< Numeri 26 >
1 Utatha mliri Yehova anati kwa Mose ndi Eliezara mwana wa Aaroni,
Lucik a om hnukah BOEIPA loh Moses neh khosoih Aaron capa Eleazar te a voek tih,
2 “Werengani Aisraeli onse mwa mabanja awo, onse a zaka makumi awiri kapena kuposera pamenepo omwe angathe kugwira ntchito ya usilikali mʼgulu lankhondo la Israeli.”
“Israel ca rhaengpuei boeih hlangmi te tongpaca khui lamloh kum kul neh a so hang tah a napa imko neh Israel khuiah caempuei la aka cet boeih te soep laeh,” a ti nah.
3 Kotero mu zigwa za Mowabu pafupi ndi mtsinje wa Yorodani ku Yeriko, Mose ndi wansembe Eliezara anayankhula nawo kuti,
Te dongah Moses neh khosoih Eleazar loh amih te Moab kolken kah Jerikho Jordan ah a voek tih,
4 “Werengani amuna a zaka makumi awiri kapena kuposera pamenepo, monga momwe Yehova walamulira Mose.” Aisraeli omwe anachokera ku Igupto ndi awa:
“Tongpaca khui lamkah kum kul neh a so hang tah BOEIPA kah a uen bangla tae,” a ti nah. Moses neh Egypt kho lamkah aka coe Israel ca rhoek tah,
5 Zidzukulu za Rubeni, mwana woyamba wamwamuna wa Israeli, zinali izi: kuchokera mwa Hanoki, fuko la Ahanoki; kuchokera mwa Palu, fuko la Apalu;
Israel caming Reuben lamloh Reuben koca rhoek, Enok lamloh Hanokhi koca, Pallu lamloh Pallu koca,
6 kuchokera mwa Hezironi, fuko la Ahezironi; kuchokera mwa Karimi, fuko la Akarimi.
Khetsron lamloh Khetsron koca, Karmee lamloh Karmee koca,
7 Awa anali mafuko a Rubeni: onse amene anawerengedwa analipo 43,730.
Reuben koca he a soep vaengah thawng sawmli thawng thum neh ya rhih sawmthum lo.
8 Mwana wa Palu anali Eliabu,
Pallu koca lamloh Eliab,
9 ndipo ana a Eliabu anali Nemueli, Datani ndi Abiramu. Datani ndi Abiramu anali gulu la akuluakulu aja amene anawukira Mose ndi Aaroni ndipo analinso mʼgulu la otsatira Kora pamene anawukira Yehova.
Eliab koca la Nemuel, Dathan neh Abiram tih, Dathan neh Abiram tah Moses neh Aron aka hnuei rhaengpuei khuikah mingthang neh pang rhoi. BOEIPA taengah a hnueih uh vaengkah Korah hlangboel khuiah khaw om rhoi.
10 Nthaka inangʼambika ndi kuwameza pamodzi ndi Kora, kotero kuti gulu lawo linafa pamene moto unapsereza anthu 250 aja, nasanduka chenjezo.
Diklai loh a ka te a ang tih amih te a dolh vaengah Korah hlangboel tah duek. Hmai loh a hlawp hlang yahnih sawmnga khaw rholik banghui la om uh.
11 Koma ana a Kora sanafe nawo.
Tedae Korah ca rhoek a duek uh moenih.
12 Zidzukulu za Simeoni mwa mafuko awo zinali izi: kuchokera mwa Nemueli, fuko la Anemuele; kuchokera mwa Yamini, fuko la Ayamini; kuchokera mwa Yakini fuko la Ayakini;
Simeon koca khaw amamih cako ah, Nemuel lamloh Nemuel koca, Jamin lamloh Jamin koca, Jakhin lamloh Jakhin koca,
13 kuchokera mwa Zera, mbumba ya Zera; kuchokera mwa Sauli, fuko la Asauli.
Zerah lamloh Zarkhii koca, Saul lamloh Saul koca,
14 Awa anali mafuko a Simeoni. Iwowa analipo amuna 22,200.
Simeon koca he thawng kul thawng hnih neh ya hnih lo.
15 Zidzukulu za Gadi mwa mafuko awo ndi izi: kuchokera mwa Zefoni, fuko la Azefoni; kuchokera mwa Hagi, fuko la Ahagi; kuchokera mwa Suni, fuko la Asuni;
Gad ca rhoek khaw amah cako ah, Zephon lamloh Zephon koca, Hakki lamloh Hakki koca, Shuni lamloh Shuni koca,
16 kuchokera mwa Ozini, fuko la Aozini; kuchokera mwa Eri, fuko la Aeri;
Ozni lamloh Ozni koca, Eri lamloh Eri koca,
17 kuchokera mwa Arodi, fuko la Aarodi; kuchokera mwa Arieli, fuko la a Areli.
Arod lamloh Arodi koca, Areli lamloh Areli koca,
18 Awa ndiwo anali mafuko a Gadi. Onse amene anawerengedwa analipo 40,500.
Gad ca rhoek kah koca he thawng sawmli neh ya nga la a soep.
19 Eri ndi Onani anali ana aamuna a Yuda, koma anafera mu Kanaani.
Judah ca rhoi he Er neh Onan dae Er neh Onan te Kanaan khohmuen ah duek.
20 Zidzukulu za Yuda monga mwa mafuko awo zinali izi: kuchokera mwa Sela, fuko la Asera; kuchokera mwa Perezi, fuko la Aperezi; kuchokera mwa Zera, mbumba ya Zera.
Judah ca rhoek khaw amah koca la om uh. Shelah lamloh Shelahni koca, Perez lamloh Perez koca, Zerah lamloh Zarkhii koca,
21 Zidzukulu za Perezi zinali izi: kuchokera mwa Hezironi, fuko la Ahezironi; kuchokera mwa Hamuli, fuko la Ahamuli.
Perez ca rhoek ah, Khetsron lamloh Khetsron koca, Hamul lamloh Hamul koca la om uh.
22 Awa ndiwo anali mafuko a Yuda. Amene anawerenga analipo 76,500.
Amih Judah koca rhoek he thawng sawmrhih thawng rhuk neh ya nga la a soep.
23 Zidzukulu za Isakara monga mwa mafuko awo zinali izi: kuchokera mwa Tola, fuko la Atola; kuchokera mwa Puwa, fuko la Apuwa;
Issakhar koca khaw amah cako lamtah, Tola lamkah Tola koca, Puvah lamloh Puni koca,
24 kuchokera mwa Yasubu, fuko la Ayasubu. Kuchokera mwa Simironi, fuko la Asimironi.
Jashub lamloh Jashub koca, Shimron lamloh Shimron koca,
25 Awa ndi amene anali a fuko la Isakara. Amene anawerengedwa analipo 64,300.
Issakhar koca he thawng sawmrhuk thawng li ya thum la a soep.
26 Zidzukulu za Zebuloni mwa mafuko awo zinali izi: kuchokera mwa Seredi, fuko la Aseredi; kuchokera mwa Eloni, fuko la Aeloni; kuchokera mwa Yahaleeli, fuko la Ayahaleeli.
Zebulun ca rhoek khaw amah cako lamtah Sered lamloh Sered koca, Elon lamloh Eloni koca, Jahleel lamloh Jahleel koca om.
27 Awa ndiwo anali mafuko a Zebuloni. Amene anawerengedwa analipo 60,500.
Amih Zebulon koca rhoek he thawng sawmrhuk neh ya nga la a soep.
28 Zidzukulu za Yosefe mwa mafuko awo kupyolera mwa Manase ndi Efereimu zinali izi:
Joseph ca rhoek he amah cako lamtah Manasseh neh Ephraim.
29 Zidzukulu za Manase: kuchokera mwa Makiri, fuko la Amakiri (Makiri anali abambo ake a Giliyadi); kuchokera mwa Giliyadi, fuko la Agiliyadi.
Manasseh koca la, Makir lamloh Makir koca om. Te dongah Makir loh Gilead a sak tih Gilead lamloh Giladi koca la om.
30 Izi ndizo zinali zidzukulu za Giliyadi; kuchokera mwa Iyezeri, fuko la Aiyezeri; kuchokera mwa Heleki, fuko la Aheleki;
Gilead ca rhoek he, Iezer lamloh Iezer koca, Helek lamloh Heleki koca,
31 kuchokera mwa Asirieli, fuko la Aasirieli; kuchokera mwa Sekemu, fuko la Asekemu;
Asriel lamloh Asriel koca, Shekhem kah Shekhemi koca,
32 kuchokera mwa Semida, fuko la Asemida; kuchokera mwa Heferi, fuko la Aheferi.
Shemida kah Shemida koca, Hepher kah Hepher koca,
33 (Zelofehadi mwana wa Heferi analibe ana aamuna koma ana aakazi okha, amene mayina awo anali: Mala, Nowa, Hogila, Milika ndi Tiriza.)
Hepher capa Zelophehad he a taengah ca tongpa om pawt tih huta rhoek dawk om. Zelophehad canu rhoek kah a ming tah Mahlah, Noah, Hoglah, Milkah neh Tirzah
34 Awa ndiwo anali mafuko a Manase. Amene anawerengedwa analipo 52,700.
Manasseh koca rhoek he khaw a hlangmi la thawng sawmnga thawng hnih neh ya rhih la a soep uh.
35 Zidzukulu za Efereimu monga mwa mafuko awo zinali izi; kuchokera mwa Sutela, fuko la Asutela; kuchokera mwa Bekeri, fuko la Abekeri; kuchokera mwa Tahani, fuko la Atahani.
Ephraim ca rhoek he amah koca lamtah, Shuthela lamloh Shutheli koca, Bekher lamloh Bekeri koca, Tahan lamloh Tahani koca la om.
36 Zidzukulu za Sutela zinali izi: kuchokera mwa Erani, fuko la Aerani.
Shuthela ca rhoek he khaw, Eran lamloh Erani koca la om.
37 Awa ndiwo anali mafuko a Efereimu. Amene anawerengedwa analipo 32,500. Zimenezi zinali zidzukulu za Yosefe monga mwa mafuko awo.
Ephraim ca koca rhoek he a hlangmi la thawng sawmthum thawng hnih neh ya nga la a soep uh. He rhoek he Joseph ca rhoek lamkah amih koca rhoek ni.
38 Zidzukulu za Benjamini monga mwa mabanja awo zinali izi: kuchokera mwa Bela, fuko la Abela; kuchokera mwa Asibeli, fuko la Aasibeli; kuchokera mwa Ahiramu, fuko la Ahiramu;
Benjamin kah ca lamkah amih koca rhoek he, Bela lamloh Belee koca, Ashbel lamloh Ashbeli koca, Akhiram lamloh Akhirami koca la,
39 kuchokera mwa Sufamu, fuko la Asufamu; kuchokera mwa Hufamu, fuko la Ahufamu;
Shupham lamloh Shuphami koca la, Hupham lamloh Humphami koca la om.
40 Zidzukulu za Bela kupyolera mwa Aridi ndi Naamani zinali izi: kuchokera mwa Aridi, fuko la Aaridi; kuchokera mwa Naamani, fuko la Anaamani;
Bela ca rhoi Ard neh Naaman om. Ardee koca neh Naaman lamkah Naamani koca om.
41 Awa ndiwo anali mabanja a Benjamini. Amene nawerengedwa analipo 45,600.
Benjamin ca rhoek he amah koca ah tah a hlangmi la thawng sawmli thawng nga neh ya rhuk la a soep uh.
42 Zidzukulu za Dani mwa mabanja awo zinali izi: kuchokera mwa Suhamu fuko la Asuhamu. Izi zinali zidzukulu za Dani.
Dan ca rhoek he amah koca ah tah Shuham lamloh Shuhami koca la om. He rhoek ni amih koca khuiah Dan koca la aka om.
43 Onse a fuko la Asuhamu amene anawerengedwa analipo 64,400.
Shuhami koca boeih he a hlangmi la thawng sawmrhuk thawng li neh ya li la a soep.
44 Zidzukulu za Aseri monga mwa mafuko awo zinali izi: kuchokera mwa Imina, fuko la Aimuna; kuchokera mwa Isivi, fuko la Ayisivi; kuchokera mwa Beriya, fuko la Aberiya;
Asher ca rhoek he amah koca ah tah, Imnah lamloh Imnah koca la, Ishee lamloh Jesuih koca la, Beriah lamloh Breiah koca la,
45 ndipo kupyolera mwa zidzukulu za Beriya: kuchokera mwa Heberi, fuko la Aheberi; kuchokera mwa Malikieli, fuko la Amalikieli;
Beriah ca rhoi, Heber lamloh Herbari koca la, Malkhiel lamloh Makhiel koca om.
46 (Aseri anali ndi mwana wamkazi dzina lake Sera)
Asher kah canu ming tah Serah ni.
47 Awa ndiwo anali mafuko a Aseri. Onse amene anawerengedwa analipo 53,400.
Asher ca rhoek kah koca he a hlangmi lamtah kah thawng sawmnga thawng thum neh ya li soep.
48 Zidzukulu za Nafutali mwa mafuko awo zinali izi: kuchokera mwa Yahazeeli, fuko la Ayahazeeli; kuchokera mwa Guni, fuko la Aguni;
Naphtali ca rhoek he amah koca lamtah, Jahzeel lamloh Jahzeeli koca la, Guni lamloh Goni koca la,
49 kuchokera mwa Yezeri, fuko la Ayezeri; kuchokera mwa Silemu, fuko la Asilemu.
Jezer lamloh Jezeri koca la, Shillem lamloh kah Shillemi koca la om.
50 Awa ndiwo anali mafuko a Nafutali. Onse amene anawerengedwa analipo 45,400.
Naphtali koca rhoek he amah koca lamtah a hlangmi khaw thawng sawmli thawng nga neh ya li louh.
51 Chiwerengero chonse cha amuna mu Israeli chinalipo 601,730.
Israel ca rhoek he hlangmi la thawng ya rhuk neh thawngkhat ya rhih sawmthum lo.
52 Yehova anawuza Mose kuti,
Te phoeiah BOEIPA loh Moses te voek tih,
53 “Uwagawire dziko anthu awa kuti likhale cholowa chawo molingana ndi chiwerengero cha mayina awo.
“Amih te a ming tarhing ah khohmuen he rho la tael uh saeh.
54 Gulu lalikulu ulipatse cholowa chachikulu, ndipo lochepa cholowa chocheperapo. Gulu lililonse lilandire cholowa chake molingana ndi chiwerengero cha amene anawerengedwa.
Miping ham tah a rho te len sak lamtah a sii ham tah a rho te hnop pah. Hlang te a ka neh a soep tarhing ah a rho te phaeng saeh.
55 Dzikolo uligawe pochita maere. Alandire cholowa chawocho potsata mayina a mafuko a makolo awo.
Khohmuen te hmulung loh dawk tael saeh lamtah a napa koca rhoek kah ming tarhing la pang uh saeh.
56 Cholowa chawo uchigawe pakati pa fuko lalikulu ndi lalingʼono mwa maere.”
hmulung kah a ka tarhing ah hlangping neh hlangsi laklo ah a rho te tael saeh,” a ti nah.
57 Alevi omwe anawerengedwa monga mwa mafuko awo ndi awa: kuchokera mwa Geresoni, fuko la Ageresoni; kuchokera mwa Kohati, fuko la Akohati; kuchokera mwa Merari, fuko la Amerari.
Levi rhoek kah hlangmi he amah koca lamtah, Gershon lamloh Gershon koca, Kohath lamloh Kohathi koca, Merari lamloh Merari koca la om.
58 Awanso anali mabanja a Alevi: banja la Alibini, banja la Ahebroni, banja la Amali, banja la Amusi, fuko la Kora banja la Akohati, (Kohati anali abambo a Amramu.
He Levi koca khui lamkah, Libni koca, Khebroni koca, Makhali koca, Musihe koca, Korah koca om tih Kohath loh Amram a sak.
59 Dzina la mkazi wa Amramu linali Yokobedi, mdzukulu wa Levi, yemwe anabadwa mwa Alevi mu Igupto. Yokobedi anaberekera Amramu Aaroni, Mose ndi Miriamu mlongo wawo.
Amram kah a yuu ming tah Levi canu Jochebed ni. Anih te Egypt ah Levi ham a cun pah coeng. Anih long khaw Amram ham Aaron, Moses neh a ngannu Miriam te a cun pah.
60 Aaroni anali abambo a Nadabu, Abihu, Eliezara ndi Itamara.
Aaron loh Nadab neh Abihu, Eleazar neh Ithamar a sak.
61 Koma Nadabu ndi Abihu anafa pamene anapereka nsembe pamaso pa Yehova ndi moto wachilendo).
Tedae Nadab neh Abihu tah BOEIPA mikhmuh ah kholong hmai a khuen rhoi dongah duek rhoi.
62 Alevi onse aamuna a mwezi umodzi kapena kuposera pamenepa analipo 23,000. Iwowo sanawerengedwe pamodzi ndi Aisraeli ena chifukwa sanalandire cholowa pakati pawo.
Te vaengah amih kah hlangmi aka om rhoek tongpa hlakhat ca neh a so hang boeih tah thawng kul neh thawng thum la a soep uh. Tedae amih te Israel ca lakli ah rho a phaeng pawt dongah Israel ca rhoek lakli ah soep uh thil pawh.
63 Awa ndi amene anawerengedwa ndi Mose ndi Eliezara wansembe pamene ankawerenga Aisraeli pa zigwa za ku Mowabu mʼmbali mwa Yorodani ku Yeriko.
He rhoek he Moses neh khosoih Eleazar loh a soep vaengah Jerikho Jordan kah Moab kolken ah Israel ca rhoek te a soep rhoi.
64 Mwa anthu amenewa panalibe ndi mmodzi yemwe amene anali mʼgulu la Aisraeli omwe Mose ndi wansembe Aaroni anawawerenga mʼchipululu cha Sinai;
Tedae Moses neh khosoih Aaron kah a soep khui lamloh Sinai khosoek kah Israel ca rhoek a soep vaengkah hlang te tah te rhoek taengah thum pawh.
65 Chifukwa Yehova anali atawuza Aisraeliwo kuti adzafera ndithu mʼchipululu, ndipo palibe ndi mmodzi yemwe amene anatsala kupatula Kalebe mwana wa Yefune ndi Yoswa mwana wa Nuni.
Amih te khosoek ah duek rhoe duek ham khaw, Jephunneh capa Kaleb neh Nun capa Joshua bueng pawt atah amih lamkah hlang a sueng pawt ham khaw BOEIPA loh a thui coeng dongah ni.