< Miyambo 23 >

1 Ngati ukhala pansi kuti udye pamodzi ndi wolamulira, uyangʼane bwino zimene zili pamaso pako,
Katta ǝrbab bilǝn ⱨǝmdastihan bolsang, Aldingdiki kim ikǝnlikini obdan oylan.
2 ngati ndiwe munthu wadyera udziletse kuti usaonetse dyera lakolo.
Ixtiying yaman bolsa, Gelingƣa piqaⱪ tǝnglǝp turƣandǝk ɵzüngni tart.
3 Usasirire zakudya zake, pakuti zimenezo ndi zakudya zachinyengo.
Uning nazunemǝtlirini tama ⱪilma, Ular adǝm aldaydiƣan tamaⱪlardur.
4 Usadzitopetse wekha ndi kufuna chuma, ukhale ndi nzeru ya kudziretsa.
Bay bolimǝn dǝp ɵzüngni upratma; Ɵzüngning zeⱨningni bu ixⱪa ⱪaratma.
5 Ukangoti wachipeza chumacho uwona posachedwa kuti palibepo. Chumacho chimachita ngati chamera mapiko mwadzidzidzi ndi kuwuluka kunka kumwamba ngati chiwombankhanga.
[Bayliⱪlarƣa] kɵz tikixing bilǝnla, ular yoⱪ bolidu; Pul-mal dǝrwǝⱪǝ ɵzigǝ ⱪanat yasap, Huddi bürküttǝk asmanƣa uqup ketǝr.
6 Usadye chakudya cha munthu waumbombo, usalakalake zakudya zake zokoma;
Aq kɵzning nenini yemǝ, Uning esil nazunemǝtlirini tama ⱪilma;
7 paja iye ndi munthu amene nthawi zonse amaganizira za mtengo wake ngakhale amati kwa iwe, “Idya ndi kumwa,” koma sakondweretsedwa nawe.
Qünki uning kɵngli ⱪandaⱪ bolƣandǝk, ɵzimu xundaⱪ. U aƣzida: — Ⱪeni, alsila, iqsilǝ! — desimu, Biraⱪ kɵnglidǝ seni oyliƣini yoⱪ.
8 Udzasanza zimene wadyazo ndipo mawu ako woyamikira adzapita pachabe.
Yegǝn bir yutum taamnimu ⱪusuwetisǝn, Uningƣa ⱪilƣan qirayliⱪ sɵzliringmu bikarƣa kǝtkǝn bolidu.
9 Usayankhule munthu wopusa akumva, pakuti adzanyoza mawu ako anzeru.
Əhmǝⱪⱪǝ yol kɵrsitip salma, Qünki u ǝⱪil sɵzliringni kɵzgǝ ilmas.
10 Usasunthe mwala wa mʼmalire akalekale kapena kulowerera mʼminda ya ana amasiye,
Ⱪǝdimdǝ bekitkǝn yǝrning pasil taxlirini yɵtkimǝ, Yetimlarning etizliriƣimu ayaƣ basma;
11 paja Mpulumutsi wawo ndi wamphamvu; iye adzawateteza pa milandu yawo kutsutsana nawe.
Qünki ularning Ⱨǝmjǝmǝt-Ⱪutⱪuzƣuqisi intayin küqlüktur; U Ɵzi ular üqün üstüngdin dǝwa ⱪilar.
12 Mtima wako uzikhala pa malangizo ndipo makutu ako azimvetsera mawu a chidziwitso.
Nǝsiⱨǝtkǝ kɵngül ⱪoy, Ilim-bilimlǝrgǝ ⱪulaⱪ sal.
13 Usaleke kumulangiza mwana; ngati umulanga ndi chikwapu sadzafa.
Balangƣa tǝrbiyǝ berixtin erinmǝ; Əgǝr tayaⱪ bilǝn ursang, u ɵlüp kǝtmǝydu;
14 Ukamukwapula ndi tsatsa udzapulumutsa moyo wake. (Sheol h7585)
Sǝn uni tayaⱪ bilǝn ursang, Bǝlkim uni tǝⱨtisaradin ⱪutⱪuziwalisǝn. (Sheol h7585)
15 Mwana wanga, ngati mtima wako ukhala wanzeru, inenso mtima wanga udzakondwera.
I oƣlum, dana bolsang, Mening ⱪǝlbim ⱪanqǝ hux bolar idi!
16 Mtima wanga udzakondwera pamene ndidzakumva ukuyankhula zolungama.
Aƣzingda orunluⱪ sɵzlǝr bolsa, iq-iqimdin xadlinimǝn.
17 Mtima wako usachite nsanje ndi anthu ochimwa, koma uziopa Yehova tsiku ndi tsiku.
Gunaⱨ sadir ⱪilƣuqilarƣa rǝxk ⱪilma, Ⱨǝrdaim Pǝrwǝrdigardin ǝyminixtǝ turƣin;
18 Ndithu za mʼtsogolo zilipo ndipo chiyembekezo chakocho sichidzalephereka.
Xundaⱪ ⱪilƣiningda jǝzmǝn kɵridiƣan yahxi kününg bolidu, Arzu-ümiding bikarƣa kǝtmǝs.
19 Tamvera mwana wanga, ndipo ukhale wanzeru, mtima wako uwuyendetse mʼnjira yabwino.
I oƣlum, sɵzümgǝ ⱪulaⱪ selip dana bol, Ⱪǝlbingni [Hudaning] yoliƣa baxliƣin.
20 Usakhale pakati pa anthu amene amaledzera kapena pakati pa anthu amene amadya nyama mwadyera.
Mǝyhorlarƣa arilaxma, Nǝpsi yaman gɵxhorlar bilǝn bardi-kǝldi ⱪilma;
21 Paja anthu oledzera ndi adyera amadzakhala amphawi ndipo aulesi adzavala sanza.
Qünki ⱨaraⱪkǝx bilǝn nǝpsi yaman ahirida yoⱪsulluⱪta ⱪalar, Ƣǝplǝt uyⱪusiƣa patⱪanlarƣa jǝndǝ kiyimni kiygüzǝr.
22 Mvera abambo ako amene anakubala, usanyoze amayi ako pamene akalamba.
Seni tapⱪan atangning sɵzini angla, Anang ⱪeriƣanda uningƣa ⱨɵrmǝtsizlik ⱪilma.
23 Gula choonadi ndipo usachigulitse; ugulenso nzeru, mwambo ndiponso kumvetsa zinthu bwino.
Ⱨǝⱪiⱪǝtni setiwal, Uni ⱨǝrgiz setiwǝtmǝ. Danaliⱪ, tǝrbiyǝ wǝ yorutuluxnimu al.
24 Abambo a munthu wolungama ali ndi chimwemwe chachikulu; Wobala mwana wanzeru adzakondwera naye.
Ⱨǝⱪⱪaniy balining atisi qong huxalliⱪ tapar; Dana oƣulni tapⱪan atisi uningdin hursǝn bolar.
25 Abambo ndi amayi ako asangalale; amene anakubereka akondwere!
Ata-anangni sɵyündürüp, Seni tuƣⱪan anangni hux ⱪil.
26 Mwana wanga, undikhulupirire ndipo maso ako apenyetsetse njira zanga.
I oƣlum, ⱪǝlbingni manga tapxur; Kɵzliringmu ⱨayatliⱪ yollirimƣa tikilsun!
27 Paja mkazi wachiwerewere ali ngati dzenje lozama; ndipo mkazi woyendayenda ali ngati chitsime chopapatiza.
Qünki paⱨixǝ ayal qongⱪur oridur, Buzuⱪ yat ayal tar zindandur;
28 Amabisala ngati mbala yachifwamba, ndipo amuna amakhala osakhulupirika chifukwa cha iyeyu.
Ular ⱪaraⱪqidǝk mɵküwelip, Insaniyǝt arisidiki wapasizlarni kɵpǝytǝr.
29 Ndani ali ndi tsoka? Ndani ali ndi chisoni? Ndani ali pa mkangano? Ndani ali ndi madandawulo? Ndani ali ndi zipsera zosadziwika uko zachokera? Ndani ali ndi maso ofiira?
Kimdǝ azab bar? Kimdǝ dǝrd-ǝlǝm? Kim jedǝl iqidǝ ⱪalar? Kim nalǝ-pǝryad kɵtürǝr? Kim sǝwǝbsiz yarilinar? Kimning kɵzi ⱪizirip ketǝr?
30 Ndi amene amakhalitsa pa mowa, amene amapita nalawa vinyo osakanizidwa.
Dǝl xarab üstidǝ uzun olturƣan, Əbjǝx xarabtin tetixⱪa aldiriƣan mǝyhorlar!
31 Usatengeke mtima ndi kufiira kwa vinyo, pamene akuwira mʼchikho pamene akumweka bwino!
Xarabning ajayib ⱪizilliⱪiƣa, uning jamdiki julaliⱪiƣa, Kixining gelidin xundaⱪ siliⱪ ɵtkǝnlikigǝ mǝptun bolup ⱪalma!
32 Potsiriza pake amaluma ngati njoka, ndipo amajompha ngati mphiri.
Ahirida u zǝⱨǝrlik yilandǝk qeⱪiwalidu, Oⱪ yilandǝk nǝxtirini sanjiydu.
33 Maso ako adzaona zinthu zachilendo ndipo maganizo ndi mawu ako adzakhala osokonekera.
Kɵz aldingda ƣǝlitǝ mǝnzirilǝr kɵrünidu, Aƣzingdin ⱪalaymiⱪan sɵzlǝr qiⱪidu.
34 Udzakhala ngati munthu amene ali gone pakati pa nyanja, kapena ngati munthu wogona pa msonga ya mlongoti ya ngalawa.
Huddi dengiz-okyanlarda lǝylǝp ⱪalƣandǝk, Yǝlkǝnlik kemining moma yaƣiqi üstidǝ yatⱪandǝk bolisǝn.
35 Iwe udzanena kuti, “Anandimenya, koma sindinapwetekedwe! Andimenya koma sindinamve kanthu! Kodi ndidzuka nthawi yanji? Ndiye ndifunefunenso vinyo wina.”
Sǝn qoⱪum: — Birsi meni urdi, lekin mǝn yarilanmidim! Birsi meni tayaⱪ bilǝn urdi, biraⱪ aƣriⱪini sǝzmidim!» — dǝysǝn. Biraⱪ sǝn yǝnǝ: «Ⱨoxumƣa kǝlsǝmla, mǝn yǝnila xarabni izdǝymǝn! — dǝysǝn.

< Miyambo 23 >