< Numeri 34 >

1 Yehova anawuza Mose kuti,
INkosi yasikhuluma kuMozisi isithi:
2 “Lamula Aisraeli ndipo uwawuze kuti, ‘Pamene mulowa mʼdziko la Kanaani, dziko lomwe lidzaperekedwa kwa inu ngati cholowa chanu, lidzakhale ndi malire awa:
Laya abantwana bakoIsrayeli uthi kubo: Lapho lingena elizweni leKhanani, leli lizakuba yilizwe elizawela kini libe yilifa, ilizwe leKhanani, ngokwemingcele yalo.
3 “‘Chigawo cha kummwera kwa dziko lanu chidzayambira ku chipululu cha Zini motsatana ndi malire a Edomu. Kummawa malire anu a kummwera adzayambira kummawa, kumathero a Nyanja ya Mchere.
Legumbi lenu leningizimu lizakuba kusukela enkangala yeZini, enhlangothini zeEdoma. Njalo uzakuba ngumngcele wenu weningizimu kusukela ekucineni kolwandle lwetshwayi empumalanga.
4 Malirewo adzapita kummwera ndipo adzakwera phiri la Akirabimu mpaka ku Zini. Mathero ake adzakhala kummwera kwa Kadesi-Baranea. Ndipo adzapitenso ku Hazari Adari mpaka kukafika ku Azimoni,
Umngcele wenu uzajika uvela eningizimu usiya emqansweni weAkirabimi, wedlulele eZini; lokuphuma kwawo kuzavela eningizimu kuye eKadeshi-Bhaneya; uzaphuma uye eHazari-Adari, wedlulele eAzimoni.
5 kumene malirewo adzakhote kuchokera ku Azimoni mpaka ku khwawa la ku Igupto ndi kukathera ku Nyanja Yayikulu.
Lomngcele uzajika uvela eAzimoni uye esifuleni seGibhithe; lokuphuma kwawo kuzakuba selwandle.
6 “‘Malire anu a ku madzulo adzakhala ku gombe la Nyanja Yayikulu. Amenewo ndiwo adzakhale malire anu a ku madzulo.
Mayelana lomngcele wentshonalanga, ulwandle olukhulu luzakuba ngumngcele wenu; lona luzakuba ngumngcele wenu ngentshonalanga.
7 “‘Malire anu a kumpoto, mzere wake uyambire ku Nyanja Yayikulu mpaka ku phiri la Hori
Lalokhu kuzakuba ngumngcele wenu wenyakatho: Kusukela elwandle olukhulu lizazidwebela intaba yeHori;
8 ndi kuchokera ku phiri la Hori mpaka ku Lebo Hamati. Malirewa apite ku Zedadi,
kusukela entabeni yeHori lizadweba umngcele oya ekungeneni kweHamathi, lokuphuma komngcele kuye eZedadi.
9 ndi kupitirira mpaka ku Ziforoni ndi kukathera ku Hazari-Enani. Awa ndiwo adzakhale malire anu a kumpoto.
Lomngcele uzaphuma uye eZifroni, lokuphuma kwawo kuzakuba eHazari-Enani. Lo uzakuba ngumngcele wenu wenyakatho.
10 “‘Za malire anu a kummawa, mulembe mzere kuchokera ku Hazari-Enani mpaka kukafika ku Sefamu.
Njalo lizazidwebela umngcele wenu wempumalanga kusukela eHazari-Enani kusiya eShefamu;
11 Malirewo adzatsikire ku Sefamu mpaka ku Ribila cha kummawa kwa Aini ndi kupitirira mpaka ku matsitso a cha kummawa kwa Nyanja ya Kinereti.
lomngcele uzakwehla uvela eShefamu uye eRibila empumalanga kweAyini, lomngcele wehle ufike eceleni kolwandle lweKinerethi ngempumalanga.
12 Tsono malirewo adzatsika motsatana ndi Yorodani ndi kukathera ku Nyanja ya Mchere. “‘Limeneli lidzakhala dziko lanu ndi malire ake mbali zonse.’”
Umngcele uzakwehlela-ke eJordani, lokuphuma kwawo kuzakuba solwandle lwetshwayi. Leli lizakuba yilizwe lenu ngemingcele yalo inhlangothi zonke.
13 Ndipo Mose analamula Aisraeli kuti, “Limeneli ndi dziko limene mudzalilandira pochita maere kuti likhale cholowa chanu. Yehova analamula kuti liperekedwe ku mafuko asanu ndi anayi ndi theka,
UMozisi waselaya abantwana bakoIsrayeli esithi: Leli yilizwe elizakudla ilifa lalo ngenkatho, iNkosi elaye ngalo ukulinika izizwe eziyisificamunwemunye lengxenye yesizwe.
14 chifukwa mabanja a fuko la Rubeni, fuko la Gadi, ndi theka la fuko la Manase analandiriratu cholowa chawo.
Ngoba isizwe sabantwana bakoRubeni ngezindlu zaboyise, lesizwe sabantwana bakoGadi ngezindlu zaboyise zemukele, lengxenye yesizwe sakoManase yemukele ilifa layo.
15 Mafuko awiriwa pamodzi ndi theka la fuko la Manase analandiriratu cholowa chawo patsidya pa mtsinje wa Yorodani ku Yeriko cha kummawa kotulukira dzuwa.”
Izizwe ezimbili lengxenye yesizwe zemukele ilifa lazo nganeno kweJordani, eJeriko, empumalanga, lapho okuphuma khona ilanga.
16 Yehova anawuza Mose kuti,
INkosi yasikhuluma kuMozisi isithi:
17 “Awa ndi mayina a anthu amene adzakugawireni dzikoli kuti likhale cholowa chanu: wansembe Eliezara ndi Yoswa mwana wa Nuni.
La ngamabizo amadoda azalabela ilizwe libe yilifa: UEleyazare umpristi loJoshuwa indodana kaNuni.
18 Musankhe mtsogoleri mmodzi kuchokera ku fuko lililonse kuti athandize kugawa dzikolo.
Njalo lizathatha isiphathamandla kuleso lalesosizwe ukwehlukanisa ilizwe libe yilifa.
19 Mayina awo ndi awa: Kalebe mwana wa Yefune, wochokera ku fuko la Yuda,
Lala ngamabizo amadoda: Esizweni sakoJuda, uKalebi indodana kaJefune.
20 Semueli mwana wa Amihudi, wochokera ku fuko la Simeoni;
Lesizweni sabantwana bakoSimeyoni, uShemuweli indodana kaAmihudi.
21 Elidadi mwana wa Kisiloni, wochokera ku fuko la Benjamini;
Esizweni sakoBhenjamini, uElidadi indodana kaKisiloni.
22 Buki mwana wa Yogili, mtsogoleri wochokera ku fuko la Dani;
Lesizweni sabantwana bakoDani, isiphathamandla uBuki indodana kaJogili.
23 Hanieli mwana wa Efodi, mtsogoleri wochokera ku fuko la Manase, mwana wa Yosefe;
Ebantwaneni bakoJosefa, esizweni sabantwana bakoManase, isiphathamandla uHaniyeli indodana kaEfodi.
24 Kemueli mwana wa Sifitani, mtsogoleri wochokera ku fuko la Efereimu, mwana wa Yosefe.
Lesizweni sabantwana bakoEfrayimi, isiphathamandla uKemuweli indodana kaShifitani.
25 Elizafani mwana wa Parinaki, mtsogoleri wochokera ku fuko la Zebuloni;
Lesizweni sabantwana bakoZebuluni, isiphathamandla uElizafani indodana kaParinaki.
26 Palitieli mwana wa Azani, mtsogoleri wochokera ku fuko la Isakara,
Lesizweni sabantwana bakoIsakari, isiphathamandla uPalitiyeli indodana kaAzani.
27 Ahihudi mwana wa Selomi, mtsogoleri wochokera ku fuko la Aseri;
Lesizweni sabantwana bakoAsheri, isiphathamandla uAhiyudi indodana kaShelomi.
28 Pedaheli mwana wa Amihudi, mtsogoleri wochokera ku fuko la Nafutali.”
Lesizweni sabantwana bakoNafithali, isiphathamandla uPedaheli indodana kaAmihudi.
29 Awa ndiwo mayina a anthu amene Yehova analamula kuti agawe cholowa cha Aisraeli mʼdziko la Kanaani.
Yibo labo iNkosi eyabalaya ukwehlukanisela abantwana bakoIsrayeli ilifa elizweni leKhanani.

< Numeri 34 >