< Afilipi 1 >
1 Paulo ndi Timoteyo, atumiki a Khristu Yesu. Kulembera anthu onse oyera mtima a ku Filipi amene ali mwa Khristu Yesu, pamodzi ndi oyangʼanira ndi atumiki awo.
Pauli ni Timoti, bhatumishi bha Kristu Yesu, kwa bhala bhatengibhu mwa kristu bhabhitema Filipi, pamonga ni bhabhiyangilila ni mashemasi.
2 Chisomo ndi mtendere zochokera kwa Mulungu Atate athu ndi Ambuye Yesu Khristu zikhale kwa inu.
Neema na j'hiyelayi kwa muenga ni amani j'hayih'omela kwa K'yara dadiyetu ni Bwana bhitu Yesu kristu.
3 Ndimayamika Mulungu wanga nthawi zonse ndikakumbukira inu.
Nikammbombesya K'yara bhengu kila pa nikabhak'homb'hoka muenga mwebhoha.
4 Mʼmapemphero anga onse opempherera inu, nthawi zonse ndimapemphera ndi chimwemwe
Mara syoha kila liombi lyangu kwa ndabha j'ha mwenga mwebhoha, huwa nikobhoka panikabhas'omela.
5 chifukwa mwakhala mukundithandiza polalikira Uthenga Wabwino kuyambira tsiku loyamba mpaka tsopano.
Niyele ni shukrani limehele kwandabha j'ha ushirika bhw'henu muinjili kuh'omela ligono lya lya kubhwandelu mpaka lelu.
6 Sindikukayika konse kuti Iye amene anayamba ntchito yabwino mwa inu adzayipitiriza ndi kuyimaliza mpaka pa tsiku la kubweranso kwa Khristu Yesu.
Niyele nibhuhakika kuj'ha muene j'haoyandisi lihengu linofu mugati mwa muenga ibeyendelela kuj'hikamilisya mpaka ligono lya Bwana YesuKristu.
7 Kwa ine ndi bwino kuti ndiziganiza zotere za nonsenu, popeza ndimakukondani, ngakhale ndikhale mʼndende, kapena pamene ndikuteteza ndi kukhazikitsa Uthenga Wabwino, inu nonse mumagawana nane chisomo cha Mulungu.
Ni sawa kwa nene kujip'heleka naha nalabha j'hamuenga mwabhoha kwa nakbha mmbabhakhili mun'teema bhwangu. Kwandabha muenga muyele bhashirika bhayinu mwa neema mukifungu kyangu ni mu utetezi ni bhuthibitishaji bhwangu bhwa injili.
8 Mulungu angandichitire umboni kuti ndimakulakalakani ndi chikondi cha Khristu Yesu.
K'yara ndo shahidi ghwa nene, ndabha kyaniyele ni shauku ndabha j'ha muenga mwebhoha mu ugati ghwa pendo lya Yesu kristu.
9 Ndipo pemphero langa ndi lakuti chikondi chanu chipitirire kukulirakulira pa chidziwitso ndi kuzama mʼmaganizo,
Na nis'oma kuj'ha: lugano lwinu bhuyongesekai zaidi ni zaidi mu maarifa ni luhala lwoha.
10 kuti mukhoza kuzindikira chabwino koposa zonse ndi chiti kuti muthe kukhala wopanda chodetsa ndi wopanda chilema kufikira tsiku la Khristu.
Nis'oma kwandabha j'ha e'le muyelai kinofu ni bhuwezo bhwa kup'hema ni kuchagula mambo ghaghayele kinofu sana. Pia nikihabhas'omela ili muyelai kinofu bila kuj'ha nihatia j'hoj'hioha y'hela muligono lya Kristu.
11 Ndipo moyo wanu udzakhala odzazidwa ndi chipatso cha chilungamo chimene chimachokera mwa Yesu Khristu. Pakuti zimenezi zidzapereka ulemerero ndi matamando kwa Mulungu.
Na pia ili mmemesibhwaya ni litunda lya haki lyalipatikana mwa Yesu Kristu, kwa bhutukufu ni sifa j'ha K'yara.
12 Tsopano abale, ndikufuna mudziwe kuti chimene chandichitikira ine chathandiza kwambiri kupititsa patsogolo Uthenga Wabwino.
Henu bhalongobhangu, nilonda mmanyayi kuj'ha mambo ghaghah'omili kwa nene ghaghaifwanjili injili iyendelelayi sana.
13 Chotsatira chake nʼchakuti zadziwika bwino lomwe kwa onse amene ali ku nyumba yaufumu kuti ine ndili mʼmaunyolo chifukwa cha Khristu.
Ndo maana fifungu fyangu mu Kristu, fimanyik'hene kwa bhalinzi bha ikulu iyoha ni kwa k'hila munu pia.
14 Moti chifukwa cha maunyolo angawa, abale ambiri alimbikitsidwa kuyankhula Mawu a Mulungu molimbika ndi mopanda mantha.
Ni bhalongo bhingi mu Bhwana kwandabha j'ha fifungu fyanene bhashawishiki nikuthubutu kulihubiri lilobhi bila khutila.
15 Nʼzoonadi kuti ena amalalikira Khristu chifukwa cha kaduka ndi mikangano, koma ena chifukwa cha zolinga zabwino.
Bhamana kuweli hata bhikhanta ngasya Kristu kwa fitina ningondo, na pia bhamana kwa nia yinofu.
16 Olalikira ndi zolinga zabwinowa amachita izi mwachikondi, podziwa kuti ine ndili muno chifukwa cha kuteteza Uthenga Wabwino.
Bhala bhabhakantangasya Kristu kwa lugano bhamanyili kuj'ha nibhekhibhu apanai kwa ndabha j'ha kuitetela injili.
17 Ena aja amalalikira Khristu modzikonda osati moona mtima namaganiza kuti kutero kubweretsa mavuto pamene ndili mʼmaunyolo.
Bali bhangi bhikantangasya Kristu, kwa bhubinafsi ni kwa nia yibaya. Bhidhanila kuj'ha bhisababisya matatizo kwa nene muminyororo ghyangu.
18 Nanga kodi zimenezo zili ndi ntchito? Chofunika ndi chakuti Khristu alalikidwe, kaya ndi mwachinyengo kapena moona. Ndipo ndikukondwera chifukwa cha chimenechi. Ndithu, ndidzapitirira kukondwera,
Henu? nijali lepi aidha nj'hela iyelai ni kwa hilarious au kwa bhukweli, Kristu itangasibhwa ni mu e'le nihobhok'hela! Ndo, nibekuhobhokila.
19 pakuti ndikudziwa kuti chifukwa cha mapemphero anu ndi thandizo lochokera kwa Mzimu wa Yesu Khristu, zimene zandionekera zidzathandiza kuti ndimasulidwe.
kwa kuj'ha nimanyili e'le libekutokula kubhopolibhwa kwa nene. like Jambo e'le libekutokula kwandabha j'ha maombi ghinu ni kwa msaada bhwa Roho j'ha yes Kristu.
20 Ndili ndi chiyembekezo chonse kuti sindidzachita manyazi ndi pangʼono pomwe, koma ndidzakhala ndi chilimbikitso chokwanira kuti monga mwa nthawi zonse, tsopano Khristu adzakwezedwa mʼthupi langa kaya ndi mʼmoyo kapena mu imfa.
kul'hengana ni matajio ghangu ghabhuhakika ni ibhukweli ni kwamba, nibebhona lepisoni. Badala yiake, kwabhujasiri bhuoha, Kama ambavyo magono ghoha ni henu, nitarajila kuj'ha Kristu ibekuyinulibhwa mu mb'hele bhwangu, ikayelaye mu bhusima au mu kafwelelu.
21 Pakuti kwa ine kukhala moyo ndi Khristu ndipo kufa ndi phindu.
kwa maana kwanene kuishi ni Kristu na kufwa ni faida.
22 Ngati nditi ndipitirire kukhala ndi moyo mʼthupi ndiye kuti kwa ine ndi kugwira ntchito yopindulitsa. Kodi ndisankhe chiyani? Sindikudziwa.
lakini Kama kutama mu m'mb'hele wihogola litunda mu lihengu lyangu, kwahenu nd'hesi l'el'eku lya kuchagula.
23 Ndathinidwa ndi zinthu ziwirizi: Ndikulakalaka kunyamuka kuti ndikakhale ndi Khristu, chimene ndi chinthu chabwino kwambiri.
Maana nisukumibhwa sana ni mawazo agha mab'hele. Niye ni hamu j'ha kuleka m'mb'hele ni kuj'ha pamonja ni Kristu, k'henu ambakyo ni kya thamani sanasana.
24 Komanso nʼkofunika kwambiri kuti ndikhalebe mʼthupi chifukwa cha inu.
Ingawa, kubakila mu m'mb'hele obho nik'henu kya mhimu sana kwa ndabha j'ha muenga.
25 Ndili ndi chitsimikizo, ndikudziwa kuti ndidzakhala ndi moyo ndipo ndidzapitirira nanu kuti nonse mupite mʼtsogolo ndi kukhala ndi chimwemwe mu chikhulupiriro
kwa kuj'ha niyele ni bhuhakika kwa ndabha j'ha e'le nimanyili nibhebakila nikuj'hendelela kuj'ha pamonja namu mwe bhoha, kwa ndabha j'ha maendeleo ni furaha j'ha muenga.
26 kuti pokhala nanunso, kudzitamandira kwanu mwa Khristu Yesu kudzasefukire chifukwa cha ine.
Na e'le libeleta furaha j'ha muenga ibhaha mwa kristu Yesu, kwa ndabha j'ha kuj'ha kwa nene yibekuyongeseka, kwa ndabha kuj'ha kwa nene kabhele pamonja namu.
27 Chilichonse chimene chingachitike, chachikulu nʼchakuti mukhale moyo ofanana ndi Uthenga Wabwino wa Khristu. Tsono ngati ndingabwere kudzakuonani kapena kumangomva za inu ndili kutali, ndidzadziwa kuti mwayima mwamphamvu mwa Mzimu mmodzi, kulimbika pamodzi ngati munthu mmodzi chifukwa cha chikhulupiriro cha Uthenga Wabwino
Mwilondeka kutama maisha gha muenga mu mwenendo unofu ghwaghukayilonda injili j'lia Kristu. Mkhetayi mebhu ili nikahialayi kubhalanga au nikabelayi kuhiola, nip'helekai kuj'ha my'emili kinofu mu Roho yimonga. Natamani kup'eleka kuj'ha myele ni Roho yimonga, mkayikhomanela imani j'ha injili kwa pamonga.
28 osachita mantha ndi pangʼono pomwe ndi amene akutsutsana nanu. Ichi ndi chizindikiro kwa iwo kuti adzawonongedwa, koma inu mudzapulumutsidwa ndi Mulungu.
msitisibhu ni k'henu kyokyok'hula kyakifwanyibhwa ni maadui bha muenga. Ey'e kwa bhene n'do ishara j'ha uharibifu. Bali kwa muenga n'do ishara j'ha bhwokovu kuh'oma kwa K'yara. kwa maana muenga mpelibhu kwa
29 Pakuti inu mwapatsidwa mwayi osati ongokhulupirira Khristu kokha, koma wakumva zowawa mʼmalo mwa Khristu.
ndabha j'ha Kristu, sio kumwamini tu, bali ni kutesibhwa pia kwa muene.
30 Inunso mukudutsa mʼzowawa zomwe zija munaona ndikudutsamo inenso ndipo pano mukumva kuti ndikukumana nazobe.
kwa maana muye ni ngondo y'elay'ela Kama kyamkayibhwene kwa nenga na mwip'eleka kuj'ha niyenabhu hata h'enu.