< Afilipi 4 >

1 Tsono abale anga, ndimakukondani ndipo ndikukulakalakani. Ndinu chimwemwe changa ndi chipewa cha ulemerero wanga. Abwenzi okondedwa, chilimikani choncho mwa Ambuye.
Kuite alowa ane, naize numusumbiye, naiulowa ningala ane. Imeki kisa mumukulu, unye ahumba alowa.
2 Ndikudandaulira Euodiya ndi Suntuke kuti akhale ndi mtima umodzi mwa Ambuye.
kuupepelya uewe Eudia, kupepelya ga nue Sintike, musushe ukupi nuaupolo wanyu. Kunsoko unyenye e miihi miabiili aimiungile mumukulu.
3 Inde, ndikupempha iwe mnzanga pa ntchitoyi, thandiza amayiwa amene ndagwira nawo ntchito ya Uthenga Wabwino pamodzi ndi Klementonso ndi ena onse antchito anzanga amene mayina awo ali mʼbuku lamoyo.
Kutai, mumupepelye gwa ung'wenso ituma milimo iane, muailye iasungi awa kunsoko aitumi palung'wi nunene muutamani inkani ninza niyamukulu kezekukoli nu Kelementi palung'we niitumi niangiza niamukulu, imani nao nainandikiwe mumbugulu naupanga.
4 Nthawi zonse muzikondwa mwa Ambuye. Ndikubwerezanso; muzikondwa!
Mumukulu mahiku ehi. Hangi kulunga, mulowe.
5 Kufatsa kwanu kuzioneka pamaso pa anthu onse. Ambuye anu ali pafupi.
Upolo wanyu ulengekile kuantu ehi. Umukulu wahugeela.
6 Musade nkhawa ndi kanthu kalikonse, koma pa china chilichonse, mwa pemphero ndi chidandaulo pamodzi ndi chiyamiko, perekani zopempha zanu kwa Mulungu.
Muleke kisumbula kulukani leji. Itumi imakani anyu ehi kunzila naulukuluku, kulompa nikusongelya. Nimaitaji anyu dengeke kung'wi Tunda.
7 Ndipo mtendere wa Mulungu, umene upambana nzeru zonse udzasunga bwino mitima yanu ndi maganizo anu mwa Khristu Yesu.
Upolo nuamukulugwa ninkulu kukila ulengi wehi, ikasunga ikulu nimasego anyu kuualigwa wang'wa Yesu Kilisto.
8 Potsiriza, abale, muziyika mtima wanu pa zinthu zilizonse zabwino ndi zotamandika monga, zinthu zoona, zinthu zolemekezeka, zinthu zolungama, zinthu zoyera, zinthu zokongola ndi zinthu zosiririka.
Impelo, aluna ane. Masigi lukulu imakani ehi nakete ita ukuligwi, ikulu welu, ulowa, naya nakete upikiligwi nuuza upolo, palung'wi naya natakewe kukuligwa.
9 Muzichita chilichonse chimene mwaphunzira kapena kulandira kapena kumva kuchokera kwa ine kapena mwaona mwa ine. Ndipo Mulungu wamtendere adzakhala nanu.
Muitumile inkani izi numumanyisigwi, nimusingilye nija naya naua nimumaine kung'wane nukung'wa Tata witu nua upolo ukutula nunyenye.
10 Ndikukondwa kwambiri mwa Ambuye kuti patapita nthawi tsopano mwayambanso kuonetsa kuti mumandiganizira. Zoonadi, mwakhala mukundikumbukira, koma munalibe mpata woti muonetsere zimenezi.
Nkete ulowa ukolo du kung'waanyu mumukulu, kunsoko unye migeela hangi isigo lakutula kung'wanyu nsoko aulompi wane hatize singamupatile ilyoma lakunzailya.
11 Sindikunena izi chifukwa choti ndikusowa thandizo, poti ine ndaphunzira kukhala wokwaniritsidwa ndi zimene ndili nazo.
Singa kulunga ite inge mpate kintu kunsoko auula wane kunsoko auuta wanyu. Kunsoko nalenga kugomba muhali yehi.
12 Ndimadziwa kusauka nʼkutani, ndipo ndimadziwa kulemera nʼkutani. Ndaphunzira chinsinsi chokhala wokhutitsidwa mwa njira ina iliyonse, kaya nʼkudya bwino kapena kukhala ndi njala, kaya kukhala ndi chuma kapena umphawi.
Ningile ulikalo lakuhielwa nulikalo lakutula nimaintu ga mumazingila ehi aya unenifunzile kinkunku kukulya imahikutungilwe hangi nukulya imahiku naanzala, yaani nedu nukutula nuula.
13 Ndikhoza kuchita zonse kudzera mwa Iye amene amandipatsa mphamvu.
Nihumile kutuma aya kuaailigwa nung'wenso nuemupeza ingulu.
14 Komatu munachita bwino kundithandiza mʼmavuto anga.
Ata uu ainitumile iza kunzailya une munzago yane.
15 Ndipo inu Afilipi mukudziwa kuti masiku oyambirira olalikira Uthenga Wabwino, nditachoka ku Makedoniya, panalibe mpingo ndi umodzi omwe umene unagwirizana nane pa nkhani yopereka ndi kulandira, kupatula inu.
Unye Afilipi mulinge kina ung'wandyo wankani ninza nainihegile ku Makedonia, kulite angilekeelo nailintindikie mumakani natakewe kupumya nukusingelya inge unyenye udu.
16 Pakuti ngakhale pamene ndinali ku Tesalonika, munanditumizira kangapo zondithandiza pa zosowa zanga.
Ganapaga nainkule Kutesalonike, unye aimuntumie umusaada singa kang'we kunsoko auula wane.
17 Osati ndikufuna mphatso zanu, koma ndikufuna kuti pa zimene muli nazo pawonjezerekepo phindu.
Muleke kugela kina kulompa musaada. Inge kulunga gwa mulije inkali nikete nsailo kung'wanyu.
18 Ndalandira zonse ndipo ndili nazo zokwanira zoposa zosowa zanga popeza ndalandira kwa Epafrodito mphatso zochuluka zimene munatumiza. Ndizo zopereka za fungo labwino, nsembe zolandiridwa zokondweretsa Mulungu.
Nasingilya maintu ehi, nitungele nizuigwe nimaintu idu, nsengeye imaintu anyu kupumiila kung'wa Epafuladito. Inge maintu maza akunyunkiila ihanganga imanukato. Nago mbekile nanso ehi isongeelyo namuloeye Itunda.
19 Ndipo Mulungu wanga adzakwaniritsa zosowa zanu monga mwa chuma chake chaulemerero mwa Khristu Yesu.
Kunsoko nanso, Itunda wane ukumizulya uula wanyu kutula ugole nua ukulu wakwe mung'wa Yesu Kilisto.
20 Kwa Mulungu ndi Atate athu, kukhale ulemerero mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
Ilungile kung'wi Tunda nu Tata witu ukule ukulu wakale na kale hueli. (aiōn g165)
21 Perekani moni kwa oyera mtima onse mwa Khristu Yesu. Abale amene ali ndi ine akupereka moni wawo.
Imelamu ane imupikile kila muhueli mung'wa Kilisto u Yesu. Alowa ninkoli nienso apa amupee milamu amulamukilye.
22 Oyera mtima onse akupereka moni, makamaka iwo a ku nyumba ya Kaisara.
Ga niahueli ehi apa akumulamusha, palung'wi nawa niamunyumba ang'wa Kaisali.
23 Chisomo cha Ambuye Yesu Khristu chikhale ndi mzimu wanu. Ameni.
Nitungele ukende wamukulu witu u Yesu Kilisto utule ukole munkolo yangu.

< Afilipi 4 >