< Numeri 31 >
1 Yehova anawuza Mose kuti,
Mluvil opět Hospodin k Mojžíšovi, řka:
2 “Uwabwezere zoyipa Amidiyani chifukwa cha zimene anachitira Aisraeli. Ukatha kuchita zimenezi, iwe udzamwalira.”
Pomsti prvé synů Izraelských nad Madianskými, a potom připojen budeš k lidu svému.
3 Ndipo Mose anati kwa Aisraeli, “Perekani zida kwa ena mwa anthu anu kuti akamenyane ndi Amidiyani ndi kuwabwezera choyipa mʼmalo mwa Yehova.
Mluvil tedy Mojžíš k lidu, řka: Vypravte některé z sebe k boji, aby šli proti Madianským a vykonali pomstu Hospodinovu nad nimi.
4 Mutumize ku nkhondoko amuna 1,000 kuchokera ku fuko lililonse la Aisraeli.”
Po tisíci z pokolení, ze všech pokolení Izraelských vyšlete k boji.
5 Choncho amuna okwana 12,000 anatenga zida kukonzekera nkhondo, anthu 1,000 kuchokera ku fuko lililonse la Aisraeli.
I vydáno jest z mnohých tisíců Izraelských po tisíci z každého pokolení, totiž dvanácte tisíců způsobných k boji.
6 Mose anawatumiza ku nkhondo, anthu 1,000 kuchokera ku fuko lililonse pamodzi ndi Finehasi mwana wa Eliezara wansembe amene ananyamula zipangizo zochokera ku malo wopatulika ndi malipenga okaliza.
I poslal je Mojžíš po tisíci z každého pokolení k boji, a Fínesa syna Eleazara kněze s nimi; a nádoby svaté i trouby k troubení byly v ruce jeho.
7 Iwo anamenyana ndi Amidiyani monga momwe Yehova analamulira Mose ndipo anapha mwamuna aliyense.
Tedy bojovali proti Madianským, jakož byl přikázal Hospodin Mojžíšovi, a zbili všecky pohlaví mužského.
8 Mwa anthu ophedwawo munali Evi, Rekemu, Zuri, Huri ndi Reba, mafumu asanu a Amidiyani. Ndipo anaphanso ndi lupanga Balaamu mwana wa Beori.
Pobili také krále Madianské mezi jinými, kteréž porazili, totiž Evi, Rekem, Sur, Hur a Rebe, pět králů Madianských; Baláma také, syna Beorova, zabili mečem.
9 Aisraeli anagwira ukapolo amayi a Chimidiyani ndi ana awo ndipo analandanso ngʼombe, ziweto zawo zina zonse ndi katundu wawo yense.
A zajali synové Izraelští ženy Madianské i děti jejich; všecka hovada jejich, i všechny dobytky jejich, a všecka zboží jejich pobrali.
10 Anawotcha mizinda yonse imene Amidiyani ankakhalamo pamodzi ndi misasa yawo yonse.
Všecka také města jejich, v kterýchž svá obydlí měli, i všecky hrady jejich vypálili ohněm.
11 Anatenga zonse zimene analanda ku nkhondoko, anthu ndi zoweta zomwe.
A všecku loupež i všecky kořisti pobravše, lidi i hovada,
12 Ndipo anabwera nawo akapolowo ndi zolanda ku nkhondozo kwa Mose ndi kwa wansembe Eliezara ndi kwa gulu lonse la Aisraeli ku misasa yawo ku chigwa cha Mowabu, mʼmbali mwa mtsinje wa Yorodani ku Yeriko.
Vedli je k Mojžíšovi a k Eleazarovi knězi, a ke všemu množství synů Izraelských, i zajaté i kořisti, i loupeže, k vojsku na roviny Moábské, kteréž jsou při Jordánu naproti Jerichu.
13 Mose, wansembe Eliezara ndi atsogoleri onse a gululo anapita kukakumana nawo kunja kwa misasa.
I vyšli Mojžíš a Eleazar kněz a všecka knížata shromáždění proti nim ven za stany.
14 Mose anakwiya nawo akuluakulu a magulu a ankhondowo: olamulira 1,000 ndi olamulira 100, amene ankachokera ku nkhondo.
Tedy rozhněval se Mojžíš na vůdce vojska, hejtmany nad tisíci a setníky, kteříž se navraceli z boje,
15 Iye anafunsa kuti, “Kodi nʼchifukwa chiyani mwawaleka amoyo amayi onsewa?”
A řekl jim Mojžíš: A což jste zachovali všecky ženy?
16 Paja iwo ndi amene ankatsatira uphungu wa Balaamu ndiponso ndi amene anachititsa Aisraeli kuti asiye Yehova pa zimene zinachitika ku Peori, kotero mliri unagwera anthu a Yehova.
Ej, onyť jsou hle synům Izraelským, podlé rady Balámovy, daly příčinu k přestoupení proti Hospodinu, při modlářství Fegor, pročež ona rána přišla byla na lid Hospodinův.
17 Tsopano iphani munthu wamwamuna aliyense. Ndiponso iphani mayi aliyense amene anagonapo ndi mwamuna,
Protož nyní zmordujte všecky děti pohlaví mužského, a všecky ženy, kteréž poznaly muže.
18 koma sungani mtsikana aliyense amene sanagonepo ndi mwamuna.
Všecky pak panny, kteréž nepoznaly muže, zachovejte sobě živé.
19 “Inu nonse amene mwaphapo wina wake, kapena kukhudza aliyense amene anaphedwa mukhale kunja kwa msasa masiku asanu ndi awiri. Pa tsiku lachitatu mudziyeretse nokha pamodzi ndi akapolo anu.
Vy pak zůstaňte vně za stany za sedm dní; všickni, kteřížkoli jste někoho zabili, aneb kteříž jste se zabitého dotkli, očišťovati se budete dne třetího a dne sedmého, sebe i zajaté své.
20 Muyeretsenso zovala zanu ndi china chilichonse chopangidwa ndi chikopa, ubweya wa mbuzi kapenanso ndi mtengo.”
Všeliké také roucho a všecky věci kožené, i všelijaké dílo z srstí kozích, i všelikou nádobu dřevěnou očistíte.
21 Tsono wansembe Eliezara anati kwa asilikali amene anapita ku nkhondo aja, “Lamulo limene Yehova anapereka kwa Mose ndi ili:
I řekl Eleazar kněz vojákům, kteříž byli šli k boji: Toto jest ustanovení zákona, kteréž byl přikázal Hospodin Mojžíšovi.
22 Golide, siliva, mkuwa, chitsulo, chiwaya, mtovu
Zlato však, stříbro, měď, železo, cín a olovo,
23 ndi china chilichonse chimene sichingapse ndi moto muchidutsitse pa moto, ndipo chidzayeretsedwa. Komanso chiyeretsedwe ndi madzi oyeretsa. Ndipo chilichonse chimene chingapse ndi moto muchidutsitse mʼmadzimo.
A cožkoli trpí oheň, ohněm přepálíte, a přečištěno bude, však tak, když vodou očišťování obmyto bude; což pak nemůže ohně strpěti, to skrze vodu protáhnete.
24 Pa tsiku lachisanu ndi chiwiri muchape zovala zanu ndipo mudzayera. Mukatero mutha kulowa mu msasa.”
Zpéřete také roucha svá v den sedmý, a čistí budete; a potom vejdete do stanů.
25 Yehova anawuza Mose kuti,
Mluvil i to Hospodin k Mojžíšovi, řka:
26 “Iwe ndi wansembe Eliezara ndiponso akuluakulu a mabanja a anthuwa, muwerenge anthu onse ndi ziweto zomwe zinagwidwa ku nkhondo.
Sečti summu kořistí zajatých, tak z lidí jako z hovad, ty a Eleazar kněz, a přední z čeledi otců v lidu;
27 Mugawe zolanda ku nkhondozo magawo awiri, lina la ankhondo amene anapita ku nkhondo, lina la anthu onse.
A rozdělíš ty kořisti na dva díly, jeden mezi vojáky, kteříž byli vytáhli na vojnu, a druhý mezi všecko shromáždění.
28 Pa gawo la ankhondowo, mutengeko gawo la Yehova, pa zofunkha 500 zilizonse mutengeko chimodzi, pa akapolo, ngʼombe, bulu ndi nkhosa.
A vezmeš díl na Hospodina od mužů bojovných, kteříž byli vyšli na vojnu, jednu duši z pěti set, buďto z lidí neb z hovad, neb z oslů, neb z ovcí.
29 Utenge zimenezo pa theka la gawo la ankhondowo ndipo upereke kwa wansembe Eliezara kuti zikhale zopereka zanu kwa Yehova.
Z jejich polovice to vezmete, a dáte Eleazarovi knězi obět vzhůru pozdvižení Hospodinu.
30 Kuchokera pa theka la gawo la Aisraeli, utengeko cholanda chimodzi pa makumi asanu aliwonse, pa anthu, ngʼombe, abulu, nkhosa, mbuzi kapena zoweta zina. Uzipereke kwa Alevi amene ntchito yawo ndi yosamalira tenti ya Yehova.”
Z polovice pak té, kteráž jest synů Izraelských, vezmeš jedno z padesáti, buďto z lidí neb z volů, neb z oslů, neb z ovcí, a tak ze všelijakých hovad, a dáš to Levítům, držícím stráž příbytku Hospodinova.
31 Ndipo Mose ndi wansembe Eliezara anachita monga Yehova analamulira Mose.
I učinil Mojžíš a Eleazar kněz tak, jakž byl rozkázal Hospodin Mojžíšovi.
32 Zotsala pa zolanda ku nkhondo zimene ankhondowo anatenga zinali nkhosa 675,000,
A bylo té kořisti z pozůstalé ještě loupeže, kteréž nabral lid válečný, ovec šestkrát sto tisíc, sedmdesáte a pět tisíců;
A volů sedmdesáte a dva tisíce;
Oslů šedesáte a jeden tisíců;
35 ndi atsikana omwe sanagonepo ndi mwamuna 32,000.
A panen, kteréž mužů nepoznaly, všech dva a třidceti tisíců.
36 Gawo la ankhondo amene anapita ku nkhondo linali: nkhosa 337,500,
Dostala se pak polovice jedna na díl těm, kteříž byli vytáhli na vojnu, dobytka drobného v počtu třikrát sto tisíc, třidceti a sedm tisíců a pět set,
37 mwa zimenezi gawo la Yehova linali 675;
A na díl vzatý Hospodinu dobytka drobného šest set, sedmdesáte pět.
38 ngʼombe zinalipo 36,000 ndipo gawo la Yehova linali 72;
A z volů šest a třidceti tisíců, z nichž přišlo na díl Hospodinu sedmdesáte a dva.
39 abulu analipo 30,500 ndipo gawo la Yehova linali 61;
Oslů také třidceti tisíc a pět set, z nichž přišlo na díl Hospodinu šedesáte a jeden.
40 anthu analipo 16,000 ndipo gawo la Yehova linali 32.
A lidí šestnácte tisíců, z nichž přišlo na díl Hospodinu třidceti a dvě duše.
41 Mose anapereka kwa wansembe Eliezara gawo limene linali loyenera kupereka kwa Yehova monga momwe Yehova analamulira Mose.
Dal tedy Mojžíš díl oddělený Hospodinu Eleazarovi knězi, jakž byl přikázal Hospodin Mojžíšovi.
42 Pa gawo la Aisraeli, Mose anapatula theka limodzi kuchotsa pa zolanda ku nkhondo zonse zimene zinabwera ndi ankhondo aja.
Z druhé pak polovice synů Izraelských, kterouž vzal Mojžíš od těch mužů, jenž bojovali,
43 Tsono gawo la Aisraeli linali ili: nkhosa 337,500,
(A bylo té polovice k shromáždění přináležející z ovec třikrát sto tisíc, třidceti a sedm tisíců a pět set;
Volů třidceti šest tisíců;
Oslů třidceti tisíců a pět set;
A lidí šestnácte tisíců; )
47 Kuchoka pa gawo la Aisraelilo, Mose anatengapo chimodzi pa zolanda ku nkhondo makumi asanu aliwonse, anthu ndi nyama, ndipo anazipereka kwa Alevi amene ankayangʼanira tenti ya Yehova monga Yehova analamulira Mose.
Z té tedy polovice synů Izraelských vzal Mojžíš po jednom zajatém z padesáti, tak z lidí jako z hovad, a dal to Levítům, držícím stráž příbytku Hospodinova, jakž byl přikázal Hospodin Mojžíšovi.
48 Pamenepo omwe ankayangʼanira magulu a ankhondo olamulira 1,000 ndi olamulira 100 anabwera kwa Mose,
Tedy přistoupili k Mojžíšovi vývodové vojska, hejtmané nad tisíci a setníci,
49 iwo anati kwa iye, “Ife anthu anu tawerenga ankhondo amene timawalamulira. Palibe munthu ndi mmodzi yemwe amene wasowa.
A řekli jemu: My služebníci tvoji sečtli jsme počet bojovníků, kteréž jsme měli pod spravou naší, a neubyl ani jeden z nás.
50 Ndipo tabweretsa zopereka kwa Yehova zimene munthu aliyense anapeza: ziwiya zagolide, zibangiri, zigwinjiri, mphete zosindikizira, ndolo ndi mikanda kuti tichitire mwambo wopepesera machimo pamaso pa Yehova.”
A protož obětujeme obět Hospodinu, každý z toho, čehož jest dostal, nádobí zlaté, zápony, náramky, prsteny, náušnice a řetízky, aby očištěny byly duše naše před Hospodinem.
51 Ndipo Mose ndi wansembe Eliezara analandira kuchokera kwa atsogoleriwo golide pamodzi ndi zipangizo zonse zosula.
Vzal tedy Mojžíš a Eleazar kněz od nich to zlato všelikého díla řemeslného.
52 Golide yense wochokera kwa atsogoleri a 1,000 ndi atsogoleri a 100 zomwe Mose ndi Eliezara anapereka ngati mphatso kwa Yehova zinali zolemera makilogalamu 200.
Bylo pak všeho zlata odděleného, kteréž obětováno Hospodinu, šestnácte tisíců, sedm set a padesáte lotů, od hejtmanů nad tisíci a od setníků.
53 Wankhondo aliyense anatenga zomwe analanda yekha ku nkhondo.
(Muži zajisté bojovní, což loupeží vzali, to sobě měli.)
54 Mose ndi Eliezara wansembe analandira golide kuchokera kwa atsogoleri a 1,000 ndi atsogoleri a 100 ndi kukamuyika mu tenti ya msonkhano ngati chikumbutso cha Aisraeli pamaso pa Yehova.
A vzavše Mojžíš a Eleazar kněz od hejtmanů nad tisíci a setníků to zlato, vnesli je do stánku úmluvy, na památku synů Izraelských před Hospodinem.