< Numeri 26 >
1 Utatha mliri Yehova anati kwa Mose ndi Eliezara mwana wa Aaroni,
and to be after [the] plague and to say LORD to(wards) Moses and to(wards) Eleazar son: child Aaron [the] priest to/for to say
2 “Werengani Aisraeli onse mwa mabanja awo, onse a zaka makumi awiri kapena kuposera pamenepo omwe angathe kugwira ntchito ya usilikali mʼgulu lankhondo la Israeli.”
to lift: count [obj] head: count all congregation son: descendant/people Israel from son: aged twenty year and above [to] to/for house: household father their all to come out: regular army: war in/on/with Israel
3 Kotero mu zigwa za Mowabu pafupi ndi mtsinje wa Yorodani ku Yeriko, Mose ndi wansembe Eliezara anayankhula nawo kuti,
and to speak: speak Moses and Eleazar [the] priest with them in/on/with Plains (of Moab) (Plains of) Moab upon Jordan Jericho to/for to say
4 “Werengani amuna a zaka makumi awiri kapena kuposera pamenepo, monga momwe Yehova walamulira Mose.” Aisraeli omwe anachokera ku Igupto ndi awa:
from son: aged twenty year and above [to] like/as as which to command LORD [obj] Moses and son: descendant/people Israel [the] to come out: come from land: country/planet Egypt
5 Zidzukulu za Rubeni, mwana woyamba wamwamuna wa Israeli, zinali izi: kuchokera mwa Hanoki, fuko la Ahanoki; kuchokera mwa Palu, fuko la Apalu;
Reuben firstborn Israel son: descendant/people Reuben Hanoch family [the] Hanochite to/for Pallu family [the] Palluite
6 kuchokera mwa Hezironi, fuko la Ahezironi; kuchokera mwa Karimi, fuko la Akarimi.
to/for Hezron family [the] Hezronite to/for Carmi family [the] Carmite
7 Awa anali mafuko a Rubeni: onse amene anawerengedwa analipo 43,730.
these family [the] Reubenite and to be to reckon: list their three and forty thousand and seven hundred and thirty
8 Mwana wa Palu anali Eliabu,
and son: child Pallu Eliab
9 ndipo ana a Eliabu anali Nemueli, Datani ndi Abiramu. Datani ndi Abiramu anali gulu la akuluakulu aja amene anawukira Mose ndi Aaroni ndipo analinso mʼgulu la otsatira Kora pamene anawukira Yehova.
and son: child Eliab Nemuel and Dathan and Abiram he/she/it Dathan and Abiram (chosen *Q(K)*) [the] congregation which to struggle upon Moses and upon Aaron in/on/with congregation Korah in/on/with to struggle they upon LORD
10 Nthaka inangʼambika ndi kuwameza pamodzi ndi Kora, kotero kuti gulu lawo linafa pamene moto unapsereza anthu 250 aja, nasanduka chenjezo.
and to open [the] land: soil [obj] lip her and to swallow up [obj] them and [obj] Korah in/on/with to die [the] congregation in/on/with to eat [the] fire [obj] fifty and hundred man and to be to/for ensign
11 Koma ana a Kora sanafe nawo.
and son: descendant/people Korah not to die
12 Zidzukulu za Simeoni mwa mafuko awo zinali izi: kuchokera mwa Nemueli, fuko la Anemuele; kuchokera mwa Yamini, fuko la Ayamini; kuchokera mwa Yakini fuko la Ayakini;
son: descendant/people Simeon to/for family their to/for Nemuel family [the] Nemuelite to/for Jamin family [the] Jaminite to/for Jachin family [the] Jachinite
13 kuchokera mwa Zera, mbumba ya Zera; kuchokera mwa Sauli, fuko la Asauli.
to/for Zerah family [the] Zerahite to/for Shaul family [the] Shaulite
14 Awa anali mafuko a Simeoni. Iwowa analipo amuna 22,200.
these family [the] Simeon two and twenty thousand and hundred
15 Zidzukulu za Gadi mwa mafuko awo ndi izi: kuchokera mwa Zefoni, fuko la Azefoni; kuchokera mwa Hagi, fuko la Ahagi; kuchokera mwa Suni, fuko la Asuni;
son: descendant/people Gad to/for family their to/for Zephon family [the] Zephonite to/for Haggi family [the] Haggi to/for Shuni family [the] Shunite
16 kuchokera mwa Ozini, fuko la Aozini; kuchokera mwa Eri, fuko la Aeri;
to/for Ozni family [the] Oznite to/for Eri family [the] Erite
17 kuchokera mwa Arodi, fuko la Aarodi; kuchokera mwa Arieli, fuko la a Areli.
to/for Arod family [the] Arodi to/for Areli family [the] Areli
18 Awa ndiwo anali mafuko a Gadi. Onse amene anawerengedwa analipo 40,500.
these family son: descendant/people Gad to/for to reckon: list their forty thousand and five hundred
19 Eri ndi Onani anali ana aamuna a Yuda, koma anafera mu Kanaani.
son: descendant/people Judah Er and Onan and to die Er and Onan in/on/with land: country/planet Canaan
20 Zidzukulu za Yuda monga mwa mafuko awo zinali izi: kuchokera mwa Sela, fuko la Asera; kuchokera mwa Perezi, fuko la Aperezi; kuchokera mwa Zera, mbumba ya Zera.
and to be son: descendant/people Judah to/for family their to/for Shelah family [the] Shelanite to/for Perez family [the] Perezite to/for Zerah family [the] Zerahite
21 Zidzukulu za Perezi zinali izi: kuchokera mwa Hezironi, fuko la Ahezironi; kuchokera mwa Hamuli, fuko la Ahamuli.
and to be son: descendant/people Perez to/for Hezron family [the] Hezronite to/for Hamul family [the] Hamulite
22 Awa ndiwo anali mafuko a Yuda. Amene anawerenga analipo 76,500.
these family Judah to/for to reckon: list their six and seventy thousand and five hundred
23 Zidzukulu za Isakara monga mwa mafuko awo zinali izi: kuchokera mwa Tola, fuko la Atola; kuchokera mwa Puwa, fuko la Apuwa;
son: descendant/people Issachar to/for family their Tola family [the] Tolaite to/for Puah family [the] Punite
24 kuchokera mwa Yasubu, fuko la Ayasubu. Kuchokera mwa Simironi, fuko la Asimironi.
to/for Jashub family [the] Jashubite to/for Shimron family [the] Shimronite
25 Awa ndi amene anali a fuko la Isakara. Amene anawerengedwa analipo 64,300.
these family Issachar to/for to reckon: list their four and sixty thousand and three hundred
26 Zidzukulu za Zebuloni mwa mafuko awo zinali izi: kuchokera mwa Seredi, fuko la Aseredi; kuchokera mwa Eloni, fuko la Aeloni; kuchokera mwa Yahaleeli, fuko la Ayahaleeli.
son: descendant/people Zebulun to/for family their to/for Sered family [the] Seredite to/for Elon family [the] Elonite to/for Jahleel family [the] Jahleelite
27 Awa ndiwo anali mafuko a Zebuloni. Amene anawerengedwa analipo 60,500.
these family [the] Zebulunite to/for to reckon: list their sixty thousand and five hundred
28 Zidzukulu za Yosefe mwa mafuko awo kupyolera mwa Manase ndi Efereimu zinali izi:
son: descendant/people Joseph to/for family their Manasseh and Ephraim
29 Zidzukulu za Manase: kuchokera mwa Makiri, fuko la Amakiri (Makiri anali abambo ake a Giliyadi); kuchokera mwa Giliyadi, fuko la Agiliyadi.
son: descendant/people Manasseh to/for Machir family [the] Machirite and Machir to beget [obj] Gilead to/for Gilead family [the] Gileadite
30 Izi ndizo zinali zidzukulu za Giliyadi; kuchokera mwa Iyezeri, fuko la Aiyezeri; kuchokera mwa Heleki, fuko la Aheleki;
these son: descendant/people Gilead Iezer family [the] Iezerite to/for Helek family [the] Helekite
31 kuchokera mwa Asirieli, fuko la Aasirieli; kuchokera mwa Sekemu, fuko la Asekemu;
and Asriel family [the] Asrielite and Shechem family [the] Shechemite
32 kuchokera mwa Semida, fuko la Asemida; kuchokera mwa Heferi, fuko la Aheferi.
and Shemida family [the] Shemidaite and Hepher family [the] Hepherite
33 (Zelofehadi mwana wa Heferi analibe ana aamuna koma ana aakazi okha, amene mayina awo anali: Mala, Nowa, Hogila, Milika ndi Tiriza.)
and Zelophehad son: child Hepher not to be to/for him son: child that if: except if: except daughter and name daughter Zelophehad Mahlah and Noah Hoglah Milcah and Tirzah
34 Awa ndiwo anali mafuko a Manase. Amene anawerengedwa analipo 52,700.
these family Manasseh and to reckon: list their two and fifty thousand and seven hundred
35 Zidzukulu za Efereimu monga mwa mafuko awo zinali izi; kuchokera mwa Sutela, fuko la Asutela; kuchokera mwa Bekeri, fuko la Abekeri; kuchokera mwa Tahani, fuko la Atahani.
these son: descendant/people Ephraim to/for family their to/for Shuthelah family [the] Shuthelahite to/for Becher family [the] Becherite to/for Tahan family [the] Tahanite
36 Zidzukulu za Sutela zinali izi: kuchokera mwa Erani, fuko la Aerani.
and these son: descendant/people Shuthelah to/for Eran family [the] Eranite
37 Awa ndiwo anali mafuko a Efereimu. Amene anawerengedwa analipo 32,500. Zimenezi zinali zidzukulu za Yosefe monga mwa mafuko awo.
these family son: descendant/people Ephraim to/for to reckon: list their two and thirty thousand and five hundred these son: descendant/people Joseph to/for family their
38 Zidzukulu za Benjamini monga mwa mabanja awo zinali izi: kuchokera mwa Bela, fuko la Abela; kuchokera mwa Asibeli, fuko la Aasibeli; kuchokera mwa Ahiramu, fuko la Ahiramu;
son: child Benjamin to/for family their to/for Bela family [the] Belaite to/for Ashbel family [the] Ashbelite to/for Ahiram family [the] Ahiramite
39 kuchokera mwa Sufamu, fuko la Asufamu; kuchokera mwa Hufamu, fuko la Ahufamu;
to/for Shephupham family [the] Shuphamite to/for Hupham family [the] Huphamite
40 Zidzukulu za Bela kupyolera mwa Aridi ndi Naamani zinali izi: kuchokera mwa Aridi, fuko la Aaridi; kuchokera mwa Naamani, fuko la Anaamani;
and to be son: descendant/people Bela Ard and Naaman (to/for Ard *X*) family [the] Ardite to/for Naaman family [the] Naamite
41 Awa ndiwo anali mabanja a Benjamini. Amene nawerengedwa analipo 45,600.
these son: descendant/people Benjamin to/for family their and to reckon: list their five and forty thousand and six hundred
42 Zidzukulu za Dani mwa mabanja awo zinali izi: kuchokera mwa Suhamu fuko la Asuhamu. Izi zinali zidzukulu za Dani.
these son: descendant/people Dan to/for family their to/for Shuham family [the] Shuhamite these family Dan to/for family their
43 Onse a fuko la Asuhamu amene anawerengedwa analipo 64,400.
all family [the] Shuhamite to/for to reckon: list their four and sixty thousand and four hundred
44 Zidzukulu za Aseri monga mwa mafuko awo zinali izi: kuchokera mwa Imina, fuko la Aimuna; kuchokera mwa Isivi, fuko la Ayisivi; kuchokera mwa Beriya, fuko la Aberiya;
son: descendant/people Asher to/for family their to/for Imnah family [the] Imnah to/for Ishvi family [the] Ishvite to/for Beriah family [the] Beriite
45 ndipo kupyolera mwa zidzukulu za Beriya: kuchokera mwa Heberi, fuko la Aheberi; kuchokera mwa Malikieli, fuko la Amalikieli;
to/for son: descendant/people Beriah to/for Heber family [the] Heberite to/for Malchiel family [the] Malchielite
46 (Aseri anali ndi mwana wamkazi dzina lake Sera)
and name daughter Asher Serah
47 Awa ndiwo anali mafuko a Aseri. Onse amene anawerengedwa analipo 53,400.
these family son: descendant/people Asher to/for to reckon: list their three and fifty thousand and four hundred
48 Zidzukulu za Nafutali mwa mafuko awo zinali izi: kuchokera mwa Yahazeeli, fuko la Ayahazeeli; kuchokera mwa Guni, fuko la Aguni;
son: descendant/people Naphtali to/for family their to/for Jahzeel family [the] Jahzeelite to/for Guni family [the] Gunite
49 kuchokera mwa Yezeri, fuko la Ayezeri; kuchokera mwa Silemu, fuko la Asilemu.
to/for Jezer family [the] Jezerite to/for Shillem family [the] Shillemite
50 Awa ndiwo anali mafuko a Nafutali. Onse amene anawerengedwa analipo 45,400.
these family Naphtali to/for family their and to reckon: list their five and forty thousand and four hundred
51 Chiwerengero chonse cha amuna mu Israeli chinalipo 601,730.
these to reckon: list son: descendant/people Israel six hundred thousand and thousand seven hundred and thirty
52 Yehova anawuza Mose kuti,
and to speak: speak LORD to(wards) Moses to/for to say
53 “Uwagawire dziko anthu awa kuti likhale cholowa chawo molingana ndi chiwerengero cha mayina awo.
to/for these to divide [the] land: country/planet in/on/with inheritance in/on/with number name
54 Gulu lalikulu ulipatse cholowa chachikulu, ndipo lochepa cholowa chocheperapo. Gulu lililonse lilandire cholowa chake molingana ndi chiwerengero cha amene anawerengedwa.
to/for many to multiply inheritance his and to/for little to diminish inheritance his man: anyone to/for lip: according to reckon: list his to give: give inheritance his
55 Dzikolo uligawe pochita maere. Alandire cholowa chawocho potsata mayina a mafuko a makolo awo.
surely in/on/with allotted to divide [obj] [the] land: country/planet to/for name tribe father their to inherit
56 Cholowa chawo uchigawe pakati pa fuko lalikulu ndi lalingʼono mwa maere.”
upon lip: according [the] allotted to divide inheritance his between many to/for little
57 Alevi omwe anawerengedwa monga mwa mafuko awo ndi awa: kuchokera mwa Geresoni, fuko la Ageresoni; kuchokera mwa Kohati, fuko la Akohati; kuchokera mwa Merari, fuko la Amerari.
and these to reckon: list [the] Levi to/for family their to/for Gershon family [the] Gershonite to/for Kohath family [the] Kohathite to/for Merari family [the] Merari
58 Awanso anali mabanja a Alevi: banja la Alibini, banja la Ahebroni, banja la Amali, banja la Amusi, fuko la Kora banja la Akohati, (Kohati anali abambo a Amramu.
these family Levi family [the] Libnite family [the] Hebronite family [the] Mahlite family [the] Mushite family [the] Korahite and Kohath to beget [obj] Amram
59 Dzina la mkazi wa Amramu linali Yokobedi, mdzukulu wa Levi, yemwe anabadwa mwa Alevi mu Igupto. Yokobedi anaberekera Amramu Aaroni, Mose ndi Miriamu mlongo wawo.
and name woman: wife Amram Jochebed daughter Levi which to beget [obj] her to/for Levi in/on/with Egypt and to beget to/for Amram [obj] Aaron and [obj] Moses and [obj] Miriam sister their
60 Aaroni anali abambo a Nadabu, Abihu, Eliezara ndi Itamara.
and to beget to/for Aaron [obj] Nadab and [obj] Abihu [obj] Eleazar and [obj] Ithamar
61 Koma Nadabu ndi Abihu anafa pamene anapereka nsembe pamaso pa Yehova ndi moto wachilendo).
and to die Nadab and Abihu in/on/with to present: bring they fire be a stranger to/for face: before LORD
62 Alevi onse aamuna a mwezi umodzi kapena kuposera pamenepa analipo 23,000. Iwowo sanawerengedwe pamodzi ndi Aisraeli ena chifukwa sanalandire cholowa pakati pawo.
and to be to reckon: list their three and twenty thousand all male from son: aged month and above [to] for not to reckon: list in/on/with midst son: descendant/people Israel for not to give: give to/for them inheritance in/on/with midst son: descendant/people Israel
63 Awa ndi amene anawerengedwa ndi Mose ndi Eliezara wansembe pamene ankawerenga Aisraeli pa zigwa za ku Mowabu mʼmbali mwa Yorodani ku Yeriko.
these to reckon: list Moses and Eleazar [the] priest which to reckon: list [obj] son: descendant/people Israel in/on/with Plains (of Moab) (Plains of) Moab upon Jordan Jericho
64 Mwa anthu amenewa panalibe ndi mmodzi yemwe amene anali mʼgulu la Aisraeli omwe Mose ndi wansembe Aaroni anawawerenga mʼchipululu cha Sinai;
and in/on/with these not to be man: anyone from to reckon: list Moses and Aaron [the] priest which to reckon: list [obj] son: descendant/people Israel in/on/with wilderness (Wilderness of) Sinai
65 Chifukwa Yehova anali atawuza Aisraeliwo kuti adzafera ndithu mʼchipululu, ndipo palibe ndi mmodzi yemwe amene anatsala kupatula Kalebe mwana wa Yefune ndi Yoswa mwana wa Nuni.
for to say LORD to/for them to die to die in/on/with wilderness and not to remain from them man: anyone that if: except if: except Caleb son: child Jephunneh and Joshua son: child Nun