< Miyambo 1 >

1 Iyi ndi miyambi ya Solomoni mwana wa Davide, mfumu ya Israeli:
O NA olelo akamai a Solomona ke keiki a Davida ke alii o ka Iseraela.
2 Ndi yothandiza kuti munthu adziwe nzeru ndi malangizo; kuti amvetse mawu a matanthauzo ozama;
He mea ia e ike ai i ka noiau a me ke aoia mai, E hoomaopopo i na olelo e naauao ai;
3 kuti alandire malangizo othandiza kuti achite zinthu mwanzeru, akhale wangwiro, wachilungamo ndiponso wosakondera.
E loaa'i ka ike e akamai ai, Ma ka pono a me ka hoopono, a me ka pololei;
4 Ndi yothandiza munthu wamba kuti aphunzire nzeru za kuchenjera, achinyamata kudziwa zinthu bwino ndi kulingalira.
E haawi i ka maalea i ka poe naaupo, A me ka ike, a me ka noonoo i ke kanaka ui.
5 Munthu wanzeru amvetse bwino miyamboyi kuti awonjezere kuphunzira kwake, ndi munthu womvetsa zinthu bwino apatepo luso,
E hoolohe ka mea naauao, a mahuahua ka ike, E loaa no i ka mea i aoia'i ka ike o naauao ai;
6 kuti azimvetsa miyambi ndi mafanizo, mawu a anthu anzeru ndi mikuluwiko.
E ike i ka olelo akamai a me ka hoakaka ana o ia mea, I na olelo a ka poe naauao, a me ka lakou olelo pohihi.
7 Kuopa Yehova ndiye chiyambi cha nzeru. Zitsiru zimanyoza nzeru ndi malangizo.
O ka makau ia Iehova, oia ka hoomaka ana o ka ike; A o ka naauao. a me ke aoia mai, ua hoowahawahaia e ka poe lapuwale.
8 Mwana wanga, mvera malangizo a abambo ako ndipo usakane mawu okuwongolera a amayi ako.
E kuu keiki, e hooloke mai i ke ao ana a kou makuakane, Aole hoi e haalele i ke kanawai o kou maku wahine;
9 Ali ngati sangamutu yokongola ya maluwa pamutu pako ndiponso ali ngati mkanda mʼkhosi mwako.
No ka mea, he mea nani ia no kou poo, He mau lei hoi no kou a-i.
10 Mwana wanga, ngati anthu oyipa afuna kukukopa usamawamvere.
E kuu keiki, ina e hoowale wale mai ka poe hewa ia oe, Mai ae aku oe.
11 Akadzati, “Tiye kuno; tikabisale kuti tiphe anthu, tikabisalire anthu osalakwa;
Ina lakou e olelo mai, E, e hele pu kakou, E hoohalua no ke koko, E hoohalua wale i ka mea hala ole;
12 tiwameze amoyo ngati manda, ndi athunthu ngati anthu otsikira mʼdzenje. (Sheol h7585)
E moni ola ia lakou me he malu make, E moni okoa hoi e like me ka poe e haule ana i ka lua: (Sheol h7585)
13 Motero tidzapeza zinthu zosiyanasiyana zamtengowapatali ndi kudzaza nyumba zathu ndi zolanda;
E loaa ia kakou ka waiwai maikai he nui, E hoopiha i ko kakou mau hale me ka waiwai pio;
14 Bwera, chita nafe maere, ndipo tidzagawana chuma chathu tonse.”
E hailona pu oe me makou i kou kuleana, I hookahi hipuu na kakou a pau:
15 Mwana wanga, usayende nawo pamodzi, usatsagane nawo mʼnjira zawozo.
E kuu kiekie e, mai hele pu oe mo lakou ma ke ala; E haalele kou wawae i ko lakou mau kuamoo;
16 Iwowatu amangofuna zoyipa zokhazokha, amathamangira kukhetsa magazi.
No ka mea, holo kiki ko lakou wawae i ka hewa, Wikiwiki hoi lakou i ka hookahe koko.
17 Nʼkopanda phindu kutchera msampha mbalame zikuona!
Make hewa no ke kau ana i ka hei, Ma ke alo o na mea eheu a pau.
18 Koma anthu amenewa amangobisalira miyoyo yawo yomwe; amangodzitchera okha msampha!
Moe malu lakou no ko lakou koko; Makaala hoi no na uhane o lakou.
19 Awa ndiwo mathero a anthu opeza chuma mwankhanza; chumacho chimapha mwiniwake.
Pela ka aoao o ka poe makee waiwai a pau, E kaili ana i ke ola o ka mea nona ia.
20 Nzeru ikufuwula mu msewu, ikuyankhula mokweza mawu mʼmisika;
Hea ae la ka naauao mawaho; Pane mai kona leo ma ke alanui;
21 ikufuwula pa mphambano ya misewu, ikuyankhula pa zipata za mzinda kuti,
Ma ka welau o na ala oia e kahea mai ai: Ma na kahua o na puka kulanakauhale kana olelo ana, I mai la,
22 “Kodi inu anthu osachangamukanu, mudzakondwera ndi kusachangamuka mpaka liti? Nanga anthu onyogodola adzakondabe kunyogodola mpaka liti? Kapena opusa adzadana ndi nzeru mpaka liti?
Pehea ka loihi, e ka poe ike ole, E makemake ai oukou i ka naaupo? A oukou hoi, e ka poe hoowahawaha, E makemake ai i ka hoowahawaha ana? A o oukou, e ka poe naaupo, e inaina aku ai i ka naauao?
23 Tamverani mawu anga a chidzudzulo. Ine ndikukuwuzani maganizo anga ndi kukudziwitsani mawu anga.
E huli mai oukou i ka'u ao ana; Aia hoi e niuini aku au i ko'u Uhane maluna o oukou. E hoike aku hoi ia oukou i ka'u mau olelo.
24 Popeza ndinakuyitanani koma inu munakana kumvera. Ndinayesa kukuthandizani koma panalibe amene anasamala.
I ko'u wa i hea aku ai, hoole mai oukou; Kikoo aku la au i ko'u lima, aohe mea i manao mai;
25 Uphungu wanga munawunyoza. Kudzudzula kwanga simunakusamale.
Haalele oukou i ko'u mau manao a pau, Aole hoi oukou i makemake i ka'u ao ana:
26 Ndiye inenso ndidzakusekani mukadzakhala mʼmavuto; ndidzakunyogodolani chikadzakugwerani chimene mumachiopacho.
Nolaila, i ko oukou popilikia e akaaka au, E hoowahawaha au i ka hiki ana o ko oukou makau;
27 Chiwonongeko chikadzakugwerani ngati namondwe, tsoka likadzakufikirani ngati kamvuluvulu, mavuto ndi masautso akadzakugwerani.
A hiki mai ko oukou makau me he mea ino la, A hookokoke mai ko oukou popilikia me he puahiohio la, A loohia oukou e ka pilihua a me ke kaumaha:
28 “Tsono mudzandiyitana koma sindidzayankha; mudzandifunafuna, koma simudzandipeza.
Alaila, e hea mai lakou ia'u, aole au e pane aku; E imi koke lakou ia'u aole e loaa mai;
29 Popeza iwo anadana ndi chidziwitso ndipo sanasankhe kuopa Yehova,
No ka mea, hoowahawaha lakou i ka ike, A o ka makau ia Iehova, aole lakou i koho mai;
30 popeza iwo sanasamale malangizo anga ndipo ananyoza chidzudzulo changa.
Aole o lakou makemake i ka'u ao ana; Manao ino hoi i ka'u mau olelo a pau.
31 Tsono adzadya zipatso zoyenera mayendedwe awo ndi kukhuta ndi ntchito zimene anachita kwa ena.
Nolaila, e ai lakou i ka hua o ko lakou aoao iho, A ma ko ka manao ana o lakou e maona ai.
32 Pakuti anthu osachangamuka amaphedwa chifukwa cha kusochera kwawo, ndipo zitsiru zimadziwononga zokha chifukwa cha mphwayi zawo.
No ka mea, o ka haalele ana aku o ka poe naaupo, oia ko lakou pepehiia mai, A o ka noho nanea ana o ka poe lapuwale, o ko lakou make ia.
33 Koma aliyense wondimvera adzakhala mwa bata; adzakhala mosatekeseka posaopa chilichonse.”
Aka, o ka mea hoolohe mai ia'u. e noho oluolu no ia, E noho no ia me ka makau ole i ka poino.

< Miyambo 1 >