< Numeri 16 >

1 Kora mwana wa Izihari, mwana wa Kohati, mwana wa Levi ndi Datani ndi Abiramu ana a Eliabu, pamodzi ndi Oni mwana wa Perezi, ana a Rubeni, anayamba kudzikuza,
Goula (e da Aisiha ea mano amola ea fi da Lifai amola ea sosogo fi da Gouha: de), e da gasa fili, Mousesema odoga: i. Liubene fi dunu udiana (Ilaia: be ea mano aduna amo Da: idia: ne, Abaila: me amola Bilede ea mano amo One) amola Isala: ili fi ouligisu dunu 250 (Isala: ili fi dunuga ilegei ouligisu dunu) ilia da Goula gilisili Mousesema odoga: i.
2 ndipo anawukira Mose. Mʼgulu mwawo munali atsogoleri a Aisraeli 250, anthu otchuka amene anasankhidwa ndi anthu pa msonkhano.
3 Iwo anasonkhana kudzatsutsana ndi Mose ndi Aaroni nawawuza kuti, “Mwawonjeza! Anthu onsewa ndi oyera, aliyense wa iwo, ndipo Yehova ali pakati pawo. Chifukwa chiyani mukudzikuza pakati pa gulu lonse la Yehova?”
Ilia da Mousese amola Elane ela midadi gilisili, amane sia: i, “Alia hou da gasa fili, baligi dagoi! Ninia fi dunu huluane da Hina Gode Ea: ! Amola Hina Gode da nini huluane gilisili esala! Amaiba: le, Mousese, di abuliba: le ninima hina agoane hamosala: ?”
4 Mose atamva izi, anagwa chafufumimba.
Mousese da amo sia: nababeba: le, hi osoboga gala: lasa: ili, Godema sia: ne gadoi.
5 Ndipo iye anawuza Kora ndi anthu onse amene ankamutsatira kuti, “Yehova mawa mmawa adzasonyeza yemwe ndi wake ndiponso amene ndi woyera mtima. Munthuyo adzabwera pafupi ndi Iye. Munthu amene adzamusankheyo adzamusendeza pafupi.
Amasea, e da Goula amola ema fa: no bobogesu dunu ilima amane sia: i, “Aya hahabe, Hina Gode da nowa da Ea: fidafa, amo olelemu. E da Ea ilegei dunu, Ema oloda gadenene doaga: ma: ne logo doasimu.
6 Iwe Kora pamodzi ndi onse amene akukutsatira chitani izi: Tengani zofukizira
Aya hahabe, dilia amola dilia fa: no bobogesu dunu, amo lalu gasa: le legesu ofodo lale, amo ganodini laluoso amola gabusiga: manoma salawane, oloda amoma gaguli misa. Amasea, ninia da Hina Gode Ea ilegei dunu dawa: mu. Dilia Lifai dunu, dilia fawane da gasa fili baligi dagoi!”
7 ndipo mawa muyikemo moto ndi lubani pamaso pa Yehova. Munthu amene Yehova amusankhe ndiye amene ali woyera. Alevi inu mwawonjeza kwambiri!”
8 Mose anawuzanso Kora kuti, “Inu Alevi, tsopano tamverani!
Mousese da bu Goula ema amane sia: i, “Dilia Lifai dunu! Nabima!
9 Kodi sizinakukwanireni kuti Mulungu wa Israeli anakupatulani pakati pa gulu lonse la Aisraeli ndi kukubweretsani pafupi ndi Iye, kuti muzigwira ntchito ku nyumba ya Yehova ndi kumayima pamaso pa gulu, kumatumikira?
Isala: ili Gode da dili eno Isala: ili fi amoga afafai dagoi. Bai dilia da Ema misini, Hina Gode Ea Abula Diasu ganodini hawa: hamoma: ne amola Isala: ili fi ilima fidisu hou hamoma: ne E da dilima ilegei. Dilia adi dawa: bela: ? Amo da hamedei hou, dilia dawa: bela: ?
10 Wakubweretsa iwe pamodzi ndi Alevi anzako kufupi ndi Iye mwini. Koma tsopano ukufuna kutenganso unsembe.
Hina Gode da amo gadodafa nodoma: ne hou dilima i dagoi. Be amo mae dawa: le, dilia da gobele salasu hou amola lamusa: dawa: lala.
11 Nʼkulakwira Yehova kuti iwe ndi gulu lako lonseli mwasonkhana kuti mutsutsane ndi Yehova. Kodi Aaroni ndani kuti muzikangana naye?”
Dilia da Elanema egane sia: sea, dilia da ema hame egasa. Be dilia dafawane Hina Gode Ema egane odoga: sa.”
12 Kenaka Mose anayitana Datani ndi Abiramu, ana aamuna a Eliabu koma iwo anati, “Sitibwera!
Amalalu, Mousese da Da: ida: ne amola Abaila: me ela ema misa: ne sia: si. Be ela da amane sia: i, “Ania da hame misunu!
13 Kodi sikukwanira kuti unatitulutsa, kutichotsa mʼdziko loyenda mkaka ndi uchi kuti udzatiphe mʼchipululu muno? Kodi tsopano ukufunanso kutilemetsa?
Di da nini Idibidi nasegagi soge amoga fisili masa: ne, goeguda: wadela: i soge ganodini medole legema: ne oule misi. Amo da defeala: ? Be amo baligili, di abuliba: le ninima hina agoane hamosala: ?
14 Kuwonjezera apo, sunatilowetse mʼdziko loyenda mkaka ndi uchi kapena kutipatsa malo wolima ndi minda ya mpesa. Kodi ukufuna kuchotsa maso a anthuwa? Ayi, sitibwera!”
Di da ninima nasegagi soge amola soge amola waini sagai ninia gaguma: ne hamedafa i. Amola wali di da ninima ogogomusa: dawa: lala. Ania da hamedafa misunu.”
15 Pamenepo Mose anakwiya kwambiri ndipo anati kwa Yehova, “Musalandire chopereka chawo. Sindinatenge kalikonse kwa iwo ngakhale bulu, ndiponso sindinalakwire wina aliyense wa iwo.”
Mousese da ougi bagade ba: i. E da Hina Godema amane sia: i “Amo dunu da Dima iasu gaguli masea, mae lama! Na da ilia dunu afae amoma wadela: le hamedafa hamoi. Na da ilia dougi afae hamedafa lai.”
16 Mose anati kwa Kora, “Iwe ndi okutsatira onse mudzaonekere pamaso pa Yehova mawa, iweyo ndi iwowo pamodzi ndi Aaroni.
Mousese da Goula ema amane sia: i, “Aya, di amola dia 250 fa: no bobogesu dunu amo Hina Gode Ea Abula Diasuga misa. Elane amola da amogawi esalebe ba: mu.
17 Munthu aliyense akatenge chofukizira ndi kuyikamo lubani, zofukizira 250 zonse pamodzi ndi kuzibweretsa pamaso pa Yehova. Iwe ndi Aaroni mudzabweretsenso zofukizira zanu.”
Dilia afae afae laluoso gasa: le legesu lale, gabusiga: manoma amoga ligisili, oloda amoga gaguli misini, olelema.”
18 Choncho munthu aliyense anatenga chofukizira chake nayikamo moto ndi lubani, ndipo anayima pamodzi ndi Mose ndi Aaroni pa khomo la tenti ya msonkhano.
Amaiba: le, ilia da dunu afae afae da ilia laluoso gasa: le legesu lale, amo ganodini laluoso amola gabusiga: manoma salawane, ilia amola Mousese amola Elane da Abula Diasu holeiga lelu.
19 Kora atasonkhanitsa omutsatira ake onse amene amatsutsa nawo pa khomo la tenti ya msonkhano, ulemerero wa Yehova unaonekera kwa gulu lonselo.
Amalalu, Goula da Isala: ili fi huluane gilisili, ilia da Mousese amola Elane ela midadi Abula Diasu ea logo holeiga lelu. Amalalu, hedolowane, Hina Gode E esalagalebeia dawa: loma: ne sinenemegi hadigi da dunu huluane ba: ma: ne misi.
20 Yehova anawuza Mose ndi Aaroni kuti,
Hina Gode da Mousese amola Elanema amane sia: i,
21 “Chokani pakati pa gulu ili kuti ndithetse mkanganowu kamodzinʼkamodzi.”
“Masa! Amo dunuma mae gilisima! Na da wahadafa ili dafawanedafa wadela: lesimu!”
22 Koma Mose ndi Aaroni anadzigwetsa chafufumimba ndipo analira mokweza, “Chonde Mulungu, Mulungu wa mizimu ya anthu onse, kodi mudzakwiyira gulu lonse pamene munthu mmodzi yekha ndiye amene wachimwa?”
Be Mousese amola Elane da osoboga mi bugila sa: ili, beguduli, amane sia: i, “Gode! Di da esalusu huluane ea bai gala. Dunu afae fawane da wadela: le hamoiba: le, Di da fi dunu huluane ilima ougima: bela: ?”
23 Pamenepo Yehova anawuza Mose kuti,
Hina Gode da Mousesema amane sia: i,
24 “Uza gulu lonse kuti, ‘Khalani kutali ndi matenti a Kora, Datani ndi Abiramu.’”
“Dunu huluane ilia da Goula, Da: ida: ne amola Abaila: me ilia abula diasu yolesili, sogebi enoga masa: ne sia: ma!”
25 Mose anayimirira napita kwa Datani, Abiramu ndi kwa akuluakulu a Israeli amene ankamutsatira.
Amalalu, Mousese, amola Isala: ili ouligisu dunu, ilia da Da: ida: ne amola Abaila: me elama asi.
26 Anachenjeza gulu lonse kuti, “Khalani kutali ndi matenti a anthu oyipawa! Musakhudze kanthu kawo kalikonse, mukatero mudzawonongedwa limodzi nawo chifukwa cha machimo awo.”
Mousese da Isala: ili dunu ilima amane sia: i, “Amo wadela: i hamosu dunu ilia abula diasu yolesili, gadenene mae leloma! Ilia liligi huluanedafa mae digili ba: ma! Dilia agoane hame hamosea, dilia da ilia wadela: i hamoiba: le bogobe defele, dilia amola da bogomu.”
27 Choncho anthuwo anachokadi ku matenti a Kora, Datani ndi Abiramu. Datani ndi Abiramu anali atatuluka nayima pamodzi ndi akazi awo, ana awo ndi makanda awo pa makomo a matenti awo.
Amaiba: le, Isala: ili dunu da Goula, Da: ida: ne amola Abaila: me ilia abula diasu yolesili asi. Da: ida: ne amola Abaila: me da ilia abula diasuga gadili asili, ela, elea uda amola mano da abula diasu logo holeiga lelebe ba: i.
28 Tsono Mose anati, “Umu ndi mmene mudzadziwire kuti Yehova ndiye amene anandituma kuti ndichite zinthu zonsezi ndipo kuti si maganizo anga.
Mousese da Isala: ili dunu ilima amane sia: i, “Dilia waha ba: mu liligi amoga, Hina Gode da na amo hou hamoma: ne asunasi amo dawa: mu. Amola na da na hanaiga hame hamoi amo dawa: mu.
29 Ngati anthu awa afa ndi imfa ya chilengedwe ndi kuwachitikira zomwe zimachitikira munthu aliyense, ndiye kuti Yehova sananditume.
Amo dunu da osobo bagade dunu ilia esalusu hou defele, Gode Ea se dabe mae lale, udigili bogosea, defea, Hina Gode da na hame asunasi dawa: ma.
30 Koma Yehova akachita china chake chachilendo, nthaka nitsekula pakamwa pake ndi kuwameza iwo pamodzi ndi zonse zimene ali nazo, iwowa nʼkulowa mʼmanda ali moyo, pamenepo mudzazindikira kuti anthu amenewa ananyoza Yehova.” (Sheol h7585)
Be Hina Gode da hou musa: hame ba: i hamosea, amola osobo ea lafi da dagale, dunu amola ilia liligi huluane amo mogo salasea, amola ilia esaleawane udigili bogoi sogega gudu dasea, amo dunu da Hina Gode da ilima higale yolesi dagoi dilia da dawa: mu.” (Sheol h7585)
31 Atangotsiriza kuyankhula zimenezi, nthaka ya pamene anayimapo inagawikana
Mousese da sia: i dagoloba, hedolowane Da: ida: ne amola Abaila: me ela lelebe hagudu dialu osobo da lafi agoane dagale gai.
32 ndipo dziko linatsekula pakamwa pake ndi kuwameza pamodzi ndi nyumba zawo ndi anthu onse a Kora ndi katundu wawo yense.
Osobo da ela amola elea sosogo fi amola Goula ea fa: no bobogesu dunu amola ilia liligi huluane amo mogosali dagoi.
33 Analowa mʼmanda amoyo pamodzi ndi zonse zimene anali nazo. Nthaka inawatsekera ndi kuwawononga ndipo sanaonekenso. (Sheol h7585)
Amaiba: le, ilia amola ilia liligi huluane da mae bogole, bogoi sogega gudu sa: i. Ilia gudu sa: i dagoloba, osobo ea lafi da bu ga: si. Ilia da bu hamedafa ba: i. (Sheol h7585)
34 Atamva kulira kwawo, Aisraeli onse amene anali pafupi ndi anthuwo anathawa akufuwula kuti, “Nthaka imezanso ife!”
Isala: ili dunu huluane da disa wesu nababeba: le, hobea: i. Ilia da amane wei, “Hobea: ma! Osobo da nini amola mogosalasa: besa: le, hehenama!”
35 Ndipo moto wochokera kwa Yehova unabwera nʼkunyeketsa anthu 250 amene ankapereka nsembe yofukiza aja.
Amalalu, Hina Gode da lalu iasi. Amo da nene gadole, dunu250 amo da gabusiga: manoma i, amo huluane nei dagoi.
36 Yehova anawuza Mose kuti,
Amalalu, Hina Gode da Mousesema amane sia: i,
37 “Uza Eliezara mwana wa Aaroni, wansembe kuti atenge zofukizirazo pakati pa mitembo yopsererayo ndipo amwazire makalawo kutali chifukwa zofukizirazo nʼzopatulika.
“Elia: isa (gobele salasu dunu Elane egefe) ema, e da balase laluoso gasa: le legesu amo dunu laluga nei ilia da: i hodo amo lale, laluoso amo da ilia laluoso gasa: le legesu ganodini diala amo soge enoga afagogoma: ne sia: ma! Bai amo laluoso gasa: le legesu da hadigi ilegei gala.
38 Izi ndi zofukizira za anthu omwe anafa chifukwa cha uchimo wawo. Musule zofukizirazo kuti zikhale zophimbira pa guwa lansembe, chifukwa zinaperekedwa kwa Yehova ndipo ndi zopatulika. Zimenezi zikhale chizindikiro kwa Aisraeli.”
Ilia da Hina Gode Ea oloda amoga i dagoiba: le, hadigi hamoi dagoi. Amaiba: le, amo dunu (ilia da wadela: le hamoiba: le medole legei dagoi ba: i) amo ilia laluoso gasa: le legesu lale, dadabili, abenale da: fe hamone, amoga oloda dedebosu hamoma. Amo da Isala: ili dunuma sisasu dawa: loma: ne agoane ba: mu.”
39 Choncho Eliezara, wansembe, anasonkhanitsa zofukizira zamkuwa zija zomwe anthu opsererawo anabwera nazo ndipo anazisula kuti zikhale zophimbira pa guwa lansembe,
Amaiba: le, gobele salasu dunu Elia: isa da laluoso gasa: le legesu lale, da: fe abenai hamoma: ne sia: i. Amalalu, ilia da amoga oloda dedeboi dagoi.
40 monga momwe Yehova anamulangizira kudzera mwa Mose. Chimenechi chinali chikumbutso kwa Aisraeli kuti munthu wina aliyense, kupatula zidzukulu za Aaroni, sayenera kupsereza lubani pamaso pa Yehova, kuopa kuti munthu woteroyo angakhale ngati Kora ndi omutsatira ake.
Amo da Isala: ili dunu ilima sisasu agoane ba: i. Sisasu da Elane egaga fi, ilia fawane da Hina Godema gabusiga: manoma ulagima: ne, oloda amoga doaga: mu da defea. Be eno dunu da amai hamonanu, e da Goula amola ea fa: no bobogesu dunu amo wadela: lesi dagoi ba: mu. Amo hou, Hina Gode da Mousesema, e da Elia: isama alofele sia: ma: ne sia: i.
41 Tsiku lotsatira, gulu lonse la Aisraeli linatsutsana ndi Mose ndi Aaroni. Iwo anati, “Inu mwapha anthu a Yehova.”
Eso eno aya amoga, Isala: ili fi dunu huluane da Mousese amola Elane elama egane sia: i, “Alia da Hina Gode Ea fi dunu mogili medole legei.”
42 Koma pamene anthuwo anasonkhana kuti atsutsane ndi Mose ndi Aaroni, atatembenuka kuyangʼana ku tenti ya msonkhano, mwadzidzidzi mtambo unaphimba tentiyo ndipo ulemerero wa Yehova unaonekera.
Ilia da Mousese amola Elane elama egane sia: musa: gilisi dagoloba, ilia da Abula Diasu ba: musa: sinidigisia, Mu Mobi Ganumu da Abula Diasu dedeboi amola Hina Gode Esalebe dawa: digima: ne sinenemegi hadigi misi dialebe ba: i.
43 Pamenepo Mose ndi Aaroni anapita patsogolo pa tenti ya msonkhano ija
Mousese amola Elane da asili, Abula Diasu ea midadi lelu.
44 ndipo Yehova anawuza Mose kuti,
Amola Hina Gode da Mousesema amane sia: i,
45 “Chokani pakati pa gulu la anthuwa kuti ndiwawononge kamodzinʼkamodzi.” Ndipo iwo anagwa pansi chafufumimba.
“Masa! Amo dunu yolesima! Na da amogawi wahadafa ili wadela: lesimu!” Mousese amola Elane ela da odagi osoboa beguduli,
46 Kenaka Mose anawuza Aaroni kuti, “Tenga chofukizira chako ndipo ikamo lubani pamodzi ndi moto wochokera pa guwa lansembe, fulumira, pita pa gulu la anthuwo ndipo ukachite nsembe yopepesera machimo awo popeza mkwiyo wa Yehova wafika, mliri wayamba.”
Mousese da Elanema amane sia: i, “Dia laluoso gasa: le legesu lale, oloda amoga laluoso lale, laluoso gasa: le legesu ganodini ligisili, gabusiga: manoma amo laluoso da: iya salima. Amasea hedolowane Isala: ili dunuma gaguli asili, dodofesu hou ilima hamomu. Hedolo! Hina Gode Ea ougi da heda: le, asi dagoi. Olo bagade da dunu fi ganodini mui dagoi.”
47 Ndipo Aaroni anachita monga ananenera Mose, nathamangira mʼkatikati mwa gulu la anthuwo. Pamenepo nʼkuti mliri utayamba kale pakati pa anthu aja ndipo Aaroni anafukiza lubani ndi kupereka nsembe yopepesera machimo awo.
Elane da Mousese ea sia: nababeba: le, ea laluoso gasa: le legesu lale, Isala: ili dunu gilisisu dogoa amo gusu hehenaiya heda: i. E da olo bagade da mui dagoi ba: beba: le, gabusiga: manoma amo laluoso ligisili, dodofesu hou dunu ili dodofema: ne hamoi dagoi.
48 Iye anayimirira pakati pa anthu amoyo ndi akufa ndipo mliri unaleka.
Amo hou da olo bagade madelai amo ea logo hedofai. Amalu, Elane da esala dunu la: idi amola bogoi dunu la: idi amoga dogoa lelebe ba: i.
49 Komabe anthu 14, 700 anafa ndi mliriwo, kuwonjezera pa aja amene anafa chifukwa cha Kora.
Dunu da olo bagadeba: le bogogia: i ilia idi da 14,700. Eno da Goula ea lelesuba: le bogoi ili da gilisili hame idi.
50 Ndipo Aaroni anabwerera kwa Mose ku khomo la tenti ya msonkhano, chifukwa mliriwo unali utatha.
Olo bagade da hedofai dagoi ba: loba, Elane da Mousese Abula Diasu logo holeiga esaloba amogai buhagi.

< Numeri 16 >