< Miyambo 11 >
1 Muyeso wachinyengo Yehova umamunyansa, koma amakondwera ndi muyeso woyenera.
balance deceit abomination LORD and stone: weight complete acceptance his
2 Kunyada kukalowa, pamafikanso manyazi, koma pamene pali kudzichepetsa pameneponso pali nzeru.
to come (in): come arrogance and to come (in): come dishonor and with humble wisdom
3 Ungwiro wa anthu olungama umawatsogolera, koma anthu osakhulupirika amawonongeka ndi chinyengo chawo.
integrity upright to lead them and crookedness to act treacherously (to ruin them *Q(K)*)
4 Chuma sichithandiza pa tsiku lawukali wa Mulungu, koma chilungamo chimapulumutsa ku imfa.
not to gain substance in/on/with day fury and righteousness to rescue from death
5 Chilungamo cha anthu angwiro chimawongolera moyo wawo, koma ntchito zoyipa zimagwetsa mwini wake yemweyo.
righteousness unblemished: blameless to smooth way: conduct his and in/on/with wickedness his to fall: fall wicked
6 Chilungamo cha anthu oyera mtima chimawapulumutsa, koma anthu onyenga adzagwidwa ndi zilakolako zawo zomwe.
righteousness upright to rescue them and in/on/with desire to act treacherously to capture
7 Pamene munthu woyipa wafa, chiyembekezo chake chimathanso. Chiyembekezo cha munthu wosalungama chimawonongeka.
in/on/with death man wicked to perish hope and hope strength to perish
8 Munthu wolungama amapulumutsidwa ku mavuto, koma mʼmalo mwake amagwa mʼmavutomo ndi anthu oyipa.
righteous from distress to rescue and to come (in): come wicked underneath: instead him
9 Munthu wosapembedza amawononga mnansi wake ndi pakamwa pake, koma munthu wolungama amapulumuka chifukwa cha kudziwa zinthu.
in/on/with lip profane to ruin neighbor his and in/on/with knowledge righteous to rescue
10 Anthu olungama zinthu zikamawayendera bwino, mzinda wonse umakondwera, ndipo oyipa akamawonongeka anthu amafuwula mwachimwemwe.
in/on/with goodness righteous to rejoice town and in/on/with to perish wicked cry
11 Mzinda umakwezeka chifukwa cha madalitso a anthu oyera mtima, koma umawonongedwa chifukwa cha pakamwa pa anthu oyipa.
in/on/with blessing upright to exalt town and in/on/with lip wicked to overthrow
12 Munthu wonyoza mnzake ndi wopanda nzeru, koma munthu wanzeru zomvetsa zinthu amakhala chete.
to despise to/for neighbor his lacking heart and man understanding be quiet
13 Amene amanka nachita ukazitape amawulula zinsinsi; koma munthu wokhulupirika amasunga pakamwa pake.
to go: went slander to reveal: reveal counsel and be faithful spirit to cover word: thing
14 Pakasoweka uphungu mtundu wa anthu umagwa; koma pakakhala aphungu ambiri pamakhalanso chipulumutso.
in/on/with nothing counsel to fall: fall people and deliverance: victory in/on/with abundance to advise
15 Woperekera mlendo chikole adzapeza mavuto, koma wodana ndi za chikole amakhala pa mtendere.
bad: evil be evil for to pledge be a stranger and to hate to blow to trust
16 Mkazi wodekha amalandira ulemu, koma amuna ankhanza amangopata chuma.
woman favor to grasp glory and ruthless to grasp riches
17 Munthu wachifundo amadzipindulira zabwino koma munthu wankhanza amadzibweretsera mavuto.
to wean soul: myself his man kindness and to trouble flesh his cruel
18 Munthu woyipa amalandira malipiro wopanda phindu, koma wochita chilungamo amakolola mphotho yeniyeni.
wicked to make: do wages deception and to sow righteousness hire truth: certain
19 Munthu wochita za chilungamo amapeza moyo, koma wothamangira zoyipa adzafa.
right righteousness to/for life and to pursue distress: evil to/for death his
20 Yehova amanyansidwa ndi anthu a mtima wokhotakhota koma amakondwera ndi anthu a makhalidwe angwiro.
abomination LORD twisted heart and acceptance his unblemished: blameless way: conduct
21 Zoonadi, anthu oyipa adzalangidwa, koma anthu olungama adzapulumuka.
hand: to to/for hand: certainly not to clear bad: evil and seed: children righteous to escape
22 Monga imaonekera mphete yagolide ikakhala pa mphuno ya nkhumba, ndi momwenso amaonekera mkazi wokongola wamʼkamwa.
ring gold in/on/with face: nose swine woman beautiful and to turn aside: remove taste
23 Zokhumba za anthu olungama zimathera pa zabwino zokhazokha, koma chiyembekezo cha anthu oyipa chimathera mu ukali wa Mulungu.
desire righteous surely good hope wicked fury
24 Munthu wina amapatsako anzake zinthu mwaufulu nʼkumangolemererabe; wina amamana chomwe akanatha kupereka, koma kumanka nasawukabe.
there to scatter and to add still and to withhold from uprightness surely to/for need
25 Munthu wopereka mowolowamanja adzalemera; iye amene amathandiza ena iyenso adzathandizidwa.
soul: myself blessing to prosper and to quench also he/she/it to shoot
26 Anthu amatemberera womana anzake chakudya, koma madalitso amakhala pamutu pa munthu amene amagulitsa chakudyacho.
to withhold grain to curse him people and blessing to/for head to buy grain
27 Iye amene amafunafuna zabwino mwakhama amapeza zabwinozo, koma wofunafuna zoyipa zidzamupeza.
to seek good to seek acceptance and to seek distress: evil to come (in): come him
28 Aliyense amene amadalira chuma chake adzafota, koma wolungama adzaphukira ngati tsamba lobiriwira.
to trust in/on/with riches his he/she/it to fall: fall and like/as leaf righteous to sprout
29 Wovutitsa a mʼnyumba mwake adzalowa mʼmavuto, ndipo chitsiru chidzakhala kapolo wa munthu wa nzeru.
to trouble house: household his to inherit spirit: breath and servant/slave fool(ish) to/for wise heart
30 Chipatso cha ntchito zabwino ndi moyo, ndipo kusatsata malamulo kumawonongetsa moyo.
fruit righteous tree life and to take: take soul wise
31 Ngati anthu olungama amalandira mphotho zawo pa dziko lapansi, kuli bwanji anthu osapembedza ndi ochimwa!
look! righteous in/on/with land: country/planet to complete also for wicked and to sin