ngati malupanga ndipo zibwano zawo zili ngati mipeni moti amadya amphawi ndi kuwachotsa pa dziko lapansi. Amachotsanso anthu osauka pakati pa anzawo.”
Amola dunu oda da hame gagui dunu ilima bagadewane ogogosa amola wadela: lesimusa: dawa: sa. Ilia da amodili ilia esalusu ba: sa.
15 “Msundu uli ndi ana aakazi awiri iwo amalira kuti, ‘Tipatseni! Tipatseni!’” “Pali zinthu zitatu zimene sizikhuta, zinthu zinayi zimene sizinena kuti, ‘Takhuta!’
Hebe da idiwi aduna gala. Ela da dio afadafa gala, amo ‘Nama ima!’ Amola liligi biyaduyale amo ilia hanai da hame sadimu.
16 Manda, mkazi wosabala, nthaka yosakhuta madzi ndiponso moto womangoyakirayakira!” (Sheol )
Amo liligi biyaduyale gala da, (age) Bogoi uli dogoi da hame sadimu. (ageyadu) Aligime uda da hame sadimu. (osoda) Hafoga: i osobo gibu hameba: le da hame sadimu. (biyadu) Amola lalu haba: domu gogolei amo da hame sadimu. (Sheol )
17 Aliyense amene amanyoza abambo ake, ndi kunyozera kumvera amayi ake, makwangwala a ku chigwa adzamukolowola maso ndipo mphungu zidzadya mnofu wake.
Nowa da eda amoma lasogole ofesega: sea, o ea eme ea da: i hamoi eso amoga ema higale ba: sea, sia misini ea da: i hodo manu da defea, amola soge buhiba amo ea si duga: mu da defea.
18 Pali zinthu zitatu zimene zimandidabwitsa, zinthu zinayi zimene ine sindizimvetsetsa.
Eno liligi biyaduyale gala amo na dawa: mu gogolei.
19 Ndipo ndi izi: mmene chiwulukira chiwombankhanga mlengalenga; mmene iyendera njoka pa thanthwe; mmene chiyendera chombo pa nyanja; ndiponso mmene mwamuna achitira akakhala ndi namwali.
Goe da wayalima muagadodafa hagili ahoa. Sania da gele da: iya sugi ahoana. Eno da dusagai hano wayabo amo ganodini masusa: logo hogolala. Dunu amola uda ela lamusa: magedaha.
20 Umu ndi mʼmene mkazi amachitira atachita chigololo: Atatha kudya ndi kupukuta pakamwa pake iye amanena kuti “Sindinachite kalikonse kolakwa.”
Goe da uda amo da egoama baligi fa: su, amo ea hou da agoaiwane gala. E da inia dunu adole lale, ha: i nanu, ea lafi dagale, amane sia: sa, “Na da wadela: le hame hamoi.”
21 Pali zinthu zitatu zimene zimanjenjemeretsa dziko lapansi, pali zinthu zinayi zimene dziko lapansi silingathe kuzipirira:
Liligi biyaduyale gala da wadela: idafaba: le, fedege agoane, osobo bagade da amo liligi biyaduyale gala higasa.
22 Kapolo amene wasanduka mfumu, chitsiru chimene chakhuta,
(age) Udigili hawa: hamosu dunu e da hina bagade hamosa. (ageyadu) Gagaousu dunu da ha: i manu bagade nawene sadisa.
23 mkazi wonyozeka akakwatiwa ndiponso wantchito wamkazi akalanda mwamuna wa mbuye wake.
(osoda) Wadela: idafa uda amo da gawa fisa. (biyadu) Hawa: hamosu uda da ea hina uda amo ea sogebi samogene lasa.
24 Pali zinthu zinayi zingʼonozingʼono pa dziko lapansi, komatu ndi zochenjera kwambiri:
Osobo bagadega da ohe fonobahadidafa biyaduyale gala. Amo ohe amo da baligili bagadedafa dawa: su gala.
25 Nyerere zili ngati anthu opanda mphamvu, komatu zimasungiratu chakudya chake nthawi ya chilimwe;
(age) Gedama! Amo da liligi fonobahadi amola gasa hame. Be amomane ilia da mugi oubiga ha: i manu momagesa.
26 mbira zili ngati anthu opanda mphamvu komatu zimakonza pokhalapo pawo mʼmiyala;
(ageyadu) Amola wasigiba ea hou dawa: ma. E da gasa hame be amomane e da diasu igi adoba gagusa.
27 dzombe lilibe mfumu, komatu lonse limakhala mʼmagulumagulu poyenda.
(osoda) Amola danuba: dawa: ma. Ilia da hina hame, amomane ilia da gilisili hagili mogodigili ahoa.
28 Buluzi ungathe kumugwira mʼmanja komatu amapezeka mʼnyumba za mafumu.
(biyadu) Amola goma: fi ilia hou dawa: ma. Amo da liligi fonobahadi amola dia da lobo afaega gagumusa: dawa: Be ilia da hina bagade ea diasu noga: i amo ganodini esalebe ba: sa.
29 “Pali zinthu zitatu zimene zimayenda chinyachinya, pali zinthu zinayi zimene zimayenda monyadira:
Liligi biyaduyale gala ilia ahoabe hou di ba: sea, noga: iwane ba: sa.
30 Mkango umene uli wamphamvu kuposa nyama zonse, ndipo suthawa kanthu kalikonse.
Amo liligi biyaduyale gala da (age) Laione wa: me e da gasa bagade amola ohe enoga e baligimu da hamedei. Amola e da ohe enoba: le hame beda: sa.
31 Tambala woyenda chinyachinya, mbuzi yayimuna, ndiponso mfumu yoyenda pakati pa anthu ake.
(ageyadu) Goudi (osoda) Gagala gawali amo ilia da dada: lole ahoa, amola (biyadu) Hina bagade dunu ilia da ilia dunu fi ilia midadi ahoa.
32 “Ngati wakhala ukupusa ndi kumadzikweza wekha, kapena ngati wakhala ukukonzekera zoyipa, ndiye khala kaye chete, uganizire bwino!
Amola di da gagousu dunu agoai, gasa fi hou hamosea, amola wadela: i hou hamomusa: dawa: sea, yolesima amola dawa: ma.
33 Paja pakutha mkaka mafuta amapangidwa, ndipo ukapsinya mphuno, magazi amatuluka, ndipo mikangano imakhalapo ukalimbikira kukwiya.”
Amola dia ohe amo ea dodo maga: me biogosea, amo da bu sefe hamomu. Amola dia eno ea mia fasea, heale masunu. Amola dia da nenege degesea, se nabasu da dima doaga: mu.