< Numeri 1 >

1 Yehova anayankhula ndi Mose mʼchipululu cha Sinai, mu tenti ya msonkhano, pa tsiku loyamba la mwezi wachiwiri, mʼchaka chachiwiri atatuluka mu Igupto, kuti,
Eso age amola oubi ageyadu amoga Isala: ili dunu ilia da Idibidi yolesi ode ageyadu ganodini, Hina Gode da Ea Abula Diasu, Sainai hafoga: i soge ganodini diala, amo ganodini Mousesema sia: i.
2 “Werengani Aisraeli onse mʼmafuko awo ndi mʼmabanja awo, lemba dzina la munthu wamwamuna aliyense, mmodzimmodzi.
E da amane sia: i, “Di amola Elane amo Isala: ili dunu ilia sosogo fi amola fidafa amoga idisu hamoma. Dunu huluane amo da ode 20 lalelegele esalu, amola ode 20 baligi, amola ilia da dadi gagui hawa: hamomusa: defele esala, amo huluane ilia dio dedema.
3 Iwe ndi Aaroni mwawerenge mwa magulu awo mu Israeli, amuna onse a zaka makumi awiri zakubadwa ndi opitirirapo omwe angathe kugwira ntchito ya usilikali.
4 Munthu mmodzi wochokera ku fuko lililonse yemwe ndi mtsogoleri wa banja lake, ndiye akuthandizeni pa ntchitoyi.
Fi huluane afae afae ilia bisilua ali fidima: ne sia: ma.
5 Mayina a anthu amene akuthandizeniwo ndi awa: Elizuri mwana wa Sedeuri, kuchokera ku fuko la Rubeni,
Fi amoga bisilua, amo hawa: hamomusa: ilia fi dunu amoga ilegei, ilia dio da haguduga dedei diala; Fi ...Fi Bisilua Liubene...Elaise (Siedia egefe) Simiane... Sieliumiele (Siulisia: dai egefe) Yuda...Na: iasione (Aminada: be egefe) Isaga...Nida: niele (Sua egefe) Sebiulane...Ilaia: be (Hilone egefe) Ifala: ime...Ilisiama (Amihade egefe) Ma: na: se...Ga: maliele (Bedase egefe) Bediamini...Abaida: ne (Gidioni egefe) Da: ne...Ahaise (Amisia: da: ia; egefe) A: sie...Ba: igiele (Ogela: ne egefe) Ga: de...Ilaiasa: fe (Diuele egefe) Na: fadalai...Ahaila (Ina: ne egefe)
6 Selumieli mwana wa Zurisadai, kuchokera ku fuko la Simeoni,
7 Naasoni mwana wa Aminadabu, kuchokera ku fuko la Yuda,
8 Netanieli mwana wa Zuwara, kuchokera ku fuko la Isakara,
9 Eliabu mwana wa Heloni, kuchokera ku fuko la Zebuloni,
10 Mwa ana a Yosefe: kuchokera ku fuko la Efereimu, Elisama mwana wa Amihudi; kuchokera ku fuko la Manase, Gamalieli mwana wa Pedazuri;
11 Abidani mwana wa Gideoni, kuchokera ku fuko la Benjamini,
12 Ahiyezeri mwana wa Amisadai, kuchokera ku fuko la Dani,
13 Pagieli mwana wa Okirani, kuchokera ku fuko la Aseri,
14 Eliyasafu mwana wa Deuweli, kuchokera ku fuko la Gadi,
15 Ahira mwana wa Enani, kuchokera ku fuko la Nafutali.”
16 Amenewa ndi anthu amene anasankhidwa kuchokera mʼmagulu mwawo, eni mbumba a mafuko a makolo awo. Iwowa anali atsogoleri a mafuko a Israeli.
17 Mose ndi Aaroni anatenga anthu amene mayina awo anaperekedwa,
Amo dunu fagoyale gala, ilia da Mousese amola Elane fidi. Ilia, da
18 ndipo pa tsiku loyamba la mwezi wachiwiri, anasonkhanitsa anthu onse pamodzi. Anthuwo anafotokoza za makolo awo mwa mafuko awo ndi mabanja awo. Ndipo mayina a amuna onse amene anali ndi zaka makumi awiri kapena kupitirirapo analembedwa, mmodzimmodzi
eso age amola oubi ageyadu amoga Isala: ili fi huluane gilisimusa: wele sia: i. Amalalu, ilia da ilia fi amola sosogo fi huluane afafane, ilia dio huluane dedei. Dunu amo da ode 20 lalelegele esalu amola amo baligi ilia da ilia dio dedene idi.
19 monga momwe Yehova analamulira Mose. Motero iyeyo anawawerenga mʼchipululu cha Sinai:
Hina Gode Ea sia: i defele, ilia da hamoi dagoi. Mousese da amo dunu idisu, Sainai hafoga: i soge ganodini hamoi.
20 Kuchokera mwa ana a Rubeni, mwana wamwamuna woyamba wa Israeli: Amuna onse a zaka makumi awiri kapena kupitirirapo, omwe akanatha kugwira ntchito ya usilikali, anawalemba mayina awo, mmodzimmodzi monga mwa mbiri ya mafuko awo ndi mabanja awo.
Dunu amo da ode 20 lalelegele esalu, amola amo baligi, amo da dadi gagumu defele ba: loba, amo huluane ilia fi amola sosogo fi defele dedei dagoi ba: i. Ilia da Liubene (Ya: igobe ea mano magobo) hidadea dedei. Idi huluane da agoane: - Fi ...Idisu Liubene ...46,500 Simiane ...59,300 Ga: de ...45,650 Yuda ...74,600 Isaga ...54,400 Sebiulane ...57,400 Ifala: ime ...40,500 Ma: na: se ...32,200 Bediamini ...35,400 Da: ne ...62,700 A: sie ...41,500 Na: fadalai ...53,400 Huluane gilisi idi da ...603,550
21 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Rubeni chinali 46,500.
22 Kuchokera mwa zidzukulu za Simeoni: Amuna onse a zaka makumi awiri kapena kupitirirapo, omwe akanatha kugwira ntchito ya usilikali anawalemba mayina awo, mmodzimmodzi monga mwa mbiri ya mafuko awo ndi mabanja awo.
23 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Simeoni chinali 59,300.
24 Kuchokera mwa zidzukulu za Gadi: Amuna onse a zaka makumi awiri kapena kupitirirapo, omwe akanatha kugwira ntchito ya usilikali anawalemba mayina awo monga mwa mbiri ya mafuko awo ndi mabanja awo.
25 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Gadi chinali 45, 650.
26 Kuchokera mwa zidzukulu za Yuda: Amuna onse a zaka makumi awiri kapena kupitirirapo, omwe akanatha kugwira ntchito ya usilikali anawalemba mayina awo monga mwa mbiri ya mafuko awo ndi mabanja awo.
27 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Yuda chinali 74, 600.
28 Kuchokera mwa zidzukulu za Isakara: Amuna onse a zaka makumi awiri kapena kupitirirapo, omwe akanatha kugwira ntchito ya usilikali anawalemba mayina awo monga mwa mbiri ya mafuko awo ndi mabanja awo.
29 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Isakara chinali 54,400.
30 Kuchokera mwa zidzukulu za Zebuloni: Amuna onse a zaka makumi awiri kapena kupitirirapo, omwe akanatha kugwira ntchito ya usilikali anawalemba mayina awo monga mwa mbiri ya mafuko awo ndi mabanja awo.
31 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Zebuloni chinali 57,400.
32 Kuchokera mwa ana aamuna a Yosefe: Kuchokera mwa zidzukulu za Efereimu: Amuna onse a zaka makumi awiri kapena kupitirirapo, omwe akanatha kugwira ntchito ya usilikali anawalemba mayina awo monga mwa mbiri ya mafuko awo ndi mabanja awo.
33 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Efereimu chinali 40,500.
34 Kuchokera mwa zidzukulu za Manase: Amuna onse a zaka makumi awiri kapena kupitirirapo, omwe akanatha kugwira ntchito ya usilikali anawalemba mayina awo monga mwa mbiri ya mafuko awo ndi mabanja awo.
35 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Manase chinali 32,200.
36 Kuchokera mwa zidzukulu za Benjamini: Amuna onse a zaka makumi awiri kapena kupitirirapo, omwe akanatha kugwira ntchito ya usilikali anawalemba mayina awo monga mwa mbiri ya mafuko awo ndi mabanja awo.
37 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Benjamini chinali 35,400.
38 Kuchokera mwa zidzukulu za Dani: Amuna onse a zaka makumi awiri kapena kupitirirapo, omwe akanatha kugwira ntchito ya usilikali anawalemba mayina awo monga mwa mbiri ya mafuko awo ndi mabanja awo.
39 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Dani chinali 62,700.
40 Kuchokera mwa zidzukulu za Aseri: Amuna onse a zaka makumi awiri kapena kupitirirapo, omwe akanatha kugwira ntchito ya usilikali anawalemba mayina awo monga mwa mbiri ya mafuko awo ndi mabanja awo.
41 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Aseri chinali 41,500.
42 Kuchokera mwa zidzukulu za Nafutali: Aamuna onse a zaka makumi awiri kapena kupitirirapo, omwe akanatha kugwira ntchito ya usilikali anawalemba mayina awo monga mwa mbiri ya mafuko awo ndi mabanja awo.
43 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Nafutali chinali 53,400.
44 Amenewa ndiwo anthu amene Mose ndi Aaroni anawawerenga mothandizidwa ndi atsogoleri khumi ndi awiri a Israeli, aliyense kuyimira fuko lake.
45 Aisraeli onse a zaka makumi awiri kapena kupitirirapo, omwe akanatha kugwira ntchito ya usilikali mʼgulu lankhondo la Israeli anawawerenga monga mwa mabanja awo.
46 Chiwerengero cha anthu onse pamodzi chinali 603,550.
47 Koma mabanja a fuko la Levi okha sanawawerenge pamodzi ndi ena.
Lifai fi da eno dunu fi ilima gilisili hame dedei.
48 Pakuti Yehova anawuza Mose kuti,
Bai Hina Gode da Mousesema amane sia: i dagoi,
49 “Usawerenge fuko la Levi kapena kuliphatikiza mʼkawundula wa Aisraeli.
“Di da dunu amo da dadi gagumu defele gala dedesea, Lifai fi dunu mae dedema.
50 Koma uyike Aleviwo kuti aziyangʼanira tenti yanga yopatulika, zipangizo zake ndi zonse zili mʼmenemo. Azinyamula tentiyo pamodzi ndi zipangizo zake zonse; azisamalira ndi kumanga misasa mozungulira tentiyo.
Be Lifai fi dunu amo ilia Na abula diasu amola hawa: hamosu liligi ganodini sali amo huluane ouligima: ne sia: ma. Ilia da Na abula diasu amola liligi huluane gaguli masunu. Ilia da amo abula diasu ganodini hawa: hamomu amola ilia fisu diasu amoga sisiga: le gagumu.
51 Pamene akusamutsa tentiyo, Alevi ndiwo aziyitsitsa, akafuna kuyimanganso, Alevi ndiwo aziyimiritsa. Wina aliyense amene adzayandikire tentiyo adzaphedwa.
Dilia fisisu mugululi masusa: dawa: sea, Lifai dunu da amo mugululi, gaguli ahoasea, gaheabolo sogebi amoga bu gagumu. Be eno dunu da abula diasuga gadenenewane doaga: sea, amo dunu medole legema.
52 Aisraeli azimanga matenti awo mʼmagulumagulu, munthu aliyense ku gulu lake pansi pa mbendera yake.
Be Isala: ili fi dunu huluane da fisisu higagale gaguli gagamu. Ilia da fi afae afae amanewane ilia abula diasu ilisu eso gosa: gisu abula haguduga gagumu.
53 Alevi nawonso, azimanga matenti awo mozungulira tenti yopatulika kuti chilango chisagwere Aisraeli onse. Ndipo Alevi aziyangʼanira ndi kusamalira tenti yopatulikayo.”
Be Lifai fi da Na Abula Diasu noga: le ouligima: ne, amogai sisiga: le fimu. Eno dunu da gadenene masea, Na ougi da Isala: ili fi fasa: besa: le, agoane noga: le ouligima.”
54 Choncho Aisraeli anachita monga Yehova analamulira Mose.
Amaiba: le, Isala: ili dunu da Hina Gode Ea Mousesema hamoma: ne sia: i huluane defele hamoi.

< Numeri 1 >