< Numeri 36 >

1 Atsogoleri a mabanja a fuko la Giliyadi, mwana wa Makiri, mwana wa Manase omwe anali ochokera ku fuko la ana a Yosefe anabwera ndi kuyankhula ndi Mose, atsogoleri ndi akuluakulu a mabanja a Aisraeli.
Un tie tēvu namu virsnieki no Gileāda bērnu cilts, - tas bija Mahira dēls, šis Manasus dēls, no Jāzepa dēlu ciltīm, - tie piegāja un runāja priekš Mozus un priekš tiem lielkungiem, Israēla bērnu tēvu namu virsniekiem, un sacīja:
2 Iwo anati, “Pamene Yehova analamula mbuye wanga kuti apereke dziko ngati cholowa kwa Aisraeli mwa maere, anakulamulani inu kupereka cholowa cha mʼbale wathu Zelofehadi kwa ana ake aakazi.
Tas Kungs ir pavēlējis manam kungam caur meslošanu izdot to zemi Israēla bērniem par īpašumu, un manam kungam caur To Kungu ir pavēlēts, mūsu brāļa Celofehada īpašumu dot viņa meitām.
3 Tsopano ngati akwatiwa ndi aamuna ochokera ku mafuko ena a mitundu ya Aisraeli, cholowa chawo chidzatengedwa kuchoka pa cholowa cha makolo athu ndipo adzachiwonjezera ku fuko limene akwatiwakolo. Ndipo gawo lina la cholowacho, lopatsidwa kwa ife lidzatengedwa.
Kad nu tās paliktu vienam no Israēla bērnu ciltīm par sievām, tad viņu īpašums taptu atrauts no mūsu tēvu īpašuma un pielikts tās cilts īpašumam, kurp tās noietu, un mūsu īpašuma daļa būtu mazināta.
4 Pamene chaka cha chikondwerero cha zaka makumi asanu, cha Aisraeli chafika, cholowa chawo chidzawonjezeredwa ku fuko limene iwo akwatiwako. Ndipo katundu wawo adzachotsedwa pa cholowa cha fuko la makolo athu.”
Un ja Israēla bērniem nāk gaviles gads, tad viņu īpašums taptu pielikts tās cilts īpašumam, kurp tās noietu, un no mūsu tēvu cilts īpašuma viņu īpašums ietu nost.
5 Tsono mwa lamulo la Yehova, Mose anapereka lamulo ili kwa Aisraeli: “Zimene ana a Yosefe akunena ndi zoona.
Tad Mozus pavēlēja Israēla bērniem pēc Tā Kunga vārda un sacīja: Jāzepa bērnu cilts runā pareizi.
6 Izi ndi zimene Yehova akulamula kwa ana aakazi a Zelofehadi: Atha kukwatiwa ndi aliyense amene angakondweretsedwe naye koma zingakhale bwino atakwatiwa mʼfuko la abambo awo
Šis ir tas vārds, ko Tas Kungs pavēlējis Celofehada meitām un sacījis: lai tās iet pie vīra, kā viņām patīk; bet lai kļūst par sievām sava tēva cilts radiem,
7 kuti cholowa cha Israeli chisapite ku fuko lina, pakuti Mwisraeli aliyense ayenera kusunga cholowa cha fuko la makolo ake.
Ka Israēla bērnu īpašums no cilts uz cilti netop pārcelts, jo Israēla bērniem būs turēties ikvienam pie savu tēvu cilts īpašuma.
8 Mwana wamkazi aliyense amene adzalandira cholowa cha dziko la fuko lililonse la Israeli ayenera kukwatiwa ndi munthu wa fuko la abambo ake.
Un ikviena meita, kam ir zemes daļa kādā Israēla bērnu ciltī, lai iet pie vīra pie kāda no savas tēva cilts radiem, ka Israēla bērni patur savu tēvu mantas daļu,
9 Cholowa chilichonse mu Israeli sichiyenera kupita ku fuko lina, popeza fuko lililonse la Israeli liyenera kusunga cholowa chimene linalandira.”
Un īpašums netop pārcelts no vienas cilts uz otru; jo Israēla bērnu ciltis lai turas ikviena pie sava īpašuma.
10 Choncho ana aakazi a Zelofehadi anachita monga Yehova analamulira Mose.
Kā Tas Kungs Mozum bija pavēlējis, tā Celofehada meitas darīja.
11 Ana aakazi a Zelofehadi amene ndi Mahila, Tiriza, Hogila, Milika ndi Nowa, anakwatiwa ndi asuweni awo a ku mbali ya abambo awo.
Jo Maēla, Tirca un Hagla un Milka un Noa, Celofehada meitas, kļuva par sievām sava tēva brāļa dēliem;
12 Anakwatiwa mʼmafuko a zidzukulu za Manase mwana wa Yosefe, ndipo cholowa chawo chinakhalabe mʼfuko la abambo awo.
Jāzepa dēla Manasus bērnu radiem tās kļuva par sievām; tā viņu īpašums palika pie viņu tēva radu cilts.
13 Awa ndi malamulo ndi malangizo amene Yehova anapereka kwa Aisraeli kupyolera mwa Mose ku chigwa cha Mowabu mʼmbali mwa Yorodani, ku Yeriko.
Šie ir tie likumi un tās tiesas, ko Tas Kungs caur Mozu Israēla bērniem ir pavēlējis Moaba klajumos pie Jardānes pret Jēriku.

< Numeri 36 >