< Obadiya 1 >
1 Masomphenya a Obadiya. Ambuye Yehova akunena kwa Edomu kuti, Tamva uthenga wochokera kwa Yehova: Nthumwi yatumidwa kupita kwa anthu a mitundu kukanena kuti, “Konzekani, tiyeni tikachite nkhondo ndi Edomu.”
Obadiah kah mangthui he ka Boeipa Yahovah loh Edom ham a thui. BOEIPA taeng lamloh olthang ka yaak uh coeng. Te dongah namtom taengah laipai a tueih coeng. Thoo uh lamtah caemtloek la a taengah thoo uh.
2 “Taona, ndidzakuchepetsani pakati pa anthu a mitundu ina; udzanyozedwa kwambiri.
Nang te namtom rhoek lakli ah canoi la kang khueh vetih nang te rhep n'hnaep pawn ni he.
3 Kudzikuza kwa mtima wako kwakusocheretsa, iwe amene umakhala mʼmapanga a mʼmatanthwe ndipo umamanga nyumba zako pa mapiri ataliatali, iwe amene umanena mu mtima mwako kuti, ‘Ndani anganditsitse pansi?’
Na lungbuei kah althanah loh nang n'rhaithi coeng. A hmuen sang kah thaelpang thaelrhaep ah kho a sak tih a lungbuei ah, “Ulong kai he diklai la n'hlak eh?,” a ti.
4 Koma ngakhale umawuluka ngati chiwombankhanga ndi kumanga chisa chako pakati pa nyenyezi, ndidzakutsitsa pansi kuchokera kumeneko,” akutero Yehova.
Thahum bangla na sang sitoe cakhaw, aisi laklo ah na bu na khueh sitoe cakhaw, te lamloh nang te kan hlak ni. He tah BOEIPA kah olphong ni.
5 “Anthu akuba akanabwera kwa iwe, kapena anthu olanda zinthu akanafika usiku, aa, tsoka lanji limene likukudikira iwe! Kodi akanangotengako zimene akuzifuna zokha? Ngati anthu othyola mphesa akanafika, kodi akanakusiyiraniko mphesa pangʼono pokha?
Hlanghuen rhoek loh nang te m'paan uh mai tih khoyin ah n'rhoelrhak koinih metlam na hmata eh? Amamih rhoeh hil huen uh mapawt nim? Aka bit rhoek te na taengla ha pawk uh koinih a yoep te hlun uh mahpawt nim?
6 Koma Esau adzalandidwa zinthu zonse, chuma chake chobisika chidzabedwa!
Esau te metlam a phuelhthaih uh a hnothuh te a yam uh eh?
7 Anthu onse ogwirizana nawo adzakupirikitsira kumalire; abwenzi ako adzakunyenga ndi kukugonjetsa; amene amadya chakudya chako adzakutchera msampha, koma iwe sudzazindikira zimenezi.”
Na huitai hlang boeih loh khorhi duela nang n'tueih uh ni. Na ngaimongnah hlang rhoek loh nang te rhaithi nah vetih nang m'vueinan thil ni. Na buh dongah nang hamla doi a khueh vetih a taengah na lungcuei mahpawh.
8 Yehova akunena kuti, “Tsiku limenelo, kodi sindidzawononga anthu onse anzeru a ku Edomu, anthu odziwa zinthu mʼmapiri a Esau?
BOEIPA kah olphong he te khohnin kah moenih a? Edom lamloh aka cueih tih Esau tlang lamkah lungcuei khaw ka milh sak ni?
9 Ankhondo ako, iwe Temani, adzachita mantha, ndipo aliyense amene ali mʼphiri la Esau adzaphedwa pa nkhondo.
Teman nang kah hlangrhalh rhoek te rhihyawp uh tih, Esau tlang kah ngawnnah loh hlang a khoe ni.
10 Chifukwa cha nkhanza zimene unachitira mʼbale wako Yakobo, udzakhala wamanyazi; adzakuwononga mpaka muyaya.
Na mana Jakob kah kuthlahnah kongah yah loh nang n'khuk vetih kumhal duela n'khoe ni.
11 Pamene adani ankamulanda chuma chake pamene alendo analowa pa zipata zake ndi kuchita maere pa Yerusalemu, pa tsikulo iwe unali ngati mmodzi wa iwo.
A hmai ah na pai khohnin ah, kholong loh a thadueng a khuen khohnin ah khaw kholong rhoek te amah vongka, vongka ah kun ni. Jerusalem ham hmulung a naan uh coeng tih nang khaw amih kah hlang pakhat la na om.
12 Iwe sunayenera kunyoza mʼbale wako pa nthawi ya tsoka lake, kapena kunyogodola Ayuda chifukwa cha chiwonongeko chawo, kapena kuwaseka pa nthawi ya mavuto awo.
A yoethaenah hnin ah tah na manuca kah khohnin te so boeh. A milh uh khohnin ah Judah ca rhoek soah kokhahnah boeh. Citcai khohnin ah na ol vikvawk boeh.
13 Iwe sunayenera kudutsa pa zipata za anthu anga pa nthawi ya masautso awo, kapena kuwanyogodola pa tsiku la tsoka lawo, kapena kulanda chuma chawo pa nthawi ya masautso awo.
Amih kah rhainah hnin ah ka pilnam kah vongka ah mop uh boeh. A rhainah hnin ah anih kah yoethaenah te nang loh so van boeh. A rhainah hnin ah tah anih ham tatthai te na tueih pah hae mahpawh.
14 Sunayenera kudikirira pamphambano ya misewu kuti uphe Ayuda othawa, kapena kuwapereka kwa adani awo Ayuda opulumuka pa nthawi ya mavuto awo.”
A hlangyong rhoek te saii hamla longrhak ah pai boeh. Citcai khohnin kah a rhaengnaeng rhoek te khoh boeh.
15 “Tsiku la Yehova layandikira limene adzaweruza mitundu yonse ya anthu. Adzakuchitira zomwe unawachitira ena; zochita zako zidzakubwerera wekha.
BOEIPA kah khohnin he namtom cungkuem hamla yoei coeng. Na saii bangla namah taengah a saii ni. Na thaphu te namah lu dongla mael ni.
16 Iwe unamwa pa phiri langa loyera, koteronso mitundu ina yonse idzamwa kosalekeza; iwo adzamwa ndi kudzandira ndipo adzayiwalika pa mbiri ya dziko lapansi.
Ka hmuencim tlang ah na ok uh bangla namtom boeih loh a ok uh yoeyah ni. A ok uh tih a dolh uh akhaw aka om pawt bangla om uh ni.
17 Koma pa Phiri la Ziyoni padzakhala chipulumutso; phirilo lidzakhala lopatulika, ndipo nyumba ya Yakobo idzalandira cholowa chake.
Tedae Zion tlang ah loeihnah om vetih hmuencim la om ni. Te vaengah Jakob imkhui loh amamih kah a hut te a pang uh ni.
18 Nyumba ya Yakobo idzasanduka moto ndipo nyumba ya Yosefe idzasanduka lawi la moto; nyumba ya Esau idzasanduka chiputu, ndipo adzayitenthe pa moto ndi kuyipsereza. Sipadzakhala anthu opulumuka kuchokera mʼnyumba ya Esau.” Yehova wayankhula.
Te vaengah Jakob im te hmai la, Joseph im te hmaisai la, Esau im te divawt la poeh ni. Amih te a toih uh vetih tlum uh ni. BOEIPA loh a thui coeng dongah Esau im lamkah rhaengnaeng om mahpawh.
19 Anthu ochokera ku Negevi adzakhala ku mapiri a Esau, ndipo anthu ochokera mʼmbali mwa mapiri adzatenga dziko la Afilisti. Adzakhala mʼminda ya Efereimu ndi Samariya, ndipo Benjamini adzatenga Giliyadi.
Tuithim loh Esau tlang neh Philisti kolrhawk te a pang ni. Ephraim khohmuen neh Samaria khohmuen khaw, Benjamin, Gilead khaw a pang uh ni.
20 Aisraeli amene ali ku ukapolo adzalandira dziko la Kanaani mpaka ku Zarefati; a ku Yerusalemu amene ali ku ukapolo ku Sefaradi adzalandira mizinda ya ku Negevi.
Israel ca rhoek he Kanaan neh Zarepthah hil rhalmahvong kah hlangsol la om. Sepharad kah Jerusalem hlangsol rhoek loh tuithim khopuei rhoek te a pang uh ni.
21 Opulumukawo adzapita ku Phiri la Ziyoni ndipo adzalamulira mapiri a Esau. Koma ufumuwo udzakhala wa Yehova.
A khang rhoek tah Esau tlang te laitloek hamla Zion tlang la luei uh vetih mangpa la BOEIPA hut la om ni.