< Numeri 28 >
1 Yehova anawuza Mose kuti,
Hina Gode da Mousesema amane sia: i,
2 “Lamula Aisraeli kuti, ‘Onetsetsani kuti mukupereka kwa Ine pa nthawi yoyikika, chopereka cha chakudya chotentha pa moto monga fungo lokoma kwa Ine.’
“Isala: ili dunu ilima ilia da sema defele, ha: i manu iasu amo Na da hahawane ba: sa, amo Nama ima: ne sia: ma.
3 Awuze kuti, ‘Nsembe ya chakudya imene muzipereka pa moto kwa Yehova tsiku ndi tsiku ndi iyi: Ana ankhosa a chaka chimodzi awiri, wopanda chilema.
Ha: i manu iasu agoane Hina Godema ima. Eso huluane, dilia da sibi mano gawali aduna ledo hamedei amo da ode afadafa esalu, amo gobele salima.
4 Mmawa muzipereka mwana wankhosa mmodzi ndipo winayo madzulo.
Hahabe, sibi mano afae amo gobele salima. Eno da daeya gobele salima.
5 Muziperekanso kilogalamu imodzi ya ufa wosalala wosakaniza ndi lita imodzi ya mafuta a olivi.
Amo sibi mano gobesea, gilisili widi falaua1gilogala: me amola1lida olife susuligi noga: i amo ima.
6 Iyi ndi nsembe yopsereza ya tsiku ndi tsiku imene analamula pa phiri la Sinai kuti ikhale fungo lokoma, nsembe yopsereza pa moto yopereka kwa Yehova.
Amo da eso huluane iasu liligi. Dafawanedafa gogo gobesima. Isala: ili dunu da musa: degabo amo iasu Sainai Goumia ha: i manu iasu agoane i. Na da amo ea gabusiga: hahawane nabi.
7 Chopereka chachakumwa chikhale lita imodzi yachakumwa chaukali pa nkhosa iliyonse. Muzithira pamalo opatulika, kupereka kwa Yehova.
Hahabe sibi mano gobele salasea, waini hano 1lida amo oloda amoga soga: sima. Amo da waini hano iasu.
8 Muzipereka mwana wankhosa winayo madzulo, pamodzi ndi chopereka chachakudya monga poyamba paja ndi chopereka chachakumwa monga mmawa. Ichi ndi chopereka chachakudya, fungo lokoma kwa Yehova.’”
Daeya eno sibi mano amo hahabe hamoi defele hamoma. Amola waini hano defele ima. Amo amola da ha: i manu iasu. Hina Gode da amo ea gabusiga: hahawane naba.
9 “‘Pa tsiku la Sabata, muzipereka nsembe ana ankhosa awiri a chaka chimodzi wopanda chilema, pamodzi ndi chopereka chachakumwa ndi chopereka chachakudya chokwana makilogalamu awiri a ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta.
Sa: bade eso amoga sibi mano gawali aduna ode afae lalelegei, ledo hamedei amo ima. Amoga2 gilogala: me widi falaua (olife susuligi bibiogoi) amola waini iasu gilisima.
10 Iyi ndi nsembe yopsereza ya pa Sabata iliyonse, kuwonjezera pa nsembe yopsereza ya nthawi zonse ndi chopereka chake chachakumwa.’”
Amo Gobei Iasu (Wadela: i Hou Dabe Ima: ne Iasu), dilia Sa: bade eso huluane hamoma. Amola amo esoha, eso huluane hamosu iasu amola ea waini hano iasu amo gilisili hamoma.
11 “Pa tsiku loyamba la mwezi uliwonse muzipereka kwa Yehova nsembe yopsereza ya ana angʼombe aamuna awiri, nkhosa yayimuna imodzi, ana ankhosa aamuna asanu ndi awiri a chaka chimodzi, onse wopanda chilema.
Eso age oubi huluane ganodini, Hina Godema Wadela: i Hou Dabe Ima: ne Iasu hamoma. Amo da bulamagau gawali waha debe aduna, sibi gawali afae amola sibi mano gawali ode afae lalelegei fesuale, huluane da ledo hamedei noga: i fawane, amo ima.
12 Pa ngʼombe yayimuna iliyonse pakhale chopereka cha chakudya cha makilogalamu atatu a ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta; ndi nkhosa yayimuna, chopereka cha chakudya cha makilogalamu awiri a ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta;
Gala: ine Iasu da falaua amola olife susuligi gilisi. Bulamagau gawali afae afae amoga widi falaua3 gilogala: me gilisima. Sibi gawali amoga 2 gilogala: me falaua gilisima.
13 ndipo pa mwana wankhosa aliyense, chopereka cha ufa wa kilogalamu imodzi ya ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta, izi ndi za nsembe yopsereza, fungo lokoma, nsembe yotentha pa moto ya kwa Yehova.
Sibi mano gawali afae afae amoga1 gilogala: me falaua gilisima. Amo Wadela: i Hou Dabe Ima: ne Iasu da ha: i manu iasu, amola amoga ea gabusiga: Hina Gode da hahawane naba.
14 Pa ngʼombe yayimuna iliyonse pakhale chopereka cha chakumwa cha malita awiri a vinyo; ndipo pa nkhosa yayimuna, lita limodzi ndi theka, ndipo pa mwana wankhosa, lita limodzi. Iyi ndi nsembe yopsereza ya mwezi ndi mwezi yoperekedwa pa mwezi watsopano mʼkati mwa chaka.
Waini iasu da agoane imunu. Bulamagau gawali afae afae amoga2lida waini hano. Sibi gawali amoga1 1/2lida waini hano. Amola sibi mano afae afae amoga 1 lida waini hano ima. Malasu da agoane gala. Oubi huluane eso age amoga, Wadela: i Hou Dabe Ima: ne Iasu gobei agoane hamoma: mu.
15 Powonjezera pa nsembe yopsereza ya nthawi zonse ndi chopereka chake cha chakumwa, mbuzi yayimuna imodzi iperekedwe kwa Yehova ngati nsembe yopepesera machimo.
Amola eso huluane Wadela: i Hou Dabe Ima: ne Iasu amola waini hano iasu amoga goudi gawali afae amo Wadela: i Hou Gogolema: ne Olofoma: ne Iasu amo hamoma.
16 “‘Pa tsiku la 14 la mwezi woyamba muzichita Paska wa Yehova.
Baligisu Lolo Nasu amo da Hina Godema nodoma: ne hamosa, amo da eso 14oubi age amoga hamoma.
17 Pa tsiku la 15 la mwezi womwewo pazikhala chikondwerero. Muzidya buledi wopanda yisiti kwa masiku asanu ndi awiri.
Eso 15 amoga, Hina Godema dawa: ma: ne gilisisu hamoma. Amo gilisisu eso fesuale hamoma, amola amoga dilia agi da yisidi hame sali liligi fawane manu.
18 Pa tsiku loyamba muzichita msonkhano wopatulika ndipo musamagwire ntchito iliyonse.
Eso age amoga gilisisu da, Hina Godema nodone sia: ne gadomusa: gilisima. Amo esoha, hawa: hamosu mae hamoma.
19 Koma muzipereka kwa Yehova nsembe yotentha pa moto, nsembe yopsereza ya ana angʼombe aamuna awiri, nkhosa yayimuna imodzi ndi ana ankhosa asanu ndi awiri aamuna a chaka chimodzi, onsewo wopanda chilema.
Wadela: i Hou Dabe Ima: ne Iasu gobele salima. Amo da Hina Godema ha: i manu iasu. Amo iasu da bulamagau gawali waha debe aduna, sibi gawali afae amola ode afae lalelegei sibi mano gawali. Amo liligi da noga: idafa ledo hamedei liligi fawane.
20 Pamodzi ndi ngʼombe yayimuna iliyonse, muzikonza chopereka cha chakudya cha makilogalamu atatu a ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta; makilogalamu awiri pa nkhosa yayimuna iliyonse.
Amola sia: i liligi gala: ine iasu amo falaua amola olife susuligi gilisi ima. Bulamagau gawali amoga gilogala: me udiana gilisima amola sibi gawali amoga gilogala: me aduna gilisima,
21 Kilogalamu imodzi pa mwana wankhosa aliyense mwa ana ankhosa asanu ndi awiri aja.
amola sibi mano afae afae amoga gilogala: me afadafa gilisima.
22 Muziphatikizapo mbuzi yayimuna monga nsembe yopepesera machimo anu.
Amola goudi gawali afae, Wadela: i Hou Gogolema: ne Olofoma: ne Iasu hamoma: ne, ima. Amo da Isala: ili dunu ilia ledo hamoi dodofema: ne hamosa.
23 Muzikonza zimenezi nthawi zonse, powonjezera pa nsembe yopsereza ya mmawa.
Amo da gilisili eso huluane Wadela: i Hou Dabe Ima: ne Iasu (Gobei Iasu) amola hamoma.
24 Motere muzikonza chakudya cha nsembe yopsereza ya tsiku ndi tsiku pa masiku asanu ndi awiri ngati fungo lokomera Yehova. Zimenezi ziziperekedwa kuwonjezera pa nsembe yopsereza ya nthawi zonse pamodzi ndi nsembe yachakumwa.
Amo defele, Hina Godema ha: i manu iasu ima! Amo ea gabusiga: , E da hahawane naba. Amola eso huluane Wadela: i Hou Dabe Ima: ne Iasu amola waini iasu gilisili hamoma.
25 Pa tsiku lachisanu ndi chiwiri muzichita msonkhano wopatulika ndipo musamagwire ntchito iliyonse.
Eso fesu ganodini, Hina Godema nodone sia: ne gadomusa: gilisima. Amola amo esoga hawa: hamosu mae hamoma.
26 “‘Pa tsiku la zipatso zoyambirira kucha, pamene mukupereka chopereka cha chakudya chatsopano kwa Yehova, pa nthawi ya chikondwerero cha Masabata, muzichita msonkhano wopatulika ndipo musagwire ntchito zolemetsa.
Ha: i Manu Gaheabolo Fai Lolo Nasu gilisisu amoga, eso agega, dilia da gagoma gaheabolo iasu Hina Godema iasea, Ema nodone sia: ne gadomusa: gilisima. Hawa: hamosudafa mae hamoma.
27 Muzipereka nsembe zopsereza za ana angʼombe aamuna awiri, nkhosa imodzi yayimuna ndi ana ankhosa aamuna asanu ndi awiri a chaka chimodzi monga fungo lokomera Yehova.
Hina Gode amo gabusiga: hahawane nabima: ne, Ema Wadela: i Hou Dabe Ima: ne Iasu (gobei) agoane ima amo bulamagau gawali waha debe aduna, sibi gawali afae amola sibi mano gawali ode afae lalelegei fesuale gala, amo huluane da noga: i ledo hamedei fawane ima.
28 Pa ngʼombe yayimuna iliyonse pazikhala chopereka cha chakudya cha makilogalamu atatu a ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta, pa nkhosa yayimuna iliyonse makilogalamu awiri.
Amola sia: i liligi Gala: ine Iasu, amo falaua amola olife susuligi gilisili ima. Bulamagau gawali amoga gilogala: me udiana gilisima amola sibi gawali amoga gilogala: me aduna gilisima,
29 Ndipo pa mwana wankhosa aliyense mwa asanu ndi awiri aja, kilogalamu imodzi.
amola sibi mano afae afae amoga gilogala: me afadafa gilisima.
30 Muziperekanso mbuzi yayimuna imodzi kuti izikhala nsembe yopepesera machimo anu.
Amola goudi gawali afae Wadela: i Hou Gogolema: ne Olofoma: ne Iasu hamoma: ne, ima. Amo da Isala: ili dunu ilia ledo hamoi dodofema: ne hamosa.
31 Muzipereka zimenezi pamodzi ndi zopereka za zakumwa ndi nsembe yake ya chakudya. Onetsetsani kuti nyamazo zilibe chilema.
Amo amola waini hano iasu, amola eso huluane Wadela: i Hou Dabe Ima: ne Iasu (Gobei Iasu) amola Gala: ine Iasu amo gilisili ima.