Aionian Verses
Ngakhale kuti ana ake onse aamuna ndi aakazi anasonkhana kudzamutonthoza, iye anakana kutonthozedwa. Iye anati, “Ayi. Ndidzalira mpaka ndidzapite kwa mwana wanga ku manda.” Choncho Israeli anapitirirabe kulira mwana wake. (Sheol )
(parallel missing)
Koma Yakobo anati, “Mwana wanga sapita nanu kumeneko; mkulu wake anamwalira ndipo watsala yekha. Ngati choyipa chitamuchitikira pa ulendo mukupitawu, ndiye kuti ndi mmene ndakalambiramu inu mudzandipha ndi chisoni chotere.” (Sheol )
(parallel missing)
Tsopano mukanditengeranso uyu, nakaphedwa mu njira ndiye kuti mudzandikankhira ku manda ndi chisoni.’ (Sheol )
(parallel missing)
ndipo akakaona kuti mnyamatayu palibe, basi akafa. Ife tidzakhala ngati takankhira abambo athu ku manda ndi chisoni. (Sheol )
(parallel missing)
Koma Yehova akachita china chake chachilendo, nthaka nitsekula pakamwa pake ndi kuwameza iwo pamodzi ndi zonse zimene ali nazo, iwowa nʼkulowa mʼmanda ali moyo, pamenepo mudzazindikira kuti anthu amenewa ananyoza Yehova.” (Sheol )
(parallel missing)
Analowa mʼmanda amoyo pamodzi ndi zonse zimene anali nazo. Nthaka inawatsekera ndi kuwawononga ndipo sanaonekenso. (Sheol )
(parallel missing)
Pakuti mkwiyo wanga wayaka ngati moto, umene umayaka mpaka ku dziko la anthu akufa. Motowo udzanyeketsa dziko lapansi ndi zokolola zake ndipo udzapsereza maziko a mapiri. (Sheol )
(parallel missing)
“Yehova amabweretsa imfa ndipo amaperekanso moyo, amatsitsira ku manda ndipo amawatulutsakonso. (Sheol )
(parallel missing)
Anandimanga ndi zingwe za ku manda; misampha ya imfa inalimbana nane. (Sheol )
(parallel missing)
Iwe uchite kwa iye molingana ndi nzeru zako, koma usalole kuti afe ndi ukalamba ndi kupita ku manda mwamtendere. (Sheol )
(parallel missing)
Koma tsopano usamuyese ngati munthu wosalakwa. Iwe ndiwe munthu wanzeru. Udzadziwa choti uchite naye. Ngakhale ndi wokalamba, aphedwe ndithu.” (Sheol )
(parallel missing)
Monga mtambo umazimirira ndi kukanganuka, momwemonso munthu amene walowa mʼmanda sabwerera. (Sheol )
(parallel missing)
Zili kutali kupambana mayiko akumwamba, nanga ungachite chiyani? Ndi zakuya kupambana kuya kwa manda, nanga ungadziwe chiyani? (Sheol )
(parallel missing)
“Aa, Inu mukanangondibisa mʼmanda ndi kundiphimba kuti ndisaoneke mpaka mkwiyo wanu utapita! Achikhala munandiyikira nthawi, kuti pambuyo pake mundikumbukirenso. (Sheol )
(parallel missing)
Ngati nyumba imene ndikuyiyembekezera ndi manda, ngati ndiyala bedi langa mu mdima, (Sheol )
(parallel missing)
Ndithu sindidzakhalanso ndi chiyembekezo chilichonse, polowa mʼmanda, pamene ndidzatsikira ku fumbi.” (Sheol )
(parallel missing)
Zaka zawo zimatha ali mu ulemerero ndipo amatsikira ku manda mwamtendere. (Sheol )
(parallel missing)
Monga momwe kutentha ndi chilala zimasungunulira madzi owundana ndi momwemonso mmene manda amachotsera omwe achimwa. (Sheol )
(parallel missing)
Dziko la anthu akufa ndi lapululu pamaso pa Mulungu; chiwonongeko ndi chosaphimbidwa. (Sheol )
(parallel missing)
Palibe amene amakukumbukirani pamene wamwalira; Amakutamandani ndani ali ku manda? (Sheol )
(parallel missing)
Oyipa amabwerera ku manda, mitundu yonse imene imayiwala Mulungu. (Sheol )
(parallel missing)
chifukwa Inu simudzandisiya ku manda, simudzalola kuti woyera wanu avunde. (Sheol )
(parallel missing)
Anandimanga ndi zingwe za ku manda; misampha ya imfa inalimbana nane. (Sheol )
(parallel missing)
Inu Yehova, munanditulutsa ku manda, munandisunga kuti ndisatsalire mʼdzenje. (Sheol )
(parallel missing)
Yehova musalole kuti ndichite manyazi, pakuti ndalirira kwa Inu; koma oyipa achititsidwe manyazi ndipo agone chete mʼmanda. (Sheol )
(parallel missing)
Monga nkhosa iwo ayenera kupita ku manda, ndipo imfa idzawadya. Olungama adzawalamulira mmawa; matupi awo adzavunda mʼmanda, kutali ndi nyumba zawo zaufumu. (Sheol )
(parallel missing)
Koma Mulungu adzawombola moyo wanga kuchoka ku manda; ndithu Iye adzanditengera kwa Iye mwini. (Sheol )
(parallel missing)
Mulole imfa itenge adani anga mwadzidzidzi; alowe mʼmanda ali amoyo pakuti choyipa chili pakati pawo. (Sheol )
(parallel missing)
Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu kwa ine; mwandipulumutsa ku malo ozama a manda. (Sheol )
(parallel missing)
Pakuti ndili ndi mavuto ambiri ndipo moyo wanga ukuyandikira ku manda. (Sheol )
(parallel missing)
Kodi ndi munthu uti angakhale ndi moyo ndi kusaona imfa? Kapena kudzipulumutsa yekha ku mphamvu ya manda? (Sela) (Sheol )
(parallel missing)
Zingwe za imfa zinandizinga, zoopsa za ku dziko la anthu akufa zinandigwera; ndinapeza mavuto ndi chisoni. (Sheol )
(parallel missing)
Ndikakwera kumwamba, Inu muli komweko; ndikakagona ku malo a anthu akufa, Inu muli komweko. (Sheol )
(parallel missing)
Iwo adzati, “Monga momwe nkhuni zimamwazikira akaziwaza, ndi momwenso mafupa athu amwazikira pa khomo la manda.” (Sheol )
(parallel missing)
tiwameze amoyo ngati manda, ndi athunthu ngati anthu otsikira mʼdzenje. (Sheol )
(parallel missing)
Mapazi ake amatsikira ku imfa; akamayenda ndiye kuti akupita ku manda. (Sheol )
(parallel missing)
Nyumba yake ndi njira yopita ku manda, yotsikira ku malo a anthu akufa. (Sheol )
(parallel missing)
Koma amunawo sadziwa kuti akufa ali kale komweko, ndi kuti alendo ake alowa kale mʼmanda akuya. (Sheol )
(parallel missing)
Manda ndi chiwonongeko ndi zosabisika pamaso pa Yehova, nanji mitima ya anthu! (Sheol )
(parallel missing)
Munthu wanzeru amatsata njira yopita ku moyo kuti apewe malo okhala anthu akufa. (Sheol )
(parallel missing)
Ukamukwapula ndi tsatsa udzapulumutsa moyo wake. (Sheol )
(parallel missing)
Manda sakhuta, nawonso maso a munthu sakhuta. (Sheol )
(parallel missing)
Manda, mkazi wosabala, nthaka yosakhuta madzi ndiponso moto womangoyakirayakira!” (Sheol )
(parallel missing)
Ntchito iliyonse imene ukuyigwira, uyigwire ndi mphamvu zako zonse, pakuti ku manda kumene ukupita kulibe kugwira ntchito, kulibe malingaliro, chidziwitso ndiponso nzeru. (Sheol )
(parallel missing)
Undiyike pamtima pako ngati chidindo, ngati chidindo cha pa dzanja lako; pakuti chikondi nʼchamphamvu ngati imfa, nsanje ndiyaliwuma ngati manda. Chikondi chimachita kuti lawilawi ngati malawi a moto wamphamvu. (Sheol )
(parallel missing)
Nʼchifukwa chake ku manda sikukhuta ndipo kwayasama kwambiri kukamwa kwake; mʼmandamo mudzagweranso anthu otchuka a mu Yerusalemu pamodzi ndi anthu wamba ochuluka; adzagweramo ali wowowo, nʼkuledzera kwawoko. (Sheol )
(parallel missing)
“Pempha chizindikiro kwa Yehova Mulungu wako, chikhale chozama ngati manda kapena chachitali ngati mlengalenga.” (Sheol )
(parallel missing)
Ku manda kwatekeseka kuti akulandire ukamabwera; mizimu ya anthu akufa, aja amene anali atsogoleri a dziko lapansi, yadzutsidwa. Onse amene anali mafumu a mitundu ya anthu ayimiritsidwa pa mipando yawo. (Sheol )
(parallel missing)
Ulemerero wako wonse walowa mʼmanda, pamodzi ndi nyimbo za azeze ako; mphutsi zayalana pogona pako ndipo chofunda chako ndi nyongolotsi. (Sheol )
(parallel missing)
Koma watsitsidwa mʼmanda pansi penipeni pa dzenje. (Sheol )
(parallel missing)
Inu mumayankhula monyada kuti, “Ife tinachita pangano ndi imfa, ife tachita mgwirizano ndi manda. Pamene mliri woopsa ukadzafika sudzatikhudza ife, chifukwa timadalira bodza ngati pothawirapo pathu ndi chinyengo ngati malo anthu obisalapo.” (Sheol )
(parallel missing)
Pangano limene munachita ndi imfa lidzathetsedwa; mgwirizano wanu ndi manda udzachotsedwa. Pakuti mliri woopsa udzafika, ndipo udzakugonjetsani. (Sheol )
(parallel missing)
Ine ndinaganiza kuti ndidzapita ku dziko la akufa pamene moyo ukukoma. (Sheol )
(parallel missing)
Pakuti akumanda sangathe kukutamandani, akufa sangayimbe nyimbo yokutamandani. Iwo amene akutsikira ku dzenje sangakukhulupirireni. (Sheol )
(parallel missing)
Mumapita kukapembedza fano la Moleki mutatenga mafuta ndi zonunkhira zochuluka. Munachita kutumiza akazembe anu kutali; inu ngakhale munapita ku manda kwenikweniko! (Sheol )
(parallel missing)
“‘Ine Ambuye Yehova ndikuti: Pa nthawi imene mkungudzawo unatsikira ku manda, ndinawuza nyanja kuti iwulire maliro pakuwuphimba. Ndinawumitsa mitsinje ndipo madzi ambiri anaphwa. Ndinabweretsa mdima pa Lebanoni chifukwa cha mtengowo ndipo mitengo yonse ya mʼdzikomo inawuma. (Sheol )
(parallel missing)
Mitundu ya anthu inagwedezeka pakumva mkokomo wa kugwa kwake, pamene ndinawutsitsira ku manda pamodzi ndi iwo amene anafa. Pamenepo ku dziko la akufa mitengo yonse ya ku Edeni pamodzi ndi ya ku Lebanoni yosankhidwa bwino inasangalatsidwa chifukwa cha zimenezi. (Sheol )
(parallel missing)
Amene ankakhala mu mthunzi wake, amene ankayanjana nawo, iwonso anapita nawo pamodzi ku manda, kukakhala pamodzi ndi amene anaphedwa ndi lupanga pakati pa mitundu ya anthu. (Sheol )
(parallel missing)
Mʼkati mwa manda atsogoleri amphamvu pamodzi ndi ogwirizana nawo azidzakambirana za Igupto nʼkumati, ‘Afika kuno anthu osachita mdulidwe aja! Ndi awa agona apawa, ophedwa pa nkhondo.’ (Sheol )
(parallel missing)
Iwo sanayikidwe mwaulemu ngati ankhondo amphamvu amakedzana, amene anatsikira ku dziko la anthu akufa ndi zida zawo zomwe za nkhondo. Malupanga awo anawayika ku mitu yawo, ndipo zishango zawo anaphimba mafupa awo. Kale anthu amphamvu amenewa ankaopsa dziko la anthu amoyo. (Sheol )
(parallel missing)
“Ndidzawapulumutsa ku mphamvu ya manda; ndidzawawombola ku imfa. Kodi iwe imfa, miliri yako ili kuti? Kodi iwe manda, kuwononga kwako kuli kuti? “Sindidzachitanso chifundo, (Sheol )
(parallel missing)
Ngakhale atakumba pansi mpaka ku malo a anthu akufa, dzanja langa lidzawatulutsa kumeneko. Ngakhale atakwera kumwamba Ine ndidzawatsakamutsa kumeneko. (Sheol )
(parallel missing)
Iye anati: “Pamene ndinali mʼmavuto anga ndinayitana Yehova, ndipo Iye anandiyankha. Ndili ku dziko la anthu akufa ndinapempha thandizo, ndipo Inu munamva kulira kwanga. (Sheol )
(parallel missing)
Ndithu, wasokonezeka ndi vinyo; ndi wodzitama ndiponso wosakhazikika. Pakuti ngodzikonda ngati manda, ngosakhutitsidwa ngati imfa, wadzisonkhanitsira mitundu yonse ya anthu ndipo wagwira ukapolo anthu a mitundu yonse. (Sheol )
(parallel missing)
Koma Ine ndikukuwuzani kuti aliyense wokwiyira mʼbale wake adzapezeka wolakwa ku bwalo la milandu. Ndiponso aliyense amene wonena mʼbale wake kuti, ‘Ndiwe wopanda phindu,’ adzapezeka wolakwa ku bwalo la milandu lalikulu. Ndipo aliyense amene anganene mnzake ‘wopandapake’ adzatengeredwa ku bwalo la milandu. Ndiponso aliyense amene angamunene mnzake kuti, ‘Chitsiru iwe,’ adzaponyedwa ku gehena. (Geenna )
កិន្ត្វហំ យុឞ្មាន៑ វទាមិ, យះ កឝ្ចិត៑ ការណំ វិនា និជភ្រាត្រេ កុប្យតិ, ស វិចារសភាយាំ ទណ្ឌាហ៌ោ ភវិឞ្យតិ; យះ កឝ្ចិច្ច ស្វីយសហជំ និព៌្ពោធំ វទតិ, ស មហាសភាយាំ ទណ្ឌាហ៌ោ ភវិឞ្យតិ; បុនឝ្ច ត្វំ មូឍ ឥតិ វាក្យំ យទិ កឝ្ចិត៑ ស្វីយភ្រាតរំ វក្តិ, តហ៌ិ នរកាគ្នៅ ស ទណ្ឌាហ៌ោ ភវិឞ្យតិ។ (Geenna )
Ngati diso lako lakumanja likuchimwitsa, ulichotse ndi kulitaya. Pakuti nʼkwabwino kwa iwe kutaya chiwalo chimodzi cha thupi lako, kusiyana ndi kuti thupi lonse liponyedwe mʼgehena. (Geenna )
តស្មាត៑ តវ ទក្ឞិណំ នេត្រំ យទិ ត្វាំ ពាធតេ, តហ៌ិ តន្នេត្រម៑ ឧត្បាដ្យ ទូរេ និក្ឞិប, យស្មាត៑ តវ សវ៌្វវបុឞោ នរកេ និក្ឞេបាត៑ តវៃកាង្គស្យ នាឝោ វរំ។ (Geenna )
Ndipo ngati dzanja lako lamanja likuchimwitsa, ulidule ndi kulitaya. Pakuti nʼkwabwino kwa iwe kutaya chiwalo chimodzi cha thupi lako, kusiyana ndi kuti thupi lonse liponyedwe mʼgehena. (Geenna )
យទ្វា តវ ទក្ឞិណះ ករោ យទិ ត្វាំ ពាធតេ, តហ៌ិ តំ ករំ ឆិត្ត្វា ទូរេ និក្ឞិប, យតះ សវ៌្វវបុឞោ នរកេ និក្ឞេបាត៑ ឯកាង្គស្យ នាឝោ វរំ។ (Geenna )
Musamaope amene amapha thupi koma sangathe kuchotsa moyo. Koma muziopa Iye amene akhoza kupha mzimu ndi kuwononga thupi mu gehena. (Geenna )
យេ កាយំ ហន្តុំ ឝក្នុវន្តិ នាត្មានំ, តេភ្យោ មា ភៃឞ្ដ; យះ កាយាត្មានៅ និរយេ នាឝយិតុំ, ឝក្នោតិ, តតោ ពិភីត។ (Geenna )
Ndipo iwe Kaperenawo, kodi udzakwezedwa kufika kumwamba? Ayi, udzatsitsidwa mpaka pansi kufika ku Hade. Ngati zodabwitsa zimene zinachitika mwa iwe, zikanachitika mu Sodomu, bwenzi iye alipo kufikira lero. (Hadēs )
អបរញ្ច ពត កផន៌ាហូម៑, ត្វំ ស្វគ៌ំ យាវទុន្នតោសិ, កិន្តុ នរកេ និក្ឞេប្ស្យសេ, យស្មាត៑ ត្វយិ យាន្យាឝ្ចយ៌្យាណិ កម៌្មណ្យការិឞត, យទិ តានិ សិទោម្នគរ អការិឞ្យន្ត, តហ៌ិ តទទ្យ យាវទស្ថាស្យត៑។ (Hadēs )
Aliyense amene anena mawu otsutsana ndi Mwana wa Munthu adzakhululukidwa koma aliyense wonena motsutsana ndi Mzimu Woyera sadzakhululukidwa mu mʼbado uno kapena umene ukubwerawo. (aiōn )
យោ មនុជសុតស្យ វិរុទ្ធាំ កថាំ កថយតិ, តស្យាបរាធស្យ ក្ឞមា ភវិតុំ ឝក្នោតិ, កិន្តុ យះ កឝ្ចិត៑ បវិត្រស្យាត្មនោ វិរុទ្ធាំ កថាំ កថយតិ នេហលោកេ ន ប្រេត្យ តស្យាបរាធស្យ ក្ឞមា ភវិតុំ ឝក្នោតិ។ (aiōn )
Zimene zinafesedwa pakati pa minga, ndi munthu amene amamva mawu koma nkhawa za moyo uno ndi chinyengo cha chuma zimalepheretsa mawuwo kuti abale chipatso. (aiōn )
អបរំ កណ្ដកានាំ មធ្យេ ពីជាន្យុប្តានិ តទត៌្ហ ឯឞះ; កេនចិត៑ កថាយាំ ឝ្រុតាយាំ សាំសារិកចិន្តាភិ រ្ភ្រាន្តិភិឝ្ច សា គ្រស្យតេ, តេន សា មា វិផលា ភវតិ។ (aiōn )
Ndipo amene anafesa namsongole ndi Satana. Kukolola ndiko kutha kwa dzikoli ndipo otuta ndi angelo. (aiōn )
វន្យយវសានិ បាបាត្មនះ សន្តានាះ។ យេន រិបុណា តាន្យុប្តានិ ស ឝយតានះ, កត៌្តនសមយឝ្ច ជគតះ ឝេឞះ, កត៌្តកាះ ស្វគ៌ីយទូតាះ។ (aiōn )
“Monga momwe namsongole azulidwa ndi kutenthedwa ndi moto, momwemonso kudzakhala pakutha kwa dziko. (aiōn )
យថា វន្យយវសានិ សំគ្ឫហ្យ ទាហ្យន្តេ, តថា ជគតះ ឝេឞេ ភវិឞ្យតិ; (aiōn )
Umu ndi mmene kudzakhalira pakutha kwa dziko. Angelo adzabwera ndi kulekanitsa oyipa ndi olungama. (aiōn )
តថៃវ ជគតះ ឝេឞេ ភវិឞ្យតិ, ផលតះ ស្វគ៌ីយទូតា អាគត្យ បុណ្យវជ្ជនានាំ មធ្យាត៑ បាបិនះ ប្ឫថក៑ ក្ឫត្វា វហ្និកុណ្ឌេ និក្ឞេប្ស្យន្តិ, (aiōn )
Ndipo Ine ndikuwuza iwe kuti ndiwe Petro ndipo pa thanthwe ili Ine ndidzamangapo mpingo wanga ndipo makomo a ku gehena sadzawugonjetsa. (Hadēs )
អតោៜហំ ត្វាំ វទាមិ, ត្វំ បិតរះ (ប្រស្តរះ) អហញ្ច តស្យ ប្រស្តរស្យោបរិ ស្វមណ្ឌលីំ និម៌្មាស្យាមិ, តេន និរយោ ពលាត៑ តាំ បរាជេតុំ ន ឝក្ឞ្យតិ។ (Hadēs )
Ngati dzanja lako kapena phazi lako likuchimwitsa, lidule ndi kulitaya. Ndi bwino kwa iwe kulowa mʼmoyo wosatha wolumala kusiyana ndi kukhala ndi manja awiri kapena mapazi awiri ndi kukaponyedwa ku moto wosatha. (aiōnios )
តស្មាត៑ តវ ករឝ្ចរណោ វា យទិ ត្វាំ ពាធតេ, តហ៌ិ តំ ឆិត្ត្វា និក្ឞិប, ទ្វិករស្យ ទ្វិបទស្យ វា តវានប្តវហ្នៅ និក្ឞេបាត៑, ខញ្ជស្យ វា ឆិន្នហស្តស្យ តវ ជីវនេ ប្រវេឝោ វរំ។ (aiōnios )
Ndipo ngati diso lako likuchimwitsa, ulichotse ndi kulitaya. Ndi bwino kwa iwe kuti ukalowe ku moyo wosatha ndi diso limodzi kuposa ndi kukhala ndi maso awiri ndi kukaponyedwa ku moto wa gehena.” (Geenna )
អបរំ តវ នេត្រំ យទិ ត្វាំ ពាធតេ, តហ៌ិ តទប្យុត្បាវ្យ និក្ឞិប, ទ្វិនេត្រស្យ នរកាគ្នៅ និក្ឞេបាត៑ កាណស្យ តវ ជីវនេ ប្រវេឝោ វរំ។ (Geenna )
Taonani mnyamata wina anabwera kwa Yesu namufunsa kuti, “Aphunzitsi, ndi chinthu chiti chabwino chimene ndiyenera kuchita kuti ndipeze moyo wosatha?” (aiōnios )
អបរម៑ ឯក អាគត្យ តំ បប្រច្ឆ, ហេ បរមគុរោ, អនន្តាយុះ ប្រាប្តុំ មយា កិំ កិំ សត្កម៌្ម កត៌្តវ្យំ? (aiōnios )
Ndipo aliyense amene wasiya nyumba, kapena abale, kapena alongo, kapena bambo kapena mayi kapena mkazi, kapena ana, kapena minda chifukwa cha Ine adzalandira madalitso ochuluka ndi kulandiranso moyo wosatha. (aiōnios )
អន្យច្ច យះ កឝ្ចិត៑ មម នាមការណាត៑ គ្ឫហំ វា ភ្រាតរំ វា ភគិនីំ វា បិតរំ វា មាតរំ វា ជាយាំ វា ពាលកំ វា ភូមិំ បរិត្យជតិ, ស តេឞាំ ឝតគុណំ លប្ស្យតេ, អនន្តាយុមោៜធិការិត្វញ្ច ប្រាប្ស្យតិ។ (aiōnios )
Ataona mtengo wamkuyu mʼmbali mwa msewu, anapitapo koma sanapeze kanthu koma masamba okhaokha. Pamenepo anati kwa mtengowo, “Usadzabalenso chipatso!” Nthawi yomweyo mtengowo unafota. (aiōn )
តតោ មាគ៌បាឝ៌្វ ឧឌុម្ពរវ្ឫក្ឞមេកំ វិលោក្យ តត្សមីបំ គត្វា បត្រាណិ វិនា កិមបិ ន ប្រាប្យ តំ បាទបំ ប្រោវាច, អទ្យារភ្យ កទាបិ ត្វយិ ផលំ ន ភវតុ; តេន តត្ក្ឞណាត៑ ស ឧឌុម្ពរមាហីរុហះ ឝុឞ្កតាំ គតះ។ (aiōn )
“Tsoka kwa inu, aphunzitsi amalamulo ndi Afarisi, achiphamaso! Mumayenda maulendo ambiri pa mtunda ndi pa nyanja kuti mutembenuze munthu mmodzi, ndipo akatembenuka, mumamusandutsa kukhala mwana wa gehena kawiri kuposa inu. (Geenna )
កញ្ចន ប្រាប្យ ស្វតោ ទ្វិគុណនរកភាជនំ តំ កុរុថ។ (Geenna )
“Njoka inu! Ana amamba! Mudzachithawa bwanji chilango cha gehena? (Geenna )
រេ ភុជគាះ ក្ឫឞ្ណភុជគវំឝាះ, យូយំ កថំ នរកទណ្ឌាទ៑ រក្ឞិឞ្យធ្វេ។ (Geenna )
Pamene Yesu anakhala pansi pa phiri la Olivi, ophunzira ake anabwera kwa Iye mwamseri nati, “Tiwuzeni, kodi izi zidzachitika liti, ndipo chizindikiro cha kubwera kwanu ndi zizindikiro za kutha kwa dziko zidzakhala chiyani?” (aiōn )
អនន្តរំ តស្មិន៑ ជៃតុនបវ៌្វតោបរិ សមុបវិឞ្ដេ ឝិឞ្យាស្តស្យ សមីបមាគត្យ គុប្តំ បប្រច្ឆុះ, ឯតា ឃដនាះ កទា ភវិឞ្យន្តិ? ភវត អាគមនស្យ យុគាន្តស្យ ច កិំ លក្ឞ្ម? តទស្មាន៑ វទតុ។ (aiōn )
“Pamenepo adzanena kwa akumanzere kwake kuti, ‘Chokani kwa Ine, inu otembereredwa, pitani ku moto wosatha wokonzedwera mdierekezi ndi angelo ake. (aiōnios )
បឝ្ចាត៑ ស វាមស្ថិតាន៑ ជនាន៑ វទិឞ្យតិ, រេ ឝាបគ្រស្តាះ សវ៌្វេ, ឝៃតានេ តស្យ ទូតេភ្យឝ្ច យោៜនន្តវហ្និរាសាទិត អាស្តេ, យូយំ មទន្តិកាត៑ តមគ្និំ គច្ឆត។ (aiōnios )
“Amenewa adzapita ku chilango chosatha pamene olungama ku moyo wosatha.” (aiōnios )
បឝ្ចាទម្យនន្តឝាស្តិំ កិន្តុ ធាម៌្មិកា អនន្តាយុឞំ ភោក្តុំ យាស្យន្តិ។ (aiōnios )
ndi kuwaphunzitsa amvere zonse zimene ndinakulamulirani. Ndipo onani, Ine ndidzakhala pamodzi ndi inu kufikira kutha kwa dziko lapansi pano.” (aiōn )
បឝ្យត, ជគទន្តំ យាវត៑ សទាហំ យុឞ្មាភិះ សាកំ តិឞ្ឋាមិ។ ឥតិ។ (aiōn )
koma aliyense amene achitira mwano Mzimu Woyera sadzakhululukidwa pakuti wachita tchimo losatha.” (aiōn , aiōnios )
កិន្តុ យះ កឝ្ចិត៑ បវិត្រមាត្មានំ និន្ទតិ តស្យាបរាធស្យ ក្ឞមា កទាបិ ន ភវិឞ្យតិ សោនន្តទណ្ឌស្យាហ៌ោ ភវិឞ្យតិ។ (aiōn , aiōnios )
Mark 4:18 (មាក៌ះ 4:18)
(parallel missing)
យេ ជនាះ កថាំ ឝ្ឫណ្វន្តិ កិន្តុ សាំសារិកី ចិន្តា ធនភ្រាន្តិ រ្វិឞយលោភឝ្ច ឯតេ សវ៌្វេ ឧបស្ថាយ តាំ កថាំ គ្រសន្តិ តតះ មា វិផលា ភវតិ (aiōn )
koma nkhawa zamoyo uno, chinyengo cha chuma ndi zokhumba za zinthu zina zimabwera ndi kutchinga mawu, ndipo amawachititsa kukhala osabala chipatso. (aiōn )
(parallel missing)
Ngati dzanja lako likuchimwitsa, lidule. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa mʼmoyo ndi dzanja limodzi kusiyana ndi kukhala ndi manja awiri ndi kupita ku gehena, kumene moto wake suzima. (Geenna )
(parallel missing)
Mark 9:44 (មាក៌ះ 9:44)
(parallel missing)
យស្មាត៑ យត្រ កីដា ន ម្រិយន្តេ វហ្និឝ្ច ន និវ៌្វាតិ, តស្មិន៑ អនិវ៌្វាណានលនរកេ ករទ្វយវស្តវ គមនាត៑ ករហីនស្យ ស្វគ៌ប្រវេឝស្តវ ក្ឞេមំ។ (Geenna )
Ndipo ngati phazi lako likuchimwitsa, lidule. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa mʼmoyo olumala kusiyana ndi kukhala ndi mapazi awiri ndi kuponyedwa mu gehena. (Geenna )
(parallel missing)
Mark 9:46 (មាក៌ះ 9:46)
(parallel missing)
យតោ យត្រ កីដា ន ម្រិយន្តេ វហ្និឝ្ច ន និវ៌្វាតិ, តស្មិន៑ ៜនិវ៌្វាណវហ្នៅ នរកេ ទ្វិបាទវតស្តវ និក្ឞេបាត៑ បាទហីនស្យ ស្វគ៌ប្រវេឝស្តវ ក្ឞេមំ។ (Geenna )
Ndipo ngati diso lako likuchimwitsa, likolowole. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa ufumu wa Mulungu ndi diso limodzi, kusiyana ndi kukhala ndi maso awiri ndi kuponyedwa mu gehena, (Geenna )
(parallel missing)
Mark 9:48 (មាក៌ះ 9:48)
(parallel missing)
តស្មិន ៜនិវ៌្វាណវហ្នៅ នរកេ ទ្វិនេត្រស្យ តវ និក្ឞេបាទ៑ ឯកនេត្រវត ឦឝ្វររាជ្យេ ប្រវេឝស្តវ ក្ឞេមំ។ (Geenna )
Yesu atanyamuka, munthu wina anamuthamangira nagwa mogwada pamaso pake. Iye anafunsa kuti, “Aphunzitsi abwino, ndichite chiyani kuti ndilandire moyo wosatha?” (aiōnios )
អថ ស វត៌្មនា យាតិ, ឯតហ៌ិ ជន ឯកោ ធាវន៑ អាគត្យ តត្សម្មុខេ ជានុនី បាតយិត្វា ប្ឫឞ្ដវាន៑, ភោះ បរមគុរោ, អនន្តាយុះ ប្រាប្តយេ មយា កិំ កត៌្តវ្យំ? (aiōnios )
adzalephera kulandira 100 (nyumba, abale, alongo, amayi, ana ndi minda, pamodzi ndi mazunzo) mʼbado uno ndi moyo wosatha nthawi ya mʼtsogolo. (aiōn , aiōnios )
គ្ឫហភ្រាត្ឫភគិនីបិត្ឫមាត្ឫបត្នីសន្តានភូមីនាមិហ ឝតគុណាន៑ ប្រេត្យានន្តាយុឝ្ច ន ប្រាប្នោតិ តាទ្ឫឝះ កោបិ នាស្តិ។ (aiōn , aiōnios )
Ndipo Iye anati kwa mtengo, “Palibe amene adzadyenso chipatso kuchokera kwa iwe.” Ndipo ophunzira ake anamva Iye akunena izi. (aiōn )
អទ្យារភ្យ កោបិ មានវស្ត្វត្តះ ផលំ ន ភុញ្ជីត; ឥមាំ កថាំ តស្យ ឝិឞ្យាះ ឝុឝ្រុវុះ។ (aiōn )
ndipo adzalamulira pa nyumba ya Yakobo ku nthawi zonse; ufumu wake sudzatha.” (aiōn )
តថា ស យាកូពោ វំឝោបរិ សវ៌្វទា រាជត្វំ ករិឞ្យតិ, តស្យ រាជត្វស្យាន្តោ ន ភវិឞ្យតិ។ (aiōn )
Luke 1:54 (លូកះ 1:54)
(parallel missing)
ឥព្រាហីមិ ច តទ្វំឝេ យា ទយាស្តិ សទៃវ តាំ។ ស្ម្ឫត្វា បុរា បិត្ឫណាំ នោ យថា សាក្ឞាត៑ ប្រតិឝ្រុតំ។ (aiōn )
Kwa Abrahamu ndi zidzukulu zake ku nthawi zonse monga ananena kwa makolo athu.” (aiōn )
(parallel missing)
(Monga mmene ananenera kudzera mwa aneneri oyera), (aiōn )
(parallel missing)
Luke 1:73 (លូកះ 1:73)
(parallel missing)
ស្ឫឞ្ដេះ ប្រថមតះ ស្វីយៃះ បវិត្រៃ រ្ភាវិវាទិភិះ។ (aiōn )
Ndipo ziwandazo zimamupempha mobwerezabwereza kuti asazitumize ku dzenje la mdima. (Abyssos )
អថ ភូតា វិនយេន ជគទុះ, គភីរំ គត៌្តំ គន្តុំ មាជ្ញាបយាស្មាន៑។ (Abyssos )
Kodi iwe Kaperenawo, adzakukweza mpaka kumwamba? Ayi, adzakutsitsa mpaka ku Malo a anthu akufa. (Hadēs )
ហេ កផន៌ាហូម៑, ត្វំ ស្វគ៌ំ យាវទ៑ ឧន្នតា កិន្តុ នរកំ យាវត៑ ន្យគ្ភវិឞ្យសិ។ (Hadēs )
Nthawi ina katswiri wa malamulo anayimirira kuti ayese Yesu. Iye anati, “Aphunzitsi, ndichite chiyani kuti ndikhale ndi moyo wosatha?” (aiōnios )
អនន្តរម៑ ឯកោ វ្យវស្ថាបក ឧត្ថាយ តំ បរីក្ឞិតុំ បប្រច្ឆ, ហេ ឧបទេឝក អនន្តាយុឞះ ប្រាប្តយេ មយា កិំ ករណីយំ? (aiōnios )
Koma Ine ndidzakuonetsani amene muyenera kumuopa: Wopani Iye, amene pambuyo pakupha thupi, ali ndi mphamvu yakukuponyani ku gehena. Inde, Ine ndikuwuzani, muopeni Iye. (Geenna )
តហ៌ិ កស្មាទ៑ ភេតវ្យម៑ ឥត្យហំ វទាមិ, យះ ឝរីរំ នាឝយិត្វា នរកំ និក្ឞេប្តុំ ឝក្នោតិ តស្មាទេវ ភយំ កុរុត, បុនរបិ វទាមិ តស្មាទេវ ភយំ កុរុត។ (Geenna )
“Bwana anayamikira kapitawo wosakhulupirikayo popeza anachita mochenjera. Pakuti anthu a dziko lino lapansi ndi ochenjera kwambiri akamachita zinthu ndi anthu ofanana nawo kuposa anthu a kuwunika. (aiōn )
តេនៃវ ប្រភុស្តមយថាត៌្ហក្ឫតម៑ អធីឝំ តទ្ពុទ្ធិនៃបុណ្យាត៑ ប្រឝឝំស; ឥត្ថំ ទីប្តិរូបសន្តានេភ្យ ឯតត្សំសារស្យ សន្តានា វត៌្តមានកាលេៜធិកពុទ្ធិមន្តោ ភវន្តិ។ (aiōn )
Ine ndikukuwuzani inu, gwiritsani ntchito chuma cha dziko lapansi kuti mudzipezere nokha abwenzi, kuti pamene chatha mudzalandiridwe mʼmalo okhala amuyaya. (aiōnios )
អតោ វទាមិ យូយមប្យយថាត៌្ហេន ធនេន មិត្រាណិ លភធ្វំ តតោ យុឞ្មាសុ បទភ្រឞ្ដេឞ្វបិ តានិ ចិរកាលម៑ អាឝ្រយំ ទាស្យន្តិ។ (aiōnios )
Ali mʼgehena kuzunzika, anakweza maso ake ndipo anaona Abrahamu ali ndi Lazaro pambali pake. (Hadēs )
បឝ្ចាត៑ ស ធនវានបិ មមារ, តំ ឝ្មឝានេ ស្ថាបយាមាសុឝ្ច; កិន្តុ បរលោកេ ស វេទនាកុលះ សន៑ ឩទ៌្ធ្វាំ និរីក្ឞ្យ ពហុទូរាទ៑ ឥព្រាហីមំ តត្ក្រោឌ ឥលិយាសរញ្ច វិលោក្យ រុវន្នុវាច; (Hadēs )
Oweruza wina wake anamufunsa Iye kuti, “Aphunzitsi abwino, ndichite chiyani kuti ndilandire moyo wosatha?” (aiōnios )
អបរម៑ ឯកោធិបតិស្តំ បប្រច្ឆ, ហេ បរមគុរោ, អនន្តាយុឞះ ប្រាប្តយេ មយា កិំ កត៌្តវ្យំ? (aiōnios )
adzalephera kulandira mowirikiza mʼmoyo uno, ndi mʼmoyo ukubwerawo, moyo wosatha.” (aiōn , aiōnios )
ឥហ កាលេ តតោៜធិកំ បរកាលេ ៜនន្តាយុឝ្ច ន ប្រាប្ស្យតិ លោក ឦទ្ឫឝះ កោបិ នាស្តិ។ (aiōn , aiōnios )
Yesu anayankha kuti, “Anthu a mʼbado uno amakwatira ndi kukwatiwa. (aiōn )
តទា យីឝុះ ប្រត្យុវាច, ឯតស្យ ជគតោ លោកា វិវហន្តិ វាគ្ទត្តាឝ្ច ភវន្តិ (aiōn )
Koma mʼmoyo umene ukubwerawo, anthu amene adzaukitsidwe kwa akufa sadzakwatira kapena kukwatiwa. (aiōn )
កិន្តុ យេ តជ្ជគត្ប្រាប្តិយោគ្យត្វេន គណិតាំ ភវិឞ្យន្តិ ឝ្មឝានាច្ចោត្ថាស្យន្តិ តេ ន វិវហន្តិ វាគ្ទត្តាឝ្ច ន ភវន្តិ, (aiōn )
kuti aliyense amene akhulupirira Iye akhale ndi moyo wosatha. (aiōnios )
តស្មាទ៑ យះ កឝ្ចិត៑ តស្មិន៑ វិឝ្វសិឞ្យតិ សោៜវិនាឝ្យះ សន៑ អនន្តាយុះ ប្រាប្ស្យតិ។ (aiōnios )
“Pakuti Mulungu anakonda dziko lapansi, kotero anapereka Mwana wake wobadwa yekha, kuti aliyense wokhulupirira Iye asatayike koma akhale ndi moyo wosatha. (aiōnios )
ឦឝ្វរ ឥត្ថំ ជគទទយត យត៑ ស្វមទ្វិតីយំ តនយំ ប្រាទទាត៑ តតោ យះ កឝ្ចិត៑ តស្មិន៑ វិឝ្វសិឞ្យតិ សោៜវិនាឝ្យះ សន៑ អនន្តាយុះ ប្រាប្ស្យតិ។ (aiōnios )
Aliyense wokhulupirira Mwanayo ali ndi moyo wosatha, koma iye amene samvera Mwanayo sadzawuona moyo, pakuti mkwiyo wa Mulungu umakhala pa iye.” (aiōnios )
យះ កឝ្ចិត៑ បុត្រេ វិឝ្វសិតិ ស ឯវានន្តម៑ បរមាយុះ ប្រាប្នោតិ កិន្តុ យះ កឝ្ចិត៑ បុត្រេ ន វិឝ្វសិតិ ស បរមាយុឞោ ទឝ៌នំ ន ប្រាប្នោតិ កិន្ត្វីឝ្វរស្យ កោបភាជនំ ភូត្វា តិឞ្ឋតិ។ (aiōnios )
koma aliyense amene adzamwa madzi amene Ine ndidzamupatsa sadzamvanso ludzu. Ndithudi, madzi amene ndidzamupatsa adzakhala kasupe wamadzi wotumphukira ku moyo wosatha.” (aiōn , aiōnios )
កិន្តុ មយា ទត្តំ បានីយំ យះ បិវតិ ស បុនះ កទាបិ ត្ឫឞាត៌្តោ ន ភវិឞ្យតិ។ មយា ទត្តម៑ ឥទំ តោយំ តស្យាន្តះ ប្រស្រវណរូបំ ភូត្វា អនន្តាយុយ៌ាវត៑ ស្រោឞ្យតិ។ (aiōn , aiōnios )
Ngakhale tsopano amene akukolola akulandira malipiro ake, ndipo akututa mbewu ku moyo wosatha kuti wofesa ndi wokolola asangalale pamodzi. (aiōnios )
យឝ្ឆិនត្តិ ស វេតនំ លភតេ អនន្តាយុះស្វរូបំ ឝស្យំ ស គ្ឫហ្លាតិ ច, តេនៃវ វប្តា ឆេត្តា ច យុគបទ៑ អានន្ទតះ។ (aiōnios )
“Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti aliyense amene amamva mawu anga ndi kukhulupirira Iye amene ananditumiza Ine, ali ndi moyo wosatha ndipo sadzaweruzidwa. Iye wachoka mu imfa ndipo walowa mʼmoyo. (aiōnios )
យុឞ្មានាហំ យថាត៌្ហតរំ វទាមិ យោ ជនោ មម វាក្យំ ឝ្រុត្វា មត្ប្រេរកេ វិឝ្វសិតិ សោនន្តាយុះ ប្រាប្នោតិ កទាបិ ទណ្ឌពាជនំ ន ភវតិ និធនាទុត្ថាយ បរមាយុះ ប្រាប្នោតិ។ (aiōnios )
Inu mumasanthula malemba chifukwa mumaganiza kuti mʼmalembamo muli moyo wosatha. Awa ndi malemba amene akundichitira umboni. (aiōnios )
ធម៌្មបុស្តកានិ យូយម៑ អាលោចយធ្វំ តៃ រ្វាក្យៃរនន្តាយុះ ប្រាប្ស្យាម ឥតិ យូយំ ពុធ្យធ្វេ តទ្ធម៌្មបុស្តកានិ មទត៌្ហេ ប្រមាណំ ទទតិ។ (aiōnios )
Gwirani ntchito, osati chifukwa cha chakudya chimene chimawonongeka koma chifukwa cha chakudya chimene sichiwonongeka mpaka ku moyo wosatha, chimene Mwana wa Munthu adzakupatsani. Mulungu Atate anamusindikiza chizindikiro chomuvomereza.” (aiōnios )
ក្ឞយណីយភក្ឞ្យាត៌្ហំ មា ឝ្រាមិឞ្ដ កិន្ត្វន្តាយុព៌្ហក្ឞ្យាត៌្ហំ ឝ្រាម្យត, តស្មាត៑ តាទ្ឫឝំ ភក្ឞ្យំ មនុជបុត្រោ យុឞ្មាភ្យំ ទាស្យតិ; តស្មិន៑ តាត ឦឝ្វរះ ប្រមាណំ ប្រាទាត៑។ (aiōnios )
Pakuti chifuniro cha Atate anga ndi chakuti aliyense amene aona Mwanayo namukhulupirira akhale ndi moyo wosatha, ndipo Ine ndidzamuukitsa kwa akufa pa tsiku lomaliza.” (aiōnios )
យះ កឝ្ចិន៑ មានវសុតំ វិលោក្យ វិឝ្វសិតិ ស ឝេឞទិនេ មយោត្ថាបិតះ សន៑ អនន្តាយុះ ប្រាប្ស្យតិ ឥតិ មត្ប្រេរកស្យាភិមតំ។ (aiōnios )
Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti Iye amene akhulupirira ali nawo moyo wosatha. (aiōnios )
អហំ យុឞ្មាន៑ យថាត៌្ហតរំ វទាមិ យោ ជនោ មយិ វិឝ្វាសំ ករោតិ សោនន្តាយុះ ប្រាប្នោតិ។ (aiōnios )
Ine ndine chakudya chamoyo chochokera kumwamba. Ngati munthu adya chakudya ichi, adzakhala ndi moyo nthawi zonse. Chakudya chimenechi ndi thupi langa, limene Ine ndidzalipereka kuti anthu pa dziko lapansi akhale ndi moyo.” (aiōn )
យជ្ជីវនភក្ឞ្យំ ស្វគ៌ាទាគច្ឆត៑ សោហមេវ ឥទំ ភក្ឞ្យំ យោ ជនោ ភុង្ក្ត្តេ ស និត្យជីវី ភវិឞ្យតិ។ បុនឝ្ច ជគតោ ជីវនាត៌្ហមហំ យត៑ ស្វកីយបិឝិតំ ទាស្យាមិ តទេវ មយា វិតរិតំ ភក្ឞ្យម៑។ (aiōn )
Aliyense amene adya thupi langa ndi kumwa magazi anga ali ndi moyo wosatha ndipo Ine ndidzamuukitsa kwa akufa pa tsiku lomaliza. (aiōnios )
យោ មមាមិឞំ ស្វាទតិ មម សុធិរញ្ច បិវតិ សោនន្តាយុះ ប្រាប្នោតិ តតះ ឝេឞេៜហ្និ តមហម៑ ឧត្ថាបយិឞ្យាមិ។ (aiōnios )
Ichi ndiye chakudya chimene chinatsika kuchokera kumwamba. Makolo athu akale anadya mana ndi kufa, koma iye amene adya chakudya ichi, adzakhala ndi moyo nthawi yonse.” (aiōn )
យទ្ភក្ឞ្យំ ស្វគ៌ាទាគច្ឆត៑ តទិទំ យន្មាន្នាំ ស្វាទិត្វា យុឞ្មាកំ បិតរោៜម្រិយន្ត តាទ្ឫឝម៑ ឥទំ ភក្ឞ្យំ ន ភវតិ ឥទំ ភក្ឞ្យំ យោ ភក្ឞតិ ស និត្យំ ជីវិឞ្យតិ។ (aiōn )
Simoni Petro anamuyankha Iye kuti, “Ambuye, ife tidzapita kwa yani? Inu muli ndi mawu amoyo wosatha. (aiōnios )
តតះ ឝិមោន៑ បិតរះ ប្រត្យវោចត៑ ហេ ប្រភោ កស្យាភ្យណ៌ំ គមិឞ្យាមះ? (aiōnios )
Pajatu kapolo alibe malo wokhazikika mʼbanja, koma mwana ndi wa mʼbanjamo nthawi zonse. (aiōn )
ទាសឝ្ច និរន្តរំ និវេឝនេ ន តិឞ្ឋតិ កិន្តុ បុត្រោ និរន្តរំ តិឞ្ឋតិ។ (aiōn )
Ine ndikukuwuzani choonadi, munthu akasunga mawu anga, sadzafa konse.” (aiōn )
អហំ យុឞ្មភ្យម៑ អតីវ យថាត៌្ហំ កថយាមិ យោ នរោ មទីយំ វាចំ មន្យតេ ស កទាចន និធនំ ន ទ្រក្ឞ្យតិ។ (aiōn )
Pamenepo Ayuda anafuwula kuti, “Tsopano ife tadziwadi kuti Inu ndi wogwidwa ndi chiwanda! Abrahamu anafa ndiponso aneneri, koma Inu mukunena kuti, ‘Ngati munthu asunga mawu anga, sadzafa.’ (aiōn )
យិហូទីយាស្តមវទន៑ ត្វំ ភូតគ្រស្ត ឥតីទានីម៑ អវៃឞ្ម។ ឥព្រាហីម៑ ភវិឞ្យទ្វាទិនញ្ច សវ៌្វេ ម្ឫតាះ កិន្តុ ត្វំ ភាឞសេ យោ នរោ មម ភារតីំ គ្ឫហ្លាតិ ស ជាតុ និធានាស្វាទំ ន លប្ស្យតេ។ (aiōn )
Palibe amene anamvapo za kutsekula maso a munthu wobadwa wosaona. (aiōn )
កោបិ មនុឞ្យោ ជន្មាន្ធាយ ចក្ឞុឞី អទទាត៑ ជគទារម្ភាទ៑ ឯតាទ្ឫឝីំ កថាំ កោបិ កទាបិ នាឝ្ឫណោត៑។ (aiōn )
Ine ndimazipatsa moyo wosatha ndipo sizidzawonongeka. Palibe amene adzazikwatula mʼdzanja langa. (aiōn , aiōnios )
អហំ តេភ្យោៜនន្តាយុ រ្ទទាមិ, តេ កទាបិ ន នំក្ឞ្យន្តិ កោបិ មម ករាត៑ តាន៑ ហត៌្តុំ ន ឝក្ឞ្យតិ។ (aiōn , aiōnios )
Aliyense amene ali ndi moyo ndi kukhulupirira Ine sadzamwalira. Kodi iwe ukukhulupirira izi?” (aiōn )
យះ កឝ្ចន ច ជីវន៑ មយិ វិឝ្វសិតិ ស កទាបិ ន មរិឞ្យតិ, អស្យាំ កថាយាំ កិំ វិឝ្វសិឞិ? (aiōn )
Munthu amene amakonda moyo wake adzawutaya, pamene munthu amene amadana ndi moyo wake mʼdziko lino lapansi adzawusungira ku moyo wosatha. (aiōnios )
យោ ជនេ និជប្រាណាន៑ ប្រិយាន៑ ជានាតិ ស តាន៑ ហារយិឞ្យតិ កិន្តុ យេ ជន ឥហលោកេ និជប្រាណាន៑ អប្រិយាន៑ ជានាតិ សេនន្តាយុះ ប្រាប្តុំ តាន៑ រក្ឞិឞ្យតិ។ (aiōnios )
Gulu la anthu linayankha kuti, “Ife tinamva kuchokera mʼmalamulo kuti Khristu adzakhala kwamuyaya, nanga bwanji Inu mukunena kuti, ‘Mwana wa Munthu ayenera kukwezedwa?’ Kodi Mwana wa Munthuyu ndani?” (aiōn )
តទា លោកា អកថយន៑ សោភិឞិក្តះ សវ៌្វទា តិឞ្ឋតីតិ វ្យវស្ថាគ្រន្ថេ ឝ្រុតម៑ អស្មាភិះ, តហ៌ិ មនុឞ្យបុត្រះ ប្រោត្ថាបិតោ ភវិឞ្យតីតិ វាក្យំ កថំ វទសិ? មនុឞ្យបុត្រោយំ កះ? (aiōn )
Ine ndikudziwa kuti lamulo lake ndi moyo wosatha. Choncho chilichonse chimene Ine ndinena ndi chimene Atate andiwuza.” (aiōnios )
តស្យ សាជ្ញា អនន្តាយុរិត្យហំ ជានាមិ, អតឯវាហំ យត៑ កថយាមិ តត៑ បិតា យថាជ្ញាបយត៑ តថៃវ កថយាម្យហម៑។ (aiōnios )
Petro anati, “Ayi, Inu simudzandisambitsa konse mapazi anga.” Yesu anayankha kuti, “Ngati Ine sindisambitsa mapazi ako, ulibe gawo mwa Ine.” (aiōn )
តតះ បិតរះ កថិតវាន៑ ភវាន៑ កទាបិ មម បាទៅ ន ប្រក្ឞាលយិឞ្យតិ។ យីឝុរកថយទ៑ យទិ ត្វាំ ន ប្រក្ឞាលយេ តហ៌ិ មយិ តវ កោប្យំឝោ នាស្តិ។ (aiōn )
Ine ndidzapempha Atate, ndipo adzakupatsani Nkhoswe ina kuti izikhala nanu nthawi zonse. (aiōn )
តតោ មយា បិតុះ សមីបេ ប្រាត៌្ហិតេ បិតា និរន្តរំ យុឞ្មាភិះ សាទ៌្ធំ ស្ថាតុម៑ ឥតរមេកំ សហាយម៑ អត៌្ហាត៑ សត្យមយម៑ អាត្មានំ យុឞ្មាកំ និកដំ ប្រេឞយិឞ្យតិ។ (aiōn )
Pakuti Inu munamupatsa Iye ulamuliro pa anthu onse kuti apereke moyo wosatha kwa onse amene mwamupatsa. (aiōnios )
ត្វំ យោល្លោកាន៑ តស្យ ហស្តេ សមប៌ិតវាន៑ ស យថា តេភ្យោៜនន្តាយុ រ្ទទាតិ តទត៌្ហំ ត្វំ ប្រាណិមាត្រាណាម៑ អធិបតិត្វភារំ តស្មៃ ទត្តវាន៑។ (aiōnios )
Tsono moyo wosathawo ndi uwu: Iwo akudziweni Inu, Mulungu yekhayo woona, ndi Yesu Khristu, amene Inu mwamutuma. (aiōnios )
យស្ត្វម៑ អទ្វិតីយះ សត្យ ឦឝ្វរស្ត្វយា ប្រេរិតឝ្ច យីឝុះ ខ្រីឞ្ដ ឯតយោរុភយោះ បរិចយេ ប្រាប្តេៜនន្តាយុ រ្ភវតិ។ (aiōnios )
Chifukwa simudzasiya moyo wanga kumalo a anthu akufa, ku manda, kapena kulekerera Woyerayo kuti awole. (Hadēs )
បរលោកេ យតោ ហេតោស្ត្វំ មាំ នៃវ ហិ ត្យក្ឞ្យសិ។ ស្វកីយំ បុណ្យវន្តំ ត្វំ ក្ឞយិតុំ នៃវ ទាស្យសិ។ ឯវំ ជីវនមាគ៌ំ ត្វំ មាមេវ ទឝ៌យិឞ្យសិ។ (Hadēs )
Davide ataoneratu zimene zinali mʼtsogolo anayankhula za kuuka kwa Khristu, kuti Iye sanasiyidwe mʼmanda, ndipo thupi lake silinawole. (Hadēs )
ឥតិ ជ្ញាត្វា ទាយូទ៑ ភវិឞ្យទ្វាទី សន៑ ភវិឞ្យត្កាលីយជ្ញានេន ខ្រីឞ្ដោត្ថានេ កថាមិមាំ កថយាមាស យថា តស្យាត្មា បរលោកេ ន ត្យក្ឞ្យតេ តស្យ ឝរីរញ្ច ន ក្ឞេឞ្យតិ; (Hadēs )
Iye ayenera kukhalabe kumwamba mpaka nthawi ya kukonzanso zinthu zonse monga Mulungu analonjeza kale kudzera mwa aneneri ake oyera mtima. (aiōn )
កិន្តុ ជគតះ ស្ឫឞ្ដិមារភ្យ ឦឝ្វរោ និជបវិត្រភវិឞ្យទ្វាទិគណោន យថា កថិតវាន៑ តទនុសារេណ សវ៌្វេឞាំ កាយ៌្យាណាំ សិទ្ធិបយ៌្យន្តំ តេន ស្វគ៌េ វាសះ កត៌្តវ្យះ។ (aiōn )
Ndipo Paulo ndi Barnaba anawayankha molimba mtima kuti, “Ife tinayenera kuyankhula Mawu a Mulungu kwa inu poyamba. Popeza inu mwawakana ndi kudziyesa nokha osayenera moyo wosatha, ife tsopano tikupita kwa anthu a mitundu ina. (aiōnios )
តតះ បៅលពណ៌ព្ពាវក្ឞោភៅ កថិតវន្តៅ ប្រថមំ យុឞ្មាកំ សន្និធាវីឝ្វរីយកថាយាះ ប្រចារណម៑ ឧចិតមាសីត៑ កិន្តុំ តទគ្រាហ្យត្វករណេន យូយំ ស្វាន៑ អនន្តាយុឞោៜយោគ្យាន៑ ទឝ៌យថ, ឯតត្ការណាទ៑ វយម៑ អន្យទេឝីយលោកានាំ សមីបំ គច្ឆាមះ។ (aiōnios )
Anthu a mitundu ina atamva izi, anakondwa ndipo analemekeza Mawu Ambuye; ndipo onse amene anawasankha kuti alandire moyo osatha anakhulupirira. (aiōnios )
តទា កថាមីទ្ឫឝីំ ឝ្រុត្វា ភិន្នទេឝីយា អាហ្លាទិតាះ សន្តះ ប្រភោះ កថាំ ធន្យាំ ធន្យាម៑ អវទន៑, យាវន្តោ លោកាឝ្ច បរមាយុះ ប្រាប្តិនិមិត្តំ និរូបិតា អាសន៑ តេ វ្យឝ្វសន៑។ (aiōnios )
zinaululidwa kuyambira kalekale.’ (aiōn )
អា ប្រថមាទ៑ ឦឝ្វរះ ស្វីយានិ សវ៌្វកម៌្មាណិ ជានាតិ។ (aiōn )
Pakuti kuyambira pamene dziko lapansi linalengedwa, zinthu zosaoneka za Mulungu, mphamvu zake zosatha ndi chikhalidwe cha umulungu, zakhala zikuoneka bwinobwino. Akhala akuzindikira poona zimene Mulungu analenga, kotero kuti anthu sangathe kuwiringula. (aïdios )
ផលតស្តស្យានន្តឝក្តីឝ្វរត្វាទីន្យទ្ឫឝ្យាន្យបិ ស្ឫឞ្ដិកាលម៑ អារភ្យ កម៌្មសុ ប្រកាឝមានានិ ទ្ឫឝ្យន្តេ តស្មាត៑ តេឞាំ ទោឞប្រក្ឞាលនស្យ បន្ថា នាស្តិ។ (aïdios )
Romans 1:24 (រោមិណះ 1:24)
(parallel missing)
ឥត្ថំ ត ឦឝ្វរស្យ សត្យតាំ វិហាយ ម្ឫឞាមតម៑ អាឝ្រិតវន្តះ សច្ចិទានន្ទំ ស្ឫឞ្ដិកត៌្តារំ ត្យក្ត្វា ស្ឫឞ្ដវស្តុនះ បូជាំ សេវាញ្ច ក្ឫតវន្តះ; (aiōn )
Iwo anasinthanitsa choonadi cha Mulungu ndi bodza ndipo anapembedza ndi kutumikira zinthu zolengedwa mʼmalo mwa Mlengi amene ali woyenera kutamandidwa mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
(parallel missing)
Iye adzapereka moyo wosatha kwa amene amafunafuna ulemerero, ulemu ndi moyo pochita ntchito zabwino mopirira. (aiōnios )
វស្តុតស្តុ យេ ជនា ធៃយ៌្យំ ធ្ឫត្វា សត្កម៌្ម កុវ៌្វន្តោ មហិមា សត្ការោៜមរត្វញ្ចៃតានិ ម្ឫគយន្តេ តេភ្យោៜនន្តាយុ រ្ទាស្យតិ។ (aiōnios )
Choncho monga momwe tchimo linkalamulira anthu ndi kubweretsa imfa pa iwo, chomwecho kunali koyenera kuti chisomo chilamulire pobweretsa chilungamo kwa anthu, ndi kuwafikitsa ku moyo wosatha mwa Yesu Khristu Ambuye athu. (aiōnios )
តេន ម្ឫត្យុនា យទ្វត៑ បាបស្យ រាជត្វម៑ អភវត៑ តទ្វទ៑ អស្មាកំ ប្រភុយីឝុខ្រីឞ្ដទ្វារានន្តជីវនទាយិបុណ្យេនានុគ្រហស្យ រាជត្វំ ភវតិ។ (aiōnios )
Koma tsopano pakuti inu mwamasulidwa ku tchimo ndipo mwasanduka akapolo a Mulungu, phindu lomwe mulipeza ndi kuyera mtima ndipo chotsatira chake ndi moyo wosatha. (aiōnios )
កិន្តុ សាម្ប្រតំ យូយំ បាបសេវាតោ មុក្តាះ សន្ត ឦឝ្វរស្យ ភ្ឫត្យាៜភវត តស្មាទ៑ យុឞ្មាកំ បវិត្រត្វរូបំ លភ្យម៑ អនន្តជីវនរូបញ្ច ផលម៑ អាស្តេ។ (aiōnios )
Pakuti malipiro a tchimo ndi imfa, koma mphatso yaulere imene Mulungu amapereka ndi moyo wosatha mwa Khristu Yesu Ambuye athu. (aiōnios )
យតះ បាបស្យ វេតនំ មរណំ កិន្ត្វស្មាកំ ប្រភុណា យីឝុខ្រីឞ្ដេនានន្តជីវនម៑ ឦឝ្វរទត្តំ បារិតោឞិកម៑ អាស្តេ។ (aiōnios )
Awo ndi makolo athu. Kuchokera kwa iwo mʼthupi ndi kumene kunachokera makolo a Khristu Yesu amene ndi Mulungu wolamulira zinthu zonse, alemekezeke mpaka muyaya! Ameni. (aiōn )
តត៑ កេវលំ នហិ កិន្តុ សវ៌្វាធ្យក្ឞះ សវ៌្វទា សច្ចិទានន្ទ ឦឝ្វរោ យះ ខ្រីឞ្ដះ សោៜបិ ឝារីរិកសម្ពន្ធេន តេឞាំ វំឝសម្ភវះ។ (aiōn )
“kapena ‘Ndani adzatsikira ku dziko la anthu akufa?’” (ndiko, kukamutenga Khristu kwa akufa). (Abyssos )
កោ វា ប្រេតលោកម៑ អវរុហ្យ ខ្រីឞ្ដំ ម្ឫតគណមធ្យាទ៑ អានេឞ្យតីតិ វាក៑ មនសិ ត្វយា ន គទិតវ្យា។ (Abyssos )
Pakuti Mulungu anasandutsa anthu onse a mʼndende ya kusamvera kuti Iye akaonetse chifundo kwa onse. (eleēsē )
ឦឝ្វរះ សវ៌្វាន៑ ប្រតិ ក្ឫបាំ ប្រកាឝយិតុំ សវ៌្វាន៑ អវិឝ្វាសិត្វេន គណយតិ។ (eleēsē )
Pakuti zinthu zonse nʼzochokera kwa Iye, nʼzolengedwa ndi Iye ndipo zimabweretsa ulemerero kwa Iye. Kwa Iye kukhale ulemerero mpaka muyaya! Ameni. (aiōn )
យតោ វស្តុមាត្រមេវ តស្មាត៑ តេន តស្មៃ ចាភវត៑ តទីយោ មហិមា សវ៌្វទា ប្រកាឝិតោ ភវតុ។ ឥតិ។ (aiōn )
Musafanizidwenso ndi makhalidwe a dziko lino koma musandulike pokonzanso maganizo anu. Ndipo mudzadziwa ndi kuzindikira chifuniro chabwino cha Mulungu chomwe ndi chokondweretsa ndi changwiro. (aiōn )
អបរំ យូយំ សាំសារិកា ឥវ មាចរត, កិន្តុ ស្វំ ស្វំ ស្វភាវំ បរាវត៌្យ នូតនាចារិណោ ភវត, តត ឦឝ្វរស្យ និទេឝះ កីទ្ឫគ៑ ឧត្តមោ គ្រហណីយះ សម្បូណ៌ឝ្ចេតិ យុឞ្មាភិរនុភាវិឞ្យតេ។ (aiōn )
Tsopano kwa Iye amene ali ndi mphamvu yokhazikitsa monga mwa uthenga wanga wabwino ndikulalikidwa kwa Yesu Khristu, monga mwa vumbulutso lachinsinsi chobisika kwa nthawi yayitali, (aiōnios )
បូវ៌្វកាលិកយុគេឞុ ប្រច្ឆន្នា យា មន្ត្រណាធុនា ប្រកាឝិតា ភូត្វា ភវិឞ្យទ្វាទិលិខិតគ្រន្ថគណស្យ ប្រមាណាទ៑ វិឝ្វាសេន គ្រហណាត៌្ហំ សទាតនស្យេឝ្វរស្យាជ្ញយា សវ៌្វទេឝីយលោកាន៑ ជ្ញាប្យតេ, (aiōnios )
koma tsopano chavumbulutsidwa ndi kudziwika kudzera mʼMalemba a uneneri mwa lamulo la Mulungu wosatha, kuti mitundu yonse ikhulupirire ndi kumvera Iye, (aiōnios )
តស្យា មន្ត្រណាយា ជ្ញានំ លព្ធ្វា មយា យះ សុសំវាទោ យីឝុខ្រីឞ្ដមធិ ប្រចាយ៌្យតេ, តទនុសារាទ៑ យុឞ្មាន៑ ធម៌្មេ សុស្ថិរាន៑ កត៌្តុំ សមត៌្ហោ យោៜទ្វិតីយះ (aiōnios )
kwa Mulungu yekhayo wanzeru kukhale ulemerero kwamuyaya kudzera mwa Yesu Khristu! Ameni. (aiōn )
សវ៌្វជ្ញ ឦឝ្វរស្តស្យ ធន្យវាទោ យីឝុខ្រីឞ្ដេន សន្តតំ ភូយាត៑។ ឥតិ។ (aiōn )
Munthu wanzeru ali kuti? Munthu wozama ndi maphunziro ali kuti? Munthu wodziwa zakuya zamakono ali kuti? Kodi Mulungu sanazipusitse nzeru za dziko lapansi? (aiōn )
ជ្ញានី កុត្រ? ឝាស្ត្រី វា កុត្រ? ឥហលោកស្យ វិចារតត្បរោ វា កុត្រ? ឥហលោកស្យ ជ្ញានំ កិមីឝ្វរេណ មោហីក្ឫតំ នហិ? (aiōn )
Komabe ife timayankhula uthenga wa nzeru kwa okhwima, koma osati ndi nzeru ya mʼbado uno kapena ya olamula a mʼbado uno, amene mphamvu yawo ikutha. (aiōn )
វយំ ជ្ញានំ ភាឞាមហេ តច្ច សិទ្ធលោកៃ រ្ជ្ញានមិវ មន្យតេ, តទិហលោកស្យ ជ្ញានំ នហិ, ឥហលោកស្យ នឝ្វរាណាម៑ អធិបតីនាំ វា ជ្ញានំ នហិ; (aiōn )
Ayi, ife timayankhula za nzeru yobisika ya Mulungu, nzeru imene inabisidwa ndipo imene Mulungu anatikonzera mu ulemerero wathu isanayambe nthawi. (aiōn )
កិន្តុ កាលាវស្ថាយាះ បូវ៌្វស្មាទ៑ យត៑ ជ្ញានម៑ អស្មាកំ វិភវាត៌្ហម៑ ឦឝ្វរេណ និឝ្ចិត្យ ប្រច្ឆន្នំ តន្និគូឍម៑ ឦឝ្វរីយជ្ញានំ ប្រភាឞាមហេ។ (aiōn )
Palibe olamulira aliyense wa mʼbado uno amene anamumvetsetsa popeza anakamumvetsetsa sakanamupachika Ambuye wa ulemerero. (aiōn )
ឥហលោកស្យាធិបតីនាំ កេនាបិ តត៑ ជ្ញានំ ន លព្ធំ, លព្ធេ សតិ តេ ប្រភាវវិឝិឞ្ដំ ប្រភុំ ក្រុឝេ នាហនិឞ្យន៑។ (aiōn )
Choncho musadzinyenge. Ngati wina wa inu akuganiza kuti ndi wanzeru pa mulingo wa mʼbado uno, ayenera kukhala “wopusa” kuti athe kukhala wanzeru. (aiōn )
កោបិ ស្វំ ន វញ្ចយតាំ។ យុឞ្មាកំ កឝ្ចន ចេទិហលោកស្យ ជ្ញានេន ជ្ញានវានហមិតិ ពុធ្យតេ តហ៌ិ ស យត៑ ជ្ញានី ភវេត៑ តទត៌្ហំ មូឍោ ភវតុ។ (aiōn )
Nʼchifukwa chake ngati zimene ine ndimadya zichititsa mʼbale wanga kugwa mu tchimo, sindidzadyanso chakudyacho kuti mʼbaleyo ndisamuchimwitse. (aiōn )
អតោ ហេតោះ បិឝិតាឝនំ យទិ មម ភ្រាតុ រ្វិឃ្នស្វរូបំ ភវេត៑ តហ៌្យហំ យត៑ ស្វភ្រាតុ រ្វិឃ្នជនកោ ន ភវេយំ តទត៌្ហំ យាវជ្ជីវនំ បិឝិតំ ន ភោក្ឞ្យេ។ (aiōn )
Zinthu izi zinawachitikira kuti zikhale chitsanzo ndipo zinalembedwa kuti zikhale chenjezo kwa ife, amene tiyandikira nthawi ya kutha kwa zonse. (aiōn )
តាន៑ ប្រតិ យាន្យេតានិ ជឃដិរេ តាន្យស្មាកំ និទឝ៌នានិ ជគតះ ឝេឞយុគេ វត៌្តមានានាម៑ អស្មាកំ ឝិក្ឞាត៌្ហំ លិខិតានិ ច ពភូវុះ។ (aiōn )
“Iwe imfa, kupambana kwako kuli kuti? Iwe imfa, ululu wako uli kuti?” (Hadēs )
ម្ឫត្យោ តេ កណ្ដកំ កុត្រ បរលោក ជយះ ក្ក តេ៕ (Hadēs )
Mulungu wa dziko lapansi anachititsa khungu anthu osakhulupirira, kuti asathe kuona kuwala kwa Uthenga Wabwino umene umaonetsa ulemerero wa Khristu, amene ndi chifaniziro cha Mulungu. (aiōn )
យត ឦឝ្វរស្យ ប្រតិមូត៌្តិ រ្យះ ខ្រីឞ្ដស្តស្យ តេជសះ សុសំវាទស្យ ប្រភា យត៑ តាន៑ ន ទីបយេត៑ តទត៌្ហម៑ ឥហ លោកស្យ ទេវោៜវិឝ្វាសិនាំ ជ្ញាននយនម៑ អន្ធីក្ឫតវាន៑ ឯតស្យោទាហរណំ តេ ភវន្តិ។ (aiōn )
Pakuti masautso athu ndi opepuka ndi a kanthawi, koma akutitengera ulemerero wamuyaya umene ndi wopambana kwambiri. (aiōnios )
ក្ឞណមាត្រស្ថាយិ យទេតត៑ លឃិឞ្ឋំ ទុះខំ តទ៑ អតិពាហុល្យេនាស្មាកម៑ អនន្តកាលស្ថាយិ គរិឞ្ឋសុខំ សាធយតិ, (aiōnios )
Motero sitiyangʼana zinthu zimene ndi zooneka ndi maso, koma zinthu zimene ndi zosaoneka. Pakuti zimene zimaoneka ndi zosakhalitsa, koma zimene sizioneka ndi zamuyaya. (aiōnios )
យតោ វយំ ប្រត្យក្ឞាន៑ វិឞយាន៑ អនុទ្ទិឝ្យាប្រត្យក្ឞាន៑ ឧទ្ទិឝាមះ។ យតោ ហេតោះ ប្រត្យក្ឞវិឞយាះ ក្ឞណមាត្រស្ថាយិនះ កិន្ត្វប្រត្យក្ឞា អនន្តកាលស្ថាយិនះ។ (aiōnios )
Popeza tikudziwa kuti ngati msasa wa dziko lapansi umene tikukhalamo uwonongeka, tili ndi nyumba yochokera kwa Mulungu, nyumba yamuyaya yakumwamba, osati yomangidwa ndi manja a anthu. (aiōnios )
អបរម៑ អស្មាកម៑ ឯតស្មិន៑ បាត៌្ហិវេ ទូឞ្យរូបេ វេឝ្មនិ ជីណ៌េ សតីឝ្វរេណ និម៌្មិតម៑ អករក្ឫតម៑ អស្មាកម៑ អនន្តកាលស្ថាយិ វេឝ្មៃកំ ស្វគ៌េ វិទ្យត ឥតិ វយំ ជានីមះ។ (aiōnios )
Paja analemba kuti, “Wopereka mphatso zake mowolowamanja kwa osauka, chilungamo chake chimanka mpaka muyaya.” (aiōn )
ឯតស្មិន៑ លិខិតមាស្តេ, យថា, វ្យយតេ ស ជនោ រាយំ ទុគ៌តេភ្យោ ទទាតិ ច។ និត្យស្ថាយី ច តទ្ធម៌្មះ (aiōn )
Mulungu, Atate a Ambuye Yesu, amene tiyenera kumutamanda nthawi zonse, akudziwa kuti sindikunama. (aiōn )
មយា ម្ឫឞាវាក្យំ ន កថ្យត ឥតិ និត្យំ ប្រឝំសនីយោៜស្មាកំ ប្រភោ រ្យីឝុខ្រីឞ្ដស្យ តាត ឦឝ្វរោ ជានាតិ។ (aiōn )
Yesuyo anadzipereka yekha chifukwa cha machimo athu kuti atipulumutse ku njira za moyo woyipa uno, molingana ndi chifuniro cha Mulungu ndi Atate athu. (aiōn )
អស្មាកំ តាតេឝ្វរេស្យេច្ឆានុសារេណ វត៌្តមានាត៑ កុត្សិតសំសារាទ៑ អស្មាន៑ និស្តារយិតុំ យោ (aiōn )
Ulemerero ukhale kwa Mulunguyo mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
យីឝុរស្មាកំ បាបហេតោរាត្មោត្សគ៌ំ ក្ឫតវាន៑ ស សវ៌្វទា ធន្យោ ភូយាត៑។ តថាស្តុ។ (aiōn )
Pakuti amene amafesa zokondweretsa thupi lake la uchimo, kuchokera ku khalidwe limenelo adzakolola chiwonongeko; amene amafesa zokondweretsa Mzimu, kuchokera kwa Mzimu adzakolola moyo wosatha. (aiōnios )
ស្វឝរីរាត៌្ហំ យេន ពីជម៑ ឧប្យតេ តេន ឝរីរាទ៑ វិនាឝរូបំ ឝស្យំ លប្ស្យតេ កិន្ត្វាត្មនះ ក្ឫតេ យេន ពីជម៑ ឧប្យតេ តេនាត្មតោៜនន្តជីវិតរូបំ ឝស្យំ លប្ស្យតេ។ (aiōnios )
Anamukhazika pamwamba pa ulamuliro onse ndi mafumu, mphamvu ndi ufumu, ndiponso pamwamba pa dzina lililonse limene angalitchule, osati nthawi ino yokha komanso imene ikubwerayo. (aiōn )
អធិបតិត្វបទំ ឝាសនបទំ បរាក្រមោ រាជត្វញ្ចេតិនាមានិ យាវន្តិ បទានីហ លោកេ បរលោកេ ច វិទ្យន្តេ តេឞាំ សវ៌្វេឞាម៑ ឩទ៌្ធ្វេ ស្វគ៌េ និជទក្ឞិណបាឝ៌្វេ តម៑ ឧបវេឝិតវាន៑, (aiōn )
Ephesians 2:1 (ឥផិឞិណះ 2:1)
(parallel missing)
បុរា យូយម៑ អបរាធៃះ បាបៃឝ្ច ម្ឫតាះ សន្តស្តាន្យាចរន្ត ឥហលោកស្យ សំសារានុសារេណាកាឝរាជ្យស្យាធិបតិម្ (aiōn )
mmene inu munkakhalamo pamene munkatsatira njira za dziko lapansi ndi za ulamuliro waufumu wa mlengalenga, mzimu umene ukugwira ntchito tsopano mwa amene samvera. (aiōn )
(parallel missing)
ndi cholinga chakuti mʼnthawi imene ikubwera, Iyeyo adzaonetse chuma choposa cha chisomo chake, choonetsedwa mwa kukoma mtima kwake kwa ife mwa Khristu Yesu. (aiōn )
ឥត្ថំ ស ខ្រីឞ្ដេន យីឝុនាស្មាន៑ ប្រតិ ស្វហិតៃឞិតយា ភាវិយុគេឞុ ស្វកីយានុគ្រហស្យានុបមំ និធិំ ប្រកាឝយិតុម៑ ឥច្ឆតិ។ (aiōn )
Ndinasankhidwa kuti ndifotokoze momveka bwino kwa munthu aliyense za chinsinsi chimenechi, chinsinsi chimene kuyambira kale chinali chobisika mwa Mulungu amene analenga zinthu zonse. (aiōn )
កាលាវស្ថាតះ បូវ៌្វស្មាច្ច យោ និគូឍភាវ ឦឝ្វរេ គុប្ត អាសីត៑ តទីយនិយមំ សវ៌្វាន៑ ជ្ញាបយាមិ។ (aiōn )
Chimenechi chinali chikonzero chamuyaya cha Mulungu, chimene chinachitika kudzera mwa Khristu Yesu Ambuye athu. (aiōn )
(parallel missing)
Ephesians 3:12 (ឥផិឞិណះ 3:12)
(parallel missing)
ប្រាប្តវន្តស្តមស្មាកំ ប្រភុំ យីឝុំ ខ្រីឞ្ដមធិ ស កាលាវស្ថាយាះ បូវ៌្វំ តំ មនោរថំ ក្ឫតវាន៑។ (aiōn )
Iyeyo akhale ndi ulemu mu mpingo ndi mwa Khristu Yesu pa mibado yonse mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
ខ្រីឞ្ដយីឝុនា សមិតេ រ្មធ្យេ សវ៌្វេឞុ យុគេឞុ តស្យ ធន្យវាទោ ភវតុ។ ឥតិ។ (aiōn )
Pakuti sitikulimbana ndi thupi ndi magazi, koma tikulimbana ndi maufumu, maulamuliro, mphamvu za dziko la mdima, ndi mphamvu zoyipa kwambiri zauzimu zamlengalenga. (aiōn )
យតះ កេវលំ រក្តមាំសាភ្យាម៑ ឥតិ នហិ កិន្តុ កត៌្ឫត្វបរាក្រមយុក្តៃស្តិមិររាជ្យស្យេហលោកស្យាធិបតិភិះ ស្វគ៌ោទ្ភវៃ រ្ទុឞ្ដាត្មភិរេវ សាទ៌្ធម៑ អស្មាភិ រ្យុទ្ធំ ក្រិយតេ។ (aiōn )
Kwa Mulungu ndi Atate athu, kukhale ulemerero mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
អស្មាកំ បិតុរីឝ្វរស្យ ធន្យវាទោៜនន្តកាលំ យាវទ៑ ភវតុ។ អាមេន៑។ (aiōn )
chinsinsi chimene chakhala chikubisika kwa nthawi ndi mibado, koma tsopano chawululidwa kwa oyera mtima. (aiōn )
តត៑ និគូឍំ វាក្យំ បូវ៌្វយុគេឞុ បូវ៌្វបុរុឞេភ្យះ ប្រច្ឆន្នម៑ អាសីត៑ កិន្ត្វិទានីំ តស្យ បវិត្រលោកានាំ សន្និធៅ តេន ប្រាកាឝ្យត។ (aiōn )
Adzalangidwa ndi chiwonongeko chamuyaya ndipo sadzaonanso nkhope ya Ambuye ndi ulemerero wamphamvu zake (aiōnios )
តេ ច ប្រភោ រ្វទនាត៑ បរាក្រមយុក្តវិភវាច្ច សទាតនវិនាឝរូបំ ទណ្ឌំ លប្ស្យន្តេ, (aiōnios )
Ambuye athu Yesu Khristu mwini ndi Mulungu Atate wathu, amene anatikonda ife ndipo mwachisomo chake anatipatsa kulimba mtima kwamuyaya ndi chiyembekezo chabwino, (aiōnios )
អស្មាកំ ប្រភុ រ្យីឝុខ្រីឞ្ដស្តាត ឦឝ្វរឝ្ចាត៌្ហតោ យោ យុឞ្មាសុ ប្រេម ក្ឫតវាន៑ និត្យាញ្ច សាន្ត្វនាម៑ អនុគ្រហេណោត្តមប្រត្យាឝាញ្ច យុឞ្មភ្យំ ទត្តវាន្ (aiōnios )
Ndipo pa chifukwa chimenechi, Mulungu anandichitira chifundo, kuti mwa ine, wochimwitsitsa, Khristu Yesu aonetse kuleza mtima kwake konse kuti ndikhale chitsanzo cha omwe angathe kumukhulupirira ndi kulandira moyo wosatha. (aiōnios )
តេឞាំ បាបិនាំ មធ្យេៜហំ ប្រថម អាសំ កិន្តុ យេ មានវា អនន្តជីវនប្រាប្ត្យត៌្ហំ តស្មិន៑ វិឝ្វសិឞ្យន្តិ តេឞាំ ទ្ឫឞ្ដាន្តេ មយិ ប្រថមេ យីឝុនា ខ្រីឞ្ដេន ស្វកីយា ក្ឫត្ស្នា ចិរសហិឞ្ណុតា យត៑ ប្រកាឝ្យតេ តទត៌្ហមេវាហម៑ អនុកម្បាំ ប្រាប្តវាន៑។ (aiōnios )
Tsopano kwa Mfumu yamuyaya, yosafa, yosaoneka, amene Iye yekha ndiye Mulungu, kukhale ulemu ndi ulemerero mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
អនាទិរក្ឞយោៜទ្ឫឝ្យោ រាជា យោៜទ្វិតីយះ សវ៌្វជ្ញ ឦឝ្វរស្តស្យ គៅរវំ មហិមា ចានន្តកាលំ យាវទ៑ ភូយាត៑។ អាមេន៑។ (aiōn )
Menya nkhondo yabwino yachikhulupiriro. Gwiritsitsa moyo wosatha umene anakuyitanira pamene unavomereza bwino lomwe pamaso pa mboni zambiri. (aiōnios )
វិឝ្វាសរូបម៑ ឧត្តមយុទ្ធំ កុរុ, អនន្តជីវនម៑ អាលម្ពស្វ យតស្តទត៌្ហំ ត្វម៑ អាហូតោ ៜភវះ, ពហុសាក្ឞិណាំ សមក្ឞញ្ចោត្តមាំ ប្រតិជ្ញាំ ស្វីក្ឫតវាន៑។ (aiōnios )
Ndiye yekha wosafa ndipo amakhala mʼkuwala koopsa. Mulungu amene munthu aliyense sanamuone. Kwa Iye kukhale ulemu ndi mphamvu mpaka muyaya. Ameni. (aiōnios )
អមរតាយា អទ្វិតីយ អាករះ, អគម្យតេជោនិវាសី, មត៌្ត្យានាំ កេនាបិ ន ទ្ឫឞ្ដះ កេនាបិ ន ទ្ឫឝ្យឝ្ច។ តស្យ គៅរវបរាក្រមៅ សទាតនៅ ភូយាស្តាំ។ អាមេន៑។ (aiōnios )
Anthu onse amene ali ndi chuma uwalamule kuti asanyade kapena kuyika mitima yawo pa chuma chimene nʼchosadalirika. Koma chiyembekezo chawo chikhale mwa Mulungu amene amatipatsa mowolowamanja zonse zotisangalatsa. (aiōn )
ឥហលោកេ យេ ធនិនស្តេ ចិត្តសមុន្នតិំ ចបលេ ធនេ វិឝ្វាសញ្ច ន កុវ៌្វតាំ កិន្តុ ភោគាត៌្ហម៑ អស្មភ្យំ ប្រចុរត្វេន សវ៌្វទាតា (aiōn )
Iye anatipulumutsa ndipo anatiyitanira ku moyo oyera mtima, osati chifukwa cha chilichonse chimene tinachita, koma chifukwa cha chikonzero ndi chisomo chake. Chisomo chimenechi anatipatsa ife mwa Khristu Yesu nthawi isanayambe. (aiōnios )
សោៜស្មាន៑ បរិត្រាណបាត្រាណិ ក្ឫតវាន៑ បវិត្រេណាហ្វានេនាហូតវាំឝ្ច; អស្មត្កម៌្មហេតុនេតិ នហិ ស្វីយនិរូបាណស្យ ប្រសាទស្យ ច ក្ឫតេ តត៑ ក្ឫតវាន៑។ ស ប្រសាទះ ស្ឫឞ្ដេះ បូវ៌្វកាលេ ខ្រីឞ្ដេន យីឝុនាស្មភ្យម៑ អទាយិ, (aiōnios )
Choncho ndikupirira chilichonse chifukwa cha osankhidwa, kuti nawonso apulumutsidwe ndi Khristu Yesu ndi kulandira ulemerero wosatha. (aiōnios )
ខ្រីឞ្ដេន យីឝុនា យទ៑ អនន្តគៅរវសហិតំ បរិត្រាណំ ជាយតេ តទភិរុចិតៃ រ្លោកៃរបិ យត៑ លភ្យេត តទត៌្ហមហំ តេឞាំ និមិត្តំ សវ៌្វាណ្យេតានិ សហេ។ (aiōnios )
Paja Dema anandisiya chifukwa chokonda dziko lapansi lino, ndipo anapita ku Tesalonika. Kresike anapita ku Galatiya ndipo Tito anapita ku Dalimatiya. (aiōn )
យតោ ទីមា ឰហិកសំសារម៑ ឦហមានោ មាំ បរិត្យជ្យ ថិឞលនីកីំ គតវាន៑ តថា ក្រីឞ្កិ រ្គាលាតិយាំ គតវាន៑ តីតឝ្ច ទាល្មាតិយាំ គតវាន៑។ (aiōn )
Ambuye adzandilanditsa ku chilichonse chofuna kundichita choyipa ndipo adzandisamalira bwino mpaka kundilowetsa chonse mu ufumu wake wakumwamba. Kwa Iye kukhale ulemerero mpaka muyaya. (aiōn )
អបរំ សវ៌្វស្មាទ៑ ទុឞ្កម៌្មតះ ប្រភុ រ្មាម៑ ឧទ្ធរិឞ្យតិ និជស្វគ៌ីយរាជ្យំ នេតុំ មាំ តារយិឞ្យតិ ច។ តស្យ ធន្យវាទះ សទាកាលំ ភូយាត៑។ អាមេន៑។ (aiōn )
Titus 1:1 (តីតះ 1:1)
(parallel missing)
អនន្តជីវនស្យាឝាតោ ជាតាយា ឦឝ្វរភក្តេ រ្យោគ្យស្យ សត្យមតស្យ យត៑ តត្វជ្ញានំ យឝ្ច វិឝ្វាស ឦឝ្វរស្យាភិរុចិតលោកៃ រ្លភ្យតេ តទត៌្ហំ (aiōnios )
ndi kuwapatsa chiyembekezo cha moyo wosatha, umene Mulungu amene sanama, analonjeza nthawi isanayambe. (aiōnios )
(parallel missing)
Chisomo chimatiphunzitsa kukana moyo osalemekeza Mulungu komanso zilakolako za dziko lapansi. Ndipo chimatiphunzitsa kukhala moyo odziletsa, olungama ndi opembedza Mulungu nthawi ino, (aiōn )
ស ចាស្មាន៑ ឥទំ ឝិក្ឞ្យតិ យទ៑ វយម៑ អធម៌្មំ សាំសារិកាភិលាឞាំឝ្ចានង្គីក្ឫត្យ វិនីតត្វេន ន្យាយេនេឝ្វរភក្ត្យា ចេហលោកេ អាយុ រ្យាបយាមះ, (aiōn )
kuti titalungamitsidwa mwachisomo chake, tikhale olowamʼmalo okhala ndi chiyembekezo cha moyo wosatha. (aiōnios )
ឥត្ថំ វយំ តស្យានុគ្រហេណ សបុណ្យីភូយ ប្រត្យាឝយានន្តជីវនស្យាធិការិណោ ជាតាះ។ (aiōnios )
Mwina chifukwa chimene unasiyana naye kwa kanthawi ndi chakuti ukhale nayenso nthawi zonse. (aiōnios )
កោ ជានាតិ ក្ឞណកាលាត៌្ហំ ត្វត្តស្តស្យ វិច្ឆេទោៜភវទ៑ ឯតស្យាយម៑ អភិប្រាយោ យត៑ ត្វម៑ អនន្តកាលាត៌្ហំ តំ លប្ស្យសេ (aiōnios )
Koma masiku otsiriza ano, Mulungu wayankhula nafe kudzera mwa Mwana wake. Mwanayu anamusankha kuti akhale mwini wa zinthu zonse, ndiponso Mulungu analenga dziko lonse kudzera mwa Iye. (aiōn )
ស ឯតស្មិន៑ ឝេឞកាលេ និជបុត្រេណាស្មភ្យំ កថិតវាន៑។ ស តំ បុត្រំ សវ៌្វាធិការិណំ ក្ឫតវាន៑ តេនៃវ ច សវ៌្វជគន្តិ ស្ឫឞ្ដវាន៑។ (aiōn )
Koma za Mwana wake akuti, “Inu Mulungu, mpando wanu waufumu udzakhala mpaka muyaya, ndipo mudzaweruza molungama mu ufumu wanu. (aiōn )
កិន្តុ បុត្រមុទ្ទិឝ្យ តេនោក្តំ, យថា, "ហេ ឦឝ្វរ សទា ស្ថាយិ តវ សិំហាសនំ ភវេត៑។ យាថាត៌្ហ្យស្យ ភវេទ្ទណ្ឌោ រាជទណ្ឌស្ត្វទីយកះ។ (aiōn )
Ndipo penanso anati, “Iwe ndiwe wansembe mpaka muyaya, monga mwa unsembe wa Melikizedeki.” (aiōn )
តទ្វទ៑ អន្យគីតេៜបីទមុក្តំ, ត្វំ មល្កីឞេទកះ ឝ្រេណ្យាំ យាជកោៜសិ សទាតនះ។ (aiōn )
Atasanduka wangwiro kotheratu, anakhala gwero la chipulumutso chosatha kwa onse omvera Iye. (aiōnios )
ឥត្ថំ សិទ្ធីភូយ និជាជ្ញាគ្រាហិណាំ សវ៌្វេឞាម៑ អនន្តបរិត្រាណស្យ ការណស្វរូបោ ៜភវត៑។ (aiōnios )
za maubatizo, za kusanjika manja, za kuuka kwa akufa ndi za chiweruzo chotsiriza. (aiōnios )
អនន្តកាលស្ថាយិវិចារាជ្ញា ចៃតៃះ បុនព៌្ហិត្តិមូលំ ន ស្ថាបយន្តះ ខ្រីឞ្ដវិឞយកំ ប្រថមោបទេឝំ បឝ្ចាត្ក្ឫត្យ សិទ្ធិំ យាវទ៑ អគ្រសរា ភវាម។ (aiōnios )
Analawa kukoma kwa mawu a Mulungu ndi mphamvu za nthawi ikubwera. (aiōn )
ឦឝ្វរស្យ សុវាក្យំ ភាវិកាលស្យ ឝក្តិញ្ចាស្វទិតវន្តឝ្ច តេ ភ្រឞ្ដ្វា យទិ (aiōn )
Yesu anatitsogolera kupita kumeneko, nalowako mʼmalo mwathu. Iye anasanduka Mkulu wa ansembe onse wamuyaya, monga mwa dongosolo la unsembe wa Melikizedeki. (aiōn )
តត្រៃវាស្មាកម៑ អគ្រសរោ យីឝុះ ប្រវិឝ្យ មល្កីឞេទកះ ឝ្រេណ្យាំ និត្យស្ថាយី យាជកោៜភវត៑។ (aiōn )
Pakuti Mulungu anamuchitira umboni kuti, “Iwe ndi wansembe wamuyaya, monga mwa dongosolo la unsembe wa Melikizedeki.” (aiōn )
យត ឦឝ្វរ ឥទំ សាក្ឞ្យំ ទត្តវាន៑, យថា, "ត្វំ មក្លីឞេទកះ ឝ្រេណ្យាំ យាជកោៜសិ សទាតនះ។ " (aiōn )
Koma Yesu ankakhala wansembe ndi lumbiro pamene Mulungu anati, “Ambuye analumbira ndipo sangasinthe maganizo ake, ‘Iwe ndi wansembe wamuyaya.’” (aiōn )
(parallel missing)
Hebrews 7:22 (ឥព្រិណះ 7:22)
(parallel missing)
"បរមេឝ ឥទំ ឝេបេ ន ច តស្មាន្និវត៌្ស្យតេ។ ត្វំ មល្កីឞេទកះ ឝ្រេណ្យាំ យាជកោៜសិ សទាតនះ។ " (aiōn )
Koma Yesu popeza ndi wamuyaya, unsembe wake ndi wosatha. (aiōn )
កិន្ត្វសាវនន្តកាលំ យាវត៑ តិឞ្ឋតិ តស្មាត៑ តស្យ យាជកត្វំ ន បរិវត៌្តនីយំ។ (aiōn )
Pakuti lamulo limasankha anthu amene ndi ofowoka kukhala akulu a ansembe; koma lumbiro, lomwe linabwera pambuyo pa lamulo, linasankha Mwana, amene anapangidwa kukhala wangwiro kwamuyaya. (aiōn )
យតោ វ្យវស្ថយា យេ មហាយាជកា និរូប្យន្តេ តេ ទៅព៌្ពល្យយុក្តា មានវាះ កិន្តុ វ្យវស្ថាតះ បរំ ឝបថយុក្តេន វាក្យេន យោ មហាយាជកោ និរូបិតះ សោ ៜនន្តកាលាត៌្ហំ សិទ្ធះ បុត្រ ឯវ។ (aiōn )
Iye sanalowemo ndi magazi ambuzi yayimuna, ana angʼombe amphongo, koma analowa Malo Opatulika kamodzi kokha ndi magazi ake, atatikonzera chipulumutso chosatha. (aiōnios )
ឆាគានាំ គោវត្សានាំ វា រុធិរម៑ អនាទាយ ស្វីយរុធិរម៑ អាទាយៃកក្ឫត្វ ឯវ មហាបវិត្រស្ថានំ ប្រវិឝ្យានន្តកាលិកាំ មុក្តិំ ប្រាប្តវាន៑។ (aiōnios )
nʼkoposa kotani magazi a Khristu, amene mwa Mzimu wamuyaya anadzipereka yekha kwa Mulungu kukhala nsembe yopanda chilema. Iye adzayeretsa chikumbumtima chathu pochotsa ntchito za imfa, kuti ife titumikire Mulungu wamoyo. (aiōnios )
តហ៌ិ កិំ មន្យធ្វេ យះ សទាតនេនាត្មនា និឞ្កលង្កពលិមិវ ស្វមេវេឝ្វរាយ ទត្តវាន៑, តស្យ ខ្រីឞ្ដស្យ រុធិរេណ យុឞ្មាកំ មនាំស្យមរេឝ្វរស្យ សេវាយៃ កិំ ម្ឫត្យុជនកេភ្យះ កម៌្មភ្យោ ន បវិត្រីការិឞ្យន្តេ? (aiōnios )
Pa chifukwa chimenechi Khristu ndi mʼkhalapakati wa pangano latsopano, kuti iwo amene anayitanidwa alandire chuma chamuyaya, pakuti Iye tsopano anafa ngati dipo lomasula iwo ku machimo amene anachita ali pansi pa pangano loyamba lija. (aiōnios )
ស នូតននិយមស្យ មធ្យស្ថោៜភវត៑ តស្យាភិប្រាយោៜយំ យត៑ ប្រថមនិយមលង្ឃនរូបបាបេភ្យោ ម្ឫត្យុនា មុក្តៅ ជាតាយាម៑ អាហូតលោកា អនន្តកាលីយសម្បទះ ប្រតិជ្ញាផលំ លភេរន៑។ (aiōnios )
Zikanatero bwenzi Khristu atamva zowawa kambirimbiri chilengedwere cha dziko lapansi. Koma tsopano anaoneka kamodzi kokha chifukwa cha onse pa nthawi yotsiriza kuti achotse tchimo podzipereka yekha nsembe. (aiōn )
កត៌្តវ្យេ សតិ ជគតះ ស្ឫឞ្ដិកាលមារភ្យ ពហុវារំ តស្យ ម្ឫត្យុភោគ អាវឝ្យកោៜភវត៑; កិន្ត្វិទានីំ ស អាត្មោត្សគ៌េណ បាបនាឝាត៌្ហម៑ ឯកក្ឫត្វោ ជគតះ ឝេឞកាលេ ប្រចកាឝេ។ (aiōn )
Ndi chikhulupiriro timazindikira kuti dziko lapansi ndi la mmwamba zinapangidwa ndi Mawu a Mulungu, ndikuti zinthu zoonekazi zinachokera ku zinthu zosaoneka. (aiōn )
អបរម៑ ឦឝ្វរស្យ វាក្យេន ជគន្ត្យស្ឫជ្យន្ត, ទ្ឫឞ្ដវស្តូនិ ច ប្រត្យក្ឞវស្តុភ្យោ នោទបទ្យន្តៃតទ៑ វយំ វិឝ្វាសេន ពុធ្យាមហេ។ (aiōn )
Yesu Khristu ndi yemweyo dzulo, lero ndi kunthawi zonse. (aiōn )
យីឝុះ ខ្រីឞ្ដះ ឝ្វោៜទ្យ សទា ច ស ឯវាស្តេ។ (aiōn )
Mulungu wamtendere, amene kudzera mʼmagazi a pangano lamuyaya anaukitsa Ambuye athu Yesu kwa akufa, amene ndi Mʼbusa wamkulu, (aiōnios )
អនន្តនិយមស្យ រុធិរេណ វិឝិឞ្ដោ មហាន៑ មេឞបាលកោ យេន ម្ឫតគណមធ្យាត៑ បុនរានាយិ ស ឝាន្តិទាយក ឦឝ្វរោ (aiōnios )
akupatseni chilichonse chabwino kuti muchite chifuniro chake ndipo Mulungu achite mwa ife, chimene chingamukomere kudzera mwa Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero ku nthawi zanthawi, Ameni. (aiōn )
និជាភិមតសាធនាយ សវ៌្វស្មិន៑ សត្កម៌្មណិ យុឞ្មាន៑ សិទ្ធាន៑ ករោតុ, តស្យ ទ្ឫឞ្ដៅ ច យទ្យត៑ តុឞ្ដិជនកំ តទេវ យុឞ្មាកំ មធ្យេ យីឝុនា ខ្រីឞ្ដេន សាធយតុ។ តស្មៃ មហិមា សវ៌្វទា ភូយាត៑។ អាមេន៑។ (aiōn )
Lilime nalonso ndi moto, dziko la zoyipa pakati pa ziwalo za thupi. Limawononga munthu yense wathunthu. Limayika zonse za moyo wake pa moto, ndipo moto wake ndi wochokera ku gehena. (Geenna )
រសនាបិ ភវេទ៑ វហ្និរធម៌្មរូបបិឞ្ដបេ។ អស្មទង្គេឞុ រសនា តាទ្ឫឝំ សន្តិឞ្ឋតិ សា ក្ឫត្ស្នំ ទេហំ កលង្កយតិ ស្ឫឞ្ដិរថស្យ ចក្រំ ប្រជ្វលយតិ នរកានលេន ជ្វលតិ ច។ (Geenna )
Popeza mwabadwanso, osati ndi mbewu imene imawonongeka, koma imene siwonongeka, ndiye kuti ndi Mawu a Mulungu amoyo ndi okhalitsa. (aiōn )
យស្មាទ៑ យូយំ ក្ឞយណីយវីយ៌្យាត៑ នហិ កិន្ត្វក្ឞយណីយវីយ៌្យាទ៑ ឦឝ្វរស្យ ជីវនទាយកេន និត្យស្ថាយិនា វាក្យេន បុនជ៌ន្ម គ្ឫហីតវន្តះ។ (aiōn )
koma mawu a Ambuye adzakhala mpaka muyaya.” Ndipo awa ndi mawu amene tinalalikira kwa inu. (aiōn )
កិន្តុ វាក្យំ បរេឝស្យានន្តកាលំ វិតិឞ្ឋតេ។ តទេវ ច វាក្យំ សុសំវាទេន យុឞ្មាកម៑ អន្តិកេ ប្រកាឝិតំ។ (aiōn )
Ngati wina ayankhula, ayankhuledi mawu enieni a Mulungu. Ngati wina atumikira, atumikire ndi mphamvu imene Mulungu amapereka, kuti pa zonse Mulungu alemekezedwe mwa Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero ndi mphamvu mpaka muyaya, Ameni. (aiōn )
យោ វាក្យំ កថយតិ ស ឦឝ្វរស្យ វាក្យមិវ កថយតុ យឝ្ច បរម៑ ឧបករោតិ ស ឦឝ្វរទត្តសាមត៌្ហ្យាទិវោបករោតុ។ សវ៌្វវិឞយេ យីឝុខ្រីឞ្ដេនេឝ្វរស្យ គៅរវំ ប្រកាឝ្យតាំ តស្យៃវ គៅរវំ បរាក្រមឝ្ច សវ៌្វទា ភូយាត៑។ អាមេន។ (aiōn )
Ndipo Mulungu wachisomo chonse, amene anakuyitanani ku ulemerero wake wamuyaya mwa Khristu, mutamva zowawa pa kanthawi, adzakukonzaninso ndi kukulimbitsani pa maziko olimba. (aiōnios )
ក្ឞណិកទុះខភោគាត៑ បរម៑ អស្មភ្យំ ខ្រីឞ្ដេន យីឝុនា ស្វកីយានន្តគៅរវទានាត៌្ហំ យោៜស្មាន៑ អាហូតវាន៑ ស សវ៌្វានុគ្រាហីឝ្វរះ ស្វយំ យុឞ្មាន៑ សិទ្ធាន៑ ស្ថិរាន៑ សពលាន៑ និឝ្ចលាំឝ្ច ករោតុ។ (aiōnios )
Kwa Iye kukhale mphamvu mpaka muyaya, Ameni. (aiōn )
តស្យ គៅរវំ បរាក្រមឝ្ចានន្តកាលំ យាវទ៑ ភូយាត៑។ អាមេន៑។ (aiōn )
Mudzalandiridwa bwino kwambiri mu ufumu wosatha wa Ambuye ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu. (aiōnios )
យតោ ៜនេន ប្រការេណាស្មាកំ ប្រភោស្ត្រាត្ឫ រ្យីឝុខ្រីឞ្ដស្យានន្តរាជ្យស្យ ប្រវេឝេន យូយំ សុកលេន យោជយិឞ្យធ្វេ។ (aiōnios )
Pakuti Mulungu sanalekerere angelo atachimwa paja, koma anawaponya mʼndende, nawayika mʼmaenje amdima, kuwasunga kuti adzaweruzidwe. (Tartaroō )
ឦឝ្វរះ ក្ឫតបាបាន៑ ទូតាន៑ ន ក្ឞមិត្វា តិមិរឝ្ឫង្ខលៃះ បាតាលេ រុទ្ធ្វា វិចារាត៌្ហំ សមប៌ិតវាន៑។ (Tartaroō )
Koma kulani mu chisomo ndi mʼchidziwitso cha Ambuye ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero tsopano mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
កិន្ត្វស្មាកំ ប្រភោស្ត្រាតុ រ្យីឝុខ្រីឞ្ដស្យានុគ្រហេ ជ្ញានេ ច វទ៌្ធធ្វំ។ តស្យ គៅរវម៑ ឥទានីំ សទាកាលញ្ច ភូយាត៑។ អាមេន៑។ (aiōn )
Moyowo unaoneka, tinawuona ndipo tikuchitira umboni. Tikukulalikirani za moyo wosatha umene unali ndi Atate ndipo unaonekera kwa ife. (aiōnios )
ស ជីវនស្វរូបះ ប្រកាឝត វយញ្ច តំ ទ្ឫឞ្ដវន្តស្តមធិ សាក្ឞ្យំ ទទ្មឝ្ច, យឝ្ច បិតុះ សន្និធាវវត៌្តតាស្មាកំ សមីបេ ប្រកាឝត ច តម៑ អនន្តជីវនស្វរូបំ វយំ យុឞ្មាន៑ ជ្ញាបយាមះ។ (aiōnios )
Dziko lapansi likupita pamodzi ndi zilakolako zake, koma amene amachita chifuniro cha Mulungu amakhalapo mpaka muyaya. (aiōn )
សំសារស្តទីយាភិលាឞឝ្ច វ្យត្យេតិ កិន្តុ យ ឦឝ្វរស្យេឞ្ដំ ករោតិ សោ ៜនន្តកាលំ យាវត៑ តិឞ្ឋតិ។ (aiōn )
Ndipo chimene anatilonjeza nʼchimenechi: moyo wosatha. (aiōnios )
ស ច ប្រតិជ្ញយាស្មភ្យំ យត៑ ប្រតិជ្ញាតវាន៑ តទ៑ អនន្តជីវនំ។ (aiōnios )
Aliyense amene amadana ndi mʼbale wake ndi wakupha, ndipo inu mukudziwa kuti wopha anthu mwa iye mulibe moyo wosatha. (aiōnios )
យះ កឝ្ចិត៑ ស្វភ្រាតរំ ទ្វេឞ្ដិ សំ នរឃាតី កិញ្ចានន្តជីវនំ នរឃាតិនះ កស្យាប្យន្តរេ នាវតិឞ្ឋតេ តទ៑ យូយំ ជានីថ។ (aiōnios )
Ndipo umboniwo ndi uwu: Mulungu anatipatsa moyo wosatha, ndipo moyowu uli mwa Mwana wake. (aiōnios )
តច្ច សាក្ឞ្យមិទំ យទ៑ ឦឝ្វរោ ៜស្មភ្យម៑ អនន្តជីវនំ ទត្តវាន៑ តច្ច ជីវនំ តស្យ បុត្រេ វិទ្យតេ។ (aiōnios )
Ine ndikulemba zimenezi kwa inu, amene mwakhulupirira dzina la Mwana wa Mulungu kuti mudziwe kuti muli ndi moyo wosatha. (aiōnios )
ឦឝ្វរបុត្រស្យ នាម្និ យុឞ្មាន៑ ប្រត្យេតានិ មយា លិខិតានិ តស្យាភិប្រាយោ ៜយំ យទ៑ យូយម៑ អនន្តជីវនប្រាប្តា ឥតិ ជានីយាត តស្យេឝ្វរបុត្រស្យ នាម្និ វិឝ្វសេត ច។ (aiōnios )
Tikudziwa kuti Mwana wa Mulungu anafika ndipo anatipatsa nzeru, kuti timudziwe Iye amene ali woona. Ndipo ife tili mwa Iye amene ndi woona, Mwana wake, Yesu Khristu. Iye ndi Mulungu woona ndi moyo wosatha. (aiōnios )
អបរម៑ ឦឝ្វរស្យ បុត្រ អាគតវាន៑ វយញ្ច យយា តស្យ សត្យមយស្យ ជ្ញានំ ប្រាប្នុយាមស្តាទ្ឫឝីំ ធិយម៑ អស្មភ្យំ ទត្តវាន៑ ឥតិ ជានីមស្តស្មិន៑ សត្យមយេ ៜរ្ថតស្តស្យ បុត្រេ យីឝុខ្រីឞ្ដេ តិឞ្ឋាមឝ្ច; ស ឯវ សត្យមយ ឦឝ្វរោ ៜនន្តជីវនស្វរូបឝ្ចាស្តិ។ (aiōnios )
Timakukondani chifukwa cha choonadi chimene chimakhala mwa ife ndipo chidzakhala mwa ife mpaka muyaya. (aiōn )
សត្យមតាទ៑ យុឞ្មាសុ មម ប្រេមាស្តិ កេវលំ មម នហិ កិន្តុ សត្យមតជ្ញានាំ សវ៌្វេឞាមេវ។ យតះ សត្យមតម៑ អស្មាសុ តិឞ្ឋត្យនន្តកាលំ យាវច្ចាស្មាសុ ស្ថាស្យតិ។ (aiōn )
Ndipo mukumbukire angelo amene sanakhutire ndi maudindo awo, koma anasiya malo awo. Angelo amenewa Mulungu anawamanga ndi maunyolo osatha, ndipo akuwasunga mʼmalo a mdima mpaka tsiku lalikulu lachiweruzo. (aïdios )
យេ ច ស្វគ៌ទូតាះ ស្វីយកត៌្ឫត្វបទេ ន ស្ថិត្វា ស្វវាសស្ថានំ បរិត្យក្តវន្តស្តាន៑ ស មហាទិនស្យ វិចារាត៌្ហម៑ អន្ធការមយេ ៜធះស្ថានេ សទាស្ថាយិភិ រ្ពន្ធនៃរពធ្នាត៑។ (aïdios )
Musayiwale mizinda ya Sodomu ndi Gomora ija, ndi mizinda yoyandikana nayo. Anthu mʼmenemo anadziperekanso kuchita zadama ndi kuchita zonyansa zachilendo. Mizinda imeneyi yakhala ngati chitsanzo cha amene adzalangidwa ndi moto wosatha. (aiōnios )
អបរំ សិទោមម៑ អមោរា តន្និកដស្ថនគរាណិ ចៃតេឞាំ និវាសិនស្តត្សមរូបំ វ្យភិចារំ ក្ឫតវន្តោ វិឞមមៃថុនស្យ ចេឞ្ដយា វិបថំ គតវន្តឝ្ច តស្មាត៑ តាន្យបិ ទ្ឫឞ្ដាន្តស្វរូបាណិ ភូត្វា សទាតនវហ្និនា ទណ្ឌំ ភុញ្ជតេ។ (aiōnios )
Iwowa ali ngati mafunde awukali apanyanja, amene amatulutsa thovu la zonyansa zawo. Amenewa ali ngati nyenyezi zosochera, ndipo Mulungu akuwasungira mdima wandiweyani mpaka muyaya. (aiōn )
ស្វកីយលជ្ជាផេណោទ្វមកាះ ប្រចណ្ឌាះ សាមុទ្រតរង្គាះ សទាកាលំ យាវត៑ ឃោរតិមិរភាគីនិ ភ្រមណការីណិ នក្ឞត្រាណិ ច ភវន្តិ។ (aiōn )
Khalani mʼchikondi cha Mulungu pamene mukudikira chifundo cha Ambuye athu Yesu Khristu kuti akubweretsereni moyo wosatha. (aiōnios )
ឦឝ្វរស្យ ប្រេម្នា ស្វាន៑ រក្ឞត, អនន្តជីវនាយ ចាស្មាកំ ប្រភោ រ្យីឝុខ្រីឞ្ដស្យ ក្ឫបាំ ប្រតីក្ឞធ្វំ។ (aiōnios )
kwa Mulungu yekhayo, Mpulumutsi wathu, kwa Iye kukhale ulemerero, ukulu, mphamvu ndi ulamuliro, mwa Yesu Khristu Ambuye athu, kuyambira isanayambe nthawi, tsopano mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
យោ ៜស្មាកម៑ អទ្វិតីយស្ត្រាណកត៌្តា សវ៌្វជ្ញ ឦឝ្វរស្តស្យ គៅរវំ មហិមា បរាក្រមះ កត៌្ឫត្វញ្ចេទានីម៑ អនន្តកាលំ យាវទ៑ ភូយាត៑។ អាមេន៑។ (aiōn )
ndipo watisandutsa mafumu ndi ansembe kuti tizitumikira Mulungu ndi Atate ake. Kwa Iye kukhale ulemerero ndi mphamvu ku nthawi zosatha, Ameni. (aiōn )
យោ ៜស្មាសុ ប្រីតវាន៑ ស្វរុធិរេណាស្មាន៑ ស្វបាបេភ្យះ ប្រក្ឞាលិតវាន៑ តស្យ បិតុរីឝ្វរស្យ យាជកាន៑ ក្ឫត្វាស្មាន៑ រាជវគ៌េ និយុក្តវាំឝ្ច តស្មិន៑ មហិមា បរាក្រមឝ្ចានន្តកាលំ យាវទ៑ វត៌្តតាំ។ អាមេន៑។ (aiōn )
Ine ndine Wamoyo; ndinali wakufa ndipo taona ndine wamoyo mpaka muyaya! Ndipo ndili ndi makiyi a imfa ndi Hade. (aiōn , Hadēs )
អហម៑ អមរស្តថាបិ ម្ឫតវាន៑ កិន្តុ បឝ្យាហម៑ អនន្តកាលំ យាវត៑ ជីវាមិ។ អាមេន៑។ ម្ឫត្យោះ បរលោកស្យ ច កុញ្ជិកា មម ហស្តគតាះ។ (aiōn , Hadēs )
Nthawi zonse zamoyozo zimapereka ulemerero, ulemu ndi mayamiko kwa uja wokhala pa mpando waufumu, amene ali ndi moyo wamuyaya. (aiōn )
ឥត្ថំ តៃះ ប្រាណិភិស្តស្យានន្តជីវិនះ សិំហាសនោបវិឞ្ដស្យ ជនស្យ ប្រភាវេ គៅរវេ ធន្យវាទេ ច ប្រកីត៌្តិតេ (aiōn )
Izi zikamachitika akuluakulu 24 aja amadzigwetsa pansi pamaso pa wokhala pa mpando waufumuyo, namupembedza wokhala ndi moyo wamuyayayo. Iwo amaponya pansi zipewa zawo zaufumu patsogolo pa mpando waufumu nati: (aiōn )
តេ ចតុវ៌ិំឝតិប្រាចីនា អបិ តស្យ សិំហាសនោបវិឞ្ដស្យាន្តិកេ ប្រណិនត្យ តម៑ អនន្តជីវិនំ ប្រណមន្តិ ស្វីយកិរីដាំឝ្ច សិំហាសនស្យាន្តិកេ និក្ឞិប្យ វទន្តិ, (aiōn )
Kenaka ndinamva mawu a cholengedwa chilichonse kumwamba, pa dziko lapansi, kunsi kwa dziko lapansi, pa nyanja ndi zonse zili mʼmenemo zikuyimba kuti, “Kwa wokhala pa mpando waufumu ndi kwa Mwana Wankhosa, kukhale mayamiko, ulemu, ulemerero ndi mphamvu (aiōn )
អបរំ ស្វគ៌មត៌្ត្យបាតាលសាគរេឞុ យានិ វិទ្យន្តេ តេឞាំ សវ៌្វេឞាំ ស្ឫឞ្ដវស្តូនាំ វាគិយំ មយា ឝ្រុតា, ប្រឝំសាំ គៅរវំ ឝៅយ៌្យម៑ អាធិបត្យំ សនាតនំ។ សិំហសនោបវិឞ្ដឝ្ច មេឞវត្សឝ្ច គច្ឆតាំ។ (aiōn )
Nditayangʼana patsogolo panga ndinaona kavalo wotuwa! Wokwerapo wake dzina lake linali Imfa ndipo Hade inali kumutsatira pambuyo pake. Anapatsidwa ulamuliro pa gawo limodzi la magawo anayi a dziko lapansi kuti aphe ndi lupanga, njala, mliri, ndi zirombo zakuthengo za mʼdziko lapansi. (Hadēs )
តតះ បាណ្ឌុរវណ៌ ឯកោ ៜឝ្វោ មយា ទ្ឫឞ្ដះ, តទារោហិណោ នាម ម្ឫត្យុរិតិ បរលោកឝ្ច តម៑ អនុចរតិ ខង្គេន ទុព៌្ហិក្ឞេណ មហាមាយ៌្យា វន្យបឝុភិឝ្ច លោកានាំ ពធាយ ប្ឫថិវ្យាឝ្ចតុត៌្ហាំឝស្យាធិបត្យំ តស្មា អទាយិ។ (Hadēs )
Iwo anati, “Ameni! Matamando ndi ulemerero, nzeru, mayamiko, ulemu, ulamuliro ndi mphamvu zikhale kwa Mulungu wathu kunthawi zanthawi, Ameni!” (aiōn )
តថាស្តុ ធន្យវាទឝ្ច តេជោ ជ្ញានំ ប្រឝំសនំ។ ឝៅយ៌្យំ បរាក្រមឝ្ចាបិ ឝក្តិឝ្ច សវ៌្វមេវ តត៑។ វត៌្តតាមីឝ្វរេៜស្មាកំ និត្យំ និត្យំ តថាស្ត្វិតិ។ (aiōn )
Mngelo wachisanu anayimba lipenga lake, ndipo ndinaona nyenyezi ikugwa pa dziko lapansi kuchokera ku thambo. Nyenyeziyo inapatsidwa kiyi ya ku chidzenje chakuya. (Abyssos )
តតះ បរំ សប្តមទូតេន តូយ៌្យាំ វាទិតាយាំ គគនាត៑ ប្ឫថិវ្យាំ និបតិត ឯកស្តារកោ មយា ទ្ឫឞ្ដះ, តស្មៃ រសាតលកូបស្យ កុញ្ជិកាទាយិ។ (Abyssos )
Nyenyeziyo itatsekula pa chidzenje chakuyacho panatuluka utsi ngati wochokera mʼngʼanjo yayikulu. Dzuwa ndi thambo zinada chifukwa cha utsi ochokera mʼdzenjemo. (Abyssos )
តេន រសាតលកូបេ មុក្តេ មហាគ្និកុណ្ឌស្យ ធូម ឥវ ធូមស្តស្មាត៑ កូបាទ៑ ឧទ្គតះ។ តស្មាត៑ កូបធូមាត៑ សូយ៌្យាកាឝៅ តិមិរាវ្ឫតៅ។ (Abyssos )
Mfumu yawo inali mngelo wolamulira Chidzenje chakuya chija. Mʼchihebri dzina lake ndi Abadoni ndipo mʼChigriki ndi Apoliyoni (tanthauzo lake ndiye kuti, Wowononga). (Abyssos )
តេឞាំ រាជា ច រសាតលស្យ ទូតស្តស្យ នាម ឥព្រីយភាឞយា អពទ្ទោន៑ យូនានីយភាឞយា ច អបល្លុយោន៑ អត៌្ហតោ វិនាឝក ឥតិ។ (Abyssos )
Mngeloyo analumbira mʼdzina la Iye wokhala ndi moyo mpaka muyaya, amene analenga kumwamba ndi zonse zili kumeneko, dziko lapansi ndi zonse zili mʼmenemo, nyanja ndi zonse zili mʼmenemo, nati, “Pasakhalenso zochedwa tsopano! (aiōn )
អបរំ ស្វគ៌ាទ៑ យស្យ រវោ មយាឝ្រាវិ ស បុន រ្មាំ សម្ភាវ្យាវទត៑ ត្វំ គត្វា សមុទ្រមេទិន្យោស្តិឞ្ឋតោ ទូតស្យ ករាត៑ តំ វិស្តីណ៌ ក្ឞុទ្រគ្រន្ថំ គ្ឫហាណ, តេន មយា ទូតសមីបំ គត្វា កថិតំ គ្រន្ថោ ៜសៅ ទីយតាំ។ (aiōn )
Tsono zikadzatsiriza umboni wawowo, chirombo chotuluka mʼChidzenje chakuya chija chidzachita nawo nkhondo nʼkuzigonjetsa mpaka kuzipha. (Abyssos )
អបរំ តយោះ សាក្ឞ្យេ សមាប្តេ សតិ រសាតលាទ៑ យេនោត្ថិតវ្យំ ស បឝុស្តាភ្យាំ សហ យុទ្ធ្វា តៅ ជេឞ្យតិ ហនិឞ្យតិ ច។ (Abyssos )
Mngelo wachisanu ndi chiwiri anawomba lipenga lake, ndipo kumwamba kunamveka mawu ofuwula amene anati, “Ufumu wa dziko lapansi uli mʼmanja mwa Ambuye athu ndi Khristu wake uja, ndipo adzalamulira mpaka muyaya.” (aiōn )
អនន្តរំ សប្តទូតេន តូយ៌្យាំ វាទិតាយាំ ស្វគ៌ ឧច្ចៃះ ស្វរៃវ៌ាគិយំ កីត៌្តិតា, រាជត្វំ ជគតោ យទ្យទ៑ រាជ្យំ តទធុនាភវត៑។ អស្មត្ប្រភោស្តទីយាភិឞិក្តស្យ តារកស្យ ច។ តេន ចានន្តកាលីយំ រាជត្វំ ប្រករិឞ្យតេ៕ (aiōn )
Kenaka ndinaona mngelo wina akuwuluka mu mlengalenga ndipo anali ndi Uthenga Wabwino wamuyaya woti akalalikire kwa anthu okhala pa dziko lapansi, kwa a mtundu uliwonse, a fuko lililonse, a chiyankhulo chilichonse ndi kwa anthu onse. (aiōnios )
អនន្តរម៑ អាកាឝមធ្យេនោឌ្ឌីយមានោ ៜបរ ឯកោ ទូតោ មយា ទ្ឫឞ្ដះ សោ ៜនន្តកាលីយំ សុសំវាទំ ធារយតិ ស ច សុសំវាទះ សវ៌្វជាតីយាន៑ សវ៌្វវំឝីយាន៑ សវ៌្វភាឞាវាទិនះ សវ៌្វទេឝីយាំឝ្ច ប្ឫថិវីនិវាសិនះ ប្រតិ តេន ឃោឞិតវ្យះ។ (aiōnios )
Ndipo utsi wa moto wowazunzawo udzakwera kumwamba mpaka muyaya. Sikudzakhala kupumula usana ndi usiku kwa amene anapembedza chirombo chija ndi fano lake kapena kwa aliyense amene analembedwa chizindikiro cha dzina lake lija.” (aiōn )
តេឞាំ យាតនាយា ធូមោ ៜនន្តកាលំ យាវទ៑ ឧទ្គមិឞ្យតិ យេ ច បឝុំ តស្យ ប្រតិមាញ្ច បូជយន្តិ តស្យ នាម្នោ ៜង្កំ វា គ្ឫហ្លន្តិ តេ ទិវានិឝំ កញ្ចន វិរាមំ ន ប្រាប្ស្យន្តិ។ (aiōn )
Ndipo kenaka chimodzi cha zamoyo zinayi zija chinapereka kwa angelo asanu ndi awiri mbale zisanu ndi ziwiri zodzaza ndi ukali wa Mulungu amene ali ndi moyo mpaka muyaya. (aiōn )
អបរំ ចតុណ៌ាំ ប្រាណិនាម៑ ឯកស្តេភ្យះ សប្តទូតេភ្យះ សប្តសុវណ៌កំសាន៑ អទទាត៑។ (aiōn )
Chirombo chimene wachionachi chinalipo kale koma tsopano kulibe ndipo chidzatuluka ku chidzenje chakuya ndi kupita kukawonongedwa. Anthu okhala pa dziko lapansi amene mayina awo sanalembedwe mʼbuku lamoyo kuyambira pa kulengedwa kwa dziko lapansi adzadabwa pamene adzaona chirombocho, chifukwa chinalipo kale, tsopano kulibe, komabe chidzabwera. (Abyssos )
ត្វយា ទ្ឫឞ្ដោ ៜសៅ បឝុរាសីត៑ នេទានីំ វត៌្តតេ កិន្តុ រសាតលាត៑ តេនោទេតវ្យំ វិនាឝឝ្ច គន្តវ្យះ។ តតោ យេឞាំ នាមានិ ជគតះ ស្ឫឞ្ដិកាលម៑ អារភ្យ ជីវនបុស្តកេ លិខិតានិ ន វិទ្យន្តេ តេ ប្ឫថិវីនិវាសិនោ ភូតម៑ អវត៌្តមានមុបស្ថាស្យន្តញ្ច តំ បឝុំ ទ្ឫឞ្ដ្វាឝ្ចយ៌្យំ មំស្យន្តេ។ (Abyssos )
Ndipo anafuwulanso kuti, “Haleluya! Utsi wochokera kwa mkazi wadamayo udzakwera kumwamba mpaka muyaya.” (aiōn )
បុនរបិ តៃរិទមុក្តំ យថា, ព្រូត បរេឝ្វរំ ធន្យំ យន្និត្យំ និត្យមេវ ច។ តស្យា ទាហស្យ ធូមោ ៜសៅ ទិឝមូទ៌្ធ្វមុទេឞ្យតិ៕ (aiōn )
Koma chirombocho chinagwidwa pamodzi ndi mneneri wonyenga uja amene anachita zizindikiro zodabwitsa pamaso pake. Ndi zizindikirozi anasocheretsa amene analembedwa chizindikiro cha chirombocho napembedza fano lake. Onse awiri anaponyedwa amoyo mʼnyanja yamoto yasulufule wotentha. (Limnē Pyr )
តតះ ស បឝុ រ្ធ្ឫតោ យឝ្ច មិថ្យាភវិឞ្យទ្វក្តា តស្យាន្តិកេ ចិត្រកម៌្មាណិ កុវ៌្វន៑ តៃរេវ បឝ្វង្កធារិណស្តត្ប្រតិមាបូជកាំឝ្ច ភ្រមិតវាន៑ សោ ៜបិ តេន សាទ៌្ធំ ធ្ឫតះ។ តៅ ច វហ្និគន្ធកជ្វលិតហ្រទេ ជីវន្តៅ និក្ឞិប្តៅ។ (Limnē Pyr )
Ndipo ndinaona mngelo akutsika kuchokera kumwamba ali ndi kiyi ya ku chidzenje chakuya chija atanyamula mʼdzanja lake unyolo waukulu. (Abyssos )
តតះ បរំ ស្វគ៌ាទ៑ អវរោហន៑ ឯកោ ទូតោ មយា ទ្ឫឞ្ដស្តស្យ ករេ រមាតលស្យ កុញ្ជិកា មហាឝ្ឫង្ខលញ្ចៃកំ តិឞ្ឋតះ។ (Abyssos )
Anamuponya ku chidzenje chakuya chija namutsekera ndi kiyi ndi kumatirira pa khomopo kuti asatulukenso kukanyenga mitundu ya anthu mpaka patapita zaka 1,000. Zikadzatha zakazo, adzamumasula kwa kanthawi pangʼono chabe. (Abyssos )
អបរំ រសាតលេ តំ និក្ឞិប្យ តទុបរិ ទ្វារំ រុទ្ធ្វា មុទ្រាង្កិតវាន៑ យស្មាត៑ តទ៑ វឞ៌សហស្រំ យាវត៑ សម្បូណ៌ំ ន ភវេត៑ តាវទ៑ ភិន្នជាតីយាស្តេន បុន រ្ន ភ្រមិតវ្យាះ។ តតះ បរម៑ អល្បកាលាត៌្ហំ តស្យ មោចនេន ភវិតវ្យំ។ (Abyssos )
Ndipo Mdierekezi amene anawanyenga, anaponyedwa mʼnyanja ya sulufule wotentha, kumene kunaponyedwa chirombo chija ndi mneneri wonama uja. Iwo adzazunzika usiku ndi usana kwamuyaya. (aiōn , Limnē Pyr )
តេឞាំ ភ្រមយិតា ច ឝយតានោ វហ្និគន្ធកយោ រ្ហ្រទេ ៜរ្ថតះ បឝុ រ្មិថ្យាភវិឞ្យទ្វាទី ច យត្រ តិឞ្ឋតស្តត្រៃវ និក្ឞិប្តះ, តត្រានន្តកាលំ យាវត៑ តេ ទិវានិឝំ យាតនាំ ភោក្ឞ្យន្តេ។ (aiōn , Limnē Pyr )
Nyanja inapereka amene anaferamo ndipo imfa ndi Hade zinapereka akufa ake ndipo munthu aliyense anaweruzidwa monga mwa ntchito zake. (Hadēs )
តទានីំ សមុទ្រេណ ស្វាន្តរស្ថា ម្ឫតជនាះ សមប៌ិតាះ, ម្ឫត្យុបរលោកាភ្យាមបិ ស្វាន្តរស្ថា ម្ឫតជនាះ សម៌ិបតាះ, តេឞាញ្ចៃកៃកស្យ ស្វក្រិយានុយាយី វិចារះ ក្ឫតះ។ (Hadēs )
Kenaka imfa ndi Hade zinaponyedwa mʼnyanja ya moto. Nyanja yamoto ndiyo imfa yachiwiri. (Hadēs , Limnē Pyr )
អបរំ ម្ឫត្យុបរលោកៅ វហ្និហ្រទេ និក្ឞិប្តៅ, ឯឞ ឯវ ទ្វិតីយោ ម្ឫត្យុះ។ (Hadēs , Limnē Pyr )
Ngati dzina la wina aliyense silinapezeke mʼBuku Lamoyo, anaponyedwa mʼnyanja yamoto. (Limnē Pyr )
យស្យ កស្យចិត៑ នាម ជីវនបុស្តកេ លិខិតំ នាវិទ្យត ស ឯវ តស្មិន៑ វហ្និហ្រទេ ន្យក្ឞិប្យត។ (Limnē Pyr )
Koma amantha, osakhulupirira, okonda zonyansa, opha anthu, achiwerewere, amatsenga, opembedza mafano ndi abodza, malo awo adzakhala nyanja yamoto ya sulufule wotentha. Iyi ndi imfa yachiwiri.” (Limnē Pyr )
កិន្តុ ភីតានាម៑ អវិឝ្វាសិនាំ ឃ្ឫណ្យានាំ នរហន្ត្ឫណាំ វេឝ្យាគាមិនាំ មោហកានាំ ទេវបូជកានាំ សវ៌្វេឞាម៑ អន្ឫតវាទិនាញ្ចាំឝោ វហ្និគន្ធកជ្វលិតហ្រទេ ភវិឞ្យតិ, ឯឞ ឯវ ទ្វិតីយោ ម្ឫត្យុះ។ (Limnē Pyr )
Sipadzakhalanso usiku. Sadzafuna kuwala kwa nyale kapena kwa dzuwa pakuti Ambuye Mulungu adzakhala kuwala kwawo. Ndipo adzalamulira kwamuyaya. (aiōn )
តទានីំ រាត្រិះ បុន រ្ន ភវិឞ្យតិ យតះ ប្រភុះ បរមេឝ្វរស្តាន៑ ទីបយិឞ្យតិ តេ ចានន្តកាលំ យាវទ៑ រាជត្វំ ករិឞ្យន្តេ។ (aiōn )