< Miyambo 17 >

1 Nʼkwabwino kudya mkute koma pali mtendere, kuposa kuchita madyerero mʼnyumba mʼmene muli mikangano.
Май бине о букатэ де пыне ускатэ ку паче декыт о касэ плинэ де кэрнурь ку чартэ!
2 Kapolo wanzeru adzalamulira mwana wochititsa manyazi, ndipo kapoloyo adzagawana nawo cholowa ngati mmodzi mwa abale.
Ун аргат ку минте стэпынеште песте фиул каре фаче рушине ши ва ымпэрци моштениря ку фраций луй.
3 Siliva amamuyesa mʼngʼanjo ndipo golide amamuyesa mʼngʼanjo, koma Yehova amayesa mitima.
Тигая лэмуреште арӂинтул ши купторул лэмуреште аурул, дар Чел че ынчаркэ инимиле есте Домнул.
4 Munthu woyipa amamvera malangizo oyipa; munthu wabodza amatchera khutu mawu osakaza.
Чел рэу аскултэ ку луаре аминте ла буза нелеӂюитэ ши минчиносул плякэ урекя ла лимба нимичитоаре.
5 Iye amene amalalatira mʼmphawi amanyoza mlengi wake; amene amakondwerera tsoka la mnzake sadzakhala osalangidwa.
Чине ышь бате жок де сэрак ышь бате жок де Чел че л-а фэкут; чине се букурэ де о ненорочире ну ва рэмыне непедепсит.
6 Zidzukulu ndiye ulemu wa anthu okalamba, ndipo makolo ndiye ulemerero wa ana.
Копиий копиилор сунт кунуна бэтрынилор ши пэринций сунт слава копиилор лор.
7 Kuyankhula bwino sikuyenerana ndi chitsiru, nanji kuyankhula bodza kungayenerane kodi ndi mfumu?
Кувинтеле алесе ну се потривеск ын гура унуй небун; ку кыт май пуцин кувинтеле минчиноасе, ын гура унуй ом де вицэ алясэ!
8 Chiphuphu chili ngati mankhwala amwayi kwa wochiperekayo; kulikonse kumene amapita zinthu zimamuyendera.
Даруриле пар о пятрэ скумпэ ын окий челор че ле примеск: орьынкотро се ынторк, избындеск.
9 Iye amene amakhululukira zolakwa za wina, amafunitsitsa chikondi; wobwerezabwereza nkhani amapha chibwenzi.
Чине акоперэ о грешялэ каутэ драгостя, дар чине о поменеште мереу ын ворбириле луй дезбинэ пе приетень.
10 Munthu wanzeru amamva kamodzi kokha, munthu wopanda nzeru ndi samvamkunkhu.
О мустраре пэтрунде май мулт пе омул причепут декыт о сутэ де ловитурь пе чел небун.
11 Munthu woyipa maganizo ake ali pa kuwukira basi; ndipo bwana adzamutumizira wamthenga wankhanza.
Чел рэу ну каутэ декыт рэскоалэ, дар ун сол фэрэ милэ ва фи тримис ымпотрива луй.
12 Nʼkwabwino kukumana ndi chimbalangondo cholandidwa ana ake kusiyana ndi kukumana ndi chitsiru mu uchitsiru wake.
Май бине сэ ынтылнешть о урсоайкэ жефуитэ де пуий ей декыт ун небун ын тимпул небунией луй.
13 Ngati munthu abwezera choyipa kusinthana ndi zabwino, ndiye choyipa sichidzachoka mʼnyumba mwake.
Челуй че ынтоарче рэу пентру бине ну-й ва пэрэси рэул каса.
14 Chiyambi cha mikangano chili ngati kukhamulira madzi, choncho uzichokapo mkangano usanayambe.
Ынчепутул уней черте есте ка слобозиря унор апе; де ачея, курмэ чарта ынаинте де а се ынтеци.
15 Kumasula munthu wolakwa kapena kumanga munthu wosalakwa, zonse ziwirizi Yehova zimamunyansa.
Чел че яртэ пе виноват ши чел че осындеште пе чел невиноват сунт амындой о скырбэ ынаинтя Домнулуй.
16 Ndalama zogulira nzeru zili ndi phindu lanji mʼmanja mwa chitsiru poti iyeyo mutu wake sumayenda bwino?
Ла че служеште арӂинтул ын мына небунулуй? Сэ кумпере ынцелепчуня?… Дар н-аре минте!
17 Bwenzi lako limakukonda nthawi zonse, ndipo mʼbale wako anabadwa kuti azikuthandiza pamavuto.
Приетенул адевэрат юбеште орькынд ши ын ненорочире ажунӂе ка ун фрате.
18 Munthu wopanda nzeru amavomereza zopereka chikole ndipo iyeyo amasanduka chikole cha mnansi wake.
Омул фэрэ минте дэ кезэшие, се пуне кезаш пентру апроапеле сэу.
19 Wokonda zolakwa amakonda mkangano, ndipo wokonda kuyankhula zonyada amadziyitanira chiwonongeko.
Чине юбеште чертуриле юбеште пэкатул ши чине-шь зидеште поарта пря ыналтэ ышь каутэ пеиря.
20 Munthu wamtima woyipa zinthu sizimuyendera bwino; ndipo woyankhula zachinyengo amagwa mʼmavuto.
Чел ку инимэ префэкутэ ну гэсеште феричиря ши чел ку лимба стрикатэ каде ын ненорочире.
21 Mwana wopusa amamvetsa chisoni abambo ake, abambo a chitsiru sakhala ndi chimwemwe.
Чине дэ наштере унуй небун ва авя ынтристаре ши татэл унуй небун ну поате сэ се букуре.
22 Mtima wosangalala uli ngati mankhwala abwino, koma mtima wokhumudwa umafowoketsa mafupa.
О инимэ веселэ есте ун бун ляк, дар ун дух мыхнит усукэ оаселе.
23 Munthu woyipa amalandira chiphuphu chamseri kuti apotoze chiweruzo cholungama.
Чел рэу примеште дарурь пе аскунс ка сэ сучяскэ ши кэиле дрептэций.
24 Munthu wozindikira zinthu, maso ake amakhala pa nzeru, koma chitsiru chimwazamwaza maso ake pa dziko lonse lapansi.
Ынцелепчуня есте ын фаца омулуй причепут, дар окий небунулуй о каутэ ла капэтул пэмынтулуй.
25 Mwana wopusa amamvetsa chisoni abambo ake ndipo amapweteketsa mtima amayi ake.
Ун фиу небун адуче неказ татэлуй сэу ши амэрэчуне челей че л-а нэскут.
26 Sibwino kulipitsa munthu wosalakwa, kapena kulanga anthu osalakwa.
Ну есте бине сэ осындешть пе чел неприхэнит ла о глоабэ, нич сэ ловешть пе чей де ням алес дин причина неприхэнирий лор.
27 Munthu wosunga pakamwa ndiye wodziwa zinthu, ndipo wodekha mtima ndiye womvetsa bwino zinthu.
Чине ышь ынфрынязэ ворбеле куноаште штиинца ши чине аре духул потолит есте ун ом причепут.
28 Ngakhale chitsiru chimakhala ngati chanzeru chikakhala chete; ndipo chikatseka pakamwa chimakhala ngati munthu wochenjera.
Кяр ши ун прост ар трече де ынцелепт дакэ ар тэчя ши де причепут дакэ шь-ар цине гура.

< Miyambo 17 >