< Numeri 8 >

1 Yehova anawuza Mose kuti,
and to speak: speak LORD to(wards) Moses to/for to say
2 “Yankhula ndi Aaroni kuti pamene uyimika nyale zisanu ndi ziwiri, nyalezo ziziyaka kutsogolo kwa choyikapo nyale.”
to speak: speak to(wards) Aaron and to say to(wards) him in/on/with to ascend: establish you [obj] [the] lamp to(wards) opposite face: before [the] lampstand to light seven [the] lamp
3 Aaroni anachitadi zomwezo. Anayimika nyale ndi kuziyangʼanitsa kumene kunali choyikapo nyale monga Yehova analamulira Mose.
and to make: do so Aaron to(wards) opposite face: before [the] lampstand to ascend: establish lamp her like/as as which to command LORD [obj] Moses
4 Choyikapo nyalecho chinapangidwa motere: chinasulidwa kuchokera ku golide, kuyambira pa tsinde pake mpaka ku maluwa ake. Choyikapo nyalecho chinapangidwa monga momwe Yehova anaonetsera Mose.
and this deed: work [the] lampstand beating gold till thigh her till flower her beating he/she/it like/as appearance which to see: see LORD [obj] Moses so to make [obj] [the] lampstand
5 Yehova anawuza Mose kuti,
and to speak: speak LORD to(wards) Moses to/for to say
6 “Tenga Alevi pakati pa Aisraeli ndipo uwayeretse.
to take: take [obj] [the] Levi from midst son: descendant/people Israel and be pure [obj] them
7 Powayeretsa uchite izi: uwawaze madzi oyeretsa ndipo amete thupi lawo lonse ndi kuchapa zovala zawo kuti adziyeretse.
and thus to make: do to/for them to/for be pure them to sprinkle upon them water sin: punishment and to pass razor upon all flesh their and to wash garment their and be pure
8 Atenge ngʼombe yayimuna yayingʼono ndi chopereka cha chakudya cha ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta. Atengenso ngʼombe ina yayimuna, yayingʼono, ya chopereka chopepesera machimo.
and to take: take bullock son: young animal cattle and offering his fine flour to mix in/on/with oil and bullock second son: young animal cattle to take: take to/for sin: sin offering
9 Ubwere nawo Aleviwo kutsogolo kwa tenti ya msonkhano ndipo usonkhanitse gulu la Aisraeli.
and to present: bring [obj] [the] Levi to/for face: before tent meeting and to gather [obj] all congregation son: descendant/people Israel
10 Ubwere nawo pamaso pa Yehova, ndipo Aisraeli asanjike manja awo pa iwo.
and to present: bring [obj] [the] Levi to/for face: before LORD and to support son: descendant/people Israel [obj] hand their upon [the] Levi
11 Aaroni apereke Alevi aja pamaso pa Yehova ngati chopereka choweyula kuchokera kwa Aisraeli kuti akhale okonzeka kugwira ntchito ya Yehova.
and to wave Aaron [obj] [the] Levi wave offering to/for face: before LORD from with son: descendant/people Israel and to be to/for to serve: minister [obj] service: ministry LORD
12 “Alevi akatsiriza kusanjika manja awo pa mitu ya ngʼombe zazimuna, imodzi ikhale ya nsembe yopepesera machimo ndipo inayo ikhale ya nsembe yopsereza ya kwa Yehova, kupepesera machimo a Alevi.
and [the] Levi to support [obj] hand their upon head [the] bullock and to make: offer [obj] [the] one sin: sin offering and [obj] [the] one burnt offering to/for LORD to/for to atone upon [the] Levi
13 Uyimiritse Aleviwo pamaso pa Aaroni ndi ana ake aamuna ndipo uwapereke ngati nsembe yoweyula kwa Yehova.
and to stand: stand [obj] [the] Levi to/for face: before Aaron and to/for face: before son: child his and to wave [obj] them wave offering to/for LORD
14 Pochita zimenezi mudzapatula Alevi pakati pa Aisraeli ndipo Aleviwo adzakhala anga.
and to separate [obj] [the] Levi from midst son: descendant/people Israel and to be to/for me [the] Levi
15 “Utatha kuyeretsa ndi kupereka Aleviwo monga nsembe yoweyula, apite kukagwira ntchito yawo ku tenti ya msonkhano.
and after so to come (in): come [the] Levi to/for to serve: minister [obj] tent meeting and be pure [obj] them and to wave [obj] them wave offering
16 Iwo ndiwo Aisraeli amene aperekedwa kwathunthu kwa Ine. Ndawatenga kuti akhale anga mʼmalo mwa mwana wamwamuna aliyense woyamba kubadwa wa Mwisraeli aliyense wamkazi.
for to give: give to give: give they(masc.) to/for me from midst son: descendant/people Israel underneath: instead firstborn all womb firstborn all from son: descendant/people Israel to take: take [obj] them to/for me
17 Mwana aliyense wamwamuna woyamba kubadwa mu Israeli, kaya wa munthu kapena wa ziweto, ndi wanga. Pamene ndinakantha ana oyamba kubadwa ku Igupto, ndinawapatulira kwa Ine mwini.
for to/for me all firstborn in/on/with son: descendant/people Israel in/on/with man and in/on/with animal in/on/with day to smite I all firstborn in/on/with land: country/planet Egypt to consecrate: consecate [obj] them to/for me
18 Ndipo ndatenga Alevi mʼmalo mwa ana aamuna onse oyamba kubadwa mu Israeli.
and to take: take [obj] [the] Levi underneath: instead all firstborn in/on/with son: descendant/people Israel
19 Mwa Aisraeli onse, ndapereka Alevi kuti akhale mphatso kwa Aaroni ndi ana ake aamuna kugwira ntchito ya ku tenti ya msonkhano mʼmalo mwa Aisraeli onse kuti azikapereka nsembe yopepesera machimo, kuti mliri usadzaphe Aisraeli pamene ayandikira ku malo wopatulika.”
and to give: give [emph?] [obj] [the] Levi to give: give to/for Aaron and to/for son: child his from midst son: descendant/people Israel to/for to serve: minister [obj] service: ministry son: descendant/people Israel in/on/with tent meeting and to/for to atone upon son: descendant/people Israel and not to be in/on/with son: descendant/people Israel plague in/on/with to approach: approach son: descendant/people Israel to(wards) [the] holiness
20 Mose, Aaroni pamodzi ndi gulu lonse la Israeli anachita kwa Alevi monga momwe Yehova analamulira Mose.
and to make: do Moses and Aaron and all congregation son: descendant/people Israel to/for Levi like/as all which to command LORD [obj] Moses to/for Levi so to make: do to/for them son: descendant/people Israel
21 Alevi anadziyeretsa ndi kuchapa zovala zawo. Kenaka Aaroni anawapereka ngati nsembe yoweyula pamaso pa Yehova ndi kuchita nsembe yopepesera machimo yowayeretsa.
and to sin [the] Levi and to wash garment their and to wave Aaron [obj] them wave offering to/for face: before LORD and to atone upon them Aaron to/for be pure them
22 Zitatha zimenezi, Alevi anapita kukagwira ntchito yawo ku tenti ya msonkhano motsogozedwa ndi Aaroni ndi ana ake aamuna. Anachita kwa Alevi monga momwe Yehova analamulira Mose.
and after so to come (in): come [the] Levi to/for to serve: minister [obj] service: ministry their in/on/with tent meeting to/for face: before Aaron and to/for face: before son: child his like/as as which to command LORD [obj] Moses upon [the] Levi so to make: do to/for them
23 Yehova anawuza Mose kuti,
and to speak: speak LORD to(wards) Moses to/for to say
24 “Ntchito za Alevi ndi izi: Amuna a zaka 24 kapena kuposera pamenepa ndiye azibwera kudzagwira ntchito ku tenti ya msonkhano.
this which to/for Levi from son: aged five and twenty year and above [to] to come (in): come to/for to serve army: duty in/on/with service: ministry tent meeting
25 Koma akakwana zaka makumi asanu, apume pa ntchito yawo ya tsiku ndi tsiku ndi kulekeratu kugwira ntchitoyo.
and from son: aged fifty year to return: again from army: duty [the] service: ministry and not to serve: minister still
26 Atha kuthandiza abale awo kugwira ntchito za ku tenti ya msonkhano, koma iwowo asamagwire ntchitoyo. Mmenemu ndimo ugawire ntchito yomwe azigwira Alevi.”
and to minister [obj] brother: male-relative his in/on/with tent meeting to/for to keep: guard charge and service: ministry not to serve: minister thus to make: do to/for Levi in/on/with charge their

< Numeri 8 >