< Numeri 28 >

1 Yehova anawuza Mose kuti,
Nagsao ni Yahweh kenni Moises ket kinunana,
2 “Lamula Aisraeli kuti, ‘Onetsetsani kuti mukupereka kwa Ine pa nthawi yoyikika, chopereka cha chakudya chotentha pa moto monga fungo lokoma kwa Ine.’
“Bilinem dagiti tattao ti Israel ket ibagam kadakuada, 'Masapul a mangidatonkayo kaniak kadagiti naituding a tiempo iti taraon kadagiti datonko a maipuor a mangipaay iti nabanglo nga ayamuom para kaniak.'
3 Awuze kuti, ‘Nsembe ya chakudya imene muzipereka pa moto kwa Yehova tsiku ndi tsiku ndi iyi: Ana ankhosa a chaka chimodzi awiri, wopanda chilema.
Masapul nga ibagam pay kadakuada, 'Daytoy ti daton a maipuor a masapul nga idatonyo kenni Yahweh—dagiti kalakian nga urbon a karnero nga agtawen iti maysa nga awan mulitna, dua iti inaldaw, kas inaldaw a daton a maipuor.
4 Mmawa muzipereka mwana wankhosa mmodzi ndipo winayo madzulo.
Maysa nga urbon a karnero iti masapul a mangidatagkayo iti agsapa, ken ti maysa ket masapul nga idatagyo iti rabii.
5 Muziperekanso kilogalamu imodzi ya ufa wosalala wosakaniza ndi lita imodzi ya mafuta a olivi.
Masapul a mangidatagkayo iti apagkapullo iti maysa nga efa ti napino nga arina a sagut a bukel a nalaokan iti apagkapat a hin ti puro a lana ti olibo.
6 Iyi ndi nsembe yopsereza ya tsiku ndi tsiku imene analamula pa phiri la Sinai kuti ikhale fungo lokoma, nsembe yopsereza pa moto yopereka kwa Yehova.
Daytoy ti inaldaw a daton a maipuor a naibilin idi idiay bantay Sinai a mangipaay iti nabanglo nga ayamuom, maysa a daton a maipuor para kenni Yahweh.
7 Chopereka chachakumwa chikhale lita imodzi yachakumwa chaukali pa nkhosa iliyonse. Muzithira pamalo opatulika, kupereka kwa Yehova.
Ti maipakuyog iti daytoy a daton a mainom ket masapul nga apagkapat iti hin iti maysa kadagiti urbon ti karnero. Masapul nga ibukbokyo iti nasantoan a lugar ti sagut a mainom a naingel nga arak kenni Yahweh.
8 Muzipereka mwana wankhosa winayo madzulo, pamodzi ndi chopereka chachakudya monga poyamba paja ndi chopereka chachakumwa monga mmawa. Ichi ndi chopereka chachakudya, fungo lokoma kwa Yehova.’”
Ti sabali a karnero a masapul nga idatagyo iti rabii a mapakuyogan manen iti sagut a bukel a kasla iti naidaton iti agsapa. Masapul met a mangidatagkayo iti sabali a sagut a mainom a nayon daytoy, maysa a daton a maipuor, a mangipaay iti nabanglo nga ayamuom para kenni Yahweh.
9 “‘Pa tsiku la Sabata, muzipereka nsembe ana ankhosa awiri a chaka chimodzi wopanda chilema, pamodzi ndi chopereka chachakumwa ndi chopereka chachakudya chokwana makilogalamu awiri a ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta.
Iti Aldaw a Panaginana, masapul a mangidatagkayo iti dua a kalakian nga urbon a karnero nga agtawen iti maysa nga awan mulitna, ken dua nga apagkapullo iti maysa nga efa iti napino nga arina a kas sagut a bukel a nalaokan iti lana, ken ti sagut a mainom a kadua daytoy.
10 Iyi ndi nsembe yopsereza ya pa Sabata iliyonse, kuwonjezera pa nsembe yopsereza ya nthawi zonse ndi chopereka chake chachakumwa.’”
Daytoy ti daton a maipuor para iti tunggal Aldaw ti Panaginana, a kas mainayon kadagiti inaldaw a daton a maipuor ken ti daton a mainom a kadua daytoy.
11 “Pa tsiku loyamba la mwezi uliwonse muzipereka kwa Yehova nsembe yopsereza ya ana angʼombe aamuna awiri, nkhosa yayimuna imodzi, ana ankhosa aamuna asanu ndi awiri a chaka chimodzi, onse wopanda chilema.
Iti rugrugi ti tunggal bulan, masapul a mangidatagkayo kadagiti daton a maipuor kenni Yahweh. Masapul a mangidatagkayo iti dua a bumbumaro a baka, maysa a kalakian a karnero, ken pito a kalakian nga urbon iti karnero nga agtawen iti maysa ken awan ti mulitna.
12 Pa ngʼombe yayimuna iliyonse pakhale chopereka cha chakudya cha makilogalamu atatu a ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta; ndi nkhosa yayimuna, chopereka cha chakudya cha makilogalamu awiri a ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta;
Masapul pay a mangidatagkayo iti tallo nga apagkapullo ti napino nga arina a kas sagut a bukbukel a nalaokan ti lana para iti tunggal kalakian a baka, ken dua nga agpagkapullo ti napino nga arina a kas daton a nalaokan iti lana para iti maysa a kalakian a karnero.
13 ndipo pa mwana wankhosa aliyense, chopereka cha ufa wa kilogalamu imodzi ya ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta, izi ndi za nsembe yopsereza, fungo lokoma, nsembe yotentha pa moto ya kwa Yehova.
Masapul pay a mangidatagkayo iti apagkapullo ti maysa efa ti napino nga arina a nalaokan ti lana a kas daton para iti tunggal maysa a karnero. Daytoy ti daton a maipuor a mangipaay iti nabanglo nga ayamuom, maysa a daton a maipuor para kenni Yahweh.
14 Pa ngʼombe yayimuna iliyonse pakhale chopereka cha chakumwa cha malita awiri a vinyo; ndipo pa nkhosa yayimuna, lita limodzi ndi theka, ndipo pa mwana wankhosa, lita limodzi. Iyi ndi nsembe yopsereza ya mwezi ndi mwezi yoperekedwa pa mwezi watsopano mʼkati mwa chaka.
Ti daton a mainom dagiti tattao ket masapul a kagudua a hin nga arak para iti maysa a kalakian a baka, ti apagkatlo ti hin nga arak para iti maysa a kalakian a karnero ken ti apagkapat iti hin para iti maysa nga urbon a karnero. Daytoy ti daton a maipuor iti binulan iti makatawen.
15 Powonjezera pa nsembe yopsereza ya nthawi zonse ndi chopereka chake cha chakumwa, mbuzi yayimuna imodzi iperekedwe kwa Yehova ngati nsembe yopepesera machimo.
Maysa a kalakian a kalding ti masapul a maidaton kenni Yahweh gapu iti basol. Mainayonto daytoy kadagiti inaldaw a daton a maipuor ken dagiti sagut a mainom.
16 “‘Pa tsiku la 14 la mwezi woyamba muzichita Paska wa Yehova.
Iti umuna a bulan, iti maika-sangapulo ket uppat nga aldaw ti bulan, rambakan ti Ilalabas ni Yahweh.
17 Pa tsiku la 15 la mwezi womwewo pazikhala chikondwerero. Muzidya buledi wopanda yisiti kwa masiku asanu ndi awiri.
Iti maika-sangapulo ket lima nga aldaw iti daytoy a bulan, maangay ti fiesta. Iti las-ud ti pito nga aldaw, masapul a kanen ti tinapay nga awan lebadurana.
18 Pa tsiku loyamba muzichita msonkhano wopatulika ndipo musamagwire ntchito iliyonse.
Iti umuna nga aldaw, masapul nga agguummong ti nasantoan a taripnong a mangdayaw kenni Yahweh. Masapul a saankayo nga agtrabaho iti dayta nga aldaw.
19 Koma muzipereka kwa Yehova nsembe yotentha pa moto, nsembe yopsereza ya ana angʼombe aamuna awiri, nkhosa yayimuna imodzi ndi ana ankhosa asanu ndi awiri aamuna a chaka chimodzi, onsewo wopanda chilema.
Nupay kasta, masapul a mangidatagkayo iti daton a maipuor, maysa a daton a maipuor para kenni Yahweh. Masapul a mangidatagkayo iti dua a bumbumaro a baka, maysa a kalakian a karnero, ken pito a kalakian nga urbon a karnero nga agtawen iti maysa nga awan ti mulitna.
20 Pamodzi ndi ngʼombe yayimuna iliyonse, muzikonza chopereka cha chakudya cha makilogalamu atatu a ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta; makilogalamu awiri pa nkhosa yayimuna iliyonse.
Masapul a mangidatagkayo iti daton a bukel a tallo nga apagkapullo iti maysa nga efa ti napino nga arina a nalaokan ti lana a maipakuyog iti baka, ken dua nga apagkapullo ti maipakuyog iti kalakian a karnero.
21 Kilogalamu imodzi pa mwana wankhosa aliyense mwa ana ankhosa asanu ndi awiri aja.
Iti tunggal maysa kadagiti pito a karnero, masapul a mangidatagkayo iti apagkapullo iti maysa nga efa ti napino nga arina a nalaokan ti lana,
22 Muziphatikizapo mbuzi yayimuna monga nsembe yopepesera machimo anu.
ken maysa a kalakian a kalding a kas daton gapu iti basol a pakapakawananyo.
23 Muzikonza zimenezi nthawi zonse, powonjezera pa nsembe yopsereza ya mmawa.
Masapul nga idatagyo dagitoy a mainayon kadagiti inaldaw a daton a maipuor a kasapulan tunggal agsapa.
24 Motere muzikonza chakudya cha nsembe yopsereza ya tsiku ndi tsiku pa masiku asanu ndi awiri ngati fungo lokomera Yehova. Zimenezi ziziperekedwa kuwonjezera pa nsembe yopsereza ya nthawi zonse pamodzi ndi nsembe yachakumwa.
Kas nailadawan ditoy, masapul nga idatagyo dagitoy a daton iti inaldaw, iti las-ud iti pito nga aldaw ti Ilalabas, ti taraon ti daton a maipuor, a nabanglo nga ayamuom para kenni Yahweh. Masapul a maidatag daytoy a mainayon kadagiti inaldaw a daton a maipuor ken iti sagut a mainom iti daytoy.
25 Pa tsiku lachisanu ndi chiwiri muzichita msonkhano wopatulika ndipo musamagwire ntchito iliyonse.
Iti maikapito nga aldaw, masapul nga adda nasantoan a panaguummongyo a mangdayaw kenni Yahweh, ken masapul a saankayo nga agtrabaho iti dayta nga aldaw.
26 “‘Pa tsiku la zipatso zoyambirira kucha, pamene mukupereka chopereka cha chakudya chatsopano kwa Yehova, pa nthawi ya chikondwerero cha Masabata, muzichita msonkhano wopatulika ndipo musagwire ntchito zolemetsa.
Kasta met iti aldaw dagiti umuna a bunga, inton mangidatagkayo iti baro a sagut a bukel kenni Yahweh iti Fiestayo iti Makalawas, masapul nga agguummongkayo iti nasantoan a taripnong a mangdayaw kenni Yahweh, ken masapul a saankayo nga agtrabaho iti dayta nga aldaw.
27 Muzipereka nsembe zopsereza za ana angʼombe aamuna awiri, nkhosa imodzi yayimuna ndi ana ankhosa aamuna asanu ndi awiri a chaka chimodzi monga fungo lokomera Yehova.
Masapul a mangidatagkayo iti daton a maipuor a mangipaay iti nabanglo nga ayamuom kenni Yahweh. Masapul a mangidatagkayo iti dua a bumbumaro a baka, maysa a kalakian a karnero, ken pito a kalakian nga urbon a karnero nga agtawen iti maysa.
28 Pa ngʼombe yayimuna iliyonse pazikhala chopereka cha chakudya cha makilogalamu atatu a ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta, pa nkhosa yayimuna iliyonse makilogalamu awiri.
Mangidatagkayo met iti sagut a bukel a maipakuyog kadagitoy: napino nga arina a nalaokan ti lana, tallo nga apagkapullo iti maysa nga efa ti napino nga arina a nalaokan ti lana para iti tunggal baka ken dua nga apagkapullo para iti maysa a kalakian a karnero.
29 Ndipo pa mwana wankhosa aliyense mwa asanu ndi awiri aja, kilogalamu imodzi.
Mangidatagkayo iti apagkapullo ti maysa nga efa ti napino nga arina a nalaokan iti lana para iti tunggal maysa kadagiti pito a karnero,
30 Muziperekanso mbuzi yayimuna imodzi kuti izikhala nsembe yopepesera machimo anu.
ken maysa a kalakian a kalding para iti pakapakawanan dagiti basbasolyo.
31 Muzipereka zimenezi pamodzi ndi zopereka za zakumwa ndi nsembe yake ya chakudya. Onetsetsani kuti nyamazo zilibe chilema.
Inton mangidatagkayo kadagitoy nga ayup nga awan mulitna, maipakuyog kadagiti datonda a mainom, masapul a mainayon daytoy iti inaldaw a daton a maipuor ken ti sagut a bukel.'”

< Numeri 28 >