< Miyambo 2 >
1 Mwana wanga, ngati ulandira mawu anga ndi kusunga malamulo anga mu mtima mwako,
Tulik nutik, lutlut ke ma nga luti nu sum, ac tia mulkunla ma nga fahk kom in oru.
2 ndiponso kutchera khutu lako ku nzeru ndi kuyikapo mtima pa kumvetsa zinthu;
Lohng kas in lalmwetmet, ac srike kom in kalem kac.
3 ngati upempha kuti uzindikire zinthu inde kupempha ndi mtima wonse kuti ukhale womvetsa zinthu,
Aok, ngisre in oasr etauk lom, ac kwafe tuh kom in liyaten.
4 ngati ufunafuna nzeruyo ngati siliva ndi kuyisakasaka ngati chuma chobisika,
Suk aklohya, in oana ke kom ac suk silver ku kutu ma saok su oan wikla.
5 ndiye udzamvetsa bwino tanthauzo la kuopa Yehova; ndipo udzapezanso tanthauzo la kumudziwa Yehova.
Kom fin oru ouinge na kom fah etu lah mea kalmen sangeng sin LEUM GOD, ac konauk in etu ke God.
6 Pakuti Yehova ndiye amapereka nzeru, ndipo mʼkamwa mwake mumachokera chidziwitso ndi kumvetsa zinthu.
LEUM GOD pa ase lalmwetmet; etauk ac kalem tuku sel me.
7 Anthu olungama zinthu zimawayendera bwino chifukwa Yehova amakhala nawo. Paja Yehova ndiye chishango cha amene amayenda mwangwiro,
El sang kasru nu sin mwet suwohs, ac El karinganang mwet moul pwaye.
8 pakuti ndiye mlonda wa njira zolungama. Iye amasamala mayendedwe a anthu ake okhulupirika.
El karinganulos su oru wo nu sin mwet ngia, ac taranulos su inse pwaye nu sel.
9 Choncho udzamvetsa tanthauzo la ungwiro, chilungamo, kusakondera ndi njira iliyonse yabwino.
Kom fin porongeyu, kom ac etu ma pwaye, suwohs, ac wo. Na kom ac etu lah mea fal kom in oru.
10 Pakuti nzeru idzalowa mu mtima mwako, kudziwa zinthu kudzakusangalatsa.
Kom ac lalmwetmet, ac etauk lom ac fah mwe insewowo nu sum.
11 Kuganizira bwino za mʼtsogolo kudzakusunga; kumvetsa zinthu bwino kudzakuteteza.
Liyaten ac kalem lom ac loangekom —
12 Nzeru idzakupulumutsa ku mayendedwe oyipa, kwa anthu amabodza,
ac sruokkomi kom in tia oru ma sutuu. Ma inge ac fah srikomla liki mwet su purakak lokoalok ke kas lalos —
13 amene amasiya njira zolungama namayenda mʼnjira zamdima,
mwet su fahsr liki moul suwohs, ac som nu ke moul in lohsr,
14 amene amakondwera pochita zoyipa namasangalala ndi kuyipa kwa ntchito zawo zonyansa.
mwet su engan in oru ma koluk, ac insewowokin moul lusrongten ac sesuwos,
15 Amenewa ndi anthu a njira zawo zokhotakhota, ndipo makhalidwe awo ndi achinyengo.
mwet kutasrik su tia ku in lulalfongiyuk.
16 Nzeruyo idzakupulumutsanso kwa mkazi wachigololo; kwa mkazi wachilendo woyankhula moshashalika,
Kom ac fah ku in kaingkunla kutena mutan koluk su ac srike in srife kom ke kas emwem lal,
17 amene wasiya mwamuna wa chitsikana wake ndi kuyiwala pangano limene anachita pamaso pa Mulungu wake.
su tia pwaye nu sin mukul tumal, ac tia esam wuleang el oru ye mutun God.
18 Pakuti nyumba yake imatsetserekera ku imfa; njira zake zimamufikitsa ku manda.
Kom fin som nu lohm sel, kom fahsr nu ke inkanek in misa. Kom fin som nu we, kom suwoswos nu ke facl sin misa.
19 Opita kwa iye palibe ndi mmodzi yemwe amabwerera kapena kupezanso njira zamoyo.
Wangin sie mwet su utyak nu yorol nu foloko. El tiana foloko nu ke inkanek in moul.
20 Choncho iwe uziyenda mʼnjira za anthu abwino, uzitsata njira za anthu ochita chilungamo.
Ouinge kom in etai moul lun mwet wo, ac moulkin moul suwoswos.
21 Pakuti anthu olungama ndiwo ati adzakhale mʼdziko ndipo anthu angwiro ndiwo ati adzakhazikike mʼmenemo;
Mwet suwoswos — elos su pwaye in ma nukewa — ac fah muta in facl sesr uh.
22 Koma anthu oyipa adzachotsedwa mʼdzikomo, ndipo anthu onyenga adzachotsedwamo.
Tuh God El ac tulakunla mwet koluk uh liki acn uh, ac fusulosyak su orekma koluk.