< Filemoni 1 >

1 Kuchokera kwa Paulo, amene ndili mʼndende chifukwa cha Khristu Yesu ndi Timoteyo mʼbale wathu. Kulembera Filemoni, bwenzi lathu lokondedwa ndi mtumiki mnzathu.
An Paulo ngʼat motwe nikech Kristo Yesu kod owadwa Timotheo, Wandikoni osiepwa mwageno kendo jatich wadwa Filemon,
2 Kwa Apiya mlongo wathu, Arkipo msilikali mnzathu, ndiponso mpingo umene umasonkhana mʼnyumba mwanu.
kaachiel gi nyaminwa Afia gi Arkipo jalweny wadwa, kod kanisa malemo e odi:
3 Chisomo ndi mtendere zochokera kwa Mulungu Atate athu ndi Ambuye Yesu Khristu zikhale ndi inu.
Ngʼwono kod kwe moa kuom Nyasaye Wuonwa kod Ruoth Yesu Kristo obed kodu.
4 Ine ndimayamika Mulungu wanga nthawi zonse ndikakukumbukira iwe mʼmapemphero anga.
Adwokone Nyasacha erokamano pile ka aluongo nyingi e lemona,
5 Pakuti ndamva za chikondi chako, za chikhulupiriro chako mwa Ambuye Yesu ndiponso za chikondi chako pa oyera mtima onse.
nikech awinjo kuom yie ma in-go kuom Ruoth Yesu, kendo kuom hera miherogo jomaler duto.
6 Ine ndikupemphera kuti mgwirizano wako ndi ife mʼchikhulupiriro ukhale opindulitsa pozamitsa nzeru zako zozindikira zinthu zilizonse zabwino zimene timagawana chifukwa cha Khristu.
Alemoni ni mondo iland yie ma in-go motegno, mondo eka ibed gi ngʼeyo matut kuom gik mabeyo duto ma wan-go ei Kristo.
7 Mʼbale, chikondi chako chandipatsa chimwemwe chachikulu ndi chilimbikitso, chifukwa umatsitsimutsa mitima ya anthu a Ambuye.
Hera ma in-go osemiya mor maduongʼ kendo osejiwa, nikech in, owadwa mahero, isedwogo chunje jomaler.
8 Tsopano ngakhale kuti mwa Khristu nditha kulimba mtima ndi kulamulira kuti uchite zimene uyenera kuchita,
Kuom mano, kata obedo ni kuom Kristo ne anyalo bedo gi chir mar chiki mondo itim gima onego itim,
9 komabe ndikupempha mwachikondi. Ine Paulo, munthu wokalamba, ndipo tsopano ndili mʼndende chifukwa cha Khristu Yesu,
to koro asayi mondo itim kamano nikech hera. Koro an Paulo awuon, ma jaduongʼ, kendo motwe nikech wach Kristo Yesu,
10 ndikukupempha chifukwa cha mwana wanga Onesimo, amene ndamubala ndili mu unyolo.
akwayi kuom wach wuoda Onesimo mane odoko wuoda ka an e twech.
11 Anali wopanda phindu kwa iwe, koma tsopano wasanduka wa phindu kwa iwe ndi kwa inenso.
Ne onge konyruok mane Onesimo keloni to sani koro okelo konyruok maduongʼ ne in kaachiel kod an bende.
12 Ine ndikumutumizanso kwa iwe tsopano, koma potero ndikukhala ngati ndikutumiza mtima wanga weniweni.
Aore mondo oduog iri, kata obedo ni chunya ogene ahinya.
13 Ndikanakonda ndikanakhala naye kuno kuti iyeyo azinditumikira mʼmalo mwako pamene ndili mu unyolo chifukwa cha Uthenga Wabwino.
Dahero bedo kode ka mondo okonya kaeni kapod an e od twech nikech Injili.
14 Koma sindikufuna kuchita kanthu osakufunsa, nʼcholinga chakuti chilichonse chabwino ungandichitire chikhale mwakufuna kwako osati mokakamiza.
To ne ok adwar timo gimoro amora ka ok in ema iyie, mondo tim ngʼwono moro amora mitimo kik bed gima ochun, to obed gima itimo nikech ihero.
15 Mwina chifukwa chimene unasiyana naye kwa kanthawi ndi chakuti ukhale nayenso nthawi zonse. (aiōnios g166)
Nyalo bet ni Onesimo nowuok iri kuom kinde manok mondo iyud thuolo mar kawe chuth bangʼe, (aiōnios g166)
16 Osati ngati kapolo, koma woposa kapolo, ngati mʼbale wokondedwa. Iyeyu ndi wokondedwa kwambiri kwa ine koma kwa iweyo ndi wokondedwa koposa, ngati munthu komanso ngati mʼbale mwa Ambuye.
ok kaka misumba to kaka owadu migeno ma en ngʼat moloyo misumba. En ohala ne an, to angʼeyo ni en ohala moloyo ne in bende, ok mana kaka ngʼato angʼata, to kaka owadu kuom Ruoth.
17 Tsono ngati umati ndine mnzako, umulandire iyeyu monga momwe ukanandilandirira ineyo.
Omiyo ka ikwana kaka ngʼama ni kodi e achiel kuom yie to rwake mana kaka dirwaka.
18 Ngati anakulakwira kapena kukongola kanthu kalikonse, ndidzalipira ineyo.
Kaponi osetimoni marach, kata ka en-gi gopi moro to kwan-gi e wiya.
19 Ine, Paulo ndikulemba zimenezi ndi dzanja langa. Ine ndidzalipira. Nʼkosafunika kukukumbutsa kuti iweyo ngongole yako kwa ine ndi moyo wakowo.
Andikoni baruwani gi lweta awuon an Paulo, ka anyisi ni abiro chuli, kata ka ok aparoni ni in kod gopa ma en ngimani owuon.
20 Mʼbale, ndikufuna kuti ndipindule nawe mwa Ambuye; tsono tsitsimutsa mtima wanga mwa Khristu.
Gima agombo maduongʼ, owadwa, en ni mondo iyie itimna ngʼwono kuom Ruoth, kidwogo chunya kuom Kristo.
21 Ine ndili ndi chitsimikizo cha kumvera kwako pamene ndikukulembera kalatayi. Ndikulemba ndikudziwa kuti udzachita ngakhale kuposa zimene ndakupemphazi.
Nikech angʼeyo maber ni iwinjo wach, andikoni ka an gi adiera ni ibiro timona maber moloyo kaka akwayi.
22 Chinthu chinanso ndi ichi: undikonzere malo, chifukwa ndikukhulupirira kuti Mulungu adzamvera mapemphero anu ndi kundibwezera kwa inu.
Kwayo machielo ma an-go en ni mondo ilosna kar nindo, nikech an-gi geno ni ibiro gonya mana kaka usebedo kulamo.
23 Epafra, wamʼndende mnzanga chifukwa cha Khristu Yesu akupereka moni.
Epafra motwe koda kaachiel nikech wach Kristo Yesu ooronu mos.
24 Atumiki anzanga awa, Marko, Aristariko, Dema ndi Luka, akuperekanso moni.
Mariko bende omosou kaachiel gi Aristarko gi Dema kod Luka, ma gin jotich wetena.
25 Chisomo cha Ambuye Yesu Khristu chikhale ndi mzimu wako.
Ngʼwono mar Ruoth Yesu Kristo mondo obed kod chunyi.

< Filemoni 1 >