< Miyambo 29 >

1 Munthu amene amawumitsabe khosi lake atadzudzulidwa kwambiri, adzawonongeka mwadzidzidzi popanda chomuchiritsa.
Joka kuritukselle on uppiniskainen, hän äkisti kadotetaan ilman yhdetäkään avuta.
2 Anthu olungama akamalamulira mʼdziko anthu amakondwa, koma ngati dziko lilamulidwa ndi anthu oyipa mtima anthu amadandaula.
Kuin vanhurskaita monta on, niin kansa iloitsee; vaan kuin jumalatoin hallitsee, niin kansa huokaa.
3 Munthu amene amakonda nzeru amasangalatsa abambo ake, koma woyenda ndi akazi achiwerewere amasakaza chuma chake.
Joka viisautta rakastaa, hän iloittaa isänsä; mutta joka huoria elättää, hän tuhlaa tavaraansa.
4 Mfumu imalimbitsa dziko poweruza mwachilungamo, koma mfumu imene imawumiriza anthu kuti ayipatse mphatso imawononga dziko.
Kuningas rakentaa oikeudella valtakunnan; vaan lahjain ottaja sen turmelee.
5 Munthu woshashalika mnzake, akudziyalira ukonde mapazi ake.
Joka lähimmäisensä kanssa liehakoitsee, hän hajoittaa verkon jalkainsa eteen.
6 Munthu woyipa amakodwa ndi machimo ake, koma wochita chilungamo amayimba lokoma.
Kuin paha syntiä tekee, niin hän hänensä paulaan sekoittaa; vaan vanhurskas riemuitsee, ja hänellä on ilo.
7 Munthu wolungama amasamalira anthu osauka, koma woyipa salabadira zimenezi.
Vanhurskas tuntee köyhän asian; vaan jumalatoin ei ymmärrä viisautta.
8 Anthu onyoza atha kuwutsa ziwawa mu mzinda, koma anthu anzeru amaletsa ukali.
Pilkkaajat hajoittavat kaupungin; vaan viisaat asettavat vihan.
9 Ngati munthu wanzeru atsutsana ndi chitsiru, chitsirucho chimachita phokoso ndi kumangoseka ndipo sipakhala mtendere.
Kuin viisas tulee tyhmän kanssa oikeutta käymään, joko hän on vihainen eli iloinen, niin ei ole hänellä yhtään lepoa.
10 Anthu okhetsa magazi amadana ndi munthu wangwiro koma anthu olungama amasamalira moyo wake.
Verikoirat vihaavat siviää; vaan vanhurskaat holhovat häntä.
11 Munthu wopusa amaonetsa mkwiyo wake, koma munthu wanzeru amadzigwira.
Tyhmä vuodattaa kaiken henkensä; vaan viisas sen pidättää.
12 Ngati wolamulira amvera zabodza, akuluakulu ake onse adzakhala oyipa.
Päämies, joka valhetta rakastaa, hänen palveliansa ovat kaikki jumalattomat.
13 Munthu wosauka ndi munthu wopondereza anzake amafanana pa kuti: Yehova ndiye anawapatsa maso onsewa.
Köyhä ja rikas kohtasivat toinen toisensa: Herra valaisee heidän molempain silmänsä.
14 Ngati mfumu iweruza osauka moyenera, mpando wake waufumu udzakhazikika nthawi zonse.
Kuningas, joka uskollisesti tuomitsee köyhiä, hänen istuimensa vahvistetaan ijankaikkisesti.
15 Ndodo ndi chidzudzulo zimapatsa nzeru koma mwana womulekerera amachititsa amayi ake manyazi.
Vitsa ja rangaistus antaa viisauden; vaan itsevaltainen lapsi häpäisee äitinsä.
16 Oyipa akamalamulira zoyipa zimachuluka, koma anthu olungama adzaona kugwa kwa anthu oyipawo.
Jossa monta jumalatointa on, siinä on monta syntiä; vaan vanhurskaat näkevät heidän lankeemisensa.
17 Umulange mwana wako ndipo adzakupatsa mtendere ndi kusangalatsa mtima wako.
Kurita poikaas, niin hän sinua virvoitaa, ja saattaa sielus iloiseksi.
18 Ngati uthenga wochokera kwa Yehova supezeka anthu amangochita zofuna zawo; koma wodala ndi amene amasunga malamulo.
Kuin ennustukset loppuvat, niin kansa hajoitetaan; vaan autuas kätkee lain.
19 Munthu wantchito sangalangizidwe ndi mawu okha basi; ngakhale awamvetse mawuwo sadzatha kuchitapo kanthu.
Palvelia ei anna itsiänsä kurittaa sanoilla; sillä vaikka hän sen ymmärtää, niin ei hän vastaa.
20 Ngakhale munthu wa uchitsiru nʼkuti ndiponi popeza chikhulupiriro chilipo kuposa munthu wodziyesa yekha kuti ndi wanzeru poyankhula.
Jos sinä näet jonkun, joka on nopsa puhumaan: enempi on toivoa tyhmästä kuin hänestä.
21 Ngati munthu asasatitsa wantchito wake kuyambira ali mwana, potsirizira adzapeza kuti wantchitoyo wasanduka mlowachuma wake.
Jos palvelia nuoruudesta herkullisesti pidetään, niin hän tahtoo sitte poikana olla.
22 Munthu wamkwiyo amayambitsa mikangano, ndipo munthu waukali amachita zolakwa zambiri.
Vihainen mies saattaa riidan, ja kiukkuinen tekee monta syntiä.
23 Kunyada kwa munthu kudzamutsitsa, koma munthu wodzichepetsa amalandira ulemu.
Ylpeys kukistaa ihmisen; vaan kunnia korottaa nöyrän.
24 Woyenda ndi munthu wakuba ndi mdani wa moyo wake womwe; amalumbira koma osawulula kanthu.
Joka varkaan kanssa on osallinen, hän vihaa sieluansa, niin myös se, joka kuulee kirouksen ja ei ilmoita.
25 Kuopa munthu kudzakhala ngati msampha, koma aliyense amene amadalira Yehova adzatetezedwa.
Joka pelkää ihmistä, hän tulee lankeemukseen; mutta joka luottaa Herraan, hän tulee pidetyksi ylös.
26 Anthu ambiri amafunitsitsa kuti wolamulira awakomere mtima, koma munthu amaweruzidwa mwachilungamo ndi thandizo la Yehova basi.
Moni etsii päämiehenkasvoja; mutta jokaisen tuomio tulee Herralta.
27 Anthu olungama amanyansidwa ndi anthu achinyengo; koma anthu oyipa amanyansidwa ndi anthu a mtima wowongoka.
Jumalatoin ihminen on vanhurskaille kauhistus; ja joka oikialla tiellä on, hän on jumalattomalle kauhistus.

< Miyambo 29 >