< Miyambo 17 >
1 Nʼkwabwino kudya mkute koma pali mtendere, kuposa kuchita madyerero mʼnyumba mʼmene muli mikangano.
Tuituknah hmueih im dongkah a bae lakah a ommongnah buhkak kamat te then.
2 Kapolo wanzeru adzalamulira mwana wochititsa manyazi, ndipo kapoloyo adzagawana nawo cholowa ngati mmodzi mwa abale.
Hlang aka cangbam sal loh hlang yah aka bai capa te a taemrhai vetih, pacaboeina taengah rho a tael ni.
3 Siliva amamuyesa mʼngʼanjo ndipo golide amamuyesa mʼngʼanjo, koma Yehova amayesa mitima.
Cak hamla cak am, sui hamla hmai-ulh om, tedae BOEIPA long tah lungbuei ni a. noem.
4 Munthu woyipa amamvera malangizo oyipa; munthu wabodza amatchera khutu mawu osakaza.
Thae aka huet loh boethae hmuilai kah a honghi te a hnatung tih, talnah ol te hna a kaeng thil.
5 Iye amene amalalatira mʼmphawi amanyoza mlengi wake; amene amakondwerera tsoka la mnzake sadzakhala osalangidwa.
Khodaeng aka tamdaeng tah amah aka saii kung ni a veet, rhainah soah ko aka hoe khaw hmil mahpawh.
6 Zidzukulu ndiye ulemu wa anthu okalamba, ndipo makolo ndiye ulemerero wa ana.
Ca rhoek kah a ca rhoek tah patong rhoek kah rhuisam la om tih a napa rhoek te khaw ca rhoek kah a boei a mang la om.
7 Kuyankhula bwino sikuyenerana ndi chitsiru, nanji kuyankhula bodza kungayenerane kodi ndi mfumu?
Hlangrhuel hmuilai he a ang ham a rhoeprhui moenih. A honghi kah hmuilai khaw hlangcong hamla koih loeng loeng van pawh.
8 Chiphuphu chili ngati mankhwala amwayi kwa wochiperekayo; kulikonse kumene amapita zinthu zimamuyendera.
Kapbaih he a kungmah kah mik ah lungto mikdaithen bangla boeih a hoilae tih a cangbam.
9 Iye amene amakhululukira zolakwa za wina, amafunitsitsa chikondi; wobwerezabwereza nkhani amapha chibwenzi.
Hlang kah dumlai aka dah loh lungnah a toem dae, olka dongah aka thovael loh a boeihlum khaw a paekboe sak.
10 Munthu wanzeru amamva kamodzi kokha, munthu wopanda nzeru ndi samvamkunkhu.
Aka ang voei yakhat n'ngawn lakah aka yakming ham tah tluungnah mah a tlaeh pah coeng.
11 Munthu woyipa maganizo ake ali pa kuwukira basi; ndipo bwana adzamutumizira wamthenga wankhanza.
Boekoek loh boethae bueng a tlap dae, anih taengah puencawn muenying muenyang ni a. tueih pa eh.
12 Nʼkwabwino kukumana ndi chimbalangondo cholandidwa ana ake kusiyana ndi kukumana ndi chitsiru mu uchitsiru wake.
Hlang kah a dueidah a laemhong sak vom neh ka hum uh palueng eh, aka ang kah a anglat nen tah ka hum uh boel eh.
13 Ngati munthu abwezera choyipa kusinthana ndi zabwino, ndiye choyipa sichidzachoka mʼnyumba mwake.
A then te thae la aka thuung tah a im lamkah a thae te nong rhoe nong mahpawh.
14 Chiyambi cha mikangano chili ngati kukhamulira madzi, choncho uzichokapo mkangano usanayambe.
Olpungkacan a tongnah tah tui a cae sak. Te dongah tuituknah a puek hlanah huu laeh.
15 Kumasula munthu wolakwa kapena kumanga munthu wosalakwa, zonse ziwirizi Yehova zimamunyansa.
Halang aka tang sak neh hlang dueng aka boe sak, amih rhoi bang te BOEIPA kah a tueilaehkoi ni.
16 Ndalama zogulira nzeru zili ndi phindu lanji mʼmanja mwa chitsiru poti iyeyo mutu wake sumayenda bwino?
Cueihnah lai ham hlang ang kut dongkah a phu te ba ham lae, a lungbuei neh a om hae moenih.
17 Bwenzi lako limakukonda nthawi zonse, ndipo mʼbale wako anabadwa kuti azikuthandiza pamavuto.
A tue boeih dongah a hui aka lungnah loh, citcai vaengkah ham manuca a cun.
18 Munthu wopanda nzeru amavomereza zopereka chikole ndipo iyeyo amasanduka chikole cha mnansi wake.
Lungbuei aka talh hlang loh kut a yuh tih, a hui mikhmuh ah mingphanah rhi a khang.
19 Wokonda zolakwa amakonda mkangano, ndipo wokonda kuyankhula zonyada amadziyitanira chiwonongeko.
Boekoek aka lungnah loh olpungnah te a lungnah, a thohka te a sang sak tih pocinah a tlap.
20 Munthu wamtima woyipa zinthu sizimuyendera bwino; ndipo woyankhula zachinyengo amagwa mʼmavuto.
Lungbuei aka voeldak loh hnothen hmu pawt tih, a ol neh hlang aka maelh khaw yoethae ah cungku.
21 Mwana wopusa amamvetsa chisoni abambo ake, abambo a chitsiru sakhala ndi chimwemwe.
Amah kah a pha-ueknah ham hlang ang te a cun, te dongah hlang ang kah a napa tah a ko a hoe moenih.
22 Mtima wosangalala uli ngati mankhwala abwino, koma mtima wokhumudwa umafowoketsa mafupa.
Lungbuei kohoe he si la a hoeih sak tih, mueihla a rhawp vaengah songrhuh khaw a koh sak.
23 Munthu woyipa amalandira chiphuphu chamseri kuti apotoze chiweruzo cholungama.
Laitloeknah a caehlong te phaelh sak ham, halang loh a huep ah kapbaih a loh.
24 Munthu wozindikira zinthu, maso ake amakhala pa nzeru, koma chitsiru chimwazamwaza maso ake pa dziko lonse lapansi.
Cueihnah he aka yakming ham tah amah mikhmuh ah a om pah tih, aka ang kah a mik ah tah diklai khobawt la a om pah.
25 Mwana wopusa amamvetsa chisoni abambo ake ndipo amapweteketsa mtima amayi ake.
Capa aka ang tah a napa ham konoinah la om tih, anih aka cun khaw hmuetphawtnah ni.
26 Sibwino kulipitsa munthu wosalakwa, kapena kulanga anthu osalakwa.
Hlang dueng te lai a sah sak khaw, a dueng dongah hlangcong taam ham then pawh.
27 Munthu wosunga pakamwa ndiye wodziwa zinthu, ndipo wodekha mtima ndiye womvetsa bwino zinthu.
A ol aka tuem tah mingnah te aka ming la om tih, mueihla phu tlo aka dingsuek tah hlang lungcuei ni.
28 Ngakhale chitsiru chimakhala ngati chanzeru chikakhala chete; ndipo chikatseka pakamwa chimakhala ngati munthu wochenjera.
Hlang ang pataeng a hil a phah atah aka cueih la, a ka a buem atah aka yakming la a ngai coeng.