< Miyambo 27 >

1 Usamanyadire za mawa, pakuti sudziwa zimene zidzachitike pa tsikulo.
MAI olioli wale oe no ka la apopo, No ka mea, aole oe i ike i ka mea a kekahi la e hoopuka mai ai.
2 Munthu wina akutamande, koma osati wekha; mlendo akakutamanda, ndiponi koma osati ndi pakamwa pako.
Na ka mea e e hoomaikai mai ia oe, aole na kou waha iho; Na ka malihini hoi, aole na kou mau lehelehe iho.
3 Mwala ndi wolemera ndipo mchenganso ndi wolemera kwambiri, koma makani a chitsiru ndi oposa zonsezo kulemera kwake.
Koikoi ka pohaku, kaumaha hoi ke one; Aka, o ka inaina o ka mea naaupo, ua kaumaha ia mamua o ia mau mea elua.
4 Mkwiyo umadzetsa nkhanza ndipo kupsa mtima kumachititsa zoopsa. Koma nsanje imachita zoopsa zopambana.
He aloha ole ka inaina, he mea make ka huhu, Owai la hoi e hiki ke ku imua o ka huahua?
5 Kudzudzula munthu poyera nʼkwabwino kuposa chikondi chobisika.
Maikai ke ao maopopo ana, Mamua o ke aloha i hunaia.
6 Munthu amene amakukonda ngakhale akupweteke zili bwino, koma mdani wako amakupsompsona mwachinyengo.
Maikai ka hoehaia mai e ka hoaaloha, He nunui hoi ka honi ana o ka enemi.
7 Iye amene wakhuta amayipidwa ndi chisa cha uchi, koma kwa munthu wanjala ngakhale chimene chili chowawa chimamukomera.
Hehi no ka mea maona i ka waihona meli; Aka, i ka mea pololi la, ua ono na mea awaawa a pau.
8 Munthu amene wasochera ku nyumba kwake, ali monga mbalame imene yasochera pa chisa chake.
E like me ka manu i auwana ae mai kona punana aku, Pela ke kanaka e auwana ana mai kona wahi aku.
9 Mafuta ndi zonunkhira zimasangalatsa mtima, ndipo kukoma mtima kwa bwenzi kwagona pa malangizo ake.
O ka aila a me ka mea ala, hoohauoli ia i ka naau; Hooluolu hoi ka hoaaloha o kekahi mea ma ka olelo oiaio.
10 Usasiye bwenzi lako ndiponso bwenzi la abambo ako, ndipo usapite ku nyumba ya mʼbale wako pamene wakumana ndi mavuto; mnzako wokhala naye pafupi amaposa mʼbale wako wokhala kutali.
O kou hoalauna a me ka hoalauna o kou makuakane, mai haalele oe; Aole hoi e komo aku i ka hale o kou hoahanau i kou manawa popilikia; Maikai ka mea e noho kokoke ana, mamua o ka hoahanau ma kahi loihi aku.
11 Mwana wanga, khala wanzeru, ndipo ukondweretse mtima wanga; pamenepo ine ndidzatha kuyankha aliyense amene amandinyoza.
E kuu keiki e, e naauao hoi oe i olioli ko'u naau, I olelo aku au i ka mea hoino mai ia'u.
12 Munthu wochenjera akaona choopsa amabisala, koma munthu wopusa amangopitirira ndipo amakumana ndi mavuto.
O ka mea noonoo la, ike e oia mamua i ka poino a huna ia ia iho; Hele wale aku hoi ka poe nanea a hihia iho la.
13 Utenge chovala cha munthu amene waperekera mlendo chikole; ngati chigwiriro chifukwa waperekera chikole mlendo wosadziwika.
E lawe i ka aahu o ka mea nana e hoopanai no ka malihini, E lawe hoi i uku nona no ka wahine e.
14 Ngati munthu apatsa mnzake moni mofuwula mmamawa kwambiri, anthu adzamuyesa kuti akutemberera.
O ka mea hoomaikai aku i kona hoanoho me ka leo nui, I kona ala ana i ke kakahiaka nui, E lilo ia i mea poino nona.
15 Mkazi wolongolola ali ngati mvula yamvumbi.
O ke kulu mau ana i ka la ua, A me ka wahine nuku wale, na like.
16 Kumuletsa mkazi wotereyu zimenezi zili ngati kuletsa mphepo kapena kufumbata mafuta mʼdzanja.
O ka mea hoonalowale i kana, hoonalowale no ia i ka makani, A me ka aila o kona lima akau e pa mai ana.
17 Chitsulo chimanoledwa ndi chitsulo chinzake, chomwechonso munthu amanoledwa ndi munthu mnzake.
Hookala kahi mea hao i kekahi mea hao, Hookala hoi ke kanaka i ka maka o kona hoalauna.
18 Amene amasamalira mtengo wamkuyu adzadya zipatso zake, ndipo iye amene amasamalira mbuye wake adzalandira ulemu.
O ka mea malama i ka laau fiku, oia ke ai i kona hua; O ka mea malama hoi i kona haku e hoonaniia oia.
19 Monga momwe nkhope imaonekera mʼmadzi, chomwechonso mtima wa munthu umadziwika ndi ntchito zake.
Ma ka wai, he helehelena e ku ana i kahi helehelena, Pela hoi ka naau kanaka i kekahi kanaka.
20 Manda sakhuta, nawonso maso a munthu sakhuta. (Sheol h7585)
O ka lua a me ka hohonu, aole i piha, A o na maka o ke kanaka aole no e maona. (Sheol h7585)
21 Siliva amasungunulira mu uvuni ndipo golide mʼngʼanjo, chomwechonso munthu amadziwika ndi zomwe akudzitamandira nazo.
He ipu hoohehee no ke kala, a he kapuahi no ke gula, Pela ke kanaka imua o kona mahaloia mai.
22 Ngakhale utakonola chitsiru mu mtondo ndi musi ngati chimanga, uchitsiru wakewo sudzachoka.
Ina e kui oe i ka mea naaupo ma ka papawiliai, Oia pu me ka ai i ka pohaku kui, Aole loa e hemo ae kona naaupo ana mai ona aku.
23 Uzidziwe bwino nkhosa zako momwe zilili. Kodi usamalire bwino ziweto zako?
E ike pono oe i ke ano o kau poe hipa, E nana hoi i ke ano o kau poe holoholona;
24 Paja chuma sichikhala mpaka muyaya, ndipo ufumu sukhala mpaka mibado yonse.
No ka mea, aole e mau ana ka waiwai: O ka papale alii hoi, oia mau anei ia i na hanauna a pau?
25 Pamene udzu watha, msipu nʼkumera; ndipo atatuta udzu wa ku mapiri,
Kupu mai ka weuweu, ikea mai ka mauu, A e ohiia ana ka mea ulu o ka mauna.
26 ana ankhosa adzakupatsani chovala ndipo pogulitsa mbuzi mudzapeza ndalama yogulira munda.
O na keikihipa no kou kapa komo, O ka poe kao kane ke kumukuai no ka aina.
27 Mudzakhala ndi mkaka wambuzi wambiri kuti muzidya inuyo ndi banja lanu ndi kudyetsa antchito anu aakazi.
A e nui ka waiu kao no kau ai ana, No ka ai ana hoi o ko ka hale ou, A he ola no kou poe kauwawahine.

< Miyambo 27 >